Efésios 1

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI

Sair da comparação
AAI TUR GEWASIN O BAIBASIT BOUBUN
1 Paulo, mtumwi wa Khristu Yesu mwachifuniro cha Mulungu.
1 Ayu Paul, God ana kokomaim rubinu Keriso Jesu ana tur abarayan amatar. Kwa God ana sabuw Ephesusamaim Keriso Jesu isan kwama kwabobosunusunub a fef iti akikirum.
2 Chisomo ndi mtendere kwa inu zochokera kwa Mulungu Atate athu ndi Ambuye Yesu Khristu.
2 Manaw kabeber naatu tufuw Tamat God naatu ata Regah Jesu Keriso’one kwa isa nama.
3 Tiyamike Mulungu, Atate a Ambuye athu Yesu Khristu, amene anatipatsa madalitso onse a uzimu kumwamba mwa Khristu.
3 God ata Regah Jesu Keriso Tamah ana merar tanay tanabora’ara’ah! Anayabin ayubit ana baigegewasin marane Keriso wanawananamaim suware tabaib isan.
4 Dziko lapansi lisanalengedwe, Mulungu anatisankhiratu mwa Khristu kuti tikhale oyera mtima ndi wopanda cholakwa pamaso pake. Mwa chikondi chake,
4 Mar tafaram matara’e ana veya God it iyabuwit, Keriso wanawananamaim God rubinit i nowan matar isan, saise kakafiyit naatu aurit ubar en tatama.
5 Iye anakonzeratu kuti ife titengedwe ngati ana mwa Yesu Khristu, molingana ndi kukonda kwake ndi chifuniro chake.
5 Iti yakitifuwen i anamaim God yabuna Jesu Keriso ana baitenowaramaim, it boro natunatun tanamatar. Iti na’atube sinaf, anayabin God ana kok yakitifuw naatu sinaf.
6 Anachita zimenezi kuti tiziyamika ulemerero wa chisomo chake, umene watipatsa kwaulere mwa Khristu amene amamukonda.
6 Isan imih manaw kabeber gewasin maiyow God Natun ana yabow bitit isan tanabora’arah.
7 Mwa Yesu Khristu, chifukwa cha magazi ake, ife tinawomboledwa ndi kukhululukidwa machimo athu molingana ndi kuchuluka kwa chisomo cha Mulungu
7 God ana manaw ana kabeber it bitit i ra’at kwanekwan. Natun ana rara’amaim tubunit, ata kakafih notawiyen.
8 chimene anatipatsa mosawumira. Mwa nzeru zonse ndi chidziwitso,
8 I ana so’ob naatu ana not rerekab tutufin etei tafat yan isuwai re.
9 Iye watiwululira chifuniro chake chimene chinali chobisika, chimene anachikonzeratu mwa Khristu, molingana ndi kukoma mtima kwake.
9 Naatu ana kok abisa sinafumih wa’iwa’irinamaim yakitifuw inu’in Keriso biyanamaim na irerereb.
10 Chimene anakonza kuti chichitike nʼchakuti, ikakwana nthawi yake asonkhanitsa pamodzi mwa Khristu zinthu zonse za kumwamba ndi pa dziko lapansi.
10 God yakitifuw inu’in ana veya nabaib ana maramaim sawar etei boro nan nita’imon. Sawar tutufin etei maramaim naatu tafaramamaim Keriso nan ni’ukwarin.
11 Iye anatisankhiratu mwa Khristu, atatikonzeratu molingana ndi machitidwe a Iye amene amachititsa zinthu zonse kuti zikwaniritse cholinga cha chifuniro chake,
11 Sawar etei i God eo yayakitifuw na’atube temamatar, imih God ana toto ana buyoy etei boro nowatamih tanabow. Anayabin it i marasika anamaim God taiyuwin nowanamih rubinit.
12 nʼcholinga chakuti, ife amene tinali oyamba kukhala ndi chiyembekezo mwa Khristu, tiyamike ulemerero wake.
12 Isan imih it iyab wan Keriso tabai nuhi fot tama tabitumitum, ata God gewasin tanabora’ara’ah.
13 Ndipo inunso pamene munamva mawu a choonadi, Uthenga Wabwino wa chipulumutso chanu, munayikidwanso mwa Khristu. Mutakhulupirira, anakusindikizani chizindikiro pokupatsani Mzimu Woyera amene Iye analonjeza.
13 Naatu kwa afa auman tur anababatun kwabai, yawas ana Tur Gewasin kwanonowar ana maramaim Jesu Keriso kwaitumitum yawas kwabai. Naatu God Anun Kakafiyin eo’omatani imaim ikwahi nowan kwamatar.
14 Mzimu Woyerayo ndi chikole chotsimikizira kuti tidzalandira madalitso athu, ndipo kuti Mulungu anatiwombola kuti tikhale anthu ake. Iye anachita zimenezi kuti timuyamike ndi kumulemekeza.
14 Imih Anun Kakafiyin i God ana ewow na’atube boro imaim nikwahit tanama God ana omatanen sabuw baitih isan eo boro it auman nit tanab naatu nafaramit tanatit, God tanifai tanabora’ara’ah i ana gewasin isan.
15 Choncho, kuyambira pamene ndinamva za chikhulupiriro chanu mwa Ambuye Yesu ndi za chikondi chanu pa oyera mtima onse,
15 Ayu kwa a baitumatum fairin anababatun Regah Jesu kwaitumitum, naatu God ana sabuw etei kwabiyabuwih ana tur anonowar ana veya,
16 ine sindilekeza kuyamika Mulungu chifukwa cha inu. Ndimakukumbukirani mʼmapemphero anga.
16 ayu au merarayow kwa isa i men kafa’imo abihamiy, mar etei au yoyobanamaim anunuhi.
17 Ndimapemphera kuti Mulungu wa Ambuye athu Yesu Khristu, Atate a ulemerero akupatseni mzimu wa nzeru ndi wa vumbulutso, kuti mumudziwe kwenikweni.
17 Naatu God, ata Regah Jesu Keriso Tamah gewasin abifefeyan Anun Kakafiyin nit, saise boro so’ob nit a not narerekab God isa nirerereb kwanasu’ub gewas.
18 Ndimapempheranso kuti maso a mitima yanu atsekuke ndi cholinga choti mudziwe chiyembekezo chimene Iye anakuyitanirani, chuma cha ulemerero chomwe chili mwa anthu oyera mtima.
18 Naatu abifefeyan dogor nabotawiy ana marakaw kwana’itin, naatu abisa isan ea’afi kwanaso’ob nuhi nafot. Naatu toto buyoy gewasin ana sabuw nowahamih bain isan eo’omatanih auman kwanaso’ob.
19 Ndiponso ndikufuna kuti mudziwe mphamvu zake zazikulu koposa zimene zili mwa ife amene timakhulupirira. Mphamvuyi ndi yofanana ndi mphamvu yoposa ija
19 Naatu ana fair gagamin na’in iyab i tabitumitum wanawanatamaim ebowabow kwana’itin kwanaso’ob. Naatu iti fair ta’imonamaim
20 imene inagwira ntchito pamene Mulungu anaukitsa Khristu kwa akufa, namukhazika Iye ku dzanja lake lamanja mʼdziko la kumwamba.
20 Keriso morobone iyawas bai yen mar bora’ara’aten ana efanamaim uman ana asukwafune ema’am.
21 Anamukhazika pamwamba pa ulamuliro onse ndi mafumu, mphamvu ndi ufumu, ndiponso pamwamba pa dzina lililonse limene angalitchule, osati nthawi ino yokha komanso imene ikubwerayo.
21 Keriso yen mamare i bonawiyenayah, roubabaruwenayah, fair ta ta hai ukwarih, aiwob ana’ahay ana mowar etei natabirih, men iti boun ana veya akisin, baise mar boro enanan auman i babanamaim, i akisinamo boro ni’aiwob.
22 Ndipo Mulungu anayika zinthu zonse pansi pa mapazi ake ndi kumusankha Iyeyo kukhala mutu pa chilichonse chifukwa cha mpingo,
22 God sawar etei Keriso anamaim yara’iyen wastanen naatu rubin ekaleisia tutufin etei isan, sawar etei hai ukwarin matar.
23 umene ndi thupi lake, chidzalo cha Iye amene adzaza chilichonse mu njira iliyonse.
23 Ekaleisia i Keriso biyan. Taiyuwin ana’itinin i efan tata’amaim bowabow ta ta wanawanan i nati’imaim ebowabow.

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Efésios 1, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.