Filipenses 2
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Ngati muli ndi chilimbikitso chilichonse chifukwa cholumikizana ndi Khristu, ngati muli ndi chitonthozo chifukwa cha chikondi chake, ngati muli ndi mtima umodzi mwa Mzimu, ndipo ngati mumakomerana mtima ndi kuchitirana chifundo,
1 Kwa ayawas Keriso wanawanan kwama’am imaim koufair ebit, ana yabowamaim ebi’afuti, Anunin ana kofaninamaim bairi kwabita’ay, gewasin kwasisinaf naatu ebiwan babani.
2 tsono tsirizani chimwemwe changa pokhala amaganizo ofanana, achikondi chimodzimodzi, amodzi mu mzimu ndi acholinga chimodzinso.
2 Imih ayu abifefeyani, akokok anot ta’imon namatar, a yabow itinin ta’imon, ayub nita’imon a dubir ta’imon kwanayai kwanabow saise ayu au yasisir nan na’asa’ub.
3 Musachite kalikonse ndi mtima odzikonda chabe kapena odzitukumula chabe. Koma khalani odzichepetsa ndipo aliyense aziona mnzake ngati womuposa iyeyo.
3 Men akokok kabat ana naniyan nabonawiy sawar hai yabih en isah nakura’ah kwani’o’orotomih, baise kwanayara’iyi taituwa hai gewasin i kwanabora’ah isan kwanao.
4 Musamangofuna zokomera inu nokha koma aliyense azifuna zokomeranso ena.
4 Kwa ta’ita’imon men kwa a gewasin isan kwananuwetamih, baise taituwa hai gewasin isan kwananuwet.
5 Pa ubale wanu wina ndi mnzake, mukhale ndi mtima wofanana ndi wa Khristu Yesu:
5 i Keriso ananotabe kwananot.
6 Iyeyu, pokhala Mulungu ndithu,
6 Keriso i God hairi hai itinin ta’imon.
7 Koma anadzichepetsa kotheratu
7 Nati efanin, i anakok etei’imak yara’iyen,
8 Ndipo pokhala munthu choncho
8 ana itinin orot na’atube tufuw,
9 Choncho Mulungu anamukweza Iye kukhala wapamwamba kwambiri,
9 Nati isan God bai efan auyomtoro’ot itin, naatu wabin bitin i wab etei natabirih.
10 kuti pakumva dzina la Yesu, bondo lililonse limugwadire,
10 Imih, sabuw tutufin etei,
11 ndipo lilime lililonse livomereze kuti Yesu Khristu ndi Ambuye
11 Tamat God aiwob hinitin wabin hinabora’ara’ah,
12 Tsono, abwenzi anga okondedwa, monga mwakhala omvera nthawi zonse, osati pamene ndinali nanu pokha, koma tsopano koposa pamene ndili kutali. Pitirizani kugwira ntchito ya chipulumutso chanu mwa mantha ndi kunjenjemera,
12 Isan imih au ofonah, bairi tama’am ana veya mar etei fanau kwabaib na’atube boun yumatau kwaboboyouw ana veya fanau kwanab. Naatu bir kakaf auman a yawas kwabaib isan kwana’onofar, kwanabow a yawas yomanin kwana’asa’ub.
13 pakuti ndi Mulungu amene amagwira ntchito mwa inu kuti mufune ndi kuchita zimene zimamukondweretsa Iyeyo.
13 Anayabin God i mar etei kwa wanawananamaim ebowabow, saise i boro kwa nakumamat i ana kokomaim kwanabow asinaf gewasih yayakitifuw kwana’as’obow. Menatan i anakok kwanabow kwanan.
14 Muzichita zonse mosawiringula kapena mosatsutsapo,
14 Sawar etei kwasisinaf i men eregamin naatu osukwaraben auman kwanasinafumih.
15 kuti mukhale wopanda cholakwa ndi angwiro, ana a Mulungu wopanda cholakwika mu mʼbado uno wachinyengo ndi wosocheretsa. Mukatero mudzawala pakati pawo ngati nyenyezi zakumwamba
15 Saife kwa boro aur ubar en, uhew bitan God natunatun aurih kakafin en, sasouwi na’atube tafaram sabuw kakafih tenagogor wanawanahimaim kwanama. Naatu daman na’atube maramaim kwanakusisiar.
16 powawuza mawu amoyo. Ndipo ine ndidzatha kunyadira pa tsiku la Khristu kuti sindinathamange kapena kugwira ntchito pachabe.
16 Naatu umamaim yawas ana tur kwanabotan, saise Keriso ana Veya’amaim ayu boro anao ra’ara’at anayabin ayu abow rarou’u bababan i men yabin enamih.
17 Koma ngakhale ndikuthiridwa ngati nsembe ya chakumwa yoperekedwa pa nsembe ndi pa utumiki wochokera mʼchikhulupiriro chanu, ndine wokondwa ndi wosangalala pamodzi ndi inu nonse.
17 Kwa a baitumatum sibor na’atube kwanayai God isan kwanabowabow ayu au rara kwa asibor tafanamaim nasuwa nare’er, ayu i boro kwa etei isa aniyasisir men kikimin ta.
18 Chomwechonso, inu khalani okondwa ndi osangalala nane pamodzi.
18 Naatu kwa auman kwanakawasa ayu bairit taniyasisir.
19 Ngati Ambuye Yesu alola, ndikukhulupirira kuti ndidzamutuma Timoteyo msanga kwanuko, kuti mwina ndingadzasangalale ndikadzamva za moyo wanu.
19 Ayu anotanot Regah Jesu au not nabibasit na’at Timothy boro’omo kwa isa aniyun nan, saise kwa a tur nab nan nao ananonowar boro imaim nakumamatu au fair anab maiye.
20 Ndilibenso wina monga iyeyu amene ali ndi chidwi chenicheni pa za moyo wanu.
20 Timothy ai’itin i men orot afa na’atube, i akisinamo kwa ama isan i enotanot gagamin maiyow.
21 Pakuti aliyense amangofuna zokomera iye yekha osati zokomera Yesu Khristu.
21 Iti ao anayabin, orot afa i taiyuwih hai gewasin akisin isan tenotanot, men Jesu Keriso ana bowabow baira’atin isan tenotanotamih.
22 Koma inu mukudziwa kuti Timoteyo wadzionetsa yekha, chifukwa watumikira ndi ine pa ntchito ya Uthenga Wabwino monga mwana ndi abambo ake.
22 Baise Timothy ana bowabowamaim biturobe i kwa kwaso’ob. Orot natun hairi tita’imon tebowabow na’atube ayu natu Timothy airi ai baibaisbonen tur gewasin isan abowabow.
23 Choncho ndikuyembekezera kumutuma msanga ndikangodziwa mmene zinthu zanga ziyendere.
23 Isan imih anotanot ayu isou mi’itube hina’o na’at Timothy boro aniyun nan kwa ninanawani.
24 Ndipo ndikukhulupirira kuti Ambuye akalola ine mwini ndidzafikanso kwanuko posachedwapa.
24 Naatu abitumatum Regah wabinamaim ayu taiyuwu boro anan aninanawan ana’iti.
25 Koma ndikuganiza kuti nʼkofunika kuti ndikutumizireni mʼbale wanga Epafrodito, mtumiki mnzanga ndi msilikali mnzanga, amenenso ndi mtumiki wanu amene munamutumiza kuti adzandithandize pa zosowa zanga.
25 Baise boun Epafaroditas ayu taiu, na’atube bow turou, tur gewasin ana baiyowayan orot gewasin, naatu kwa a tur bow remorayan, kwaiyafar na ayu bibaisu isan i anotanot ana ef nama’am na’at boro aniyafar maiye kwa isan nan.
26 Pakuti akukulakalakani nonsenu ndipo akusauka mu mtima chifukwa munamva kuti akudwala.
26 Anayabin kwa ayumat itinin isan ma ekakaibababan, naatu sawow inu’in ana tur kwanonowar isan ana yababan ra’at.
27 Zoonadi ankadwala ndipo anatsala pangʼono kumwalira. Koma Mulungu anamuchitira chifundo, ndipo sanangomuchitira chifundo iye yekhayu komanso ine, kuti chisoni changa chisachuluke.
27 Tur anababatun i sawow kafa’imo tamorob, baise God kabibir yawas itin, men i akisin baise ayu auman kabibiru, anayabin i men kok boro au yababan tafan taya’abar atarerey ati’akir.
28 Choncho khumbo langa lofulumiza kumutumiza lakula, kuti pamene mumuonenso musangalale komanso kuti nkhawa yanga ichepe.
28 Isan imih ayu au naniyan gagamin i akokok aniyafar kwa isa nan, saise ana yumat kwana’itin maiye kwaniyasisir, naatu ayu au yababan nasawar.
29 Mulandireni mwa Ambuye ndi chimwemwe chachikulu, ndipo anthu onga iyeyu muziwachitira ulemu.
29 Regah wabinamaim kwaniyasisir ana merar kwanay kwanab, orot gagamih hai merar kwayi kwarusagiyih kwabubuwih na’atube.
30 Iyeyu anatsala pangʼono kufa chifukwa cha ntchito ya Khristu, anayika moyo pa chiswe kuti akwaniritse thandizo limene inu simukanatha.
30 Anayabin Keriso ana bowabow isan kafa’imo tamorob, ana yawas kwahir kwa ayu kwatibibaisu efanin ayu ibaisu.
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Filipenses 2, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.