João 16

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI

Sair da comparação
AAI TUR GEWASIN O BAIBASIT BOUBUN
1 “Ine ndakuwuzani zonsezi kuti musadzakhumudwe.
1 “Sawar etei’imak i ao kwanowar sawar, saise kwa boro men ef kwanarukasiy.
2 Iwo adzakuchotsani mʼsunagoge mwawo. Kunena zoona, nthawi ikubwera imene aliyense amene adzakuphani adzaganiza kuti akutumikira Mulungu.
2 Jew hai Kou’ay Bar wanawanan boro hinanuni ufun kwanatit, veya nanan anamaramaim o yait ta na’a’asbuni, i boro asir nanot God ana sibor eya’iy narouw.
3 Iwo adzachita zoterozo chifukwa sanadziwe Atate kapena Inenso.
3 Sabuw boro kakafin isa hinasinaf, anayabin Tamat men hisu’ub naatu ayu auman men hisu’ubu.
4 Ine ndakuwuzani izi kuti nthawi ikadzafika mudzakumbukire kuti Ine ndinakuchenjezani kale. Ine sindinakuwuzeni izi poyamba paja chifukwa ndinali nanu.”
4 Ayu kwa a tur ao’owen, saise ana veya nanan kwa boro kwananot ayu i ai’matnuwi sawar, anayabin ayu kwa bairit tama’am isan, men saise a tur aowenamih.
5 “Tsopano Ine ndikupita kwa Iye amene anandituma koma palibe wina mwa inu akundifunsa kuti, ‘Kodi mukupita kuti?’
5 “Boun ayu amatabir maiye anan, yait ayu iyunu anan i biyan anatit, naatu men yait ta ayu ibatiyu’umih, ‘O menika kwenan’
6 Muli ndi chisoni kwambiri chifukwa ndakuwuzani zimene.
6 Anayabin ayu tur iti ao isan, kwa yababan yen bufuti.
7 Komatu ndakuwuzani zoona. Ine ndikuti kuli bwino kwa inu kuti ndichoke. Ngati sindichoka, Nkhosweyo sidzabwera kwa inu, koma ngati Ine ndipita, ndidzamutumiza kwa inu.
7 Baise turobe a tur ao’owen. Iti i kwa a gewasin isan ayu amamatabir maiye. Ayu men ananan na’at, Baibaisayan boro men nan, baise ayu ananan i boro aniyun nan kwa isa.
8 Iye akabwera, adzatsutsa dziko lapansi za uchimo, zachilungamo ndi zachiweruzo.
8 I nanan ana maramaim sabuw iti tafaram ana kakafinamaim hima tesisinaf nabotabirih hinan yawas roumutuforen hinab naatu God ana baibabatiyen saise hinaso’ob gewas.
9 Za uchimo, chifukwa anthu sakhulupirira Ine.
9 sabuw ayu men tebitutumu anayabin i kakafin wanawanan tema’am;
10 Za chilungamo, chifukwa Ine ndi kupita kwa Atate, kumene simudzandionanso.
10 naatu tenotanot roumutufuren i kakafin terarouw, anayabin ayu anan Tamai biyan, naatu boro men kwana’itu maiye;
11 Za chiweruzo, chifukwa wolamulira dziko lino lapansi waweruzidwa tsopano.
11 naatu baibabatiyen i boro nan, anayabin God marasika iti tafaram ana kaifenayan i ibabatiy sawar.
12 “Ine ndili ndi zambiri zoti ndiyankhule nanu, koma simungathe kuzilandira tsopano.
12 “Ayu auru tur moumurin maiyow boro atao kwatanowar, baise boun kwa isa ana’o boro men naniyan kwanab.
13 Koma pamene Iye, Mzimu wachoonadi, abwera, adzakutsogolerani mʼchoonadi chonse. Iye sadzayankhula mwa Iye yekha, adzayankhula zokhazo zimene wamva ndipo Iye adzakuwuzani zimene zikubwera.
13 Baise anamaramaim turobe ana Anun Kakafiyin nanan, i Boro turobe ana ef etei nabonawiyi. I boro men taiyuwin ana notamaim na’omih, abistanawat enonowar i akisinamo nao, naatu sawar uf hinamamatar isan boro a tur na’owen.
14 Iye adzalemekeza Ine chifukwa adzatenga za Ine nadzakudziwitsani.
14 Ayu boro nabora’ara’ahu, anayabin ayu au tur biyau’une bai na kwa a tur eo’owen isan.
15 Zonse za Atate ndi zanga. Ichi nʼchifukwa chake Ine ndanena kuti Mzimu Woyera adzatenga kwa Ine zanga kuti muzidziwe.”
15 Sawar etei ayu Tamai biyan tema’am i ayu nowau naatu abistan ayu biyau ema’am boro Anun Kakafiyin nab nan niwa’an kwa isa nirerereb, anayabin iti isan kwa a tur ao’owen.
16 Yesu anapitiriza kuyankhula kuti, “Mwa kanthawi kochepa, simudzandionanso, ndipo patatha nthawi pangʼono mudzandionanso.”
16 “Mar kikimin kwa boro men ayu kwana’itu naatu mar kafai kikimin kwa boro ayu kwana’itu.
17 Ena a ophunzira ake anati kwa wina ndi mnzake, “Kodi Iye akutanthauza chiyani ponena kuti, ‘Mwa kanthawi kochepa, simudzandionanso,’ ndi ‘ndipo patatha nthawi pangʼono mudzandionanso,’ ndiponso ‘chifukwa ndikupita kwa Atate?’ ”
17 Ana bai’ufununayah afa taiyuwih hima hibabatiyih? “Anayabin abistan isan i tur iti na’atube eo, ‘Mar kikimin kwa boro men kwana’itu, naatu mar kafai ufunamaim ayu boro kwana’itu’ naatu ‘Anayabin ayu anan Tamai biyan?’
18 Iwo anapitiriza kufunsana kuti, “Kodi akutanthauza chiyani, ‘kanthawi kochepa?’ Ife sitikumvetsetsa chimene Iye akuyankhula.”
18 Naatu i hima hi’o hibabatiyih, Iti anayabin nam abisa isan eo’o, ‘Iti mar kikimin?’ Aki men aso’ob i abistan eo’o.”
19 Yesu anadziwa kuti ankafuna kuti amufunse za zimenezi, choncho anawafunsa kuti, “Kodi mukufunsana wina ndi mnzake chimene Ine ndimatanthauza pamene ndinati, ‘Mwa kanthawi kochepa simudzandionanso,’ ndi ‘patatha nthawi pangʼono mudzandionanso?’
19 Jesu itih so’ob iti isan boro hinibatiy, imih i isah eo, “Ayu iti tur ao isan kwa tayuwiwat kwama kwabibabatiyi anayabin isan, anamaramaim ayu iti na’at ao, ‘Mar kikimin ayu boro men kwana’itu, naatu mar kafai ufunamaim ayu boro kwana’itu.’
20 Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti inu mudzalira ndi kubuma pomwe dziko lapansi lidzakhale likukondwera. Inu mudzamva chisoni, koma chisoni chanu chidzasandulika chimwemwe.
20 Ayu anababatun a tur ao’owen, Kwa boro kwanarererey naatu kwanigagamat baise tafaram naben nakawasa. Kwa boro kwaniyababan, baise kwa a yababan boro nabotabir yasisir namatar.
21 Mayi akamabereka mwana amamva ululu chifukwa nthawi yake yafika; koma mwana wake akabadwa amayiwala ululu wake chifukwa cha chimwemwe chake chakuti mwana wabadwa mʼdziko lapansi.
21 Babin anatoub ana veya nakabom ebiyababan na’atube anayabin biyababan ana veya i na kabom; baise anamaramaim kek tufuw, i ana biyababan inatbuhuruw anayabin kek tafaramamaim tufuw i ebiyasisir.
22 Chimodzimodzinso ndi inu. Tsopano ino ndi nthawi yanu yomva chisoni, koma Ine ndidzakuonaninso ndipo inu mudzasangalala, ndipo palibe amene adzachotsa chimwemwe chanu.
22 Imih kwa auman. Boun i kwa a veya kwaniyababan, baise ayu boro kwa ana’iti maiye naatu kwaniyasisir naatu men karam yait ta kwa a yasisir biyane nabosair.
23 Tsiku limenelo inu simudzandipemphanso kalikonse. Ine ndikukuwuzani zoona kuti Atate anga adzakupatsani chilichonse chimene mudzapempha mʼdzina langa.
23 Nati anamaramaim o men yait ta ayu isou sawaramih inafefeyan. Tur anababatun a tur ao’owen, sawar abistan isan ayu wabu’umaim inabifefeyan, ayu Tamai boro nit.
24 Mpaka tsopano simunapemphe kalikonse mʼdzina langa. Pemphani ndipo mudzalandira, ndipo chimwemwe chanu chidzakhala chathunthu.
24 Marasika na iti boun kwa men yait ta iti na’atube ayu wabu’umaim fefeyanamih. Boun kwanafefeyan, naatu kwa boro kwanab, naatu kwa boro mar etei yasisiramaim kwanama.
25 “Ngakhale ndakhala ndikuyankhula mʼmafanizo, nthawi ikubwera imene Ine sindidzagwiritsanso ntchito mafanizo otere koma ndidzakuwuzani momveka za Atate anga.
25 “Ayu mar etei kawen turamaim ao kwanowar sawar, mar i enan ayu boro men kafa’imo kawen turamaim anao, baise ayu Tamai isan i boro mutufor bebeyanamaim anao kwananowar,
26 Tsiku limenelo inu mudzapempha mʼdzina langa. Ine sindikunena kuti ndidzapempha Atate mʼmalo mwanu ayi.
26 Nati ana veya’amaim kwa boro ayu wabu’umaim kwanafefeyan. Ayu ao i men kwa au kou anabat Tamai anifefeyanimih.
27 Atate mwini anakukondani chifukwa inu mwandikonda Ine ndipo mwakhulupirira kuti Ine ndinabwera kuchokera kwa Atate.
27 Aiyabin, Tamai i taiyuwin kwa isa ebiyabow, anayabin kwa ayu isou kwabiyabow naatu kwabitumatum ayu i God iyafaru ana.
28 Ine ndinabwera kuchokera kwa Atate ndi kulowa mʼdziko lapansi. Tsopano ndikulisiya dziko lapansi kubwerera kwa Atate.”
28 Ayu Tamai iyafaru ana, tafaram wanawanan arun abow aremor, boun ayu tafaram abihamiy naatu anan Tamai biyan.
29 Kenaka ophunzira ake anati, “Tsopano mukuyankhula momveka bwino ndi mopanda mafanizo.
29 Naatu Jesu ana bai’ufununayah hi’o, “Bounabo tur bebeyanamaim ku’o’o naatu men kawenamaim ku’o’omih.
30 Tsopano ife tikuona kuti Inu mumadziwa zinthu zonse ndi kuti sipafunika wina aliyense kukufunsani. Mwa ichi ife takhulupirira kuti Inu munachokera kwa Mulungu.”
30 Bounabo aki mataito’iwa’an a’i’itin o sawar etei i so’ob, naatu o men yait ta kukokok boro o isa baibat nabow natit. Aki iti’imaim i’obaiyi abitumatum o i Godane ina.”
31 Yesu anawafunsa kuti, “Kodi tsopano mwakhulupirira?”
31 Jesu iyafutih eo, “Kwa bounabo kwabitumatum?”
32 Koma nthawi ikubwera ndipo yafika, pamene inu mudzabalalitsidwa, aliyense ku nyumba yake. Inu mudzandisiya ndekhandekha. Koma Ine sindili ndekha, pakuti Atate anga ali nane.
32 “Baise veya i enan, naatu na titaka, anamaramaim kwa boro na’abargiyi taiyuw a bar a merar na’at kwanabihir. Ayu boro kwanihamiyu nakutatabu ana bat. Baise ayu men akisu anayabin Tamai ayu airi ama’am.
33 “Ine ndakuwuzani izi kuti mwa Ine mukhale nawo mtendere. Mʼdziko lapansi mudzakhala nawo mavuto. Koma limbikani mtima! Ine ndaligonjetsa dziko lapansi.”
33 “Ayu sawar etei ao kwanowaraka, saise ayu wanawana’umaim kwanama’am kwa karam boro tufuwamaim kwanama. Iti tafaramamaim kwa boro yare wanawanan kwanarun kwani’akir. Baise kwanafair kwanabat! Ayu Tafaram aigegesair.”

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar João 16, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.