Filipenses 3

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI

Sair da comparação
AAI TUR GEWASIN O BAIBASIT BOUBUN
1 Abale anga, ndikupitiriza kunena kuti, kondwani mwa Ambuye! Sizondivuta kuti ndilembenso mawu omwewo, ndipo zimenezi nʼzokuthandizani inuyo.
1 Taitu, au tur yomanin, Regah wanawananamaim kwaniyasisir, sawar ta’imon kwa isa akikirum maiye isan i men biyou eo’ohow, anayabin iti tur boro kwa natafafari.
2 Chenjerani ndi agalu amenewa, anthu ochita zoyipa, anthu amene amadula thupi lawo.
2 Sabuw haru’ube tuwetuwenih naatu kakafin sinafuyah isah i matatoniwa’an, anayabin boro hinaokikin a’ar mo’oh hina’afuw.
3 Pakuti ochita mdulidwe weniweni ndife. Ife amene timatumikira Mulungu motsogozedwa ndi Mzimu. Ife amene timanyadira Khristu, ndipo sitidalira zinthu za thupi
3 Baise kwanaso’ob it i anababatun afu’afuw tabaika, naatu Anunin Kakafiyin ana fairamaim God takwafir Jesu Keriso ana gewasin isan tao ra’ara’at, naatu biyat ana’a’afuw isan men tabitumitum.
4 ngakhale kuti ineyo ndili ndi zifukwa zokwanira kudalira zinthu za thupizo.
4 Ayu nati biyat ana’a’afuw isan i ayu abitumatum,
5 Ndinachita mdulidwe pa tsiku lachisanu ndi chitatu nditangobadwa. Ndine wa mtundu wa Israeli, wa fuko la Benjamini, Mhebri wa Ahebri, kunena za malamulo, ndinali Mfarisi.
5 Anayabin ayu atufuw fur ta’imon ufunamaim au ar kanabin hi’afuw, naatu ayu Israel hai rara, Benjamin ana bigane ana, Hebrew hai rara anababatun, ofafar baifanabowayan, naatu Pharisee ana kou’ay orot ta,
6 Kunena za changu changa, ndinkazunza mpingo. Kunena za chilungamo chopezeka chifukwa chotsata malamulo, ineyo ndinali wopanda cholakwa.
6 baibobowenayan, ekaleisia ana gurusenayan orot, ofafar etei abosiyasiyar naatu men yait ta ubar itu’umih.
7 Koma zonse zimene ndinkaziyesa zaphindu, tsopano ndikuziona kuti nʼzosapindulitsa chifukwa cha Khristu.
7 Naatu sawar iti aitah hai yabih gagamih arouw ao, Keriso bi’obaiyu iti sawar etei hai yabin i en.
8 Kuwonjeza pamenepo, ndikuziona zonse kuti nʼzopanda phindu poyerekeza ndi phindu lopambana la kudziwa Khristu Yesu Ambuye anga. Nʼchifukwa cha Yesuyo ndataya zinthu zonse ndipo ndikuziyesa zinyalala kuti ndipindule Khristu
8 Men nati sawar akisin, baise sawar etei’imak hai yabih i en, anayabin ata Regah Jesu Keriso ana gewasin iti sawaramaim afufufun ana gewasin i ra’at sawar etei natabiren. Imih ayu Jesu wabinamaim sawar etei kakafih arou ao ai hamiyen abi’akir, saise Keriso anab
9 ndi kuti ndipezeke mwa Iyeyo, osati ndi chilungamo changa chobwera chifukwa chotsata malamulo, koma chimene chimabwera chifukwa chokhulupirira Khristu. Chilungamochi nʼchochokera kwa Mulungu, timachilandira mwachikhulupiriro.
9 nowau’umih namatar nayamutufuru, men ofafaramaim, baise Keriso anabitumitumimaim boro nayamutufuru anan God biyan anatit.
10 Ine ndikufuna kudziwa Khristu, ndithu, kudziwa mphamvu zake za kuuka kwa akufa. Ndikufuna kuyanjana naye mʼmasautso ake, kufanana naye pa imfa yake
10 Ayu akokok i Keriso anaso’ob, morobone mimisir ana fair auman anaso’ob, naatu ana bai’akir turin anab ani’akir, momorobobe ana morob.
11 kuti nanenso ndidzaukitsidwe kwa akufa.
11 Saise God boro morobone niyawasu anamisir.
12 Sikuti ndazipeza kale zonsezi, kapena kuti ndakhala kale wangwiro, koma ndikuthamangabe ndi kuyesetsa kuti ndipeze chimene Khristu Yesu anandiyitanira.
12 Men kwananot ayu sawar etei i abaika, o anunuw ana yomanin aisawarika, en baise boro’ika bainamih anununuw, anayabin Keriso au siwar baitu isan i inonowatika inu’in.
13 Abale, sindidziyesera ndekha kuti ndachipeza kale chimenechi. Koma chinthu chimodzi chimene ndimachita, nʼkuyiwala zamʼmbuyo ndi kuthamangira molimbika zinthu zimene zili mʼtsogolo mwanga.
13 Taitu, ayu aso’ob nati sawar bain isan i boro’ika bainamih anan, baise sawar ta’imon asisinaf i tit, abisa ufu’une i nuhubur naatu abisa nou’une inu’in i bainamih anununuw.
14 Ndikuthamangira kokathera mpikisanowo kuti ndikalandire mphotho imeneyi kumwamba, imene Mulungu anandiyitanira mwa Khristu Yesu.
14 Ayu asinaftobon ananunuw yomanin anisawar, naatu mar ana siwar Keriso Jesu wanawananamaim God ea’afu anab.
15 Choncho ife tonse amene tili okhwima pa moyo wauzimu, tikhale ndi maganizo omwewa. Ndipo ngati pena ndi pena muli ndi maganizo osiyana ndi amenewa, pameneponso Mulungu adzakuwunikirani.
15 It moumurit na’in iyabowat ayubitane orot babin tamamatar i boro not ta’imon iti na’atube tananot, baise sawar afa isah o men kubibasit, God boro isa nasinaf hinirerereb inaso’ob.
16 Tiyeni ife tizikhala mogwirizana ndi zimene tinapeza kale basi.
16 Imih, it abisa turobe marasika tabaib i tanabukikin tani’ufunun.
17 Abale, nonsenu pamodzi mudzinditsanzira ine, ndipo monga inu muli ndi chitsanzo, phunzirani kwa amene akukhala moyo motsatira momwe timakhalira.
17 Taitu au yawas kwani’u’uru, naatu sabuw afa hai yawas gewasin abi’obaiyi i kwani’ufnunih.
18 Pakuti monga ndakhala ndikukuwuzani kawirikawiri mʼmbuyomu, ndipo tsopano ndikunenanso ndi misozi kuti, anthu ambiri akukhala monga adani a mtanda wa Khristu.
18 Anayabin abisa boun ao kwanonowar i marasika mar moumurih maiyow ao kwanowaraka. Baise boun i yau rererey yen maturu re auman ao, sabuw moumurih na’in hai ma hai remoramaim hisinaf Keriso onaf afe’en momorob i hai rakit matar.
19 Mapeto awo ndi chiwonongeko, mulungu wawo ndi mimba zawo, ndipo ulemerero wawo ndi manyazi awo. Mtima wawo uli pa zinthu za dziko lapansi.
19 Naatu hai yomanin i gurugurusenamaim ema’am, kabutih i hai god matar, tibi’o’orot boro biyah na’ohow, anayabin hai not i tafaram ana sawar.
20 Koma ife ndife nzika za kumwamba ndipo tikudikirira mwachidwi Mpulumutsi wochokera kumeneko, Ambuye Yesu Khristu.
20 Baise it i mar ana fef tabai tama’am, imih ata baiyawasenayan ata Regah Jesu Keriso nati’ine na isan tama takaif tanuwanuw.
21 Iyeyo, ndi mphamvu imene imamuthandiza kukhazikitsa zinthu zonse pansi pa ulamuliro wake, adzasintha matupi athu achabewa kuti akhale ofanana ndi thupi lake la ulemerero.
21 I boro ana fairamaim sawar etei nabow babanamaim naya naatu it biyat himorob tiriririm boro nabotabiren hinan bonamanamarin hinamatar.

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Filipenses 3, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.