João 17
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Yesu atatha kunena izi, anayangʼana kumwamba ndipo anapemphera:
1 Jesu ana bai’ufununayah isah eo sasawar ufunamaim, au mar nuwra’at naatu yoyoban eo,
2 Pakuti Inu munamupatsa Iye ulamuliro pa anthu onse kuti apereke moyo wosatha kwa onse amene mwamupatsa.
2 Anayabin sabuw etei kaifih isan fair itin, saise sabuw iyab o ibitin etei boro yawas wanatowanin nitih.
3 Tsono moyo wosathawo ndi uwu: Iwo akudziweni Inu, Mulungu yekhayo woona, ndi Yesu Khristu, amene Inu mwamutuma.
3 Iti yawas wanatowan anayabin o su’ubi isan, o akisimo i turobe ana God, naatu Jesu Keriso ibiyafar i auman su’ubin isan.
4 Ine ndabweretsa ulemerero wanu pa dziko pamene ndamaliza ntchito imene munandipatsa kuti ndi igwire.
4 Iti tafaramamaim a fair ibitu sabuw ai’obaiyih hi’itin, naatu bowabow sinafumih ibitu etei abow aisawar.
5 Ndipo tsopano, Atate, ndilemekezeni Ine pamaso panu ndi ulemerero uja umene ndinali nawo kwa Inu dziko lapansi lisanayambe.
5 Tamai nati fair mar tafaram matara’e ana veya ayu itu airit tama’am boun i ayu kwitu maiye.”
6 “Ine ndawadziwitsa za Inu anthu amene munandipatsa mʼdziko lapansi. Iwo anali anu. Inu munawapereka kwa Ine ndipo amvera mawu anu.
6 “Iyabowat tafaramamaim hima hibowabow ibow ayu ibitu ai obaiyih o hisu’ubi sawar. Nati sabuw i o nowa ibow ayu itu, naatu o a tur hibosiyasiyar hibow.
7 Tsopano akudziwa kuti zonse zimene munandipatsa nʼzochokera kwa Inu.
7 Naatu bounabo sabuw hiso’ob, sawar ibow ayu ibitu etei o biyane hina.
8 Pakuti Ine ndiwapatsa mawu amene Inu munandipatsa ndipo awalandira. Iwo akudziwa ndithu kuti Ine ndinachokera kwa Inu, ndipo akukhulupirira kuti Inu ndiye amene munandituma Ine.
8 Tur ayu ibitu etei au bai’ufnunayah ao hinowar sawar naatu hibai hibukikin, hiso’ob i men baifuwenamih. Naatu hiso’ob hitumatum ayu o biyane iyafaru ana.
9 Ine ndikuwapempherera. Ine sindikupempherera dziko lapansi, koma anthu amene Inu mwandipatsa, pakuti ndi anu.
9 Ayu ibitu isah ayoyoyoban, men tafaram wanawanan sabuw tema’am isah ayoyoyobanamih baise iyabowat ayu ibitu i isah ayoyoyoban, anayabin nati sabuw i o nowa.
10 Zonse zimene Ine ndili nazo ndi zanu, ndipo zonse zimene Inu muli nazo ndi zanga. Choncho Ine ndalemekezedwa mwa iwowo.
10 Naatu abistanawat ayu biyau tema’am etei i o nowa naatu abistanawat o biya tema’am i ayu nowau, naatu ayu au fair bonamanamarin i bai’ufununayah biyahimaim irerereb sabuw hi’itin.
11 Ine sindikukhalanso mʼdziko lapansi nthawi yayitali, koma iwo akanali mʼdziko lapansi. Ine ndikubwera kwa Inu. Atate Woyera, atetezeni ndi mphamvu za dzina lanu. Dzina limene munandipatsa Ine, kuti iwo akhale amodzi monga Ife tili amodzi.
11 Naatu boun i ayu o isa anan, ayu boro men tafaramamaim anama maiye’emih, baise i boro tafaramamaim hinama. Tamai o i Kakafiyin o wab ana fairamaim inatarfafarih nati wab o ibitu’umaim saise hinan ta’imon hinamatar, boun o ayu airit ta’imon tama’am na’atube.
12 Pamene ndinali nawo, ndinawateteza ndi kuwasunga mosamala mʼdzina limene munandipatsa. Palibe ndi mmodzi yemwe amene anatayika kupatula yekhayo amene anayenera kuwonongeka kuti malemba akwaniritsidwe.
12 Ayu i bairi ama’am anamaramaim, o wab ayu ibitu imaim atafafarih akaifih gewas bairi ama. Men ta kasiyomih, baise orot ta’imonamo i bai’akir kakafin bai, saise abisa Buk Atamaninamaim hikikirum na iturobe.
13 “Tsopano ndikubwera kwa Inu. Ndikunena izi ndikanali mʼdziko lapansi, kuti iwo akhale ndi muyeso wodzaza wachimwemwe changa mʼkati mwawo.
13 Naatu ayu boun i o isa anan, iti tafaram wanawanan ama’am anamaramaim iti sawar etei isah aobo, saise ayu au yasisir tutufin i wanawanahimaim nakarsuwei.
14 Ine ndawapatsa mawu anu ndipo dziko lapansi likudana nawo, pakuti sali a dziko lapansi monga Ine sindilinso wa dziko lapansi.
14 Ayu a tur aitih, naatu tafaram kwahirih, anayabin i men tafaram nowanamih, boun ayu na’atube men iti tafaram nowanamih.
15 Sindikupempha kuti muwachotse mʼdziko lapansi koma kuti muwateteze kwa woyipayo.
15 Ayu au yoyoban i men au bai’ufununayah bosairih isan, baise ayu abifefeyani o wagabur kakafihine inatarfafarih.
16 Iwo si a dziko lapansi, monga Ine sindilinso wa dziko lapansi.
16 Ayu i men iti tafaram nowan, imih i auman men iti tafaram nowanamih.
17 Ayeretseni ndi choonadi chanu. Mawu anu ndiye choonadi.
17 O a turobe’emaim kweiwa’an uhew tematar, O a tur i turobe anababatun.
18 Monga Inu munandituma Ine mʼdziko lapansi, Inenso ndikuwatuma mʼdziko lapansi.
18 Ayu tafaram wanawanan aiyafarih hin boun ayu tafaram wanawanan i yafaru anan na’atube.
19 Chifukwa cha iwowa Ine ndikudziyeretsa, kuti iwo ayeretsedwenso kwenikweni.
19 I isah ayu taiyuwu aiwa’an uhew amatar, saise ibo auman o isa anababatun uhew hitamatar.
20 “Ine sindikupempherera iwo okhawa, komanso amene adzandikhulupirira chifukwa cha uthenga wawo.
20 “Ayu men i akisih isah ayoyoyobanamih, baise iyab i hai turamaim ayu isou tebitutumu i isah auman ayoyoyoban,
21 Ndikuwapempherera kuti onsewa akhale amodzi. Monga Inu Atate muli mwa Ine ndi Ine mwa Inu, iwonso akhale mwa Ife kuti dziko lapansi likhulupirire kuti Inu munandituma Ine.
21 saise i etei hinan ta’imon hinamatar. Tamai boun ayu wanawana’umaim kuma’am na’atube ayu o wanawanamaim anama. Karam i auman hitan wanawanatamaim hitama, saise tafaram hititumatum o i ayu iyafaru ana.
22 Ine ndawapatsa ulemerero umene munandipatsa Ine, kuti akhale amodzi monga Ife tili amodzi.
22 O a gewasin ayu ibitu, i aitih, saise i hinan ta’imon hinamatar, boun o ayu airit ta’imon tama’amabe.
23 Ine ndikhale mwa iwo ndipo Inu mwa Ine kuti umodzi wawo ukhale wangwiro. Choncho dziko lapansi lidzadziwa kuti Inu munandituma Ine ndipo Inu mwawakonda iwowa monga momwe Inu munandikondera Ine.
23 Ayu i wanawanahimaim naatu o ayu wanawana’umaim, saise i hinan anababatun ta’imon hinamatar. Saise tafaram boro naso’ob ayu i o iyafaru, naatu o i kubiyabuwih boun ayu kubiyabuwu na’atube.
24 “Atate, Ine ndikufuna kuti anthu amene mwandipatsa Ine adzakhale ndi Ine kumene kuli Ine, ndi kuona ulemerero wanga, ulemerero umene munandipatsa chifukwa Inu munandikonda dziko lapansi lisanalengedwe.
24 “Tamai iyab ayu ibitu i akokok menamaim ama’am bairi imaim anama, saise ayu au marakaw bonamanamarin hina’itin, nati marakaw bonamanamarin o ayu itu, anayabin o iyabuwu ufibo tafaram matar.
25 “Atate wolungama, ngakhale kuti dziko lapansi silikudziwani Inu, Ine ndimakudziwani, ndipo iwo amadziwa kuti Inu munandituma Ine.
25 “Tamai mokob maiyow; sabuw iti tafaramamaim o men hisu’ubi, baise ayu wan asu’ubi, naatu etei hiso’ob ayu i o iyafaru ana.
26 Ine ndawadziwitsa dzina lanu, ndipo ndidzapitiriza kuwadziwitsa dzina lanulo, kuti chikondi chomwe munandikonda nacho chikhale mwa iwo, ndipo Ine mwa iwo.”
26 O isa ayu aorereb hinowar sawar, naatu ayu boro’ika boro o isa anao’rerereb saise yabow nati ayu ibitu i wanawanahimaim nama naatu ayu taiyuwu i wanawanahimaim anama.”
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar João 17, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.