Gálatas 2

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI

Sair da comparação
AAI TUR GEWASIN O BAIBASIT BOUBUN
1 Kenaka, patatha zaka khumi ndi zinayi, ndinapitanso ku Yerusalemu, nthawi iyi ndinapita ndi Barnaba. Ndinatenganso Tito kuti apite nafe.
1 Kwamur etei 14 sasawar ufunamaim ayu Barnabas airi Titus abai auman bairi amatabir ayen ana Jerusalem atit.
2 Ine ndinapita chifukwa Mulungu anachita kundionetsera kuti ndipite ndipo ndinakakumana ndi atsogoleri mu msonkhano mwamseri ndi kuwafotokozera Uthenga Wabwino umene ndimalalikira pakati pa anthu a mitundu ina. Ndinachita zimenezi kuti ndikhale ndi chitsimikizo kuopa kuti mwina ndinathamanga kapena ndimathamanga liwiro pachabe.
2 Ayu ayey au an i God ana tur isou iwa’an birerereb i orot ukwarih bairi wa’iwa’iramaim omih ayen an. Ayu mi’itube Ufun Sabuw isah Tur Gewasin abibinan ata kubuna hitanowar, saise abisa abusuruf abowabow naatu abisa bowamih ayayakitifuw men hita’otanu au bowabow yomanin yabin en tamataramih.
3 Komatu ngakhale Tito, amene anali nane sanakakamizidwe kuti achite mdulidwe, ngakhale iyeyo anali Mgriki.
3 Ayu au baitur Titus Greek orot isan i men ana’ar kanabin afuwinamih aokikin.
4 Nkhani iyi inayambika chifukwa abale ena achinyengo amene analowerera pakati pathu kuti adzaone za ufulu umene tili nawo mwa Khristu Yesu ndikuti atisandutse akapolo.
4 Baise sabuw afa hikokok i ana’ar kanabin hita’afuw, iti sabuw i hikirisiyan moyamoy hina ata kou’ayomaim hirun rafot rouwayah na’atube, saise Keriso Jesu wanawananamaim roufamen tabaib hitatita’ur naatu hita’uwit ata ar kanabih tata’afuw akir sabuw tatamataramih.
5 Ife sitinawagonjere ndi pangʼono pomwe, nʼcholinga chakuti choonadi cha Uthenga Wabwino chikhalebe ndi ife.
5 Baise aki men kafai veya ta aitih, anayabin aki akok turobe naatu Tur Gewasin atabotan kwa a gewasin isan tama.
6 Koma kunena za aja ankaoneka ngati ofunika kwambiri, chimene iwo anali sichisintha kanthu kwa ine; chifukwa Mulungu alibe tsankho, iwowo sanawonjezepo kanthu pa uthenga wanga.
6 Orot iyab tibi’ukwarin isah, ayu boro iti na’atube atao, men ta gagamin, naatu men ta kikimin etei i ta’imon. Anayabin God men orot ukwarih ufuhine i’itinimih, baise wanawanahine i’itin. Imih nati orot ukwarih ayu au tur ao men tafan hinaya’abarimih.
7 Makamaka anaona kuti ine ndinapatsidwa ntchito yolalikira Uthenga Wabwino kwa anthu a mitundu ina monga momwe Petro anapatsidwa ntchito yolalikira Uthenga Wabwino kwa Ayuda.
7 Hinotanot ayu tur boubuh afa ayabaren hirouw higamigam, ufibo hinunuwariy God Tur Gewasin Peter itin Jew sabuw isah bibinan na’atube ayu itu Ufun Sabuw isah abibinan hi’itin.
8 Pakuti Mulungu, amene amagwira ntchito mu utumiki wa Petro monga mtumwi kwa Ayuda, amagwiranso ntchito mu utumiki wanga monga mtumiki kwa anthu a mitundu ina.
8 God ana fairamaim Peter tur abarayan matar Jew sabuw wanawanahimaim bowabow na’atube God ana fair itu tur abarayan amatar Ufun Sabuw wanawanahimaim abowabow.
9 Yakobo, Petro ndi Yohane, amene ankatengedwa ngati mizati, atazindikira chisomo chimene chinapatsidwa kwa ine, anagwirana chanza ndi ine ndi Barnaba kusonyeza chiyanjano chathu. Iwo anavomereza kuti ife tipite kwa anthu a mitundu ina ndipo iwo apite kwa Ayuda.
9 James, Peter, John baitumatumayah hai tutut, God ana bowabow ta ayu bowamih bitu hi’inan, imih ayu Barnabas airi umai hibow ai’ofbonen etei ai basit. Ayu Barnabas airi Ufun Sabuw wanawanahimaim ana bow naatu i Jew sabuw wanawanahimaim hinabow.
10 Chimene iwo anapempha ndi chakuti ife tipitirize kukumbukira osauka, chinthu chimene ine ndinali okonzeka kuchichita.
10 Naatu hai baifefeyan i mi’itube hai kou’ayomaim sabuw yababan wairafih atanuhih baibais atitih naatu nati sawar i ayu sinafumih akokok hio.
11 Petro atafika ku Antiokeya, ine ndinamudzudzula pa gulu chifukwa anapezeka wolakwa.
11 Baise Peter na Antioch binanawan ana maramaim, abisa biwa’an kakaf isan sabuw nahifunik yumatanamaim agam au.
12 Pakuti asanafike anthu otumidwa ndi Yakobo, iye ankadya pamodzi ndi anthu a mitundu ina. Koma atafika, iyeyo anachoka pakati pa anthuwo nakakhala pa yekha chifukwa ankaopa anthu a mʼgulu la mdulidwe.
12 Anayabin James orot afa men biyafarih ana veya i nanamaim Ufun Sabuw iyab baitumatumayah himamatar, Peter wanawanah run bairi hima hi’aa hitomatom. Baise orot James iyafarih hin hititit ufunamaim Peter taitin ihamiyih mataweyan, anayabin sabuw iyab ar kanabih afuw isan hai baibasit ma’am isah bir.
13 Ayuda enanso anamutsata pochita zachinyengozi, kotero kuti ngakhale Barnaba anasocheretsedwa chifukwa cha chinyengo chawocho.
13 Peter ana rerekab turin Jew baitumatumayah hibai hikofan hirerekab, Barnabas itih run i auman rerekab.
14 Koma nditaona kuti iwo sankachita molingana ndi choonadi cha Uthenga Wabwino, ndinawuza Petro pamaso pa anthu onse kuti, “Iwe ndiwe Myuda koma ukukhala ngati munthu wa mtundu wina, osati Myuda. Nanga nʼchifukwa chiyani ukukakamiza anthu a mitundu ina kuti akhale ngati Ayuda?
14 Ayu ai’itih ana veya hai ef i hiwas sa’ir men Tur Gewasin eo’omaim hinan, imih ayu sabuw etei nahimaim Peter au, “O i Jew orot, baise ama i Ufun Sabuw hai ma’abe kuma’am, men Jew sabuw hai ma’abe kuma’am, naatu boro mi’itube Ufun Sabuw inabonawiyih, Jew sabuw hai binanakwar hini’ufunun?”
15 “Ife amene ndife Ayuda mwachibadwa, osati anthu a mitundu ina ochimwa,
15 It ata tufuw an i men iti Ufun Sabuw kakafih tarouw tao imaim tatufuwamih. Baise it ata tufuw an i Jew hai rara’ane tatufuw.
16 tikudziwa kuti munthu salungamitsidwa pochita ntchito za lamulo koma ndi chikhulupiriro mwa Yesu Khristu. Chomwecho, ifenso tinakhulupirira Khristu Yesu kuti tilungamitsidwe mwachikhulupiriro mwa Khristu ndipo osati pochita ntchito za lamulo, chifukwa palibe amene adzalungamitsidwa pochita ntchito za lamulo.
16 Tanaso’ob orot yamutufurin na God biyan tit isan i men ofafaramaim eyayamutufurimih, baise baitumatum Jesu Keriso wanawananamaim. Imih it auman ata baitumatum Keriso Jesu wanawananamaim tanayai, saise baitumatum Keriso Jesu wanawananamaim boro nayamutufurit, men ofafaramaim nayamutufuritamih. Anayabin ofafar eo’omaim inasisinaf boro men nayamutufurimih.
17 “Tsono ngati ife, pamene tikufuna kulungamitsidwa mwa Khristu, zikuonekeratu poyera kuti ndifenso ochimwa, kodi zikutanthauza kuti Khristu amalimbikitsa uchimo? Ayi. Nʼkosatheka!
17 Keriso wanawananamaim yamutufurit isan ef tana nunuwet na’at, taiyuwit tana’i’itit i bowabow kakafin tasisinaf, kwanotanot Keriso bowabow kakafin ana kou’obowayan? En anababatun.
18 Ngati ine ndimanganso chimene ndinachigumula, ndikuonetsa kuti ndine wophwanya lamulo.
18 Ayu ofafar agurus re’er iban ana wowab maiye nayey na’at, nati ebiturobe ayu i ofafar asto’obenayan.
19 “Pakuti pamene ndinayesera kutsatira lamulo, lamulolo linandionetsa kuti ndine wochimwa. Choncho ndinasiya kutsatira lamulo kuti ndikhale ndi moyo kwa Mulungu.
19 Anayabin ayu i ofafaramaim, ofafar e’asbunu amorob, saise God isan ata bow.
20 Ndinapachikidwa pa mtanda pamodzi ndi Khristu, kotero kuti sindinenso amene ndili ndi moyo, koma ndi Khristu amene ali ndi moyo mwa ine. Moyo umene ndili nawo tsopano mʼthupi lino, ndi moyo mwachikhulupiriro mwa Mwana wa Mulungu, amene anandikonda nadzipereka yekha chifukwa cha ine.
20 Ayu i Keriso airi onaf afe’en hi’onafi, imih iti i men ayu ama’am, baise Keriso wanawana’umaim ema’am. Yawas iti boun ama’am i God Natun a bitumitumimaim ama’am, anayabin ayu iyabuwu naatu ana yawas isou i’inuw.
21 Ine sindikukankhira kumbali chisomo cha Mulungu, chifukwa ngati chilungamo chikanapezeka pochita ntchito za lamulo, ndiye kuti Khristu anafa pachabe.”
21 Ayu men karam God ana bosiyasiyar boro ana kwahir. Baise orot yait ofafaramaim yamutufurin na God biyan tit isan nasisinaf na’at, Keriso onaf afe’en momorob i boro yabin en.

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Gálatas 2, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.