João 14

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI

Sair da comparação
AAI TUR GEWASIN O BAIBASIT BOUBUN
1 “Mtima wanu usavutike. Khulupirirani Mulungu; khulupirirani Inenso.
1 Jesu ana bai’ufununayah isa eo, “Men kwaniyababan, God kwanitumatum naatu ayu auman kwanitutumu.
2 Mʼnyumba mwa Atate anga muli zipinda zambiri. Kukanakhala kuti mulibemo ndikanakuwuzani. Ine ndikupita kumeneko kukakukonzerani malo.
2 Ayu Tamai ana baremaim bar awah moumurih na’in ti’inu’in naatu ayu anan kwa isa a bar awah anayabuna naatu bar awah men hitama’am na’at, aisim boro a tur ata’owen.
3 Ndipo ndikapita kukakukonzerani malo, ndidzabweranso kudzakutengani, kuti kumene kuli Ineko, inunso mukakhale komweko.
3 Ayu anan kwa a efan anayayabuna ufunamaim boro taiyuwu anamatabir anan ananawiyi bairi tanan ayu menamaim ama’am kwa boro imaim kwanama.
4 Inu mukudziwa njira ya kumene Ine ndikupita.”
4 Ayu efan menamaim anan kwa i kwaso’ob.”
5 Tomasi anati kwa Iye, “Ambuye ife sitikudziwa kumene Inu mukupita, nanga tingadziwe bwanji njirayo?”
5 Thomas Jesu isan eo, “Regah, aki men aso’ob o menamaim kwenan, ef boro mi’itube anaso’ob?”
6 Yesu anayankha kuti, “Ine ndine njira, choonadi ndi moyo. Palibe munthu angafike kwa Atate popanda kudzera mwa Ine.
6 Jesu iya’afut eo, “Ayu i ef, turobe, naatu yawas. Men yait ta nan Tamai biyan baise ayu’une nan Tamai biyan natit.
7 Mukanandidziwadi Ine, mukanadziwanso Atate anga. Kuyambira tsopano, mukuwadziwa ndipo mwawaona.”
7 Kwa anababatun ayu kwanasusu’ubu gewas na’at, Tamai boro auman kwanasu’ub. Bounabo kwasoso’ob naatu kwa’i’itin.”
8 Filipo anati, “Ambuye, tionetseni Atatewo ndipo ife tikhutitsidwa.”
8 Philip eo, “Regah Tamat kwi’obaiyi a’itin saise aki boro nuhinafot.”
9 Yesu anayankha kuti, “Kodi iwe Filipo, ndakhala pakati panu nthawi yonseyi ndipo iwe sukundidziwabe? Aliyense amene waona Ine, waonanso Atate. Tsono ukunena bwanji kuti, ‘Tionetseni Atate?’
9 Jesu iya’afut eo, “Philip manin maiyow airit tama baise men isu’ubu? Yait ta ayu i’itu Tamai i’itin? Aisimamih ayu isou i’o, ‘Tamat kwi’obaiyi a’itin?’
10 Kodi sukukhulupirira kuti Ine ndili mwa Atate, ndipo Atate ali mwa Ine? Mawu amene Ine ndiyankhula kwa inu si mawu anga okha koma ndi mawu Atate wokhala mwa Ine, amene akugwira ntchito yake.
10 Ayu i Tamai wanawananamaim ama’am naatu Tamai ayu wanawana’umaim ema’am. Philip o men kubitumatum? Iti tur i kwa isa ao’o, i men ayu au kokomaim ao’omih baise Tamai ayu wanawana’umaim ema’am bowabow i esisinaf.
11 Khulupirirani Ine pamene ndi kuti Ine ndili mwa Atate ndipo Atate ali mwa Ine. Koma ngati si chomwecho, khulupiriranitu Ine chifukwa cha ntchito zanga zodabwitsa.
11 Kwanitumatum ana maramaim iti tur anao’o, ayu i Tamai wanawanan ama’am naatu Tamai i ayu wanawanau ema’am, o men kwanabitumatum na’at ina’inan asisinaf imaim boro ni’obaiyi kwana’itin.
12 Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti aliyense amene akhulupirira Ine adzachita zimene Ine ndakhala ndikuchita. Iye adzachita ngakhale zinthu zazikulu kuposa zimenezi, chifukwa ndikupita kwa Atate.
12 Ayu anababatun a tur ao’owen yait ayu ebitutumu ayu abistan asisinaf boro nasinaf hinamatar, naatu sawar boro au gagamihika nasinaf. Anayabin ayu Tamai isan anan.
13 Ndipo Ine ndidzachita chilichonse chimene inu mudzapempha mʼdzina langa kuti Atate alemekezedwe mwa Mwana.
13 Naatu abistanawat ayu wabu’umaim kwafefefeyan boro ana sinaf saise Natun Tamah wabin nabora’ara’ah.
14 Ngati mudzapempha kanthu kalikonse mʼdzina langa, Ine ndidzachita.
14 Kwa sawar abistanawat ayu wabu’umaim kwanafefeyan boro anasinaf namatar.
15 “Ngati mundikonda Ine, sungani malamulo anga.
15 “Ayu kwanabiyabuwu na’at, au obaiyunen tur boro kwanabosiyasiyar.
16 Ine ndidzapempha Atate, ndipo adzakupatsani Nkhoswe ina kuti izikhala nanu nthawi zonse.
16 Naatu ayu boro Tamai anifefeyan i boro kwa a Baibaisayan ta wabin Turobe Ana Anun Kakafiyin nit bairi kwanama wanatowan.
17 Nkhosweyo ndiye Mzimu wachoonadi. Dziko lapansi silingalandire Nkhosweyi chifukwa samuona kapena kumudziwa. Koma inu mumamudziwa pakuti amakhala nanu ndipo adzakhala mwa inu.
17 Iti tafaram men nab, anayabin i boro men na’itin o boro men nasu’ub. Baise kwa i kwasu’ub, anayabin kwa bairi kwama’am naatu boro wanawanamaim nama.
18 Ine sindikusiyani nokha kuti mukhale ana amasiye. Ine ndidzabweranso kwa inu.
18 Ayu boro men anihamiyi kwanigaganamih, Ayu boro kwa isa anamatabir maiye anan.
19 Patsala nthawi yochepa dziko lapansi silidzandionanso koma inu mudzandiona. Popeza kuti Ine ndili ndi moyo, inunso mudzakhala ndi moyo.
19 Mar kafai iti tafaram boro men na’itu, baise kwa boro kwana’itu. Anayabin ayu ama’am isan kwa auman kwama’am.
20 Tsiku limenelo inu mudzazindikira kuti Ine ndili mwa Atate, ndipo inu muli mwa Ine, ndipo Ine ndili mwa inu.
20 Nati anamaramaim kwa boro kwanaso’ob ayu i Tamai wanawanan ama’am naatu kwa i ayu wanawanau kwama’am naatu ayu i kwa wanawan ama’am.
21 Iye amene amadziwa malamulo anga ndi kuwasunga ndiye amene amandikonda. Wokonda Ine adzakondedwa ndi Atate wanga ndipo Inenso ndidzamukonda ndikudzionetsa ndekha kwa iye.”
21 “Yait obaiyunen tur bai, ebobosiyasiyar, i ayu ebiyabuwu. Yait ayu ebiyabuwu i Tamai ebiyabuw naatu ayu auman boro aniyabuw naatu ayu taiyuwu anirerereb i isan.”
22 Kenaka Yudasi (osati Yudasi Isikarioti) anati, “Koma Ambuye, nʼchifukwa chiyani mukufuna kudzionetsa nokha kwa ife, osati ku dziko lapansi?”
22 Judas (men Judas Iscariot) Jesu isan eo, “Regah aisimamih tafaram ana sabuw men isah inirerereb baise aki akisi isai inirerereb?”
23 Yesu anamuyankha kuti, “Ngati wina aliyense andikonda Ine, adzasunga mawu anga. Atate wanga adzamukonda, ndipo Ife tidzabwera ndi kukhala naye.
23 Jesu iya’afutih eo, “Yait ta ayu isou ebiyabow boro au bai’obaiyen nabosiyasiyar? Ayu Tamai boro isan niyabow, naatu ayu Tamai airi biyanamaim ai bar anawowab bairi anama.
24 Iye amene sandikonda Ine sasunga mawu anga. Mawu awa amene mukumva si anga ndi a Atate amene anandituma Ine.
24 Yait ayu isou men ebiyabow au bai’obaiyen boro men nabosiyasiyar naatu iti tur ao kwanonowar i men ayu au turamih baise iti tur ayu Tamai iyafaru anan i biyanane enan.
25 “Ndayankhula zonsezi ndikanali nanu.
25 “Boun bairit tama’amamaim sawar etei’imak ao kwanowaraka.
26 Koma Nkhosweyo, Mzimu Woyera, amene Atate adzamutumiza mʼdzina langa adzakuphunzitsani zinthu zonse, ndipo adzakukumbutsani zonse zimene ndinakuwuzani.
26 Baise Baibaisayan, Anun Kakafiyin, boro Tamai niyun ayu wabu’umaim nan, i boro sawar etei ni’obaibiyi naatu sawar etei’imak au’uwi boro a not nakusisib.
27 Ine ndikukusiyirani mtendere. Ndikukupatsani mtendere wanga. Ine sindikukupatsani monga dziko lapansi limaperekera. Mtima wanu usavutike ndipo musachite mantha.
27 “Tufuw kwa biyamaim abihamiy, ayu tufuw kwa abit. Iti tufuw i men tafaram kwa bit na’atube abitimih. Yare kouh kwanayey a not men narukasiy naatu men kwanabir.
28 “Inu munamva Ine ndikunena kuti, ‘Ine ndikupita ndipo ndidzabweranso kwa inu.’ Mukanandikonda, mukanasangalala kuti Ine ndikupita kwa Atate, pakuti Atate ndi wamkulu kuposa Ine.
28 Iti tur i ao kwanowaraka. ‘Ayu i anan kwa isa boro anamatabir anan.’ Ayu kwanabiyabuwu na’at, kwaniyasisir ayu i Tamai isan anan anayabin Tamai i ra’at ayu natabiru.
29 Ine ndakuwuzani tsopano zisanachitike, kuti zikadzachitika mudzakhulupirire.
29 Bounaika a tur ao’owenabo sawar hinamatar, imih abistan hinamamatar kwa i kwanitumatum.
30 Ine sindiyankhulanso nanu zambiri nthawi yayitali popeza wolamulira dziko lapansi akubwera. Iye alibe mphamvu pa Ine,
30 Ayu boro men tur manin bairit tanao, anayabin tafaram ana kaifenayan kakafin i enan. I aurin fair men ema’am ayu nisnowahu.
31 koma kuti dziko lapansi lizindikire kuti Ine ndimakonda Atate ndi kuti ndimachita zokhazokha zimene Atate wandilamulira Ine.
31 Baise sabuw iti tafaramamaim i hinaso’ob ayu Tamai abiyabow isan imih Tamai abistan eo etatarbaiyunu imaim asisinaf.

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar João 14, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.