Efésios 2
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Kunena za inu, kale munali akufa chifukwa cha zolakwa zanu ndi machimo anu,
1 Marasika kwa ayub i himorob, anayabin kwa afanasair i ra’at, naatu a bowabow kakafih auman i ra’at.
2 mmene inu munkakhalamo pamene munkatsatira njira za dziko lapansi ndi za ulamuliro waufumu wa mlengalenga, mzimu umene ukugwira ntchito tsopano mwa amene samvera.
2 Nati ana veya’amaim kwa i tafaram ana yawas kakafin buw dogor wanawanan bowabow kakafin awan karatan, gagub wanawanan afiy hai bonawiyenayan fanah kwabai kwabi’ufununih, naatu boun nati afiy kakafih i hima sabuw hinawiyih God tibifanasair.
3 Nthawi ina tonsefe tinalinso ndi moyo wonga wawo, tinkachitanso zilizonse zimene matupi ndi maganizo athu ankafuna. Mwachibadwa chathu, tinali oyenera chilango monga anthu ena onse.
3 Marasika it auman ata yawas i nati sabuw hai yawasabe wanawanahimaim bairi tama, biyat ana kok naatu ata not kakafih abisa sinafumih tanotanot i tasisinafumo. Naatu nati yawas atamanin biyat ana kokomaim tama tasisinaf God ana baimakiy sabuw afa baitihimih bobogaigiwas it auman boro tatab.
4 Koma chifukwa cha chikondi chake chachikulu pa ife, Mulungu amene ndi olemera mʼchifundo,
4 Baise God ana kabeber i ra’at karsuwei, naatu ana yabow it isat i ra’at kwanekwan,
5 anatipanga kukhala amoyo ndi Khristu ngakhale pamene ife tinali akufa mu zolakwa zathu. Koma tinapulumutsidwa mwachisomo.
5 basit it ata kakafihine God fanan tasair ayubit morob. Baise God buwit tana Keriso wanawananamaim tarun yawas itit. Iti i God ana bosiyasiyaramaim kwa yawas kwabai.
6 Ndipo Mulungu anatiukitsa pamodzi ndi Khristu ndi kutikhazika pamodzi ndi Iye mmwamba mwa Khristu Yesu,
6 Naatu God Keriso Jesu bobora’ah ana maramaim, it i wanawananamaim bairit bora’ahit tayen bairi tabi’aiwob,
7 ndi cholinga chakuti mʼnthawi imene ikubwera, Iyeyo adzaonetse chuma choposa cha chisomo chake, choonetsedwa mwa kukoma mtima kwake kwa ife mwa Khristu Yesu.
7 saise God ana kabeber wanatowanin etei iti Jesu Keriso wanawananamaim ana yabow i’obaiyit ta’itin.
8 Pakuti mwapulumutsidwa mwachisomo, kudzera mʼchikhulupiriro ndipo izi sizochokera mwa inu eni, koma ndi mphatso ya Mulungu,
8 Anayabin God ana manaw ana kabeberamaim kwa kwaitumatum yawas kwabai. Men kwa raro bababanamaim yawas kwabaimih, baise God ana siwar kwa isa.
9 osati ndi ntchito, kuti wina aliyense asadzitamandire.
9 Men a bowabowamaim kwabai, imih men yait ta iti yawas isan nao ra’ara’atamih.
10 Pakuti ndife ntchito ya Mulungu, olengedwa mwa Khristu Yesu kuti tichite ntchito zabwino, zimene Mulungu anazikonzeratu kale kuti tizichite.
10 Anayabin it etei i God ana bowayah sabuw, God sinafit Keriso Jesu wanawanan tarun ta’imon tamatar, God bowabow gewasih bowamih marasika yayakitifuw i tanabow.
11 Chifukwa chake kumbukirani kuti poyamba inu amene munali anthu a mitundu ina mwachibadwa ndipo munkatchedwa “osachita mdulidwe” ndi amene amadzitcha okha “a mdulidwe” (zimene zinachitika mʼthupi ndi manja a anthu).
11 Marasika kwa a tufuwamaim i Ufun Sabuw, “A’ar mo’oh tutufih kwatufuw, imih Jew sabuw kwa isa i men God ana sabuw hirouw hio’omih, anayabin kwa a’ar kanabih i men hi’afuw, baise Jew sabuw hai a’ar kanabih i afu’afuw, (nati i ibo hai kwafirin ana baimonok imih orot isah tisisinaf) kwa marasika mi’itube kwama’am i kwananot.
12 Kumbukirani kuti nthawi imene inu munali wopanda Khristu, simunkawerengedwa ngati nzika za Israeli ndipo munali alendo pa pangano la lonjezo, wopanda chiyembekezo ndi opanda Mulungu mʼdziko lapansi.
12 Nati ana veya’amaim kwa i Keriso biyanamaim kusibi kwatit, naatu Israel hai baibasit ana fef men kwabai, tauman sabuw obaibasit ana omatanen ufunane kwama’ama. Naatu men kafa’imo sawar ta boro uf nan isan kwanot nuhifot kwama’amamih, aur God en asir kwama’am kwanekwan.
13 Koma tsopano mwa Khristu Yesu, inu amene nthawi ina munali kutali, mwabweretsedwa pafupi kudzera mʼmagazi a Khristu.
13 Baise boun Keriso Jesu wanawananamaim kwa iyab marasika nabineika kwama’am, Keriso morob ana rara re’ere imaim kwa buwi kwana kwaiyubin.
14 Pakuti Iye mwini ndiye mtendere wathu, amene anachita kuti awiri akhale mmodzi ndipo anagumula chotchinga, khoma la udani lotilekanitsa,
14 Anayabin Keriso taiyuwin biyanamaim ma toutuman ana fur tarakwib itaiy re, tufuw bai tit, Jew sabuw naatu Ufun Sabuw etei buwit tana ita’imonit.
15 pothetsa mʼthupi lake lamulo pamodzi ndi zolamulira zake ndi malangizo. Cholinga chake chinali chakuti alenge mwa Iye mwini, munthu mmodzi watsopano kuchokera kwa abwino, motero nʼkupanga mtendere,
15 Jew hai ofafar, hai obaiyunen tur, naatu hai bonawiyen tur etei bosair, sabuw big rou’ab hima’am bow hina ita’imon big ta’imon matar, tufuw e’afuw.
16 ndi kuyanjanitsa onse awiriwa mʼthupi lake kwa Mulungu, kudzera pa mtanda, umene Iye anaphapo udani wawo.
16 Keriso anamorob onaf afe’enamaim momorob ana veya big rou’ab hairi ufu’ufut hima’am i biyanamaim big buwih hina God bairi hitounuw.
17 Iye anabwera ndipo analalikira mtendere kwa inu amene munali kutali ndi mtendere ndiponso kwa iwonso amene anali pafupi.
17 Imih Keriso na Tur Gewasin Tufuw isan, kwa Jew sabuw iti yubin kwama’am isa binan naatu Ufun Sabuw ef yok kwama’am isa binan.
18 Pakuti mwa Iye, ife tonse titha kufika kwa Atate mwa Mzimu mmodzi.
18 Anayabin Jesu wanawananamaim, it Jew sabuw naatu Ufun Sabuw etei i karam boro Anun Kakafiyin ta’imon ana baibaisamaim tanan Tamat God nanamaim tana tit.
19 Kotero kuti, inu sindinunso alendo ndi adani, koma nzika pamodzi ndi anthu a Mulungu ndiponso a mʼbanja la Mulungu.
19 Imih kwa Ufun Sabuw, boun ana veya kwa i men tauman sabuw o nanawan sabuw na’atube kwama’amamih. Baise kwa i boun kwana God ana sabuw bairi big ta’imon matar, naatu God kwaifamen i ana nibur kwamatar.
20 Ndinu okhazikika pa maziko a atumwi ndi a aneneri, pamodzi ndi Khristu Yesu mwini ngati mwala wa pa ngodya.
20 Kwa i kob abarayah naatu dinab oro’orot hitutut hibatabat tafanamaim auman hiwowabari, tutut an i Keriso Jesu akisin.
21 Mwa Iyeyo, nyumba yonse yalumikizidwa pamodzi ndipo yakwezedwa kukhala Nyumba yoyera mwa Ambuye.
21 I akisinamo bar tutufin etei bai na ku’ay naatu wowab yen bar kakafiyin matar ya’asair God nowanamih itin.
22 Ndipo mwa Iye, inunso mukamangidwa pamodzi ndi ena onse kukhala nyumba yokhalamo imene Mulungu amakhala mwa Mzimu wake.
22 I wanawananamaim kwa auman wowabari, sabuw afa bairi, naatu i ana ma’ama efan kwamatar, God Anuninane imaim ema’ama.
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Efésios 2, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.