Ezequiel 40
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs BKJ
1 Kumayambiriro a chaka cha 25, cha ukapolo wathu, tsiku la khumi lamwezi, patapita zaka khumi ndi zinayi mzinda wa Yerusalemu utawonongedwa, pa tsiku lomwelo dzanja la Yehova linali pa ine ndipo Iye anapita nane ku Yerusalemu.
1 No vigésimo quinto ano do nosso cativeiro, no início do ano, no décimo dia do mês, no décimo quarto ano após a cidade ter sido atingida, naquele mesmo dia a mão do SENHOR esteve sobre mim, e me trouxe para lá.
2 Mʼmasomphenyawo Yehova ananditenga ndi kupita nane ku dziko la Israeli ndipo anandiyika pa phiri lalitali kwambiri, moti ndinaona ngati mzinda.
2 Nas visões de Deus ele me trouxe à terra de Israel, e me pôs sobre um monte muito alto, sobre a qual estava como uma estrutura de uma cidade ao sul.
3 Atandifikitsa kumeneko ndinaona munthu wonyezimira ngati mkuwa. Iye anali atayima pa chipata ndipo mʼdzanja lake munali chingwe cha nsalu yabafuta ndi ndodo yoyezera.
3 E ele me levou para lá, e eis que havia ali um homem cuja aparência era como a aparência do bronze, com uma linha de linho na sua mão e uma cana de medir, e ele estava em pé no portão.
4 Munthuyo anandiwuza kuti, “Iwe mwana wa munthu, penyetsetsa ndipo umvetse bwinobwino. Uyikepo mtima wako pa zonse zimene ndikukuonetsa pakuti anakubweretsa kuno kuti uwone zimenezi. Tsono ukawawuze Aisraeli zonse zimene uzione.”
4 E disse-me o homem: Filho do homem, contempla com os teus olhos, e ouve com os teus ouvidos, e põe o teu coração sobre tudo quanto eu te mostrar; porque para que eu pudesse mostrá-lo a ti é que foste trazido aqui; declara tudo o que viste à casa de Israel.
5 Ine ndinaona khoma litazungulira mbali zonse za Nyumba ya Mulungu. Mʼdzanja la munthuyo munali bango lopimira limene kutalika kwake kunali kwa mamita atatu. Atayeza chipupacho anapeza kuti kuchindikira kwake kunali mamita atatu, ndiponso kutalika kwake kunalinso mamita atatu.
5 E, eis um muro do lado de fora da casa ao redor, e na mão do homem uma cana de medir, de seis côvados de comprimento, por um côvado e um palmo; então ele mediu a largura da edificação, uma cana; e a altura, uma cana.
6 Anapita ku chipata chakummawa. Anakwera pa makwerero a nyumbayo, nayeza chiwundo choyamba cha chipatacho; kutalika kwake kunali mamita atatu.
6 Então, ele veio ao portão que olhava em direção ao leste, e subiu suas escadas e mediu a soleira do portão, que tinha a largura de uma cana e a outra soleira do portão que tinha a largura de uma cana.
7 Kudutsa chiwundo choyambachi, panali zipinda za alonda zisanu ndi chimodzi, zitatu kudzanja lamanja, zitatu kudzanja lamanzere. Chilichonse chinali cha mamita atatu mulitali mwake, chimodzimodzinso mulifupi mwake. Mipata ya pakati pa zipindazo inali ya mamita awiri ndi theka. Ndipo chiwundo cha pa chipata pafupi ndi khonde lapachipata, chinali mamita atatu.
7 E cada pequena câmara tinha o comprimento de uma cana, e a largura de uma cana; e entre as pequenas câmaras havia cinco côvados; e a soleira do portão no alpendre do portão por dentro, era de uma cana.
8 Ndipo iye anayeza khonde la chipata ndipo chinali cha mamita atatu.
8 Ele também mediu o alpendre do portão, por dentro, uma cana.
9 Anayeza khonde ndipo linali mamita anayi. Mphuthu zake zinali mita imodzi kuchindikira kwake. Khonde lamʼkati lapachipata linali kumapeto kwenikweni pafupi ndi Nyumba ya Mulungu.
9 Então, mediu o alpendre do portão, oito côvados, e os seus pilares, dois côvados, e o alpendre do portão estava por dentro.
10 Mʼkati mwa chipata chakummawa munali zipinda za alonda zitatu mbali iliyonse. Zitatu zonsezo zinali zofanana, ndipo khonde la pakati pa zipindazo linali lofanana.
10 E as pequenas câmaras do portão em direção ao leste eram três deste lado e três daquele lado; os três eram de uma medida; e os pilares tinham uma medida deste lado e naquele lado.
11 Kenaka anayeza chipata cholowera; mulifupi mwake munali mamita asanu ndipo mulitali mwake munali mamita asanu ndi limodzi ndi theka.
11 E ele mediu a largura da entrada do portão, dez côvados; e o comprimento do portão, treze côvados.
12 Kutsogolo kwa chipinda chilichonse cha alonda kunali khoma lalifupi lotalika theka la mita, ndipo mbali iliyonse ya zipinda za alondazo inali yotalika mamita atatu.
12 E o espaço também diante das pequenas câmaras era de um côvado deste lado, e o espaço era de um côvado daquele lado; e as pequenas câmaras tinham seis côvados deste lado e seis côvados daquele lado.
13 Ndipo anayeza kutalika kwa mulifupi mwa chipata cholowera, kuchokera ku khoma lakumbuyo la chipinda chimodzi mpaka ku khoma la chipinda china; kuchokera ku chitseko mpaka ku chitseko china. Kutalika kwake kunali mamita khumi ndi awiri ndi theka.
13 Então, ele mediu o portão desde o telhado de uma pequena câmara até ao telhado de uma outra; a largura era de vinte e cinco côvados, porta contra porta.
14 Anayezanso khonde lamʼkati ndipo linali la mamita makumi atatu. Ndipo mozungulira khondelo munali bwalo. Muyesowu sukuphatikiza khonde loyangʼanana ndi bwalo.
14 Ele fez também pilares, de sessenta côvados, até o pilar do átrio, ao redor do portão.
15 Kuchokera pa chipata cholowera mpaka ku mapeto a khonde la chipata, kutalika kwake kunali mamita 27.
15 E, desde a face do portão da entrada até a face do alpendre do portão interno, havia cinquenta côvados.
16 Makoma a zipinda ndiponso makoma a pakati pa zipindazo anali ndi mazenera. Khonde lamʼkati linalinso ndi mazenera mʼkati mwake. Pa makoma onsewo anajambulapo zithunzi za kanjedza.
16 E havia ali janelas estreitas para as pequenas câmaras, e para os seus pilares, dentro do portão ao redor, e da mesma forma para os arcos; e as janelas estavam ao redor, para dentro, e sobre cada pilar havia palmeiras.
17 Kenaka munthuyo anandilowetsa mʼbwalo lakunja, ndipo ndinaona zipinda zina ndi msewu wa miyala wozungulira bwalo lonse. Zipinda zonse zinali makumi atatu ndipo zinkayangʼana msewuwo.
17 Então, ele me trouxe ao átrio exterior, e eis que havia ali câmaras, e um pavimento feito para o átrio em redor; trinta câmaras havia sobre o pavimento.
18 Utali wa mulifupi mwa msewuwo unkayenda mamita 27 kufanana ndi utali wa chipata cholowera. Uwu unali msewu wa mʼmunsi.
18 E o pavimento ao lado dos portões defronte o comprimento dos portões era o pavimento mais baixo.
19 Tsono, anayeza kutalika kwa bwalo kuyambira chipata cholowera choyamba mpaka polowera pa chipata chakunja cha bwalo la mʼkati. Kutalika kwake kunali mamita makumi asanu.
19 Então, ele mediu a largura desde a dianteira do portão inferior até a dianteira do átrio interior, por fora, cem côvados, em direção ao leste, e em direção ao norte.
20 Kenaka munthuyo anayeza mulitali ndi mulifupi mwa chipata chimene chimayangʼana kumpoto, chotulukira kunja.
20 E o portão do átrio externo que olhava em direção ao norte, ele mediu o seu comprimento e a sua largura.
21 Zipinda za alonda zimene zinalipo zitatu mbali iliyonse, makoma ake ndi khonde zinali ndi muyeso wofanana ndi wachipata choyamba chija. Kutalika kwake kunali mamita 27 ndipo mulifupi mwake munali mamita 13.
21 E as suas pequenas câmaras eram três deste lado, e três daquele lado, e os seus pilares e os seus arcos eram segundo a medida do primeiro portão: seu comprimento era de cinquenta côvados, e a largura vinte e cinco côvados.
22 Mipata yake, khonde lake ndi zojambula za kanjedza zinali ndi miyeso yofanana ndi za chipata chakummawa. Chipatacho chinali ndi makwerero asanu ndi awiri ndipo kotsirizira kwa chipatacho kunali khonde.
22 E as suas janelas, e os seus arcos, e as suas palmeiras, eram segundo a medida do portão que olhava em direção ao leste; e eles subiam para elas por sete degraus, e os seus arcos estavam diante delas.
23 Panalinso chipata cholowera ku bwalo lamʼkati chofanana ndi chakummawa chimene chimayangʼanana ndi chipata chakumpoto, chofanana ndi cha mbali ya kummawa. Anachiyeza kuchokera ku chipata china mpaka ku chipata china. Kutalika kwake kunali mamita makumi asanu.
23 E o portão do átrio interior estava defronte o portão em direção ao norte, e em direção ao leste; e ele mediu de portão a portão cem côvados.
24 Ndipo munthuyo anapita nane ku mbali yakummwera ndipo ndinaona chipata chakummwera. Iye anayeza mphuthu zake ndi khonde ndipo zinali ndi miyeso yofanana ndi ya zina zija.
24 Então, ele me levou em direção ao sul, e contemplou um portão em direção ao sul, e mediu seus pilares e seus arcos de acordo com estas medidas.
25 Mʼzipinda za chipata cholowera chimenechi ndi mʼkhonde lake munali mipata yofanana ndi ya mʼzipinda zina. Mulitali mwake munali mamita 27, mulifupi mwake munali mamita 13.
25 E havia janelas nele e nos seus arcos ao redor, como aquelas janelas; o comprimento era de cinquenta côvados, e a largura vinte e cinco côvados.
26 Chipatacho chinali ndi makwerero asanu ndi awiri ndi khonde kotsirizira kwake. Chipindacho chinali ndi zojambula za kanjedza ku mbali zonse za makoma.
26 E havia ali sete degraus para subir, e os seus arcos estavam diante deles, e ele tinha palmeiras, uma deste lado, e outra daquele lado, sobre seus pilares.
27 Bwalo lamʼkati linalinso ndi chipata kummwera. Munthuyo analiyeza kuchokera ku chipata chimenechi mpaka ku chipata chakunja. Kutalika kwake kunali mamita makumi asanu.
27 E havia ali um portão no átrio interior em direção ao sul; e ele mediu de portão a portão em direção ao sul, cem côvados.
28 Ndipo munthu uja anandilowetsa mʼbwalo lamʼkati kudzera ku chipata chakummwera. Anayeza chipatachi ndipo chinali chofanana ndi zinzake zija.
28 E ele me levou ao átrio interior pelo portão sul; e mediu o portão do sul, de acordo com estas medidas;
29 Zipinda zake za alonda, makoma ake ndi khonde lake zinali zofanana ndi zina zija. Chipata cholowera ndi khonde lake zinali ndi mipata mʼmbali zonse. Mulitali mwake munali mamita 27 ndipo mulifupi munali mamita 13.
29 e as suas pequenas câmaras, e os seus pilares, e os seus arcos, de acordo com estas medidas; e havia janelas nele e nos seus arcos ao redor; este tinha cinquenta côvados de comprimento, e vinte e cinco côvados de largura.
30 (Khonde lililonse la makonde atatu a zipata zolowera bwalo lamʼkati aja linali la mamita ozungulira mʼbwalo lamʼkati anali mamita 13 mulitali mwake, mamita awiri ndi theka mulifupi mwake).
30 E os arcos ao redor tinham vinte e cinco côvados de comprimento, e cinco côvados de largura.
31 Khonde lake linayangʼanana ndi bwalo lakunja. Pa mphuthu pake anajambulapo zithunzi za kanjedza mbali zonse ziwiri, ndipo linali ndi makwerero asanu ndi atatu.
31 E os seus arcos estavam em direção ao átrio exterior, e havia palmeiras sobre os seus pilares; e a subida para ele tinha oito degraus.
32 Kenaka munthuyo anapita nane ku bwalo la mʼkati mbali ya kummawa, ndipo anayeza chipata cholowera; chinali chofanana ndi zinzake zina zija.
32 E, ele me levou ao átrio interior, em direção ao leste, e mediu o portão de acordo com estas medidas.
33 Zipinda zake za alonda, makoma ake ndi khonde lake zinali zofanana ndi zina zija. Chipata cholowera ndi khonde lake chinali ndi mipata mʼmbali zonse. Mulitali mwake munali mamita 27 ndipo mulifupi mwake munali mamita 13.
33 E as suas pequenas câmaras, e os seus pilares, e os seus arcos, eram de acordo com estas medidas, e havia janelas nela e nos seus arcos ao redor; ele tinha cinquenta côvados de comprimento, e vinte e cinco côvados de largura.
34 Khonde lake linayangʼanana ndi bwalo lakunja. Pa mphuthu pake anajambulapo zithunzi za kanjedza mbali zonse ziwiri, ndipo linali ndi makwerero asanu ndi atatu.
34 E os seus arcos ficavam em direção ao átrio externo; e havia palmeiras sobre seus pilares, deste lado e daquele lado; e a subida para ele tinha oito degraus.
35 Kenaka anapita nane ku chipata chakumpoto ndipo anachiyeza. Chinali chofanana ndi zina zija.
35 Então, me levou ao portão norte, e o mediu conforme estas medidas;
36 Zipinda zake za alonda, makoma ake ndiponso khonde lake zinali zofanana ndi zina zija, ndipo chinalinso ndi mipata mbali zonse ziwiri. Mulitali mwake munali mamita 27 ndipo mulifupi mwake munali mamita 13.
36 as suas pequenas câmaras, os seus pilares, e os seus arcos; e as janelas para ele ao redor; o comprimento era de cinquenta côvados, e a largura de vinte e cinco côvados.
37 Khonde lake limayangʼanana ndi bwalo lakunja. Pa mphuthu zake anajambulapo zithunzi za kanjedza mbali zonse ziwiri, ndipo linali ndi makwerero asanu ndi atatu.
37 E os seus pilares estavam direcionados ao átrio exterior; e havia palmeiras sobre os seus pilares deste lado e daquele lado; e a subida para ele tinha oito passos.
38 Panali chipinda ndipo khomo lake linali pafupi ndi khonde la chipata cholowera chamʼkati. Mʼchipinda mʼmenemo ankatsukira nyama ya nsembe yopsereza.
38 E as suas câmaras e as suas entradas estavam junto aos pilares dos portões onde eles lavavam as suas ofertas queimadas.
39 Pa khonde la chipatacho panali matebulo awiri, lina kuno lina uko. Ankapherapo nsembe zopsereza, nsembe zopepesera machimo ndi nsembe zopepesera kupalamula.
39 E no alpendre do portão havia duas mesas deste lado, e duas mesas daquele lado, para se matar em cima a oferta queimada e a oferta pelo pecado e a oferta pela transgressão.
40 Panali matebulo anayi, awiri a iwo anali kunja kwa khoma la khonde pafupi ndi makwerero olowera pa chipata chakumpoto ndi awiri enawo anali mbali inayo ya makwerero.
40 E do lado de fora, ao subir para a entrada do portão norte, havia duas mesas, e do outro lado, que ficava no alpendre do portão, havia duas mesas.
41 Choncho ku mbali imodzi ya chipata kunali matebulo anayi, ndiponso ku mbali inayo kunali matebulo anayi. Onse pamodzi anali matebulo asanu ndi atatu. Pa matebulopo ankapherapo nyama za nsembe zopsereza.
41 Quatro mesas haviam deste lado, e quatro mesas daquele lado; ao lado do portão, oito mesas, sobre as quais eles matavam seus sacrifícios.
42 Matebulo anayiwa anali a miyala yosema. Lililonse mulitali mwake linali la masentimita 75, mulifupi mwake linali la masentimita 75, ndipo msinkhu wake unali wa masentimita makumi asanu. Pa matebulopo amayikapo zipangizo zophera nsembe zopsereza ndi nsembe zina.
42 E as quatro mesas eram de pedra esculpida para a oferta queimada; de um côvado e meio de comprimento, e um côvado e meio de largura, e um côvado de altura; sobre as quais também se punham os instrumentos com os quais eles matavam a oferta queimada e o sacrifício.
43 Choncho pa matebulopo ankayikapo nyama za nsembe zopsereza. Mbedza zitatu zazitali ngati chikhatho amazikoleka pa makoma pozungulira ponse.
43 E dentro havia ganchos de um palmo de largura, presos ao redor, e sobre as mesas estava a carne da oferta.
44 Munthu uja anapita nane mʼkati mwa bwalo ndipo ndinaona zipinda ziwiri. Chimodzi chinali pafupi ndi chipata chakumpoto kuyangʼana kummwera ndi china chinali pafupi ndi chipata chakummwera kuyangʼana kumpoto.
44 E fora do portão interior estavam as câmaras dos cantores, no átrio interior, que estava ao lado do portão do norte e sua vista ficava em direção ao sul; uma do lado do portão leste tendo a vista em direção ao norte.
45 Munthuyo anandiwuza kuti, “Chipinda chimene chikuyangʼana kummwera ndi cha ansembe amene amayangʼanira Nyumba ya Mulungu,
45 E ele me disse: Esta câmara cuja vista está virada para o sul é para os sacerdotes, os guardiões encarregados pela casa.
46 ndipo chipinda chimene chikuyangʼana kumpoto ndi cha ansembe amene amayangʼanira guwa lansembe. Amenewa ndiwo ana a Zadoki, ndipo ndi okhawo mwa zidzukulu za Levi amene ayenera kutumikira pamaso pa Yehova mʼNyumba ya Mulungu.”
46 E a câmara cuja vista está virada para o norte é para os sacerdotes, os guardiões encarregados do altar; estes são filhos de Zadoque dentre os filhos de Levi, que se aproximam do SENHOR para ministrarem para ele.
47 Kenaka munthuyo anayeza bwalo; linali lofanana mbali zonse kutalika kwake, mulitali mwake munali mamita 53, ndipo mulifupi mwake munali mamita 53. Ndipo guwa lansembe linali kutsogolo kwa Nyumba ya Mulungu.
47 Então, ele mediu o átrio; cem côvados de comprimento e cem côvados de largura, quadrangular; e o altar que estava diante da casa.
48 Munthuyo anapita nane pa khonde la Nyumba ya Mulunguyo. Anayeza mphuthu za khondelo ndipo zinali mamita awiri ndi theka mbali zonse. Mulifupi mwa chipatacho munali mamita asanu ndi awiri ndipo mulifupi mwa makoma ake munali mamita awiri mbali zonse.
48 E me levou ao alpendre da casa, e mediu a cada pilar do alpendre, cinco côvados deste lado, e cinco côvados daquele lado; e a largura do portão era de três côvados deste lado, e três côvados daquele lado.
49 Mulitali mwa khonde munali mamita khumi, mulifupi mwake munali mamita asanu ndi limodzi kuchokera kutsogolo mpaka kumbuyo. Panali makwerero khumi, ndipo mbali zonse kunali nsanamira.
49 O comprimento do alpendre era de vinte côvados, e a largura de onze côvados, e ele me levou pelos degraus por onde se subia a ele; e ali havia pilares junto aos pilares, um deste lado e outro daquele lado.
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Ezequiel 40, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.