Isaías 13

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA)

1 Uthenga onena za Babuloni umene Yesaya mwana wa Amozi anawulandira:

2 Kwezani mbendera yankhondo pa phiri loti see,

3 Ine Yehova, ndalamulira ankhondo anga;

4 Tamvani phokoso ku mapiri,

5 Iwo akuchokera ku mayiko akutali,

6 Lirani mofuwula, pakuti tsiku la Yehova layandikira;

7 Zimenezi zinafowoketsa manja onse,

8 Anthu adzagwidwa ndi mantha aakulu,

9 Taonani, tsiku la Yehova likubwera,

10 Nyenyezi zakumwamba ndiponso zonse zamlengalenga

11 Ndidzalanga dziko lonse chifukwa cha zolakwa zake,

12 Ndidzasandutsa anthu kukhala ovuta kupeza kuposa mmene amasowera golide wabwino.

13 Tsono ndidzagwedeza miyamba

14 Ngati mbawala zosakidwa,

15 Aliyense amene atadzapezeke ndi kugwidwa

16 Ana awo akhanda adzaphwanyidwa iwo akuona;

17 Taona, Ine ndidzadzutsa Amedi amene safuna siliva

18 Adzapha anyamata ndi mauta awo;

19 Babuloni, ufumu wake ndi waulemerero kuposa mafumu onse.

20 Anthu sadzakhalamonso

21 Koma nyama zakuthengo ndizo zidzakhale kumeneko,

22 Mu nsanja zake muzidzalira afisi,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Isaías 13, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.