Filipenses 1
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Paulo ndi Timoteyo, atumiki a Khristu Yesu.
1 Ayu Paul Timothy airi i Keriso Jesu ana’akir wairafi. God ana sabuw etei Keriso Jesu wanawananamaim kwaikofan nati Philipi kwama’am naatu kwa Nutetenayah, baibaisayah bairi a fef iti abiyafar. Paul diburumaim fef kirum baiyowayan bat i’itin|alt="Paul writing in prison" src="CN02069B.TIF" size="span" loc="Php 1.1" copy="©1978 David C. Cook Publishing Co." ref="1.1"
2 Chisomo ndi mtendere zochokera kwa Mulungu Atate athu ndi Ambuye Yesu Khristu zikhale kwa inu.
2 Manaw kabeber Tamat Godane naatu ata Regah Jesu Keriso’one kwa etei isa nama.
3 Ndimayamika Mulungu wanga nthawi zonse ndikakumbukira inu.
3 Ayu au God ana merar ayiy ana veya mar etei kwa anunuhi.
4 Mʼmapemphero anga onse opempherera inu, nthawi zonse ndimapemphera ndi chimwemwe
4 Matan fufur au yoyobanamaim, ayu mar etei ereyasisir kwa etei isa ayoyoyoban.
5 chifukwa mwakhala mukundithandiza polalikira Uthenga Wabwino kuyambira tsiku loyamba mpaka tsopano.
5 Anayabin tur gewasin wantoro’ot abai ana biyat atitit ana veya, kwa a baibais kwaitu bairi iti tur tafaram tanan iti boun tatit.
6 Sindikukayika konse kuti Iye amene anayamba ntchito yabwino mwa inu adzayipitiriza ndi kuyimaliza mpaka pa tsiku la kubweranso kwa Khristu Yesu.
6 Naatu ayu i abitumatum, God iti bowabow gewasin kwa wanawananamaim bubusuruf boro nabow nan yomanin na’asa’ubibo Keriso Jesu ana veya natit.
7 Kwa ine ndi bwino kuti ndiziganiza zotere za nonsenu, popeza ndimakukondani, ngakhale ndikhale mʼndende, kapena pamene ndikuteteza ndi kukhazikitsa Uthenga Wabwino, inu nonse mumagawana nane chisomo cha Mulungu.
7 Kwa i mar etei ayu dogorou’umaim kwama’am, naatu au naniyan iti na’atube mar etei kwa isa anotanot, anayabin dibur baremaim, o tur gewasin awawasfarimaim, o aitafofor tur ao’orerebamaim. Kwa etei i ayu bairit God ana manaw ana kabeber tafafarambonen.
8 Mulungu angandichitire umboni kuti ndimakulakalakani ndi chikondi cha Khristu Yesu.
8 Ayu dogorou wanawanan au naniyan tutufin etei Keriso ekukura’ara’ah na kwa iti isan, God i etei so’ob, ayu men abifuwen.
9 Ndipo pemphero langa ndi lakuti chikondi chanu chipitirire kukulirakulira pa chidziwitso ndi kuzama mʼmaganizo,
9 Ayu ayoyoyoban kwa a yabow i akokok tafan nayababar nara’at, anot hinarerekab, naatu turobe hai naniyah etei kwanaso’ob gewas,
10 kuti mukhoza kuzindikira chabwino koposa zonse ndi chiti kuti muthe kukhala wopanda chodetsa ndi wopanda chilema kufikira tsiku la Khristu.
10 saise kwa tur nowar fufunin gewas yabuna’in isan boro kwanasinaf gewas. Naatu Keriso ana Veya’amaim kwa boro aur ubar en sasouwi kwanabat.
11 Ndipo moyo wanu udzakhala odzazidwa ndi chipatso cha chilungamo chimene chimachokera mwa Yesu Khristu. Pakuti zimenezi zidzapereka ulemerero ndi matamando kwa Mulungu.
11 Naatu roumutufuren ana ro’on gewasih Jesu Keriso’one hinanan boro dogor wanawanan nare naatu imaim kwa boro God merarayow kwanitin kwanabora’ara’ah.
12 Tsopano abale, ndikufuna mudziwe kuti chimene chandichitikira ine chathandiza kwambiri kupititsa patsogolo Uthenga Wabwino.
12 Taitu tuwai’inah, ayu akokok kwanaso’ob, sawar abistan isou himamatar imaim Tur Gewasin ibais ra’at etatasasar.
13 Chotsatira chake nʼchakuti zadziwika bwino lomwe kwa onse amene ali ku nyumba yaufumu kuti ine ndili mʼmaunyolo chifukwa cha Khristu.
13 Sinaf ana itinin iti’imaim aiwob orot ana bar wanawanan ana kaifenayah naatu sabuw afa nati’imaim hima’am auman hiso’ob, ayu i Keriso ana bowayan orot, imih hifatumu.
14 Moti chifukwa cha maunyolo angawa, abale ambiri alimbikitsidwa kuyankhula Mawu a Mulungu molimbika ndi mopanda mantha.
14 Ayu dibur arurumaim taituwau iyab Regah wanawananamaim hima’ama moumurihika koufair hibai himisir hitafofor God ana tur tibibinan.
15 Nʼzoonadi kuti ena amalalikira Khristu chifukwa cha kaduka ndi mikangano, koma ena chifukwa cha zolinga zabwino.
15 Binanuyah i turobe Keriso isan tebibinan, baise afa dogoroh wanawanan i geg bobowen ayu isou ma auman tibibinan, naatu afa i not gewasinamaim tebibinan, anayabin tekokok ayu hinibaisu.
16 Olalikira ndi zolinga zabwinowa amachita izi mwachikondi, podziwa kuti ine ndili muno chifukwa cha kuteteza Uthenga Wabwino.
16 Iti binanuyah i yabowamaim bonawiyih tebibinan, anayabin ayu Tur Gewasin atafafar isan dibur ama’ama i hiso’ob.
17 Ena aja amalalikira Khristu modzikonda osati moona mtima namaganiza kuti kutero kubweretsa mavuto pamene ndili mʼmaunyolo.
17 Binanuyah afa Keriso isan tibibinan baise geg bobowenamaim tibibinan, anayabin tekokok hinasinaf ayu dibur baremaim yababan anab isan.
18 Nanga kodi zimenezo zili ndi ntchito? Chofunika ndi chakuti Khristu alalikidwe, kaya ndi mwachinyengo kapena moona. Ndipo ndikukondwera chifukwa cha chimenechi.
18 Baise ayu nati isan men anotanot! Anayabin binanuyah not gewasinamaim tibibinan o geg bobowenamaim tibibinan, ana’an gagamin Keriso ana tur gewasin i hibinan sabuw tenonowar isan ayu abiyasisir, naatu boro mar etei aniyasisir.
19 pakuti ndikudziwa kuti chifukwa cha mapemphero anu ndi thandizo lochokera kwa Mzimu wa Yesu Khristu, zimene zandionekera zidzathandiza kuti ndimasulidwe.
19 Anayabin kwa ayoyobanamaim naatu Jesu Keriso Anunin ana baibaisamaim ayu aso’ob iti biyababanane boro nabotaitu anatit.
20 Ndili ndi chiyembekezo chonse kuti sindidzachita manyazi ndi pangʼono pomwe, koma ndidzakhala ndi chilimbikitso chokwanira kuti monga mwa nthawi zonse, tsopano Khristu adzakwezedwa mʼthupi langa kaya ndi mʼmoyo kapena mu imfa.
20 Ayu au naniyan tutufin etei nuhufot ama akakaif wanawanan boro men kafa’imo ef ta’amaim anasinaf kakaf biya’ohow anabaimih, en baise, biyou yawasin ema’ama o biyou emomorob, ayu boro mar etei anitafofor anabinan sabuw etei Keriso hinarusagisagiy.
21 Pakuti kwa ine kukhala moyo ndi Khristu ndipo kufa ndi phindu.
21 Anayabin yawasu ama’am i Keriso isan ama’am, naatu anamomorob na’at au gewasin i gagaminaka ema’am.
22 Ngati nditi ndipitirire kukhala ndi moyo mʼthupi ndiye kuti kwa ine ndi kugwira ntchito yopindulitsa. Kodi ndisankhe chiyani? Sindikudziwa.
22 Biyau yawasin anama’am na’at, Regah isan boro ana ma anabow, baise men aso’ob boro menatan anarubin?
23 Ndathinidwa ndi zinthu ziwirizi: Ndikulakalaka kunyamuka kuti ndikakhale ndi Khristu, chimene ndi chinthu chabwino kwambiri.
23 Ayu i sawar rou’ab hitarsibu. Baise ayu au kok gagamin i ata morob Keriso airi atama i igewasin kwanekwan.
24 Komanso nʼkofunika kwambiri kuti ndikhalebe mʼthupi chifukwa cha inu.
24 Naatu baise gewasin anababatun i yawasu anama, saise kwa anibaisi.
25 Ndili ndi chitsimikizo, ndikudziwa kuti ndidzakhala ndi moyo ndipo ndidzapitirira nanu kuti nonse mupite mʼtsogolo ndi kukhala ndi chimwemwe mu chikhulupiriro
25 Tur anababatun a tur ao’owen, aso’ob boro yawasu anama kwa etei anibaisi a baitumatum wanawanan kwanara’at kwanayen kwaniyasisir,
26 kuti pokhala nanunso, kudzitamandira kwanu mwa Khristu Yesu kudzasefukire chifukwa cha ine.
26 saise ayu anabinanawani maiye, kwa boro abisa asisinaf isan Keriso Jesu ana merar kwanay wabin kwanabora’ara’ah.
27 Chilichonse chimene chingachitike, chachikulu nʼchakuti mukhale moyo ofanana ndi Uthenga Wabwino wa Khristu. Tsono ngati ndingabwere kudzakuonani kapena kumangomva za inu ndili kutali, ndidzadziwa kuti mwayima mwamphamvu mwa Mzimu mmodzi, kulimbika pamodzi ngati munthu mmodzi chifukwa cha chikhulupiriro cha Uthenga Wabwino
27 Au not gagamin i iti a tur ao’owen, akokok ama yawasamaim Keriso ana tur gewasin sabuw hinakakafiy. Ayu itimih ananan na’at, o men ananan, ayu akokok kwa a not etei i ta’imon, roun roun kwanabat kwanibaibaisbonen sabuw tur gewasin batkikin isan kwabowabow ana tur ananowar.
28 osachita mantha ndi pangʼono pomwe ndi amene akutsutsana nanu. Ichi ndi chizindikiro kwa iwo kuti adzawonongedwa, koma inu mudzapulumutsidwa ndi Mulungu.
28 Arakit sabuw wanawanah kwanarur na hini’aiseyasey kwanabat, kwa abatkikinamaim nati sabuw gurugurusen wanawanan tirur boro hina’itin hinaso’ob, kwa i boro God yawas nit, naatu i boro nagurusih, iti i God boro nasinaf.
29 Pakuti inu mwapatsidwa mwayi osati ongokhulupirira Khristu kokha, koma wakumva zowawa mʼmalo mwa Khristu.
29 Anayabin God ana baigegewasin it bitit i men baitutumin akisin, baise isan tani’akir auman.
30 Inunso mukudutsa mʼzowawa zomwe zija munaona ndikudutsamo inenso ndipo pano mukumva kuti ndikukumana nazobe.
30 Ayu bairit tama’am ana veya wawainabu i kwa’itin, naatu boun ewawainabu ana tur i kwanonowar, imih kwa wainaben i nati ta’imon wanawanan kwarun ewawainabi.
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Filipenses 1, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.