Colossenses 2
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Ndikufuna mudziwe kuti ndikukuvutikirani kwambiri, inuyo pamodzi ndi anzanu a ku Laodikaya, ndi ena onse amene sitinaonane maso ndi maso.
1 Ayu bowabow fokarin maiyow kwa isa, naatu Laodicea ekaleisia isah abowabow, i akokok anao kwananowar, naatu sabuw afa ayu men hisusu’ubu auman isah abowabow i anao kwanaso’ob.
2 Cholinga changa nʼchakuti alimbikitsidwe ndi kuyanjana pamodzi mʼchikondi, akhale odzaza ndi nzeru zomvetsa zinthu, ndi kuti azindikire chinsinsi cha Mulungu, chimene ndi Khristu.
2 Ayu au kok gagamin iti sabuw dogoroh i kaufair awan nakaratan, naatu yabowamaim naku’ayih saise so’ob tutufin enan naniyan hinab naatu God ana kirikirifot Keriso wanawananamaim hinaso’ob.
3 Mwa Iyeyu muli chuma chonse chobisidwa cha nzeru ndi chidziwitso.
3 Keriso akisin maiyow i ata ukwar rerekab isan ana so’ob an, naatu so’ob gewasih etei nugunug na’atube awan ma’afut ma’atan ema’am.
4 Ndikukuwuzani zimenezi kuti wina aliyense asakunamizeni ndi kukukopani ndi mawu ake.
4 A tur ao’owen, orot babin men ta veya kwanitin a natain nifufuwimih, ana tur nayare hamehamen mumunin nao men kwananowar.
5 Pakuti ngakhale sindili pakati panu mʼthupi, ndili nanu pamodzi mu mzimu, ndipo ndikukondwa kuona kuti mukulongosola bwino zonse ndiponso kuti chikhulupiriro chanu mwa Khristu ndi chokhazikika ndithu.
5 Basit ayu biyau’umaim i kwaboyouwu baise ayubu’umaim i bairit tama’am. Kwa a baitumatum Keriso wanawananamaim kwafatum badowan kwabatabat isan, ayu i abiyasisir yawas tutufin Keriso’omaim.
6 Tsono popeza munavomereza Khristu Yesu kukhala Ambuye anu, mupitirire kukhala mwa Iyeyo.
6 Keriso kwaibasit a Regahamih kwabai, imih Jesu wanawanan kwanarun i ana kokomaim kwanama.
7 Mukhale ozikika mizu mwa Iye, ndipo moyo wanu umangike pa Iye. Mulimbike mʼchikhulupiriro monga momwe munaphunzirira, ndipo kuyamika kwanu kusefukire.
7 A wairoroh Jesu wanawanan na’of barur, a yawas i tafanamaim kwanawowab naatu a baitumatum nara’at fair nab hibi’obaiyi na’atube. Naatu dogor merarayow awan nakaratan.
8 Musalole kuti wina aliyense akutengeni ukapolo ndi mʼnzeru zachinyengo zolongosola zinthu zozama, zomwe zimachokera ku miyambo ya anthu ndi ku maganizo awo okhudza za dziko lapansi osati kwa Khristu.
8 Kwana’itin gewas men yait ta orot ana so’obamaim nifufuwi nanawiyi dibur kwanarunamih, iti bai’obaiyen, i orot hiyabunibun re enan naatu iti tafaram ana sabuw hai ofafar hio hikikirum, i hiyabunibun enan men Keriso biyanane enan.
9 Pakuti mʼthupi la Khristu mumakhala umulungu wonse wathunthu.
9 Anayabin Keriso biyan i God biyan tutufin etei nati’imaim ema’am.
10 Ndipo inunso ndinu athunthu mwa Khristu. Iye ndiye mtsogoleri wa pamwamba pa maufumu onse ndi maulamuliro wonse.
10 Imih o Keriso inabaib ana veya yawas tutufin etei boro inab naatu o biya tutufin etei God boro niwani. Anayabin o Keriso ana kou’ayomaim kuma’am, i ana aiwob i auyomtoro’ot, yoyom bonawiyenayah naatu roubabaruwen hai aiwob etei hai fair tafahimaim.
11 Mwa Iye inunso munachita mdulidwe mʼthupi lanu, osati mdulidwe ochitidwa ndi manja a anthu ayi, koma ochitidwa ndi Khristu pamene anavula khalidwe lanu lauchimo lija.
11 Kwa kwana Keriso nowan kwamamatar i men orot hai a’afuw hibimatarimaim kwa a’ar hi’afuw kwana Keriso nowan kwa mataramih. Baise Keriso taiyuwin ana a’afuwamaim dogor a kakafin e’afuw bosair.
12 Mu ubatizo, munayikidwa mʼmanda pamodzi ndi Khristu ndi kuukitsidwa naye pamodzi, pokhulupirira mphamvu za Mulungu amene anamuukitsa kwa akufa.
12 Anayabin bapataito kwabaib ana veya’amaim, kwa i Keriso bairi hubemaim hitouni; naatu God ana fairamaim Jesu morobone biyawas ana maramaim, kwa auman abaitumatumamaim God yawas it kwamisir maiye.
13 Pamene munali akufa chifukwa cha machimo anu ndi osachita mdulidwe mʼmitima mwanu, Mulungu anakupatsani moyo mwa Khristu. Iye anatikhululukira machimo athu onse.
13 Kwa ayubimaim i kwamorob, anayabin a bowabow kakafinamaim naatu Ufun Sabuw aur ofafar en. Baise Keriso wanawananamaim God kwa yawas it, naatu ata kakafih etei notawiyen.
14 Anafafaniza kalata ya ngongole yathu, pomwe panali milandu yotitsutsa ife. Iye anayichotsa, nayikhomera pa mtanda.
14 Ata kakafih etei sasamen, abisa ofafar eo men tabi’ufunun ana bit tabaib. Naatu ata kakafih etei fefemaim hikirumen hi’inu’in bai in Jesu onaf afe’en hio’onaf ana veya’amaim gurus.
15 Ndipo atalanda zida maufumu ndi maulamuliro, Iye anawachititsa manyazi powayendetsa pamaso pa anthu onse atawagonjetsa ndi mtanda.
15 Naatu onaf afe’en Keriso taiyuwin afiy hai bonawiyenayan ana fair rufam tit bebeyan i’obaiyit kakafin wasatan.
16 Nʼchifukwa chake musalole wina aliyense kukuzengani mlandu chifukwa cha zimene mumadya kapena kumwa, kapena za masiku achikondwerero cha chipembedzo, za chikondwerero cha mwezi watsopano, kapena za tsiku la Sabata.
16 Imih o a bay ku’aa o a harew kutomatom men yait ta nao fafarimih, na’atube veya gagamih, o sumar bebegawan ana hiyuw, o Baiyarir ana veya men kwanabi’ufunun isan sabuw men hina’uwimih.
17 Zimenezi ndi chithunzithunzi chabe cha zinthu zimene zikubwera, koma choonadi chenicheni chikupezeka mwa Khristu.
17 Iti sawar etei i ina’inan na’atube, uwatanah no marasika hima’am imaim i’obaiyih God hikwakwafir, abisa boro uf tamamatar isan. Baise Keriso i na sawar hai yabih anababatun sinaf himatar, imih nati sawar atamanih i sawar.
18 Musalole kuti wina aliyense amene amakonda kudzichepetsa mwachiphamaso ndi kumapembedza angelo akulepheretseni kukalandira mphotho. Munthu woteroyu amayankhulanso mwatsatanetsatane zinthu zimene akuti anaziona mʼmasomphenya. Anthuwa ndi odzitukumula ndi fundo zopanda pake zochokera mʼmaganizo mwawo amene si auzimu.
18 Men yait ta taiyuwin ufunane ana itinin nigewasin nayara’iy nao, ayu i ina’inan afa aitah, tounamatar hai kwafirinamaim tanakwafir. Nati sabuw isah men kwanibasit hina’uwi, sabuw bai’o’orotoyah hai not moumurih.
19 Iwo sakulumikizananso ndi mutu, kumene kumachokera thupi lonse, logwirizidwa ndi kumangiriridwa pamodzi ndi mʼmitsempha yake ndi mnofu, limene limakula monga mmene Mulungu afunira kuti likulire.
19 Nati sabuw Keriso biyanamaim hai murab i turu’um. Keriso i ukwarin. Naatu it etei i biyan turin, yabin it etei i ana murab fokarinamaim irarit, naatu God ana kokomaim tara’at ata not etataseseb.
20 Popeza munafa pamodzi ndi Khristu kusiyana nayo miyambo ya dziko lapansi lino, nʼchifukwa chiyani mukukhalanso ngati a dziko lapansi lino? Bwanji mukumvera malamulo monga awa:
20 Kwa i Keriso bairi kwamorob naatu iti tafaram ana afiy hai bonawiyenane rufami. Baise aisim kwama’am ana itinin i iti tafaram nowanabe? Aisim sawar iti na’atube kwabi’ufunun?
21 “Usagwire chakuti,” “Usalawe chakuti,” “Usakhudze chakuti?”
21 Iti bay men kwana’aan, nati men kwanakartubun, iti men kwanabutubun,
22 Malamulo amenewa amakhudza zinthu zimene zimatha zikamagwiritsidwa ntchito, ndipo malamulo ndi zophunzitsa za anthu chabe.
22 sawar iti etei i orot hai bai’obaiyen, bay i anin isan matar imih etei tanaa.
23 Ndithu malamulo oterewa amaoneka ngati anzeru, pakuti amalamulira anthu ambiri pa zachipembedzo ndi pa zakudzichepetsa kwa chiphamaso, ndi pa zakuzunza thupi lawo, koma alibe mphamvu zoletsa kuchita zofuna za thupilo.
23 Iti sawar etei i gewasih, anayabin boro nibaisit tanayoyoban gewas, tanayohar gewas, naatu taiyuwit boro tana yara’iyit tanakakaf, baise boro men nanunuw gewas. Anayabin orot babin ana not kakafin sinaf isan not ekukura’ara’ah boro men karam tanahirimih.
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Colossenses 2, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.