João 10

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI

Sair da comparação
AAI TUR GEWASIN O BAIBASIT BOUBUN
1 “Zoonadi, Ine ndikukuwuzani inu Afarisi, kuti munthu amene salowera pa khomo mʼkhola la nkhosa, koma amalowera pena pake ndi wakuba ndi wachifwamba.
1 “Turobe a tur ao’owen, bobaituw hai fur ana etawanamaim orot men imaim narun, baise nakayam ef ta’ane narun, nati orot i bainowan mowan.
2 Munthu amene amalowera pa khomo ndi mʼbusa wankhosazo.
2 Orot yait etawanamaim erur, i bobaituw kaifenayan.
3 Mlonda amamutsekulira khomo, ndipo nkhosa zimamvera mawu ake. Iye amaziyitana mayina nkhosa zakezo, nazitulutsa.
3 Orot fur kaifenayan boro etawan isan nabotawiy naatu bobaituw boro orot fanan hina’inan naatu ana bobaituw ta’ita’imon wabih naso’oben na’afih hinanowar naatu nabotaitih ufun hinatit.
4 Akazitulutsa nkhosa zake zonse, iye amazitsogolera, ndipo nkhosa zakezo zimamutsata chifukwa zimadziwa mawu ake.
4 I ebotaitih ufun tetitit anamaramaim, i wan ebi’iyon, naatu ana bobaituw ti’ufunun bairi tenan anayabin i fanan hiso’ob.
5 Koma nkhosazo sizidzatsatira mlendo. Izo zidzamuthawa chifukwa sizizindikira mawu a mlendo.”
5 Baise fanan ta boro men hini’ufunun, anayabin i fanan men hi’inan imih boro hinabihir.”
6 Yesu ananena mawu ophiphiritsawa, koma Afarisi sanazindikire zimene ankawawuza.
6 Jesu iti kawen turamaim eo, baise tur ana naniyan i men hibaimih abistan isan eo’o.
7 Choncho Yesu anatinso, “Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti Ine ndine khomo la nkhosa.
7 Imih Jesu tur ibanak eo maiye, “Turobe a tur ao’owen, Ayu i etawan bobaituw isah.
8 Onse amene anadza ndisanabwere Ine ndi akuba ndi achifwamba, ndipo nkhosa sizinawamvere.
8 Sabuw afa wan hinan i bainowah naatu bokwanekwaneyah, baise bobaituw men tainih isah hirub fanah hinowaramih.
9 Ine ndine khomo, aliyense amene alowa kudzera mwa Ine adzapulumuka. Iye adzalowa ndi kutuluka ndi kupeza msipu.
9 Ayu i etawan, yait ayu wanawana’umaim run enan boro yawas nab, boro hinarun hinatit fotan gewasin hinagatur.
10 Mbala sibwera chabe koma kuti idzabe, kupha ndi kuwononga. Ine ndabwera kuti iwo akhale ndi moyo, ndi kukhala nawo wochuluka.
10 Bainowan tenan i bain, asbunin naatu gurusin akisin hinot tenan; Ayu anan i boro yawas gewasin hinab hinama boro men abistan ta isan hiniyababan.”
11 “Ine ndine Mʼbusa wabwino. Mʼbusa wabwino amataya moyo wake chifukwa cha nkhosa zake.
11 “Ayu i bobaituw gewasu. Bobaituw Kaifenayan gewasin ana bobaituw isah ana yawas ebi’inuw.
12 Wantchito ndi mʼbusa amene nkhosazo si zake. Choncho, pamene aona mmbulu ukubwera, iye amazisiya nkhosazo ndi kuthawa. Ndipo mmbulu umagwira nkhosazo ndikuzibalalitsa.
12 Bobaituw kaifenayan orot ta men karam bobaituw nakaifen naatu i men nowan. Imih anamaramaim haru tuwetuwenih nan na’i’itin, i boro bobaituw nihamiyih nabihir. Naatu haru tuwenituwenih boro bobaituw bairi hiniyow naatu hina’abargiyih nanabin hinabihir.
13 Munthuyo amathawa chifukwa ndi wantchito ndipo sasamalira chilichonse cha nkhosazo.
13 Orot boro nabihir anayabin i orot ta hibai na ma ekakaifen, imih bobaituw isah i men enotanot gagamin.
14 “Ine ndine mʼbusa wabwino. Ine ndimazidziwa nkhosa zanga ndipo nkhosa zangazo zimandidziwa,
14 Ayu i bobaituw kaifenayan gewasu. Au bobaituw asu’ubih naatu i ayu hisu’ubu.
15 monga momwe Atate amandidziwa Ine, ndiponso Ine kudziwira Atatewo. Ndimapereka moyo wanga chifukwa cha nkhosa.
15 Tamai ayu susu’ubu na’atube, ayu Tamai asu’ub naatu au yawas bobaituw isah ai’inuw.
16 Ine ndili ndi nkhosa zina zimene sizili za gulu ili. Ine ndiyenera kuzibweretsanso. Izonso zidzamvera mawu anga, ndipo zidzakhala gulu limodzi ndi mʼbusa mmodzi.
16 Bobaituw afa ayu nowau i men iti fur wanawanan tema’am. I auman anabuwih hinan hinarun. I auman ayu fanau hinanowar, nati’imaim i boro bobaituw ta’imon naatu kaifenayan ta’imon.
17 Nʼchifukwa chake Atate anga amandikonda, popeza Ine ndikupereka moyo wanga kuti ndiwutengenso.
17 Tamai ebiyabuwu anayabin ayu au yawas ani’inuw, saise yawasu anama maiye.
18 Palibe amene angawuchotse mwa Ine, koma ndikuwupereka mwakufuna kwanga. Ine ndili ndi ulamuliro wa kuwupereka ndi ulamuliro wakuwutenganso. Lamulo ili ndinalandira kwa Atate anga.”
18 Men yait ta ayu au yawas nabosair, baise ayu taiyuwu au kokomaim au yawas anayara’iy. Ayu au fair ema’am anayara’iy naatu au fair ema’am anabora’ah maiye. Iti obaiyunen i Tamai biyanane abai.”
19 Pa mawu awa Ayuda anagawikananso.
19 Iti tur hinonowar anamaramaim Jew sabuw tarsibih maiye.
20 Ambiri a iwo anati, “Iye ndi wogwidwa ndi ziwanda ndi wamisala. Chifukwa chiyani mukumvera Iye?”
20 Sabuw moumurih maiyow hi’o, “I demon hitounbubur ema’am naatu ebikoko’aw. Aisim ana tur kwanonowar.”
21 Koma ena anati, “Awa si mawu a munthu wogwidwa ndi ziwanda. Kodi ziwanda zingathe bwanji kutsekula maso a wosaona?”
21 Baise sabuw afa hi’o, “Tur iti na’atube men karam orot demon hinatounbubur ema’am nao’omih. Mi’itube demon orot matan fim nabotawiy?
22 Ku Yerusalemu kunali chikondwerero chokumbukira kupatulidwa kwa Nyumba ya Mulungu. Inali nthawi yozizira,
22 Nati rarabkokou wanawanan Tafaror Bar ana hiyuw wabin Koksouwen i Jerusalemamaim hibogaigiwas.
23 ndipo Yesu ankayenda mʼbwalo la Nyumbayo ku malo a Solomoni.
23 Naatu Jesu Solomon ana efan awan ta Tafaror Bar wanawanan imaim bat reremor.
24 Ayuda anamuzungulira Iye akunena kuti, “Kodi iwe udzazunguza malingaliro athu mpaka liti? Ngati iwe ndi Khristu, tiwuze momveka.”
24 Jew hai ukwarih hiru’ay hi’arbebera’uh hi’u, “Mar bai’ab boro inabotani anama anakaifi? O Keriso na’at, bebeyanamaim ku’o anowar.”
25 Yesu anayankha kuti, “Ine ndimakuwuzani, koma inu simukhulupirira. Ntchito zimene ndikuchita mʼdzina la Atate anga zikundichitira umboni,
25 Jesu iyafutih eo, “Ayu kwa a tur aowen, baise kwa men kwaitumatum. Ina’inanen ayu Tamai wabinamaim asisinaf i ayu isou eo’orereb.
26 koma inu simukhulupirira chifukwa simuli a gulu lankhosa zanga.
26 Baise kwa men kwabitumatum anayabin kwa men ayu au bobaituw.
27 Nkhosa zanga zimamva mawu anga, Ine ndimazidziwa, ndipo zimanditsata Ine.
27 Ayu au bobaituw asu’ubih imih fanau hinowar tebi’ufnunu.
28 Ine ndimazipatsa moyo wosatha ndipo sizidzawonongeka. Palibe amene adzazikwatula mʼdzanja langa.
28 Ayu yawas wanatowan abitih; naatu boro men ta nakasiy; men ta ayu umou’umaim nabosair.
29 Atate anga, amene anandipatsa Ine, ndi akulu kuposa onse. Palibe amene angazikwatule mʼdzanja la Atate anga.
29 Tamai ayu bow bitu i ra’at etei natabirih, imih ayu Tamai umanamaim men yait ta nabosairen.
30 Ine ndi Atate ndife amodzi.”
30 Tamai naatu Ayu airi i ta’imon.
31 Ayuda anatolanso miyala kuti amugende Iye,
31 Ibanak maiye Jew sabuw kabay hibow hitarabimih,
32 koma Yesu anawawuza kuti, “Ine ndakuonetsani zinthu zambiri zabwino zodabwitsa kuchokera kwa Atate. Nʼchifukwa chiti mwa izi chimene mukundigendera?”
32 baise Jesu sabuw isah eo, “Ayu Tamai biyanane ina’inan gagamih moumurih maiyow ai’obaiyi. Anayabin iti isan ayu kabayamaim kwanarabu.”
33 Ayuda anayankha kuti, “Ife sitikukugenda chifukwa cha izi, koma popeza ukunyoza Mulungu, chifukwa iwe, munthu wamba, ukuti ndiwe Mulungu.”
33 Jew hiya’afut hi’o, “Aki men nati isan kabayamaim anarabi, baise o God kubi’i’iyab, anayabin o i orot maiyow, naatu taiyuw God kurarouw.”
34 Yesu anawayankha kuti, “Kodi sizinalembedwa mʼmalamulo anu kuti, ‘Ine ndanena kuti ndinu milungu?’
34 Jesu iyafutih eo, “Kwa a Buk Atamaninamaim iti na’atube hikirum ema’am, ayu ao’o kwa etei i god?
35 Ngati anawatcha milungu anthu amene analandira mawu a Mulungu, pajatu Malemba sangasweke,
35 I etei god narouw na’a’afih na’at, tur God i menane na naatu Buk Atamaninamaim hikikirum men hina’astu’ub.
36 nanga bwanji uyu amene Atate anamuyika padera monga wake weniweni ndi kumutuma ku dziko lapansi? Nanga ndi chifukwa chiyani mukundinena Ine kuti ndikuchita chipongwe? Kodi nʼchifukwa choti ndanena kuti, ‘Ine ndine Mwana wa Mulungu?’
36 Ayu Tamai yasairu i nowanamih amatar naatu irubinu naatu iyafaru ana iti tafaramaim atitit i boro mi’itube? Mi’itube ayu God bai’i’iyabin kwarouw kwa’o’o, anayabin ayu God Natun arouw ao’omih?
37 Musandikhulupirire Ine ngati sindichita ntchito za Atate anga.
37 Ayu Tamai sisinafube men ana sisinaf bibaitutumu.
38 Koma ngati Ine ndikuchita zimenezi, ngakhale kuti simundikhulupirira, khulupirirani ntchito zodabwitsazo, ndipo mudziwe ndi kuzindikira kuti Atate ali mwa Ine, ndiponso Ine ndili mwa Atate.”
38 Baise ayu ata sinaf kwa men kwatabitutumu na’at, karam nati ina’inanen kwata’itah kwataso’ob imaim kwatitumatum, ayu i Tamai wanawanan, naatu Tamai i ayu wanawanau.”
39 Iwo anafuna kumugwiranso koma anawapulumuka mʼmanja mwawo.
39 Ibanak maiye bain rabinamih hiwa’an, baise i umahine soratait tit.
40 Kenaka Yesu anabwereranso kutsidya la mtsinje wa Yorodani kumalo kumene Yohane ankabatiza mʼmasiku akale. Iye anakhala kumeneko
40 Naatu Jesu ibanak matabir maiye Jordan rabon rounane, marasika John sabuw imaim bapataito bitih efan imaim tit naatu Jesu imaim ma.
41 ndipo anthu ambiri anabwera kwa Iye. Iwo anati, “Ngakhale kuti Yohane sanachite chizindikiro chodabwitsa, zonse zimene Yohane ananena za munthu uyu zinali zoona.”
41 Naatu sabuw moumurin maiyow hina biyan hitit, naatu hi’o, “John ina’inan men ta sinaf a’itin, baise John iti orot isan eo’o i turobe.”
42 Ndipo pamalo amenewo ambiri anakhulupirira Yesu.
42 Efan nati’imaim sabuw moumurin maiyow Jesu hitumitum.

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar João 10, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.