João 20

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI

Sair da comparação
AAI TUR GEWASIN O BAIBASIT BOUBUN
1 Mmamawa tsiku loyamba la sabata, kukanali kamdimabe, Mariya wa ku Magadala anapita ku manda ndipo anaona kuti mwala unali utachotsedwa pa khomo la manda.
1 Fur an bubusuruf, maraumanika Mary Magdalin eregugumin auman in hubemaim tit, nuwanuw hub awan kabay hifururuw tit inu’in itin. |alt="women see stone rolled away" src="cn01850B.tif" size="col" loc="Jhn 20.1" copy="©1978 David C. Cook Publishing Co." ref="John 20.1"
2 Choncho anabwerera akuthamanga kwa Simoni Petro ndi wophunzira winayo, amene Yesu anamukonda, ndipo anati, “Iwo amuchotsa Ambuye mʼmanda, ndipo ife sitikudziwa kumene iwo amuyika Iye!”
2 Imih i matabir erenunuw in Simon Peter biyan naatu bai’ufununayan orot ta Jesu biyabuw i hairi biyah tit naatu eo, “Sabuw hina Regah biyan hubemaim hibosair naatu i menamaim hiya’iy, it men taso’ob.”
3 Choncho Petro ndi wophunzira winayo ananyamuka kupita ku manda.
3 Imih Peter naatu bai’ufununayan orot ta hairi hub itinamih hin.
4 Onse awiri anathamanga pamodzi koma wophunzira winayo anamupitirira Petro, nafika ku manda moyambirira.
4 Naatu hairi erenununuw hin, baise bai’ufununayan orot ta Peter i gegesair i wan in hubemaim tit.
5 Ndipo mmene anawerama nasuzumira mʼkati mwa manda anaona nsalu zili potero koma sanalowemo.
5 Naatu i kwafure nuwariy waifuw Jesu hisumisum inu’in itin baise men runamih.
6 Kenaka Simoni Petro, amene anali pambuyo pake, anafika ndi kulowa mʼmanda. Iye anaona nsaluzo zili pamenepo,
6 Naatu Simon Peter, uf nunuw na tit naatu in hub wanawanan run, waifuw Jesu hisum inu’in itin.
7 pamodzinso ndi nsalu imene anakulungira nayo mutu wa Yesu. Nsaluyi inali yopindidwa pa yokha yosiyanitsidwa ndi inayo.
7 naatu murubih tesumasum ana faifuw Jesu nukwarin himetan auman inu’in itin. Nati waifuw i taiyuwinawat nu nabin in, men Jesu biyan hisumisum aumanamih.
8 Pomaliza wophunzira winayo, amene anafika ku manda moyambirira, analowanso mʼkati, iye anaona ndi kukhulupirira.
8 Naatu bai’ufunenayan orot ta wan na hubamaim titit, i auman run. Itin itumatum.
9 (Iwo sanazindikire kuchokera mʼmalemba kuti Yesu anayanera kuuka kuchokera kwa akufa).
9 Naatu Buk Atamaninamaim eo i men hiso’ob, Jesu i boro morobone namisir.
10 Kenaka ophunzira anabwerera ku nyumba zawo,
10 Naatu bai’ufnunenayah himatabir hai ubar hin.
11 koma Mariya anayima kunja kwa manda akulira. Pamene akulira, anawerama ndi kusuzumira mʼmanda
11 baise Mary hub ufunane bat rererey. Rerey auman kwafure hub wanawanan nuwariy
12 ndipo anaona angelo awiri atavala zoyera, atakhala pamene panali mtembo wa Yesu, mmodzi kumutu ndi wina kumapazi.
12 naatu tounamatar rou’ab hai waifuw kwes Jesu inu’in ana efanamaim hima’am, ta nukwarinane ta anane.
13 Iwo anamufunsa iye kuti, “Amayi, nʼchifukwa chiyani mukulira?”
13 I babin hibatiy, “O aisim kurererey?” Babin eo, “Au Regah hibosair hibai hin menamaim hiyai, naatu ayu men aso’ob.”
14 Atanena izi, iye anatembenuka ndipo anaona Yesu atayima potero koma iye sanazindikire kuti anali Yesu.
14 Iti na’atube eo ana veya tatatabir Jesu nati’imaim batabat itin, baise i men so’ob nati i Jesu.
15 Iye anati, “Amayi, mukulira chifukwa chiyani? Ndani amene mukumufunafuna?”
15 Jesu eo, “Babin, o aisim kurererey? O i yait kununuwih” Babin notanot i masaw bowayan ta, imih i eo, “O inab inanan na’at, kuo anowar menamaim iyai saise ayu anan anab.”
16 Yesu anati kwa iye, “Mariya.”
16 Jesu babin isan eo, “Mary” Naatu Mary tatabir Jesu isan rerey Aramaic turamaim eo, “Rabboni.” Anayabin i Bai’obaiyenayan.
17 Yesu anati, “Usandigwire Ine, pakuti sindinapite kwa Atate. Mʼmalo mwake pita kwa abale anga ndikukawawuza kuti, ndikupita kwa Atate ndi kwa Atate anunso, kwa Mulungu wanga ndi Mulungu wanunso.”
17 Jesu eo, “Biyau men inabutubun, anayabin ayu men amatabir an Tamai biyan atitamih. baise kwen taitu hai tur ku’owen. Ayu amamatabir Tamai isan na’atube kwa Tamat, ayu au God kwa auman a God.”
18 Mariya wa ku Magadala anapita kwa ophunzira ndi uthenga wakuti, “Ndamuona Ambuye!” Iye anawawuza iwo kuti Yesu ananena zinthu izi kwa iye.
18 Mary Magdalin tur bai matabir in bai’ufnunenayah biyah tit, eo, “Ayu Regah aitin.” Naatu Jesu abistanawat eo nonowar i hai tur eowen.
19 Madzulo a tsiku limenelo limene linali loyamba la Sabata ophunzira ake ali pamodzi, atatseka ndi kukhoma zitseko chifukwa choopa Ayuda, Yesu anabwera ndi kuyima pakati pawo nati, “Mtendere ukhale nanu!”
19 Fur antoro’ot bubusuruf ana rabirab, bai’ufununayah etei’imak hiru’ay bar wanawanan etawan hitufabon hima’am, anayabin Jew hai ukwarih isah hibir. Jesu na hai founamaim bat naatu eo, “Tufuw isa nama.”
20 Iye atatha kunena izi, anawaonetsa manja ake ndi mʼnthiti mwake. Ophunzira anasangalala kwambiri pamene anaona Ambuye.
20 Iti na’atube eo’o ufunamaim, i uman naatu sisibin i’obaiyih. Anamaramaim Regah hi’i’itin, bai’ufununayah yasisir dogoroh awan karatan.
21 Yesu anatinso, “Mtendere ukhale nanu! Monga Atate anandituma Ine, Inenso ndikukutumani.”
21 Jesu ibanak eo maiye, “Tufuw isa nama! Tamat ayu iyunu ana, na’atube ayu kwa abiyuni.”
22 Ndi mawu amenewo Iye anawapumira ndipo anati, “Landirani Mzimu Woyera.
22 Naatu earatit tafahimaim yen naatu eo, “Anun Kakafiyin kwabai.
23 Ngati mukhululukira aliyense machimo ake, iwo akhululukidwa; ngati simuwakhululukira, iwo sanakhululukidwe.”
23 O yait ta tura ana kakafin inanonotawiy na’at, i i notawiy, o men hai kakafih inanonotawiyen na’at, God men nanotawiyihimih.”
24 Koma Tomasi (otchedwa Didimo), mmodzi wa khumi ndi awiriwo, sanali ndi ophunzira pamene Yesu anabwera.
24 Thomas, wabin ta Kikifukek, bai’ufununayah nah 12 i orot ta, i men bairi hima’am Jesu natitamih.
25 Ophunzira enawo atamuwuza Tomasi kuti iwo anaona Ambuye, iye ananenetsa kuti, “Pokhapokha nditaona zizindikiro za misomali mʼmanja ake ndi kuyikamo chala changa mʼmene munali misomali ndi kukhudza dzanja langa mʼnthiti mwake, ine sindidzakhulupirira.”
25 Bai’ufnunenayah afa ana tur hi’owen, “Aki Regah a’itin.”
26 Patapita sabata, ophunzira ake analinso mʼnyumbamo ndipo Tomasi anali nawo. Ngakhale makomo anali otsekedwa, Yesu anabwera nayima pakati pawo, ndipo anati, “Mtendere ukhale nanu!”
26 Fur nati ufunamaim ana baitumatumayah ibanak hiru’ay maiye bar wanawanan hima’am, naatu Thomas i nati’imaim bairi etawan hitufabon hima’am, Jesu na hai founamaim bat naatu eo, “Tufuw isa nama!”
27 Kenaka anati kwa Tomasi, “Ika chala chako apa; ona manja anga. Tambasula dzanja lako ndi kukhudza mʼnthiti mwanga. Leka kukayika, khulupirira.”
27 Naatu Thomas isan eo, “Uma kim iti’imaim kuyai, umu kwi’itah. Uma ku’ut ena au fit kubutubun. Kasiy kwihamiy naatu kwitumatum.”
28 Tomasi anati kwa Iye, “Ambuye wanga ndi Mulungu wanga!”
28 Thomas Jesu isan eo, “Ayu au Regah, au God.”
29 Kenaka Yesu anamuwuza kuti, “Kodi wakhulupirira chifukwa wandiona Ine? Ndi odala amene amakhulupirira ngakhale asanaone.”
29 Naatu Jesu Thomas iu, “Anayabin o ayu i’itu imih kubitumatum; iyab men ayu ti’i’itu baise tebitumatum i baigegewasin tebaib.”
30 Yesu anachita zodabwitsa zambiri pamaso pa ophunzira ake zimene sizinalembedwe mʼbuku lino.
30 Jesu ina’inanen afa gewagewasih moumurih maiyow sinafen ana bai’ufununayah matahimaim, nati afa men bukamaim hikirumen ti’inu’in.
31 Koma izi zalembedwa kuti mukhulupirire kuti Yesu ndi Khristu, Mwana wa Mulungu, ndi kuti mukakhulupirira mukhale nawo moyo mʼdzina lake.
31 Baise iti afa i hikirumen ti’inu’in saise imaim kwana’itin kwanitumatum Jesu Keriso, i God Natun, naatu i wabinamaim kwanabitumitum kwa boro yawas kwanab.

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar João 20, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.