João 19
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Kenaka Pilato anatenga Yesu namukwapula mwankhanza.
1 Naatu Pilate ma’utenayah uwih, Jesu hibai hibowabiwabir sawar.
2 Asilikali analuka nkhata yaminga ndi kumuveka pamutu pake. Kenaka anamuveka mkanjo wapepo
2 imaibo ma’utenayah kokor hi’afuw hififin ana kowasimih ukwarin hiyoun, naatu faifuw wair hibai hi’osenawein,
3 ndipo ankapita kwa Iye mobwerezabwereza ndi kumanena kuti, “Moni mfumu ya Ayuda?” Ndipo amamumenya makofi.
3 naatu hiyen hin biyan hitit naatu hi’o, “Jew hai aiwob ma’ama’anin!” Naatu yumatanamaim hifafar.
4 Pilato anatulukanso ndipo anati kwa Ayuda, “Taonani, ine ndikumubweretsa kuti inu mudziwe kuti ine sindikupeza chifukwa chomuyimbira mlandu.”
4 Pilate ibanak tit maiye sabuw rou’ay isah eo, “Ayu iti orot kwa namaim abai atitit i anao kwanaso’ob, i biyanamaim ayu men kakafin ta atita’ur.”
5 Pamenepo Yesu anatuluka atavala nkhata yaminga ndi mkanjo wapepo ndipo Pilato anawawuza kuti, “Nayu munthu uja!”
5 Jesu ana kowas kokor ukwarin hiyow naatu ana waifuw wair hi’osenawein imaibo hibai hititit. Pilate sabuw isah eo, “Orotoban iti.”
6 Atangomuona Iye akulu a ansembe ndi akuluakulu ena anafuwula kuti, “Mpachikeni! Mpachikeni!”
6 Firis ukwarih naatu i ana sabuw ukwa’ukwarih bairi hinuw hi’i’itin anamaramaim hitarakouw hi’o, “ku’onaf, ku’onaf!”
7 Ayuda anayimirira nati, “Ife tili ndi lamulo, ndipo molingana ndi lamulolo, Iyeyu ayenera kuphedwa chifukwa akudzitcha kuti ndi Mwana wa Mulungu.”
7 Sabuw hiya’afut maiye hi’o, “Aki ai ofafar eo i boro namorob, anayabin i taiyuwin eorerereb God natun rauw eo.”
8 Pilato atamva zimenezi, anachita mantha kwambiri,
8 Pilate iti nonowar i ana bir ra’at,
9 ndipo anabwereranso mʼnyumba yaufumu. Iye anafunsa Yesu kuti, “Kodi umachokera kuti?” Koma Yesu sanayankhe.
9 matabir maiye bar wanawanan run naatu Jesu ibatiy, “O menane ina?” Baise Jesu men tur ta eomih.
10 Pilato anati, “Kodi ukukana kundiyankhula ine? Kodi sukuzindikira kuti ine ndili ndi mphamvu yokumasula ndiponso mphamvu yokupachika?”
10 Pilate Jesu isan eo, “O men kukokok tur ta ayu isou inao?” “Inaso’ob, ayu isou i fair ema’am boro o ana botaiti inatit o boro ana onafi.”
11 Yesu anayankha kuti, “Inu simukanakhala ndi mphamvu pa Ine akanapanda kukupatsani kumwamba. Nʼchifukwa chake amene wandipereka Ine kwa inu ndiye wochimwa kwambiri.”
11 Jesu iya’afut, “Iti fair ayu tafau’umaim ibai kuma’am, anayabin iti fair i God it. Imih orot yait ayu o isa yayabunu i bowabow kakafin gagamin maiyow bai.
12 Kuyambira pamenepo Pilato anayesa kuti amumasule Yesu, koma Ayuda anapitirira kufuwula kuti, “Ngati mumumasula munthuyu kuti apite, inu si bwenzi la Kaisara.”
12 Ana maramaim Pilate iti tur nonowar ef nuwet mi’itube Jesu tabotait isan. Baise rou’ay hitarakouw i matabir maiye run, “o nati orot inabobotait ana itinin o i men Caesar ana ofamih. O yait ta aiwob inararouw, o i Ceaser ana wosai orot”.
13 Pilato atamva zimenezi, iye anamutulutsa Yesu kunja ndi kukhala pansi pa mpando wa woweruza pamalo otchedwa Mwala Wowaka (umene pa Chiaramaiki ndi Gabata).
13 Pilate iti tur nonowar ana maramaim Jesu bai tit ufun efan wabin teo kabay ana’ubun imaim baibabatiyen ana ura ma’ama tafan mare (Hebrew tur i te’o Gabbatha).
14 Linali tsiku lokonzekera Sabata la Paska ndipo nthawi inali ora lachisanu ndi chimodzi masana.
14 Veya na bi’ouyit nati i Tar Nowaten ana hiyuw ana veya nanamaim Pilate sabuw isah eo. “Kwa a aiwob orot i iti”.
15 Koma iwo anafuwula kuti, “Choka nayeni! Choka nayeni! Mpachikeni!”
15 Hitarkoukuw hi’o, “kwa’asabun! kwa’asabun!” kwa’onaf! Pilate ibatiyih, “Kwakokok ayu a aiwob ana onaf?” Firis ukwa’ukwarih hiya’afut hi’o, “Aki ai aiwob i ta’imon maiyow, Caesar akisinamo”.
16 Pomaliza Pilato anamupereka kwa iwo kuti akapachikidwe. Choncho asilikali anamutenga Yesu.
16 Imaibo Pilate Jesu ya’abun i isah onafinamih hibai hin.
17 Atanyamula mtanda wake, anapita kumalo otchedwa “Malo a Bade” (mʼChiaramaiki amatchedwa Gologota).
17 Jesu tit ana onaf abar remor in ukwarih rarik ana efanamaim tit. (Hebrew fanahimaim Golgotha). Jesus ana koros eabar enan|alt="Jesus carrying cross" src="cn01833B.tif" size="col" loc="Jhn 19.17" copy="©1978 David C. Cook Publishing Co." ref="19.17"
18 Pamenepo iwo anamupachika Iye pamodzi ndi anthu ena awiri, mmodzi mbali ina ndi wina mbali inanso ndipo Yesu pakati.
18 Nati’imaim hi’onafen, naatu orot rou’ab auman, Jesu foun in, orot rou’ab roun roun hi’in.
19 Pilato analemba chikwangwani chomwe anachikhoma pa mtandapo. Panalembedwa mawu akuti, yesu wa ku nazareti, mfumu ya ayuda.
19 Pilate fef kirum naatu onafamaim hidudun, Kikirum i JESU NASARETH OROT, JEWS HAI AIWOB.
20 Ayuda ambiri anawerenga chikwangwanichi, pakuti pamalo pamene Yesu anapachikidwapo panali pafupi ndi mzinda ndipo chikwangwanicho chinalembedwa mu Chiaramaiki, Chilatini ndi Chigriki.
20 Sabuw moumurih maiyow iti kikirum hi’itin hiyab, anayabin efan iti Jesu hio’onaf i men yokomih bar merar gagamin sisibin. Iti tur i Hebrew, Latin naatu Greekamaim kirum.
21 Kenaka mkulu wa ansembe wa Ayuda anakadandaula kwa Pilato nati, “Musalembe kuti ‘Mfumu ya Ayuda,’ koma kuti munthuyu amadzitcha kuti ndi mfumu ya Ayuda.”
21 Firis ukwarih, Pilate isan hio, “Jew hai aiwob bikirumin, i eo i Jew hai aiwob.”
22 Pilato anayankha kuti, “Chimene ine ndalemba, ndalemba.”
22 Pilate iya’afut, “Abistan ayu akikirum, i kirum.”
23 Asilikali atamupachika Yesu, anatenga zovala zake ndi kuzigawa zigawo zinayi, gawo limodzi la aliyense wa iwo, ndi kutsala mwinjiro wamʼkati wokha. Chovala ichi chinawombedwa kuyambira pamwamba mpaka pansi wopanda msoko.
23 Rakit wairafih Jesu hio’onaf ufunamaim ana waifuw hibow hiyarouseben matah kwafe’en himatar, matah taita’imon hiya, rakit wairafih taita’imon isah. Naatu faifuw tafan ebiyoun aurin sakisakir en auman hibai.
24 Iwo anati kwa wina ndi mnzake, “Tiyeni tisachingʼambe koma tichite maere kuti tione amene achitenge.”
24 Rakit sabuw taiyuwih isah hio, “Men tanasib baise tani’arow tana’itin yait boro nab.” Iti mamatar i tur marasika hio hikirum inu’in i titurobe isan.
25 Pafupi ndi mtanda wa Yesu panayima amayi ake, mngʼono wa amayi ake, Mariya mkazi wa Kaliyopa ndi Mariya wa ku Magadala.
25 Jesu ana onaf anamaim i hinah batabat, naatu i hinah rubun, Mary Clopas aawan naatu Mary Magdalin.
26 Yesu ataona amayi ake pamenepo ndi wophunzira amene Iye anamukonda atayima pafupipo, Iye anati kwa amayi ake, “Amayi nayu mwana wanu.”
26 Jesu hinah naatu ana bai’ufununayan orot i ana yabow hairi hibatabat itih, imih hinah isan eo, “Natu ina’itin.”
27 Anawuzanso wophunzirayo kuti, “Nawa amayi ako.” Kuyambira nthawi imeneyo, wophunzirayo anatenga amayiwo kupita nawo kwawo.
27 Naatu bai’ufununayan orot isan eo, “Hinat ina’itin”. Nati ana veya’amaim bai’ufununayan orot hinah bai hairi hin ana baremaim hima.
28 Atadziwa kuti zonse zatha tsopano komanso kuti malemba akwaniritsidwe, Yesu anati, “Ine ndili ndi ludzu.”
28 Jesu so’ob bounabo sawar etei’imak na ana yomanin tit, marasika Buk Atamaninamaim hikirum inu’in na iturobe. Jesu eo “Ayu sikou mamah.”
29 Pomwepo panali mtsuko wodzaza ndi vinyo wosasa, choncho iwo ananyika chinkhupule ndi kuchisomeka ku mtengo wa hisope nachifikitsa kukamwa kwa Yesu.
29 Tew ta nati’imaim harew tenakuyakuy awan karatan batabat, wanabir hibai harew hibu’utu’ub isikar wan himetan hi’otra’ah Jesu ufurinamaim hiyei.
30 Yesu atalandira chakumwachi anati, “Kwatha.” Ndipo Iye anaweramitsa mutu wake napereka mzimu wake.
30 Jesu harew kartoman naatu eo, “Iti’imaim sawar.” Imaibo sikan sir naatu ayubin tabaratait.
31 Popeza linali Tsiku Lokonzekera ndipo tsiku linalo linali Sabata lapadera; Ayuda sanafune kuti mitembo ikhale pa mtanda pa Sabata, iwo anapempha Pilato kuti akathyole miyendo ndi kutsitsa mitemboyo.
31 Jew ukwa’ukwarih Pilate hifefeyan baibasit baitih orot hio’onafih ah tarkakakiren isan, naatu biyah onaf afe’enane bow yara’iyen isan. Hifefeyan anayabin ana mar natot i Baiyarir Ana Veya. I men hikok biyah boro auyom hita’in.
32 Chifukwa chake asilikali anabwera ndi kuthyola miyendo ya munthu oyamba amene anapachikidwa ndi Yesu ndipo kenaka ya winayo.
32 Imih baiyowayah hin orot ta wan an hitarkakiren naatu hin orot bairu’abin an hitar kakiren, iti orot hairi i Jesu bairi hio’onafih.
33 Koma atafika pa Yesu ndi kupeza kuti anali atamwalira kale, iwo sanathyole miyendo yake.
33 Baise hina Jesu biyan hititit i moroboka inu’in hi’itin, isan imih an men hitarkakiren.
34 Mʼmalo mwake, mmodzi wa asilikaliwo anamubaya Yesu ndi mkondo mʼnthiti, ndipo nthawi yomweyo munatuluka magazi ndi madzi.
34 An hitatakakiren efanin sorodiy kiram robra’at Jesu naiwan yi naatu mar ta’imon rara naatu harew auman suwa re.
35 Munthu amene anaona izi wapereka umboni ndipo umboni wake ndi woona. Iye akudziwa kuti akunena choonadi kuti inunso mukhulupirire.
35 Orot iti matar i’itin i eo’orereb, naatu anaorerereb i turobe. I so’ob abistan eo i turobe, isan imih kwa auman kwana’itin kwanitumatum.
36 Zinthu izi zinachitika kuti malemba akwaniritsidwe: “Palibe limodzi la mafupa limene lidzathyoledwa,”
36 Iti na’atube matar saise abisa Buk Atamaninamaim hikikirum na iturobe. “Boro men ana rarik ta natato’ob.”
37 ndi monga lemba linanso linena, “Iwo adzayangʼana Iye amene iwo anamubaya.”
37 Tur tabo Buk Atamaninamaim eo, “Sabuw boro hinanuw nati hiyiy hina’itin.”
38 Kenaka, Yosefe wa ku Arimateyu anakapempha mtembo wa Yesu kwa Pilato. Tsono Yosefe anali wophunzira wa Yesu koma mobisa chifukwa iye ankaopa Ayuda. Atalandira chilolezo kwa Pilato, anakatsitsa mtembo wa Yesu.
38 Iti ufunamaim Joseph Arimathea orot, Jesu ana bai’ufununayan ta wa’iwa’iramaim na Pilate ifefeyan Jesu biyan tab isan. Anayabin Jew hai ukwarih isah bir. Pilate ana baibasitamaim, Joseph na Jesu biyan bai yare.
39 Nekodimo, munthu amene poyamba pake anabwera kwa Yesu usiku, anatenga mafuta osakaniza ndi mure ndi aloe wolemera pafupifupi makilogalamu 32.
39 Nicodemus gugumin ta i wan in Jesu i’itin, i boun raiy ta wabin myrrh naatu raiy ta wabin aloes auman higagamuw ana bit i 30 kilos bai na Joseph hairi hin.
40 Pamenepo anatenga mtembo wa Yesu nawukulunga pamodzi ndi zonunkhiritsa mu nsalu za mtundu woyera monga mwa mwambo wa maliro wa Ayuda.
40 Orot hairi Jesu biyan hibu’ub hiyare naatu Jew hai bairahiya ana efamaim biyan raiyamaim hibobunei naatu rah ana faifuwamaim hisum.
41 Pamalo pamene anapachikidwa Yesu panali munda ndipo mʼmundamo munali manda atsopano mʼmene munali simunayikidwemo aliyense.
41 Efan menamaim Jesu momorob i sisibinamaim i masaw ta, naatu nati masaw wanawanan hub boubun men yait ta imaim hiyai.
42 Chifukwa linali Tsiku la Ayuda Lokonzekera ndi kuti mandawo anali pafupipo, iwo anayika Yesu mʼmenemo.
42 Iti ufunamaim i Baiyarir Ana Veya, anayabin hub i yubin, isan imih Jesu biyan hibai hin imaim hiyai.
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar João 19, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.