João 1
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Pachiyambi panali Mawu, ndipo Mawu anali kwa Mulungu, ndipo Mawu ndiye Mulungu.
1 Tafaram matara’e ana veya Tur i wan ma, naatu Tur i God hairi hima, naatu Tur i God taiyuwin.
2 Mawuwa anali ndi Mulungu pachiyambi.
2 Tur i God hairi wan hima’abo tafaram matar.
3 Zinthu zonse zinalengedwa ndi Iye; ndipo popanda Iye sikukanakhala kanthu kalikonse kolengedwa.
3 Tur wanawananamaim God sawar etei’imak sinafen himatar; iti sawar himamatar i etei tur wanawananamaim himatar men ta asir matar kwaneyanamih.
4 Mwa Iye munali moyo, ndipo moyowo unali kuwunika kwa anthu.
4 Tur i yawas an anababatun, naatu iti yawas i sabuw isah marakaw bai na.
5 Kuwunika kunawala mu mdima, koma mdimawo sunakuzindikire.
5 Iti marakaw guguminamaim kusisiar, naatu gugumin men karam boro marakaw na’asabun.
6 Kunabwera munthu amene anatumizidwa kuchokera kwa Mulungu; Iyeyo dzina lake linali Yohane.
6 God ana kob abarayan wabin John iyafar na tit;
7 Iye anabwera ngati mboni kudzachitira umboni kuwunikako kuti kudzera mwa iye anthu onse akhulupirire.
7 marakaw isan sif ruboun eorereb sabuw hinowar, naatu sabuw iyab tur hinonowar hitumatum.
8 Iyeyu sanali kuwunika; koma anabwera ngati mboni ya kuwunika.
8 I taiyuwin i men marakaw; i marakaw akisin ana sif narubonamih na.
9 Kuwunika koona kumene kuwunikira munthu aliyense kunabwera ku dziko lapansi.
9 Iti marakaw i turobe, marakaw anababatun, tafaramaim na sabuw tafahimaim ekukusisiar.
10 Iye anali mʼdziko lapansi, ndipo ngakhale kuti dziko lapansi linalengedwa ndi Iye, dziko lapansilo silinamuzindikire Iye.
10 Tur i na tafaram eo mamatar wanawananamaim ma, baise tafaram i men inanimih.
11 Iye anabwera kwa iwo amene anali akeake, koma akewo sanamulandire Iye.
11 I na ana tafaram tit, baise taiyuwin ana sabuw i men hibaimih.
12 Koma kwa onse amene anamulandira Iye, kwa amene anakhulupirira mʼdzina lake, Iye anawapatsa mphamvu yokhala ana a Mulungu;
12 Baise sabuw afa hibai naatu wabinamaim hitumitum, naatu baibasit itih i hina God natunatun himatar.
13 ana wobadwa osati monga mwachilengedwe, kapena chisankho cha munthu, kapena chifuniro cha mwamuna koma wobadwa mwa Mulungu.
13 God natunatun himamatar i men orot anarara, o men orot babin aawan hairi hi’in kek tetutufu na’atube’emih, baise i God akisin anakokok sinaf i natunatun himatar.
14 Mawu anasandulika thupi ndipo anakhala pakati pathu. Ife tinaona ulemerero wake, ulemerero wa Iye amene ndi Mwana mmodzi yekhayo wa Atate, wodzaza ndi chisomo ndi choonadi.
14 Tur i na orot matar, naatu wanawanatamaim ma, ana marakaw bonamanamarin i taitin, iti marakaw bonamanamarin i God Natun ta’imonamo ebitin. Iti tur wanawanan i turobe naatu manaw kabeber awan karatan.
15 Yohane achitira umboni za Iye. Iye akufuwula kuti, “Uyu ndi Iye amene ndinati, ‘Iye amene akubwera pambuyo panga ndi wondiposa ine chifukwa, Iyeyo analipo ine ndisanabadwe.’ ”
15 John iti orot isan fanan sib binan eo,” Iti orot ayu isan ao’oban iti enan, anamaramaim ayu iti na’at ao, ‘I ayu ufu enan i ana fair ra’at ayu natabiru, anayabin i wan ma’abo ayu atufuw.’”
16 Kuchokera mʼkuchuluka kwa chisomo chake ife tonse talandira madalitso pamwamba pa madalitso.
16 I wanawanan manaw kabeber karsuwei it etei ebigegewasinit, ana baigegewasin tafan baban ebitit.
17 Pakuti lamulo linapatsidwa kudzera mwa Mose; chisomo ndi choonadi zinabwera kudzera mwa Yesu Khristu.
17 Anayabin God ana ofafar i Moses itin, baise manaw kabeber naatu turobe i Jesu Keriso’one na.
18 Palibe munthu amene anaona Mulungu, koma Mwana mmodzi yekhayo amene ali wa pamtima pa Atate, ndiye anafotokoza za Iye.
18 Men yait ta God itin. baise God Natun ta’imon Tamah wanawananamaim ema’am akisinamo God bai na bebeyanamaim tasusu’ub.
19 Tsopano uwu ndi umboni wa Yohane pamene Ayuda a ku Yerusalemu anatumiza ansembe ndi Alevi kudzamufunsa kuti iye anali yani.
19 Jew hai ukwarih Jerusalem hima’am firis afa naatu hai baibaisayah afa hiyafarih hin John hibatiy? “O i yait?”
20 Iye sanalephere kuvomereza, koma iye anavomereza momasuka kuti, “Ine sindine Khristu.”
20 I men baifuwenamaim iyafutih, baise i mutufor bebeyanamaim eorereb, “Ayu i men Keriso.”
21 Iwo anamufunsa kuti, “Nanga iwe ndiwe yani? Kodi ndiwe Eliya?”
21 Naatu hibatiy, “Bo o i yait? Om Elizah?” John eo, “Ayu men Elizah.” Ai o dinab orot?” John iya’afutih eo, “Ayu men dinab orot.”
22 Pomaliza iwo anati, “Ndiwe yani? Tipatse yankho kuti tipite nalo kwa amene anatituma. Kodi iwe ukuti chiyani za iwe mwini?”
22 Ibanak hibatiy maiye hio, “O i yait? Ku’o anowar saise anamatabir anan iyab hiyafari anan hai tur ana’owen. O taiyuw isa boro inakubuna ananowar.”
23 Yohane anayankha ndi mawu a mneneri Yesaya kuti, “Ine ndi mawu a wofuwula mʼchipululu, ‘Wongolani njira ya Ambuye.’ ”
23 John iya’afutih dinab orot Isaiah Buk Atamaninamaim kirum inu’in imaim eo, “Ayu i orot ta fanan araramaim eafa’af. Ef kwanarumutufur Regah ana remor isan!”
24 Tsopano Afarisi ena amene anatumidwa
24 Kob nayah Pharisee hiyafarih hina,
25 anamufunsa Iye kuti, “Kodi ndi chifukwa chiyani, umabatiza ngati iwe si Khristu, kapena Eliya, kapena Mneneri?”
25 John hibatiy, “Bo o men Keriso, o Elizah o dinab orot na’at, aisim sabuw bapataito kubitih?”
26 Yohane anayankha kuti, “Ine ndimabatiza ndi madzi, koma pakati panu payima amene simukumudziwa.
26 John hai tur eowen eo, “Ayu harewamaim sabuw bapataito abitih, Baise kwa wanawanamaim orot ta ebatabat kwa men kwaso’ob.
27 Iye ndi amene akubwera pambuyo panga, ine siwoyenera kumasula zingwe za nsapato zake.”
27 I Ayu ufu’umaim enan, an ana baibaiyon murab men gewasu boro anarufamen.”
28 Zonsezi zinachitika ku Betaniya kutsidya lina la mtsinje wa Yorodani, kumene Yohane ankabatizira.
28 Iti sawar etei i Bethany himatar harew Jordan sisibin veya yeninane, John sabuw bapataito bitihimaim.
29 Pa tsiku lotsatira Yohane anaona Yesu akubwera kwa iye ndipo anati, “Taonani, Mwana Wankhosa wa Mulungu, amene achotsa tchimo la dziko lapansi!
29 Mar to John nuw Jesu nan itin eo, “Kwanuw God Ana Lamb tafaram ana kakafin bosairenayan enan kwa’itin!”
30 Uyu ndi amene ndimatanthauza pamene ndinanena kuti, ‘Munthu amene akubwera pambuyo panga ndi wondiposa ine chifukwa analipo ine ndisanabadwe.’
30 Iti orot isan ao’orereb anamaramaim iti na’atube ao, ‘Orot ayu ufu’umaim enan i ana fair ra’at kwanekwan, anayabin i wan ma’abo ayu a tufuw.’
31 Ine mwini sindinamudziwe Iye, koma ndinabwera kubatiza ndi madzi kuti Iye adziwike mu Israeli.”
31 Ayu taiyuwu auman iti orot men asu’ub, baise anayabin nati isan ayu harewamaim sabuw bapataito abitih imaim Israel sabuw isah tirerereb hitaso’ob’.
32 Kenaka Yohane anapereka umboni uwu: “Ine ndinaona Mzimu Woyera ngati nkhunda kuchokera kumwamba nakhala pa Iye.
32 Naatu John iti tur eorereb. “Ayu Anunin mamu imag na’atube marane ra’iy naatu i tafanamaim mamara’at aitin.
33 Ine sindikanamudziwa Iye, koma kuti amene anandituma ine kudzabatiza ndi madzi anati kwa ine, ‘Munthu amene udzaona Mzimu Woyera akutsika nakhazikika pa Iye ndi amene adzabatize ndi Mzimu Woyera.’
33 Ayu iti orot i boro men ataso’ob, baise God iyunu ana harewamaim sabuw bapataito abitih i au tur eowen, ‘Orot yait Anunin nara’iy tafanamaim namara’at ina’i’itin, i boro Anun Kakafiyinamaim bapataito nitih.’”
34 Ine ndaona ndipo ndikuchitira umboni kuti uyu ndi Mwana wa Mulungu.”
34 John eo, “Ayu aitinika naatu ao’orereb iti i God Natun.”
35 Pa tsiku lotsatira Yohane analinso pamenepo pamodzi ndi awiri a ophunzira ake.
35 Ana martot John iban maiye ana bai’ufununayah orot rou’ab bairi hina efan ta’imonamaim hibatabat.
36 Iye ataona Yesu akudutsa anati, “Taonani Mwana Wankhosa wa Mulungu!”
36 Naatu Jesu na natabirih inan i’itin anamaramaim, John eo, “God ana Lamb enan kwa’itin!”
37 Ophunzira ake awiriwo atamva iye akunena izi, iwo anamutsatira Yesu.
37 Anamaramaim bai’ufununayah orot rou’ab iti hinonowar, i hairi Jesu hi’ufunun.
38 Atatembenuka, Yesu anaona iwo akumutsatira ndipo anawafunsa kuti, “Kodi mukufuna chiyani?”
38 Jesu nunutabir, orot rou’ab hibi’ufunun itih naatu ibatiyih, “Kwa abistan kwakokok?”
39 Iye anayankha kuti, “Bwerani mudzaone.”
39 I iya’afutih eo, “Kwanatan, kwa taiyuw efan kwa’itin.”
40 Andreya mʼbale wake wa Simoni Petro, anali mmodzi wa awiriwo amene anamva zimene Yohane ananena ndiponso amene anamutsata Yesu.
40 John abistan eo’o orot rou’ab hinowar Jesu hibi’ufunun orot ta i Andrew, Simon Peter tain
41 Choncho chimene Andreya anachita ndi kukapeza mʼbale wake Simoni ndipo anamuwuza kuti, “Ife tamupeza Mesiya,” (kutanthauza kuti Khristu).
41 Andrew Jesu bihamiy ufunamaim wantoro’ot i tuwah Simon nuwih, naatu tita’ur ana tur eowen, “Ayu i Roubininenayan atita’ur, nati i Keriso.”
42 Kenaka iye anabweretsa Simoni kwa Yesu, amene anamuyangʼana ndipo anati, “Iwe ndiwe Simoni, mwana wa Yohane. Udzatchedwa Kefa” (limene litanthauza kuti Petro).
42 Naatu Andrew tuwah Simon nawiy in Jesu biyan tit.
43 Pa tsiku lotsatira Yesu anaganiza zopita ku Galileya. Atamupeza Filipo, anati kwa iye, “Nditsate.”
43 Ana marto, Jesu au Galilee namih bobogaigiwas, Philip tita’ur naatu iu, “Kuna kwi’ufnunu tan.”
44 Filipo monga Andreya ndi Petro, anali wochokera ku mzinda mudzi Betisaida.
44 Philip ana tafaram i Betsaida, Andrew tuwah Peter bairi hai bar merar ta’imon.
45 Filipo anakapeza Natanieli ndipo anamuwuza kuti, “Ife tapeza amene Mose analemba za Iye mʼmalamulo, ndi zimene aneneri analembanso za Iye, Yesu wa ku Nazareti, mwana wa Yosefe.”
45 Philip na Nathanael tita’ur naatu iu, “Iti orot isan Moses Buka Atamaninamaim eo kikirum naatu dinab oro’orot auman hikikirum i boun atita’ur, iti orot tamah i Joseph ana bar ana merar i Nazareth.”
46 Natanieli anafunsa kuti, “Nazareti! Kodi kanthu kalikonse kabwino kangachokere kumeneko?”
46 “Nazareth! Sawar gewasin ta boro imaim namatar?” Nathanael ibat.
47 Yesu atamuona Natanieli akuyandikira, anati kwa iye, “Uyu ndi Mwisraeli weniweni, mwa iye mulibe chinyengo.”
47 Anamaramaim Jesu nuw Nathanael nan itin, isan eo, “I turobe Israel mowan, i orot ana yawas gewasin men baifufuwenayan.”
48 Natanieli anafunsa kuti, “Kodi mwandidziwa bwanji?”
48 Nathanael ibatiy, “O mi’itube ayu isu’ubu?”
49 Kenaka Natanieli ananena kuti, “Rabi, Inu ndinu Mwana wa Mulungu; Inu ndinu Mfumu ya Israeli.”
49 Imaibo Nathanael eorereb eo, “Rabbi, Bai’obaiyenayan o i God Natun! o i Israel hai Aiwob.”
50 Yesu anati, “Ukukhulupirira chifukwa chakuti ndakuwuza kuti Ine ndinakuona iwe uli pansi pamtengo wamkuyu? Iwe udzaona zinthu zazikulu kuposa izo.”
50 Jesu eo, “O i tumatum anayabin ayu a tur aowen o i ai fig an ima’am ait. O boro sawar gagamihika ina’itan men iti i’i’itin na’atube.”
51 Ndipo Iye anapitirira kuti, “Zoonadi, Ine ndikuwuza kuti iwe udzaona kumwamba, kutatsekuka ndi angelo a Mulungu akukwera ndi kutsika pa Mwana wa Munthu.”
51 Tur tafan ya’abar maiye eo, “Turobe a tur ao’owen, kwa boro mar ana etawan nabotawiy, naatu God ana tounamatar Orot Natun biyanamaim hinayen hinarara’iy kwana’itih.”
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar João 1, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.