Filipenses 4

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI

Sair da comparação
AAI TUR GEWASIN O BAIBASIT BOUBUN
1 Tsono abale anga, ndimakukondani ndipo ndikukulakalakani. Ndinu chimwemwe changa ndi chipewa cha ulemerero wanga. Abwenzi okondedwa, chilimikani choncho mwa Ambuye.
1 Isan imih taituwau, kwa i ayu au yabow, au yasisir naatu au yey, akokok kwanekwan i ayumat ata itin, Regah wanawananamaim kwanabatkikin.
2 Ndikudandaulira Euodiya ndi Suntuke kuti akhale ndi mtima umodzi mwa Ambuye.
2 Kwa Euodia naatu Sinataike airi abifefeyani, akokok Regah wanawananamaim tura airi a tur ta’imon kwanabow.
3 Inde, ndikupempha iwe mnzanga pa ntchitoyi, thandiza amayiwa amene ndagwira nawo ntchito ya Uthenga Wabwino pamodzi ndi Klementonso ndi ena onse antchito anzanga amene mayina awo ali mʼbuku lamoyo.
3 Naatu o bit abar turou auman abifefeyani, akokok iti baibin hairi inibaisih. Anayabin i hairi ayu hibaisu raro’oh baban tur gewasin abosemor, Clement auman naatu bow turou’unah afa moumurih na’in auman hibaisu tur gewasin abobosemor, wabih i yawas ana buk wanawanan hikirum ti’inu’in.
4 Nthawi zonse muzikondwa mwa Ambuye. Ndikubwerezanso; muzikondwa!
4 Regah wanawananamaim mar etei kwaniyasisir. Iban ao maiye, kwaniyasisir!
5 Kufatsa kwanu kuzioneka pamaso pa anthu onse. Ambuye anu ali pafupi.
5 Ayu akokok yara’iyen ana yawas i sabuw kwani’obaiyih. Regah na isan i na iyubin.
6 Musade nkhawa ndi kanthu kalikonse, koma pa china chilichonse, mwa pemphero ndi chidandaulo pamodzi ndi chiyamiko, perekani zopempha zanu kwa Mulungu.
6 Men sawar isah kwananot kwaniyababan, baise mar etei ayoyobanamaim abisa kwakokok i dogor merarayow auman God kwanifefeyan.
7 Ndipo mtendere wa Mulungu, umene upambana nzeru zonse udzasunga bwino mitima yanu ndi maganizo anu mwa Khristu Yesu.
7 Naatu God ana tufuw ra’at orot babin ana so’ob nanatabir i boro kwa dogor naatu anot nafafar Keriso Jesu wanawananamaim kwanama.
8 Potsiriza, abale, muziyika mtima wanu pa zinthu zilizonse zabwino ndi zotamandika monga, zinthu zoona, zinthu zolemekezeka, zinthu zolungama, zinthu zoyera, zinthu zokongola ndi zinthu zosiririka.
8 Naatu ayu au tur yomanin i boro iti na’atube anao. Sawar abisa gewasih, sawar abisa tirursagiyen, sawar abisa i turobe anababatun, sawar abisa ya ebaib, sawar abisa hai ef mutufurin, sawar abisa kouksouwenamaim ti’inu’in, sawar abisa i mumunih, sawar abisa i mokobfouh, nati sawar isah anot imaim kwanaya mar etei kwananot.
9 Muzichita chilichonse chimene mwaphunzira kapena kulandira kapena kumva kuchokera kwa ine kapena mwaona mwa ine. Ndipo Mulungu wamtendere adzakhala nanu.
9 Abisa ayu asinaf kwa’itin biyou’une kwabaib naatu ao kwanonowar i kwani’a’ait. Naatu tufuw ana God boro mar etei bairi kwanama.
10 Ndikukondwa kwambiri mwa Ambuye kuti patapita nthawi tsopano mwayambanso kuonetsa kuti mumandiganizira. Zoonadi, mwakhala mukundikumbukira, koma munalibe mpata woti muonetsere zimenezi.
10 Regah wanawananamaim ama’ama i abiyasisir gagamin maiyow, anayabin kwa iban maiye nuhitaseb baibaisu isan kwanotanot. Turobe kwa i baibaisu isan kwanotanot, baise ef men ta ema’am boro a baibais kwanitu.
11 Sindikunena izi chifukwa choti ndikusowa thandizo, poti ine ndaphunzira kukhala wokwaniritsidwa ndi zimene ndili nazo.
11 Iti ao’o i men au huramaim i’en ama’ama baibaisu isan ao’omih, ayu makakaf naatu ma gewas hai ef etei aso’ob, imih abisa kikimin biyou ema’am karam boro anama.
12 Ndimadziwa kusauka nʼkutani, ndipo ndimadziwa kulemera nʼkutani. Ndaphunzira chinsinsi chokhala wokhutitsidwa mwa njira ina iliyonse, kaya nʼkudya bwino kapena kukhala ndi njala, kaya kukhala ndi chuma kapena umphawi.
12 Mour ana veya naatu baimar ana veya i ayu aso’ob, makakaf ta ta wanawanahimaim mi’itube inaa inatomatom naatu mi’itube inabi’aamorob hai kirikirifot etei ayu aso’ob.
13 Ndikhoza kuchita zonse kudzera mwa Iye amene amandipatsa mphamvu.
13 Sawar etei i wanawananamaim ayu fair abaib, imaim karam boro anasinaf.
14 Komatu munachita bwino kundithandiza mʼmavuto anga.
14 Baise a merar ayiy au makakaf wanawanan kwabibaisu i kwa a gewasin ayu kwabi’obaiyu isan.
15 Ndipo inu Afilipi mukudziwa kuti masiku oyambirira olalikira Uthenga Wabwino, nditachoka ku Makedoniya, panalibe mpingo ndi umodzi omwe umene unagwirizana nane pa nkhani yopereka ndi kulandira, kupatula inu.
15 Kwa Philipi sabuw marasika ayu boubu ana tur gewasin abibinan ufunamaim Masedonia abihamiy ana veya, kwa akisimo a baitinin ayu kwabibaisu i kwaso’ob naatu anawayow kwabaib auman i kwaso’ob, ekaleisia afa i men hibaisu.
16 Pakuti ngakhale pamene ndinali ku Tesalonika, munanditumizira kangapo zondithandiza pa zosowa zanga.
16 Naatu ana Thessalonica atit ama’am ana veya kwa a siwar i men mar ta’imon kwaiyafar baibais kwaitu’umih, baise mar maumurih maiyow kwaiyafar.
17 Osati ndikufuna mphatso zanu, koma ndikufuna kuti pa zimene muli nazo pawonjezerekepo phindu.
17 Ayu i men nati siwar baiyafarin ayu bain isan ao’omih, en baise akokok a baitininamaim baigegewasin kwanab.
18 Ndalandira zonse ndipo ndili nazo zokwanira zoposa zosowa zanga popeza ndalandira kwa Epafrodito mphatso zochuluka zimene munatumiza. Ndizo zopereka za fungo labwino, nsembe zolandiridwa zokondweretsa Mulungu.
18 Sawar kwabiyafaren etei i abow, naatu tafan kwaya’abar auman na abaib i ra’at kwanekwan, naatu au kok abisa anotanot etei Epafaroditas kwaitin bow nan i abow umou awan karatan. Siwar nati kwaiyafar abaib i sibor yamurin gewasin faur yamurinabe eyen God eyun ebiyasisir na’atube abai.
19 Ndipo Mulungu wanga adzakwaniritsa zosowa zanu monga mwa chuma chake chaulemerero mwa Khristu Yesu.
19 Imih ayoyoyoban, Regah God boro a kok etei na’itin Jesu Keriso ana toto ana buyoy wanawanan ma’agiy ema’am ine kwa etei boro nigegewasini.
20 Kwa Mulungu ndi Atate athu, kukhale ulemerero mpaka muyaya. Ameni.
20 Tamat God merarayow bora’ara’aten tanitin wanatowan, wanatowan. Amen.
21 Perekani moni kwa oyera mtima onse mwa Khristu Yesu. Abale amene ali ndi ine akupereka moni wawo.
21 God ana sabuw etei’imak hai tur ina’owen hai merar ayiy. Taituwa bairi iti ama’am a merar tiyiy.
22 Oyera mtima onse akupereka moni, makamaka iwo a ku nyumba ya Kaisara.
22 God ana sabuw bairi iti ama’am kwa a merar tiyiy. Naatu merarayow gagamin i Caesar ana nibur bairi kwa a merar tiyiy.
23 Chisomo cha Ambuye Yesu Khristu chikhale ndi mzimu wanu. Ameni.
23 Ayu ayoyoyoban, ata Regah Jesu Keriso ana manaw ana kabeber kwa ayub nikofan bairi kwanama. Amen.

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Filipenses 4, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.