Gálatas 6

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs BKJ

Sair da comparação
1 Abale, ngati munthu agwa mʼtchimo lililonse, inu amene Mzimu amakutsogolerani, mumuthandize munthuyo ndi mtima wofatsa kuti akonzekenso. Koma mukhale maso kuti inu nomwe mungayesedwe.
1 Irmãos, se algum homem for surpreendido em uma falta, vós, que sois espirituais, restaurai o irmão no espírito de mansidão, considereis a vós mesmos para que também não sejais tentados.
2 Thandizanani kusenza zolemetsa zanu, ndipo mʼnjira imeneyi mudzakwanitsa lamulo la Khristu.
2 Carregai os fardos uns dos outros para que a lei de Cristo seja cumprida.
3 Ngati wina adziyesa kanthu pamene iyeyo sali kanthu konse, akudzinamiza yekha.
3 Porque, se algum homem pensa ser alguma coisa, quando nada é, ele engana-se a si mesmo.
4 Munthu aliyense aziyesa yekha ntchito zake mmene zilili. Ngati zili bwino, adzatha kunyadira chifukwa cha ntchito zake zokhazo, iyeyo asadzifanizire ndi munthu wina wake,
4 Porém, que cada homem prove sua própria obra, e então poderá gloriar-se em si mesmo, e não em outro.
5 pakuti aliyense ayenera kusenza katundu wake.
5 Porque cada um deve carregar o seu próprio fardo.
6 Koma munthu amene akuphunzira mawu, agawireko mphunzitsi wake zinthu zonse zabwino zimene iye ali nazo.
6 Que aquele que está sendo instruído na palavra reparta todas as coisas boas àquele a quem ensina.
7 Musanamizidwe: nʼkosatheka kupusitsa Mulungu. Munthu amakolola zimene wafesa.
7 Não vos enganeis; de Deus não se zomba; porque tudo o que o homem semear, isso também colherá.
8 Pakuti amene amafesa zokondweretsa thupi lake la uchimo, kuchokera ku khalidwe limenelo adzakolola chiwonongeko; amene amafesa zokondweretsa Mzimu, kuchokera kwa Mzimu adzakolola moyo wosatha.
8 Pois aquele que semeia na sua carne, da carne colherá a corrupção; mas aquele que semeia no Espírito, do Espírito colherá a vida eterna.
9 Tisatope nʼkuchita zabwino, pakuti pa nthawi yoyenera tidzakolola ngati sititopa.
9 E não nos cansemos de fazer o bem, porque na estação certa colheremos, se não desistirmos.
10 Nʼchifukwa chake ngati tapeza mpata, tiyenera kuchitira zabwino anthu onse, makamaka amene ndi a banja la okhulupirira.
10 Por isso, enquanto temos a oportunidade, façamos o bem a todos os homens, mas particularmente àqueles que são domésticos na fé.
11 Onani zilembo zazikulu zimene ine ndikulemba ndi dzanja langa.
11 Vede com que tamanho de letras vos escrevi com minha própria mão.
12 Onse amene akufuna kuoneka abwino pamaso pa anthu akukukakamizani kuti muchite mdulidwe. Akuchita izi ndi cholinga chimodzi chokha, chakuti apewe kuzunzidwa chifukwa cha mtanda wa Khristu.
12 Muitos desejam ser bem vistos na carne, eles vos constrangem a ser circuncidados, apenas para não serem perseguidos por causa da cruz de Cristo.
13 Pakuti ngakhale iwowa amene anachita mdulidwe satsata Malamulo, komabe akufuna kuti muchite mdulidwe kuti anyadire mdulidwe wanuwo.
13 Porque nem mesmo eles que são circuncidados observam à lei; mas querem que vós sejais circuncidados, para que possam se gloriar em vossa carne.
14 Ine sindingathe kunyadira kanthu kena koma mtanda wa Ambuye athu Yesu Khristu, kudzera mwa mtandawo dziko lapansi linapachikidwa kwa ine ndi ine ku dziko lapansi.
14 Porém, de maneira alguma eu devo me gloriar, exceto na cruz de nosso Senhor Jesus Cristo, por quem o mundo está crucificado para mim e eu para o mundo.
15 Pakuti kaya mdulidwe kapena kusachita mdulidwe, sizitanthauza kanthu; chofunika ndi kulengedwa mwatsopano.
15 Porque em Jesus Cristo, nem a circuncisão e nem incircuncisão de nada valem, mas uma nova criatura.
16 Mtendere ndi chifundo zikhale kwa onse amene amatsata chiphunzitso ichi, ndi pa Israeli wa Mulungu.
16 E com todos os que andarem de acordo com esta regra, estejam sobre eles a paz e a misericórdia, e também sobre o Israel de Deus.
17 Pomaliza wina asandivutitse, pakuti mʼthupi mwanga muli zizindikiro za Yesu.
17 De agora em diante que nenhum homem me cause problema, porque trago em meu corpo as marcas do Senhor Jesus.
18 Chisomo cha Ambuye athu Yesu Khristu zikhale ndi mzimu wanu abale. Ameni.
18 Irmãos, que a graça de nosso Senhor Jesus Cristo esteja com vosso espírito. Amém (Aos Gálatas escrito desde Roma).

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Gálatas 6, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.