Hebreus 5

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI

Sair da comparação
AAI TUR GEWASIN O BAIBASIT BOUBUN
1 Mkulu wa ansembe aliyense amasankhidwa kuchokera pakati pa anthu ndipo amayikidwa kuti aziwayimirira pamaso pa Mulungu, kuti azipereka mphatso ndi nsembe chifukwa cha machimo.
1 Firis gagamih etei i orot wanawanahimaim God boro narubin, naatu naya’asair sabuw wabihimaim God isan nabow. Bowabow kakafin notawiyen isan siwar nabow sibor na’afusar.
2 Popeza kuti iye mwini ali ndi zofowoka zake, amatha kuwalezera mtima amene ali osadziwa ndi osochera.
2 Nati firis ef tata’ane ririm re’ere i so’ob, imih sabuw iyab tefofokar naatu tisisinaf kakaf i karam boro yaten nanub nibaisih.
3 Chifukwa cha ichi, iye amadziperekera nsembe chifukwa cha machimo ake omwe ndiponso chifukwa cha machimo a anthu ena.
3 Anayabin i auman ririmin, imih boro men sabuw akisih hai bowabow kakafin isan sibor nayai’imih, baise i auman ana kakafin isan sibor boro nayai.
4 Palibe amene amadzipatsa yekha ulemu wotere, koma amachita kuyitanidwa ndi Mulungu monga momwe anayitanidwira Aaroni.
4 Men yait ta i wabin isan taiyuwin erubin firis gagamin emamataramih, baise God akisin ana kokomaim orot erubin firis gagamin emamatar, Aaron rurubin na’atube.
5 Nʼchifukwa chake Khristu sanadzipatse yekha ulemu wokhala Mkulu wa ansembe. Koma Mulungu anamuwuza kuti,
5 Ef i ta’imon, Keriso men i taiyuwin wabin isan firis gagamin ana efan baimih, baise God akisin Keriso isan eo,
6 Ndipo penanso anati,
6 Buk Atamanin wanawanan efan ta’ane eo maiye,
7 Yesu, pa nthawi imene anali munthu pa dziko lapansi pano, anapereka mapemphero ake ndi zopempha mofuwula ndi misozi kwa Iye amene akanamupulumutsa ku imfa, ndipo anamumvera chifukwa anagonjera modzipereka.
7 Jesu tafaramamaim ma’am ana veya, erererey naatu ere maturin auman God isan dogoron tutufin etei yoyoban, naatu ifefeyan, kokok i morobone tiyawas. Anayabin taiyuwin yayare i God itin, imih God ana yoyoban nowar.
8 Ngakhale Iye anali Mwana wa Mulungu anaphunzira kumvera pomva zowawa.
8 Turobe i God Natun, baise biyababanane fanabow ana ef so’ob.
9 Atasanduka wangwiro kotheratu, anakhala gwero la chipulumutso chosatha kwa onse omvera Iye.
9 Naatu rurusouw ana maramaim, na sabuw iyab God fanan hibaib hai yawas wanatowan ana tutut matar.
10 Ndipo Mulungu anamuyika kukhala Mkulu wa ansembe, monga mwa dongosolo la unsembe wa Melikizedeki.
10 Iti na’atube sinaf, imih God kurereb Firis Gagamin matar, Melkisedek Firis Gagamin ma’am na’atube.
11 Tili ndi zambiri zoti tinganene pa zimenezi, koma ndi zovuta kukufotokozerani chifukwa ndinu ochedwa kuphunzira.
11 Ayu akok kwanekwan tur moumurih ata kirum firis gagamin isan atao kwatanowar. Baise kaubuna gewas nowar isan i hifokar, anayabin kwa tur naniyan boro men kwanabaimih.
12 Ngakhale kuti pa nthawi ino munayenera kukhala aphunzitsi, pakufunikabe munthu wina kuti abwerezenso kudzakuphunzitsani maphunziro oyambira a choonadi cha Mulungu. Ndinu ofunika mkaka osati chakudya cholimba!
12 Iti ao anayabin, kwa i marasika kwana baitumatumayah kwamatar, boun i sabuw afa kwatabi’obaibiyih. Baise boro’ika sabuw afa hima tibi’obaibiyi, bay fokarin kwata’ani’aanifunik, kwama kek gidigihibe nun kwatomatom.
13 Aliyense amene amangodya mkaka okha, akanali mwana wakhanda, sakudziwa bwino chiphunzitso cha chilungamo.
13 Orot yait nun etomatom i kek sosof, kakafin o gewasin hai naniyan men so’ob.
14 Koma chakudya cholimba ndi cha anthu okhwima msinkhu, amene pogwiritsa ntchito nzeru zawo, aphunzira kusiyanitsa chabwino ndi choyipa.
14 Baise bay mafur i orot baibin gagamih isah, sabuw iyab hibi’a’ait i karam boro kakafin naatu gewasin hairi nakusib.

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Hebreus 5, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.