João 15

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI

Sair da comparação
AAI TUR GEWASIN O BAIBASIT BOUBUN
1 “Ine ndine mpesa weniweni, ndipo Atate anga ndiye mwini munda.
1 “Ayu i ai an anababatun, naatu Tamai i masaw Matuwan.
2 Iye amadula nthambi iliyonse ya mwa Ine imene sibala chipatso, koma nthambi iliyonse imene imabala chipatso amayisadzira bwino kuti ibale zipatso zambiri.
2 Ayu famufamu ro’oro’on men ebiw gewas boro na’afuw nisaroun, naatu ro’oro’on ebiw gewas boro famufamu natobubunei saise ro’o’ro’on moumurihika niw naya.
3 Inu ndinu oyera kale chifukwa cha mawu amene ndayankhula inu.
3 Kwa i marasika kwaigewasin sawar, anayabin ayu turamaim ao kwanowar sawar.
4 Khalani mwa Ine, monga Ine ndili mwa inu. Palibe nthambi imene ingabereke chipatso pa yokha ngati sinalumikizike ku mpesa. Chomwechonso inu simungathe kubereka chipatso pokhapokha mutakhala mwa Ine.
4 Wanawana’umaim kwanitubonen kwanama, naatu ayu kwa wanawanamaim anitubonen anama. Famen akisin men karam taiyuwin niw ro’on nayai, baise i boro ai naiwan nituw. Ef ta’imon kwa ayu wanawanau kwanitubonen boro ro’oro’o moumurihika kwanaya.
5 “Ine ndine mpesa; inu ndinu nthambi zake. Ngati munthu akhala mwa Ine ndi Ine mwa iye, adzabereka zipatso zambiri; popanda Ine simungathe kuchita kanthu.
5 “Ayu i ai, naatu kwa i ai famefamen, o yait ayu wanawana’umaim inabituwabon naatu ayu o wanawananamaim anabituwabon, i boro ro’oro’o moumurihika naya; anayabin, o akis men karam boro inasinaf namatar.
6 Ngati wina aliyense sakhala mwa Ine, iyeyo ali ngati nthambi imene yatayidwa ndi kufota. Nthambi zotero zimatoledwa, kuponyedwa pa moto ndi kupsa.
6 O yait ta ayu airit men tanibitubonen na’at, i boun ai famefamen hituw batabat kekerer na’atube, nati boro hina’o’on wairaf wan hinaroura’aten hinikubaren hina’arat.
7 Ngati inu mukhala mwa Ine ndipo mawu anga akhala mwa inu, pemphani chilichonse chimene mukufuna ndipo mudzapatsidwa.
7 O yait ayu wanawana’umaim inabitubonen naatu ayu au tur o wanawanamaim nabitubonen na’at, o a kok abistan isan kufefefeyan o boro anit.
8 Atate anga amalemekezedwa mukamabereka zipatso zochuluka, ndipo potero mudzionetsa kuti ndinu ophunzira anga.
8 Kwa ro’oro’o moumurihika kwanaya’ay kwa boro taiyuw kwana’inani, kwa i ayu au bai’ufununayah naatu Tamai ana gewasin boro sabuw kwani’obaiyih.
9 “Monga momwe Atate amandikondera Ine, Inenso ndakukondani. Tsopano khalani mʼchikondi changa.
9 Tamai ebiyabuwu na’atube; kwa abiyabuwi. Au yabowamaim kwanitubonen kwanama.
10 Ngati mumvera malamulo anga, mudzakhala mʼchikondi changa, monga Ine ndimamvera malamulo a Atate anga, ndipo ndimakhala mʼchikondi chawo.
10 Kwa ayu ou’obaiyunen tur kwanabobosiyasiyar na’at, boro ayu au yabowamaim kwanitubonen kwanama, boun ayu Tamai ana’obaiyunen tur abosiyasiyar naatu i ana yabowamaim aitubonen ama’am na’atube.
11 Ine ndakuwuzani izi kuti chimwemwe changa chikhale mwa Inu, kuti chimwemwe chanu chikhale chokwanira.
11 “Ayu a tur aowen kwanowar sawar saise au yasisir kwa wanawanamaim nama, naatu kwa mar etei yasisiramaim kwanama.
12 Lamulo langa ndi ili: ‘Kondanani wina ndi mnzake monga Ine ndakonda inu.’
12 Ayu au obaiyunen tur i iti. Turanah bairi kwaniyabowbonen, ayu kwa abiyabuwi na’atube.
13 Palibe munthu ali ndi chikondi choposa ichi, choti munthu nʼkutaya moyo wake chifukwa cha abwenzi ake.
13 Yait ta ana ofonah isah namomorob na’at, nati ebi’obaiy i ana yabow ra’at kwanekwan.
14 Inu ndinu abwenzi anga ngati muchita zimene Ine ndikulamulani.
14 Ayu obaiyunen tur abistan sinaf isan ou’uwi, i kwanasisinaf na’at, kwa i ayu au ofonah.
15 Ine sindikutchulaninso antchito, chifukwa wantchito sadziwa zimene bwana wake akuchita. Mʼmalo mwake Ine ndakutchani abwenzi pakuti zilizonse zimene ndinaphunzira kwa Atate, Ine ndakudziwitsani.
15 Ayu boro men kafa’imo kwa isa akir anarouw ana’af, anayabin akir orot i men so’ob ana orot ukwarin abistan esisinaf. Nati efanin ayu kwa isa au ofonah arouw ao’o, anayabin ayu Tamai biyanane tur abistanawat anonowar etei’imak a tur aowen kwanowar sawar.
16 Inu simunandisankhe Ine, koma Ine ndinakusankhani kuti mupite ndi kukabereka zipatso, zipatso zake za nthawi yayitali. Choncho Atate adzakupatsani chilichonse chimene mudzapempha mʼdzina langa.
16 Kwa men ayu kwarubinu, ayu kwa arubini naatu atarbaiyuni kwanatit kwanan kwaniw ro’oro moumurihika kwanaya–nati ro’o’ro’on boro men hinamun. Naatu abistan isan ayu wabu’umaim kwafefefeyan Tamai boro nit.
17 Lamulo langa ndi ili: ‘Muzikondana.’
17 Iti i ayu ou’obaiyunen tur. Turanah bairi kwaniyabowbonen.
18 “Ngati dziko lapansi lidana nanu, dziwani kuti linayamba kudana ndi Ine.
18 “Kwa sabuw hinabifutuwi na’at, kwa kwanaso’ob nati ayu wan ifutuwu’ubo kwa uf ifutuw.
19 Inu mukanakhala anthu a dziko lapansi, dziko lapansi likanakukondani ngati anthu ake omwe. Koma mmene zilili, inu si anthu a dziko lapansi. Ine ndakusankhani kuchokera mʼdziko lapansi, nʼchifukwa chake dziko lapansi limakudani.
19 Kwa tafaram nowan kwanama’am na’at, tafaram boro niyabuwi nowan na’atube kwanamatar kwanama, kwa i men iti tafaram nowan, baise kwa tafaramane arubini abotaiti kwatit. Nati isan tafaram kwa ebifutuwi.
20 Kumbukirani mawu amene ndinayankhula nanu akuti, ‘Palibe wantchito amene amaposa bwana wake.’ Ngati anandizunza Ine, iwo adzakuzunzaninso inu. Ngati anamvera chiphunzitso changa, iwo adzamvera chanunso.
20 Iti tur kwa isa ao’o i a notamaim nama. ‘Orot ana bowayan i men ra’at ana orot ukwarin natabirimih.’ Kwa hinarabi hinabi’a’afiyi na’at, ayu auman hirabu tibi’afiyu. Ayu au bai’obaiyen hinabobosiyasiyar na’at, kwa auman boro hinabosiyasiyari.
21 Iwo adzakuchitani zimenezi chifukwa cha dzina langa, popeza sakudziwa amene anandituma Ine.
21 Ayu wabu isan, kwa isa boro iti na’atube hinamatar. anayabin i men hiso’ob yait ayu iyunu ana.
22 Ine ndikanapanda kubwera ndi kuyankhula nawo, sakanakhala ndi mlandu. Koma tsopano alibe choti nʼkukanira mlandu wawo.
22 Ayu men atan biyah atatit naatu tur gewasin men atao hitanonowar na’at, kakafin isan boro men ubar hitabaimih; baise boun boro men hai kakafin isan hinifufuwenamih.
23 Iye amene amadana ndi Ine amadananso Atate anga.
23 Yait ayu ebifutuwu Tamai auman i ebifutuw.
24 Ine ndikanapanda kuchita pakati pawo zinthu zimene wina aliyense sanachitepo, iwo sakanakhala ochimwa. Koma tsopano aona zodabwitsa izi, komabe akundida Ine pamodzi ndi Atate anga.
24 Ayu wanawanahimaim asisinaf men yait ta sisinaf na’atube asinafumih, imih i boro men kakafin hitasinaf. Baise boun ina’inan hi’itah, naatu ayu Tamai airi’ika hikwahiri.
25 Koma zatere kuti zikwaniritse zimene zinalembedwa mʼmalamulo awo: ‘Iwo anandida Ine popanda chifukwa.’
25 Baise iti mamatar, i abistanawat hai ofafaramaim hi’o hikikirum i na iturobe, Anayabin en ayu hifutuwu.
26 “Nkhoswe ikadzabwera imene Ine ndidzakutumizireni kuchokera kwa Atate, ndiye Mzimu Woyera wachoonadi amene achokera kwa Atate, Iyeyo adzandichitira umboni Ine.
26 “Ayu boro Baibaisayan aniyafar nan, nati i turobe ana Anun Kakafiyin, i boro Tamai biyanane niyafar nan kwa biya natit, naatu ayu isou boro nao rerereb.
27 Inunso mudzandichitira umboni Ine, popeza mwakhala nane kuchokera pachiyambi.”
27 naatu kwa auman boro ayu isou kwana’orerereb, anayabin no aneika kwa ayu bairit tama.

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar João 15, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.