Efésios 4

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI

Sair da comparação
AAI TUR GEWASIN O BAIBASIT BOUBUN
1 Ine monga wamʼndende chifukwa chotumikira Ambuye, ndikukulimbikitsani kuti mukhale moyo woyenera mayitanidwe amene munalandira.
1 Ayu i Regah wabinamaim dibur arun ama’ama, imih kwa ao’ototofari, God ayawas ya’asair eaf kwana kwabaib imaim kwanama.
2 Mukhale odzichepetsa kwathunthu ndi ofatsa; mukhale oleza mtima, ololerana wina ndi mnzake mwachikondi.
2 Mar etei taiyuw kwanayara’iyi, kwanakakaf, yatenanub, yabowamaim taituwa kwanabuwih.
3 Muyesetse kusunga umodzi wa Mzimu; umodzi umene umatimangirira pamodzi mu mtendere.
3 Anun Kakafiyin buwi kwana bita’imoni i kwanasinaftobon a kou’ay nati i kwanabukikin tufuwamaim kwanama.
4 Pali thupi limodzi ndiponso Mzimu mmodzi, monganso pali chiyembekezo chimodzi chimene anakuyitanirani.
4 Biyat i ta’imon, Anun Kakafiyin i ta’imon, God ea’afit i nuhifot ta’imon tabai,
5 Pali Ambuye mmodzi, chikhulupiriro chimodzi, ubatizo umodzi;
5 Regah i ta’imon, baitumatum i ta’imon, bapataito i ta’imon.
6 Mulungu mmodzi ndi Atate a onse, ndipo ali mwa onse.
6 Naatu God i ta’imon, sabuw tutufin etei’imak Tamat, naatu iti etei’imak ata ukwarin, Regah ta’imon, etei’imak wanawanatamaim ebowabow, naatu wanawanatamaim ema’am.
7 Koma aliyense wa ife wapatsidwa chisomo molingana ndi muyeso wa mphatso ya Khristu.
7 It ta’ita’imon manaw kabeberamaim Keriso ana usar bitit i ra’at naatu igewasin kwanekwan.
8 Nʼchifukwa chake akunena kuti,
8 Buk Atamaninamaim iti na’atube eo,
9 Kodi mawu akuti, “Iye anakwera” akutanthauza chiyani, ngati Iyeyo sanatsikire kunsi kwa dziko lapansi?
9 Tur iti, “Yen Auyom.” Ana’an i iti, wantoro’ot i marane ra’iy, re anababatun me wanawanan run.
10 Iye amene anatsika ndi yemweyo anakwera koposa mʼmayiko a kumwamba onse, ndi cholinga choti zinthu zonse zikhale zodzaza ndi Iye.
10 Imih orot nati taiyuwin yara’iy re’er, nati orot ta’imon yen auyomtoro’ot tit, naatu mar ana hanef etei natabir rabon mar tafaram tutufin etei ana’itinin bai karatan.
11 Iye ndiye amene anapereka mphatso kwa ena kuti akhale atumwi ndi ena aneneri, ena alaliki, ndi ena abusa ndi aphunzitsi.
11 Naatu i taiyuwin siwar bow orot ta ta faramih, orot afa tur abarayah himatar, afa dinab tur faramayah himatar, afa binanuyah himatar, afa Kirisiyan hai bonawiyenayah himatar, naatu afa bai’obaiyenayah himatar,
12 Ntchito yawo ndi kukonza oyera mtima kuti agwire ntchito ya utumiki kuti thupi la Khristu lilimbikitsidwe.
12 saise God ana sabuw tatabobuna’ih bowabow ana ef hitaso’ob. Naatu bowabow tataburiri tatabow Keriso biyan tatawowab tara’at tayen
13 Izi zidzatifikitsa tonse ku umodzi wachikhulupiriro, kumudziwa Mwana wa Mulungu, kukhwima msinkhu ndi kufika pa muyeso wangwiro weniweni wopezeka mwa Khristu.
13 tanan it etei ata baitumatum an ta’imon tamatar. Naatu God Natun ana kirikirifot tataso’ob gewas, wanawanat takwat Keriso ana tutufin tatab.
14 Motero sitidzakhalanso makanda, ogwedezekagwedezeka ndi mafunde, otengekatengeka ndi mphepo iliyonse ya chiphunzitso ndi kuchenjera kwa anthu achinyengo amene amasocheretsa anthu ndi kuchenjera kwawo.
14 Saise it boro men kek na’atube tatama’am, sabuw baifufuwenayah hitan hitifufuwit ata baitumatum hitiyuwiyuwimih. Kotar yabat nane ebabin ebiyuwiyuwibe. Anayabin sabuw hai notamaim baifuwen tur afa himataren sabuw afa hifufuwih hinawiyih sa’ab tenan.
15 Mʼmalo mwake, poyankhula choonadi mwachikondi, tidzakula mu zinthu zonse ndi kukhala thupi la Khristu, amene ndi Mutu, omwe ndi mpingo.
15 En baise nati efanin, yabowamaim tur anababatun tanao, ef tata’ane ata orot ukwarin Keriso wanawananamaim tanawowabit tanayen.
16 Mwa Iye thupi lonse lalumikizidwa ndi kugwirana pamodzi ndi mitsempha yothandizira. Likukula ndi kudzilimbitsa lokha mwachikondi, pomwe chiwalo chilichonse chikugwira ntchito yake.
16 I ana bainakokomaim biyat tutufin etei bai na ikokofan wowab gewas. Naatu biyat hai bowabow Regah bitih na’atube tebowabow ana veya biyat i erara’at naatu yabowamaim ewowowab gewas.
17 Tsono ine ndikukuwuzani izi, ndipo ndikunenetsa mwa Ambuye, kuti musayendenso monga amachitira anthu a mitundu ina potsata maganizo awo opanda pake.
17 Regah ana onowatenamaim ayu kwa abimatnuwi, Eteni Sabuw tema’am na’atube men kwanama’amih, anayabin nati sabuw i hai not hikwaris koko’awabe tema’am.
18 Maganizo awo ndi odetsedwa, ndi osiyanitsidwa ndi moyo wa Mulungu chifukwa cha umbuli umene uli mwa iwo chifukwa cha kuwuma mtima kwawo.
18 Hai not etei i gugumin awan karatan, God ana yawasamaim i hitabaratait nabin anababatun tebatabat, anayabin ukwarih i hifokar naatu dogoroh hikabay.
19 Popeza sazindikiranso kanthu kalikonse, adzipereka okha kuti akhumbe zonyansa, kuti achite mtundu uliwonse wa zoyipa ndi zilakolako zosatha.
19 Biya’ohow naniyan i men kafai hiso’ob, hai yawas tutufin etei kakafin nowanamih hitin bai susuw, naatu in sesebar teo’onofar.
20 Koma inu simunadziwe Khristu mʼnjira yotere.
20 Baise kwa i men iti na’atube hi’obaiyi kwana Keriso kwasu’ubimih.
21 Zoonadi munamva za Iye ndipo munaphunzitsidwa mwa Iye molingana ndi choonadi chimene chili mwa Yesu.
21 Kwa Keriso isan i hio kwanowar, naatu Turobe yawas gewasin Jesu wanawananamaim ema’ama isan i hi’obaiyi.
22 Inu munaphunzitsidwa molingana ndi moyo wanu wakale, kuchotsa umunthu wakale, umene ukupitirira kuwonongeka ndi zilakolako zachinyengo;
22 Imih kanab atamanin nawiyi yawas kakafih, baifufuwen in kura’ara’ahi kwasinaf gugurusi, nati kanab atamanin i kwanikiya’ub kwanabosair.
23 kuti mukonzedwe mwatsopano mʼmitima mwanu;
23 Dogor naatu a not etei i kwanabow kwaniwa’an boubuh hinamatar,
24 ndi kuti muvale umunthu watsopano, wolengedwa kuti ufanane ndi Mulungu mu chilungamo chenicheni ndi chiyero.
24 naatu kanab boubun God ana’itininabe wowab yai inu’in i kwanab kwaniyoun, saise yawas anababatun, ana ef mutufor naatu kakafiyin boro imaim nirerereb.
25 Chifukwa chake, aliyense wa inu aleke kunama ndipo ayankhule zoona kwa mʼbale wake, pakuti ife tonse ndife ziwalo za thupi limodzi.
25 Naatu baifufuwen i kwanihamiy, taituwa isah i turobe hai tur kwana’owen, anayabin it etei tana taita’imon Keriso biyan tamatar.
26 Kwiyani koma musachimwe. Dzuwa lisalowe mukanali chikwiyire.
26 Ya nasoso’ar na’at, men yaso’ar nabonawiyi bowabow kakafin inasinaf. Naatu men yaso’ar auman inama nan veya nare.
27 Musamupatse mpata Satana.
27 Men Demon Mowan veya nati’imaim initin narunamih.
28 Iye amene wakhala akuba asabenso, koma agwire ntchito ndi kuchita kenakake kaphindu ndi manja ake, kuti akhale ndi kenakake kogawana ndi amene akusowa.
28 Orot yait ebabain, i bain nihamiy naatu nabusuruf nabow, saise ma gewasin nab nama gewas. Naatu sabuw yababan wairafih nibaisih.
29 Mʼkamwa mwanu musatuluke mawu aliwonse onyansa, koma okhawo amene ndi othandiza kulimbikitsa ena molingana ndi zosowa zawo, kuti athandize amene akawamve.
29 A tur men womararin ina’omih, baise baibais ana tur gewasin inao, saise sabuw baibais abisa tekokok boro hinab nawowabih hinara’at. Naatu sabuw iyab tur tenonowar boro nibaisih.
30 Ndipo musamvetse chisoni Mzimu Woyera wa Mulungu amene mwasindikizidwa naye chizindikiro cha tsiku la kuwomboledwa.
30 Naatu God Anun Kakafiyin men yababan kwanitin. Anayabin Anun Kakafiyin i God ana’i’inanen wanawanatamaim ema’am it i nowan. Saise nati Veya gagamin nanan ana veya it boro narufamit nabotaitit tanatit.
31 Chotsani kuzondana, ukali ndi kupsa mtima, chiwawa ndi kuyankhula zachipongwe, pamodzi ndi choyipa chilichonse.
31 Imih dogor wanawanan tenakuyakuy, gagamat, yaso’ar, okwanekwan naniyah kakafih ta ta etei kwanihamiyen.
32 Mukomerane mtima ndi kuchitirana chifundo wina ndi mnzake. Khululukiranani wina ndi mnzake, monga momwe Mulungu anakukhululukirani mwa Khristu.
32 Naatu nati sawar efanih, kwa i taituwa etei isah kwanamanaw kwanakabeber, kwaniwanbabanih. Naatu notawiyen isa nama, Jesu Keriso ana bowabowamaim God notanotawiyit na’atube.

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Efésios 4, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.