João 3
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Ndipo panali Mfarisi wotchedwa Nekodimo, wa mʼgulu lolamulira la Ayuda.
1 Jew hai ukwarin orot wabin Nicodemus i Pharisee ana kou’ayamaim orot ta.
2 Iye anabwera kwa Yesu usiku ndipo anati, “Rabi, ife tikudziwa kuti ndinu aphunzitsi wochokera kwa Mulungu, pakuti palibe amene angachite zizindikiro zodabwitsa zimene Inu mukuchita ngati Mulungu sali naye.”
2 Guguminamaim na Jesu biyan tit, naatu eo, “Bai’obaiyenayan, aki aso’ob o i bai’obaiyenayan God biyanane ina. Men yait ta karam boro ina’inanen fairih o kusisinafube nasinaf, God men hairi hinama’am na’at.” Jesus Nicodemus hairi bar tafan hima tibidudur|alt="Jesus and Nicodemus" src="CN01670b.tif" size="col" loc="Jhn 3.2" copy="©1978 David C. Cook Publishing Co." ref="3.1-4"
3 Poyankha Yesu ananena kuti, “Zoonadi, Ine ndikukuwuza kuti, ngati munthu sabadwanso mwatsopano sangathe kuona ufumu wa Mulungu.”
3 Mar ta’imonamo Jesu iya’afut, “Ayu tur anababatun a tur ao’owen, men yait ta boro God ana ma’ama wanatowan na’itin, baise i boro natufuw maiye’ebo.”
4 Nekodimo anati, “Kodi munthu angabadwenso bwanji atakalamba? Kodi angalowe kachiwiri mʼmimba ya amayi ake kuti abadwenso?”
4 “Orot ra’at gagamin na’in ema’am, boro mi’itube natufuw maiye?” Nicodemus ibat. “Men karam hinah yan wanawanan narun mar bairou’abin natufuw maiye!”
5 Yesu anayankha kuti, “Zoonadi, Ine ndikukuwuza kuti ngati munthu sabadwa mwa madzi ndi Mzimu Woyera, sangalowe mu ufumu wa Mulungu.
5 Jesu iya’afut eo, “Turobe a tur ao’owen, men yait ta boro God ana ma’ama wanatowan narun, baise i harew naatu Anuninamaim natufuw.
6 Thupi limabereka thupi, koma Mzimu amabereka mzimu.
6 Biyat etatoub, i biyat eya’iy, baise Anun Kakafiyin etatoub Anun Kakafiyin iya’iy.
7 Iwe usadabwe chifukwa ndakuwuza kuti, ‘Uyenera kubadwanso.’
7 O boro men ita’ororsa’ir ayu tur iti tufuw maiye ao isan.
8 Mphepo imawomba kulikonse kumene ikufuna. Ungathe kumva kuwomba kwake, koma sungathe kudziwa kumene ikuchokera kapena kumene ikupita. Nʼchimodzimodzi ndi amene abadwa ndi Mzimu Woyera.”
8 Waruw ana kokomaim ebababin. O i nidun kunonowar, baise o men karam boro inao, i menane na enan, o au mena’at babin enan. Imih orot babin anunihine i nati na’atube tetutufuw.”
9 Nekodimo anafunsa kuti, “Kodi izi zingatheke bwanji?”
9 Nicodemus i bat, “Iti i mi’itube?”
10 Yesu anati, “Iwe mphunzitsi wa Israeli, kodi sukuzindikira zimenezi?
10 Jesu eo, “O i Israel hai bai’obaiyenayan naatu o iti sawar men imanamamih?”
11 Zoonadi, Ine ndikukuwuza kuti ife tiyankhula zimene tikuzidziwa ndi kuchitira umboni zimene taziona, komabe inu simuvomereza umboni wathu.
11 Jesu iya’afut eo, “Ayu turobe a tur ao’owen, aki abisa asoso’ob i a’o, naatu abisa aki a’i’itin i isan a’o, baise kwa i boro’ika aki ai tur naniyan men kwabaibimih.
12 Ine ndikuyankhula kwa iwe zinthu za dziko lapansi ndipo sukukhulupirira. Nanga kodi udzakhulupirira bwanji ngati nditayankhula zinthu zakumwamba?
12 Ayu tafaram ana sawar isah ao kwanowar baise kwa men kwabitumatum. Kwa boro mi’itube kwanitumatum ayu mar ana sawar isah ana’o na’at?”
13 Palibe wina aliyense anapita kumwamba, koma yekhayo amene watsika kuchokera kumwamba, Mwana wa Munthu.
13 Men yait ta in mar run, baise orot Natun marane nan akisinamo.
14 Tsono monga Mose anapachika njoka mʼchipululu, moteronso Mwana wa Munthu ayenera kupachikidwa,
14 Moses mi’itube arar yan kok bora’ah na’atube, orot natun hinabora’ah nayen,
15 kuti aliyense amene akhulupirira Iye akhale ndi moyo wosatha.
15 saise iyabowat i tebitumatum boro ma’ama wanatowan hinab.
16 “Pakuti Mulungu anakonda dziko lapansi, kotero anapereka Mwana wake wobadwa yekha, kuti aliyense wokhulupirira Iye asatayike koma akhale ndi moyo wosatha.
16 God tafaram iyabuw kwanekwan imih i Natun ta’imonamo iyafar na, saise yait i ebitumitum boro men namorob, baise boro yawas wanatowan nab.
17 Pakuti Mulungu sanatume Mwana wake ku dziko lapansi, kuti akaweruze, koma kuti akapulumutse dziko lapansi.
17 God i men tafaram bai’afiyin isan Natun iyafar na tafaramaim titamih, baise tafaram baiyawasin isan na tit.
18 Aliyense wokhulupirira Iye saweruzidwa, koma aliyense wosakhulupirira waweruzidwa kale chifukwa sanakhulupirire dzina la Mwana wobadwa yekha wa Mulungu.
18 O yait I kubitumitum boro men ina’afemih, baise o yait men ebitumitum i eaf sawar, anayabin i men God Natun Ta’imon, i akisinamo wabin itumitumamih.
19 Ndipo chiweruzo ndi ichi: kuwunika kunabwera mʼdziko lapansi, koma anthu anakonda mdima mʼmalo mwa kuwunikako, chifukwa ntchito zawo zinali zoyipa.
19 Iti i baib’afiyen. Marakaw na tafaramamaim tit, baise orot marakaw efanin gugumin iyabuw anayabin hai sinaf kakafih.
20 Aliyense wochita zoyipa amadana ndi kuwunika, ndipo sabwera poyera chifukwa cha mantha kuti ntchito zake zingaonekere.
20 Orot babin etei sinaf kakafih tesisinaf i marakaw hikwahir naatu boro men hinan marakaw wanawanan hinarun, tebirubir hai sinaf boro hinirerereb.
21 Koma aliyense wokhala mu choonadi amabwera ku kuwunika, kuti zionekere poyera zimene iye wachita zachitika kudzera mwa Mulungu.”
21 Baise yait ta turobe’emaim ema’am marakaw wanatowan erur, saise i ana bowabow God wanawananamaim bowabow boro nirerereb.
22 Zitatha izi, Yesu ndi ophunzira ake anapita mʼmadera a ku midzi ya ku Yudeya, kumene Iye anakhala kanthawi akubatiza.
22 Iti ufunamaim, Jesu ana bai’ufununayah bairi hitit hin Judea tafaram ufunane hirun, nati’imaim mar kikimin hima naatu bapataito itih.
23 Ndipo Yohane amabatizanso ku Ainoni kufupi ndi Salimu, chifukwa kumeneko kunali madzi ambiri ndipo anthu amabwererabwererabe kudzabatizidwa.
23 Nati’imaim John auman tafaram Aenonamaim sabuw bapataito bitih, Salim i men ef yok i sisibinamaim, anayabin nati’imaim i harew moumurih, naatu sabuw i nan ufun hinan bapataito bain isan.
24 (Apa nʼkuti Yohane asanatsekeredwe mʼndende).
24 (Iti John dibur hiyaru’uy ma’am nanamaim.)
25 Mkangano unabuka pakati pa ophunzira ena a Yohane ndi Ayuda ena pa zamwambo wodziyeretsa wa Ayuda.
25 John ana bai’ufununayah afa naatu Jew sabuw afa wanawanahimaim gamin matar, bapataito ana ofafaren isan.
26 Iwo anabwera kwa Yohane anati, “Rabi, munthu uja munali naye mbali inayo ya mu mtsinje wa Yorodani, amene munamuchitira umboni, taonani naye akubatizanso, ndipo aliyense akupita kwa Iye.”
26 I hina John biyan hitit naatu hi’o, “Bai’obaiyenayan, orot nati o airi no Jordan harew rounane menatan isan o i’o’orerereb, i boun bapataito sabuw ebitih, naatu sabuw etei i isan tenan.”
27 Atamva zimenezi, Yohane anayankha kuti, “Munthu amalandira chokhacho chapatsidwa kwa iye kuchokera kumwamba.
27 Nati isan John iya’afut eo, “Orot abistanawat marane tebitin iwat nab.
28 Inuyo ndinu mboni zanga kuti ine ndinati, ‘Ine sindine Khristu koma ndatumidwa patsogolo pa Iye.’
28 Kwa taiyuw i karam ayu ao i kwanao’rereb, Ayu i men Keriso, baise ayu i nanamaim hiyafaru ana.
29 Mwini wake wa mkwatibwi ndi mkwati. Ndipo bwenzi lamkwati limadikira ndi kumvetsera iye, ndipo amakondwa akamva mawu a mkwatiyo. Ine changa ndi chimwemwe ndipo ndine wosangalala kwambiri.
29 Babin orot ana rum hi’o ema’am, orot ana of menatan i bai’awaninamih i orot isan ma tainin rub ma ekakaif, naatu i ana rum fanan enonowar ana veya i anababatun ekakawasa. Iti kawasa i ayu nowau, naatu kawasa i boun ana yomanin a’asa’ub.
30 Nʼkoyenera kuti Iyeyo akule, ine ndichepe.
30 I ana fair ra’at natabiru, ayu fair i men ra’at.”
31 “Iye wochokera kumwamba ndi wapamwamba pa onse: iye wochokera mʼdziko lapansi ndi wa dziko lapansi, ndipo amayankhula monga mmodzi wa adziko lapansi. Iye wochokera kumwamba ndi wopambana onse.
31 Yeit auyomane nan i ra’at etei natabirih, menatan iti tafaramane nan i tafaram nowan, naatu tafaram ana sawar isah i ebidudur. Menatan marane nan i sawar etei tafahimaim.
32 Iye achita umboni pa zimene waziona ndi kuzimva, koma palibe avomereza umboni wake.
32 I abis nonowar, i’itanen i isah eo’orerereb, baise men yait ta ana tur ebaibimih.
33 Munthu amene amawulandira akutsimikizira kuti Mulungu ndi woona.
33 Orot yait ta i ana tur nabitumitum na’at, i ebi’obaiyit i ebitumatum God abistan eo’o i turobe.
34 Pakuti amene Mulungu wamutuma amayankhula mawu a Mulungu; Mulungu wamupatsa Mzimu Woyera mopanda malire.
34 Menatan God biyafar i God ana tur eo’orerereb; anayabin God i Anun i nowanamih itin anababatun
35 Atate amakonda Mwana ndipo apereka zonse mʼmanja mwake.
35 Tamah Natun iyabuw kwanekwan naatu sawar etei i ana fair babanamaim ya.
36 Aliyense wokhulupirira Mwanayo ali ndi moyo wosatha, koma iye amene samvera Mwanayo sadzawuona moyo, pakuti mkwiyo wa Mulungu umakhala pa iye.”
36 Yait ana baitumatum Natunamaim naya’iy boro yawas wanatowan nab, baise yait ta God Natun nabifutuw boro men yawas nitinimih, God ana yaso’ar tafahimaim nama.
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar João 3, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.