Colossenses 1
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Paulo, mtumwi wa Khristu Yesu mwachifuniro cha Mulungu, ndi Timoteyo mʼbale wathu.
1 Ayu Paul God ana kokomaim rubinu, Keriso Jesu ana tur abarayan amatar, taituwa Timothy airi.
2 Kulembera abale oyera mtima ndi okhulupirira a ku Kolose mwa Khristu.
2 Kwa God ana sabuw kakafiyih naatu bosunusunubayah Keriso wanawananamaim, nati Colosai wanawanan kwama’am etei a merar ayiy.
3 Timayamika Mulungu Atate wa Ambuye athu Yesu Khristu, nthawi zonse pamene tikukupemphererani.
3 Aki Mar etei kwa isa ayoyoyoban ana maramaim, ata Regah Jesu Keriso Tamah God ana merar ayiy.
4 Timayamika chifukwa tinamva za chikhulupiriro chanu mwa Khristu Yesu ndi za chikondi chanu pa oyera mtima onse.
4 Anayabin kwa ata Regah Jesu Keriso kwabitumitum naatu God ana sabuw kwabiyabuwih ana tur hina hio anowar.
5 Chikhulupiriro ndi chikondi, gwero lake ndi chiyembekezo chomwe muli nacho chodzalandira zimene anakusungirani kumwamba. Munamva kale za zimenezi kudzera mʼmawu a choonadi, Uthenga Wabwino
5 Tur anababatun Tur Gewasin wantoro’ot hina hio kwanonowar ana veya’amaim, kwa a baitumatum naatu a yabow etei i mar ana yasisir isan nuhi fot kwama kwakakaif.
6 umene unafika kwa inu. Pa dziko lonse lapansi Uthenga Wabwino ukubereka chipatso ndi kukula monga momwe zakhala zikuchitikira pakati panu kuyambira tsiku limene munawumva ndi kuzindikira chisomo cha Mulungu mu choonadi chonse.
6 Tur Gewasin ana baigegewasin i tit tafaram wanawanan tuw ra’at orot babin hai yawas ebobotabitabir, ana itinin i boubuntoro’ot hina, manaw kabeber isan hio kwanowar, turobe kwaso’ob naniyan kwabaib, na’atube emamatar.
7 Inu munaphunzira zimenezi kuchokera kwa Epafra, mtumiki mnzathu wokondedwa, amene ndi mtumiki wokhulupirika wa Khristu mʼmalo mwathu.
7 Iti tur etei i aki bow turai wabin Epaphras, Keriso ana bowayan gewasin ta, aki efani manaw kabeber Godane bai na eo kwanonowar,
8 Iye anatiwuza za chikondi chanu chimene Mzimu anakupatsani.
8 Aki auman kwa mi’itube Anun Kakafiyin yabow bit isan, eo anowar.
9 Chifukwa cha ichi, kuyambira tsiku limene tinamva za inu, sitinasiye kukupemphererani ndi kumupempha Mulungu kuti akudzazeni ndi chidziwitso cha chifuniro chake kudzera mu nzeru yonse yauzimu ndi kumvetsetsa.
9 Ana’an nati isan, aki tur anonowar ana veya, kwa isa mar etei ayoyoban God abifefeyan, kwa ayawasamaim abisa sinaf isan ekokok saise so’ob tutufin etei ni’obaiyi. Naatu ayoyoyoban ayubine ana so’ob buriburih auman nit ukwar hina rerekab, sawar etei hai yabih kwanaso’ob.
10 Ndipo tikupempherera zimenezi ndi cholinga chakuti inu mukhale moyo oyenera Ambuye ndi kumukondweretsa mʼnjira zonse. Kubereka chipatso pa ntchito iliyonse yabwino, ndi kukula mʼchidziwitso cha Mulungu.
10 Aki iti na’atube ayoyoyoban saise yawas gewasin Regah ekokok na’atube kwanama, mar etei a sinafumaim Regah boro niyasisir. A bowabow tata’ane gewasih kwabowabow boro ro’on namatar. Naatu God ana so’obamaim anot nara’at natasasar.
11 Timapempheranso kuti Mulungu akulimbikitseni ndi mphamvu yake yonse ya ulemerero wake, kuti muzipirira zonse ndi mitima yofatsa ndi ya chimwemwe
11 Naatu i ana fair bonamanamarinamaim nakura’ara’ahi, saise kwa boro biyababan gagamih wanawanan wainabi ana ef boro kwanaso’ob yate nanub.
12 ndi kuyamika Atate nthawi zonse, amene wakuyenerezani kuti mulandire nawo chuma cha oyera mtima mu ufumu wa kuwunika.
12 Yasisiramaim Tamat ana merar kwanay, anayabin i ana sinafumaim ef botawiy ana baibasit itit, ana sabuw kakafiyih bairi aiwob marakawin ninowat tanafaram.
13 Pakuti Iye anatipulumutsa ku ulamuliro wa mdima ndi kutibweretsa mu ufumu wa Mwana wake wokondedwa.
13 Gugumin kakafin ana fairane iyawasit naatu nawiyit tatit I Natun ebiyabow ana aiwob wanawanan yariyit.
14 Mwa Iyeyu ife tinawomboledwa ndi kukhululukidwa machimo.
14 I Natun wanawananamaim it rufamit tatit ata bowabow kakafih notawiyen.
15 Mwanayu ndiye chithunzi cha Mulungu wosaonekayo. Iye ndiye Mwana wake woyamba kubadwa ndi wolamulira zolengedwa zonse.
15 Keriso i God wa’iwa’irin ana itinin bai na irerereb ta’itin. Natun orot ain fewawawar sawar etei himamatar hai ukwarin
16 Pakuti zinthu zonse zinalengedwa kudzera mwa Iye. Zinthu zakumwamba ndi za pa dziko lapansi, zooneka ndi zosaoneka, maufumu, akuluakulu, aulamuliro ndi amphamvu. Zinthu zonse zinalengedwa kudzera mwa Iye ndipo anazilengera Iyeyo.
16 Anayabin Ine sawar tutufin etei God imataren; sawar iti tafaram wanawanan naatu sawar no mar wanawanan ta’i’itah naatu men ta’i’itah etei, na’atube aiwob, wagabur, fair, bonawiyenayah, roubabaruwenayah, etei God awanamaim eo himatar naatu i isan sinaf himatar.
17 Iyeyo analipo zinthu zonse zisanalengedwe ndipo zinthu zonse zimamangika pamodzi mwa Iye.
17 I mat ma’abo sawar uf himatar naatu ana fair wanawananamaim sawar etei hai efanamaim iu’uman hifokar ti’inu’in.
18 Iye ndiyenso mutu wa thupi, limene ndi mpingo. Iye ndiye chiyambi chake, woyamba kuuka kwa akufa, kuti Iyeyo akhale wopambana zonse.
18 Jesu i ekaleisia tutufin etei ana ukwarin, yawas an anababatun naatu murumurubih wanawanahimaim I wantoro’ot morobone misir maiye kek ain wan etutufuw na’atube. Imih sawar tutufin etei’imak i akisin ebi’ukwarin.
19 Pakuti kunamukomera Mulungu kuti umulungu wake wonse ukhalemo mwa Khristu.
19 Anayabin God iyasisir men kafaita, imih i taiyuwin ana itinin bai na Jesu wanawananamaim run ma.
20 Ndipo kudzera mwa Iye Mulungu ayanjanitsenso zinthu zonse ndi Iye mwini, zinthu za pa dziko lapansi, kapena zinthu za kumwamba. Iye anachita mtendere kudzera mʼmagazi ake, wokhetsedwa pa mtanda.
20 Naatu Jesu ana morobomaim mar tafaram God bai na ita’imon tounuw matar Jesu ana rara onaf afe’enamaim suwa re’er ana veya God tufuw e’afuw.
21 Kale inu munali kutali ndi Mulungu ndipo munali adani a Mulungu mʼmaganizo mwanu chifukwa cha khalidwe lanu loyipa.
21 Marasika kwa i bowabow kakafih kwanotanot naatu kwasisinaf, imih God ana kamabiy kwamatar ef yok na’in kwama’am.
22 Koma tsopano Iye anakuyanjanitsani mʼthupi la Khristu kudzera mu imfa kuti akuperekeni pamaso pake oyera, opanda banga ndi opanda chotsutsidwa nacho
22 Baise boun i Natun Keriso biyan momorobomaim kwa I ana tounuw kwamatar, saise kwa yayasairen kwamatar, aur kato en biya etei sasouwin nanamaim boro kwanatit.
23 ngati mupitirirabe kukhala mʼchikhulupiriro chanu, okhazikika ndi olimba, osasunthidwa kuchoka pa chiyembekezo chimene munachigwira mu Uthenga Wabwino. Uwu ndi Uthenga Wabwino umene munawumva, umene wakhala ukulalikidwa kwa olengedwa onse a pansi pa thambo, ndi umenenso, ine Paulo ndinakhala mtumiki wake.
23 A baitumatum kwanabotan kwananan na’at basit, kwanabatkikin gewas a dariniwa’an kwanabat, tur gewasin kwanowar nuhifot kwama’ama men kwanihamiy. Anayabin nati tur gewasin kwanonowar i tafaram wanawanan tutufin etei tibibinan, ayu Paul auman nati tur gewasin isan ai’akir abowabow.
24 Tsopano ine ndikukondwa kuti ndinavutika chifukwa cha inu, ndipo ndikukwaniritsa mʼthupi langa zimene zikuperewera pa masautso a Khristu, chifukwa cha thupi lake, limene ndi Mpingo.
24 Naatu boun ayu biyababan kwa isa abaib, i abiyasisir, anayabin Keriso ana ekaleisia isah biyan bababan na’atube turin anibais biyou nababan yomanin ana’asa’ub.
25 Ine ndakhala mtumiki wake mwa lamulo limene Mulungu anandipatsa kuti ndipereke Mawu a Mulungu athunthu,
25 Naatu ayu i God ana ekaleisia isan bowamih rubinu, bowabow iti itu, kwa a ma gewas isan tur etei ana binan yomanin ana’asa’ub.
26 chinsinsi chimene chakhala chikubisika kwa nthawi ndi mibado, koma tsopano chawululidwa kwa oyera mtima.
26 Iti tur i God ana kirikirifot, marasika sabuw hitutufuw yabunibun renan matahimaim ibun wa’ir in, baise boun i bai tit ana sabuw etei nahimaim ebirerereb.
27 Kwa iwo amene Mulungu anawasankha kuti awadziwitse pakati pa a mitundu ina, ulemerero wa chuma cha chinsinsi ichi, amene ndi Khristu mwa inu, chiyembekezo cha ulemerero.
27 Iti kirikirifot i God yakitifuw ana sabuw itih, hitab hitatit Eteni Sabuw isah tirerereb, saise kirikirifot ana yasisir hita’itin. Naatu kirikirifot i Jesu Keriso wanawananamaim kwanarun naatu kwa nuhi nafot God ana aiwobomaim boro ana marakaw bonamanamarin bairi kwafaram.
28 Ife tikulalikira Khristu, kulangiza ndi kuphunzitsa aliyense mwa nzeru zonse kuti timupereke aliyense wangwiro mwa Khristu.
28 Imih God ana so’ob aki biti’imaim Keriso I abibinan sabuw etei nahimaim, sabuw abimatnuwih naatu abi’obaiyih saise Keriso wanawananamaim hinarun nakusouwih ana bow anan God nanamaim ana tit
29 Ndi cholinga chimenechi, ine ndikugwira ntchito molimbika ndi mwamphamvu zonse zimene Iye anachita mwa ine.
29 Iti bowabow baisawarin isan abow ai’akir yuwou a’asfufur, anayabin i ana fair ayu wanawana’umaim ma kura’ara’ahu abowabow.
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Colossenses 1, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.