Atos 8

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI

Sair da comparação
AAI TUR GEWASIN O BAIBASIT BOUBUN
1 Ndipo Saulo anavomerezana nawo pa imfa ya Stefano.
1 Stephen hi’asabun momorob isan Saul auman isaito.
2 Anthu okonda Mulungu anayika maliro a Stefano ndipo anamulira kwambiri.
2 Kwafirenayah sabuw afa Stephen hiyai naatu isan hiyababan rerey gagamin maiyow hima hirererey.
3 Koma Saulo anayamba kuwononga mpingo. Amapita nyumba ndi nyumba, ndipo amagwira amuna ndi amayi ndi kukawatsekera ku ndende.
3 Naatu Saul ekaleisia gurusin busuruf bar awan awan run tit orot babin bow rouw fatum iteten in dibur baremaim yaririyen.
4 Okhulupirira amene anabalalika amalalikira konse kumene amapita.
4 Iyab hitagey nanabin hititit i God ana tur hibinan auman hinan.
5 Filipo anapita ku mzinda wa ku Samariya ndipo analalikira za Khristu kumeneko.
5 Philip re in Samaria bar merar gagaminamaim Keriso ana tur binan in.
6 Gulu la anthu litamva Filipo akulalikira komanso kuona zizindikiro zozizwitsa zimene ankazichita, onse anamvetsetsa zimene iye amanena.
6 Philip eo sabuw hinonowar naatu ina’inanen sinaf hi’i’itan etei hina hiyubin ana tur nowar isan.
7 Mizimu yoyipa inatuluka mwa anthu ambiri ikufuwula kwambiri ndipo ambiri amene anali akufa ziwalo ndi olumala anachiritsidwa.
7 Sabuw moumurih maiyow wanawanahimaim afiy kakafih tarsumih hima’am erefanah auman hititit, naatu ah umah kafikafirih naatu ah umah murumurubih moumurih maiyow auman iyayawasih
8 Kotero munali chimwemwe chachikulu mu mzindawo.
8 Imih nati bar meraramaim yasisir gagamin maiyow tafair tit.
9 Koma mu mzindawo munali munthu dzina lake Simoni, amene amachita za matsenga ndi kudabwitsa anthu a mu Samariya. Iye amadzitamandira kuti ndi wopambana,
9 Baise nati bar meraramaim i orot ta wabin Simon ma farum eafusar farum Samaria orot babin bibibiruwih, naatu taiyuwin wabin bora’ara’ah orot gagamin rouw eo.
10 ndipo anthu onse, aakulu ndi aangʼono anamumvera ndi kunena kuti, “Munthu uyu ndi mphamvu ya Mulungu yotchedwa Mphamvu yayikulu.”
10 Naatu sabuw etei nati bar merar hima’am, orot kikimin yen in orot gagamin etei fanan akisin hinonowar hio, “Iti orot i God ana fair bai, wabin ‘Fair Gagamih.’”
11 Anthu amamutsata chifukwa kwa nthawi yayitali amawadabwitsa ndi matsenga akewo.
11 Sabuw etei hibi’ufunun anayabin manin maiyow ana farumamaim bibibiruwih.
12 Koma atakhulupirira Filipo akulalikira Uthenga Wabwino wa ufumu wa Mulungu ndiponso dzina la Yesu Khristu, anthuwo anabatizidwa amuna ndi amayi.
12 Baise ana maramaim Philip na tur gewasin God ana aiwob isan naatu Jesu Keriso ana fair isan binan hinonowar, orot babin etei hitumatum naatu bapataito hibai.
13 Nayenso Simoni anakhulupirira ndipo anabatizidwa, natsatira Filipo kulikonse, ndipo anadabwa kwambiri pamene anaona zizindikiro zazikulu ndi zozizwitsa.
13 Simon taiyuwin auman itumatum naatu bapataito bai misir Philip mi’itube inan na’atube i’ufunun hairi hin naatu ina’inan gagamih maiyow himamatar i’itah isan ifofofor morob.
14 Atumwi a ku Yerusalemu atamva kuti anthu a ku Samariya analandira Mawu a Mulungu, anatumiza Petro ndi Yohane.
14 Tur Abarayah Jerusalem hima’am Samaria sabuw God ana tur hibasit hibaib tur hinowar, Peter John hairi hiyafarih isah hin.
15 Atafika anawapempherera kuti alandire Mzimu Woyera,
15 Hin hititit ana veya isah hiyoyoban, saise Anun Kakafiyin hitab.
16 chifukwa Mzimu Woyera anali asanafike pa wina aliyense wa iwo; anali atangobatizidwa mʼdzina la Ambuye Yesu.
16 Anayabin Jesu Keriso wabinamaim bapataito hibaib ana veya, Anun Kakafiyin men yait ta tafanamaim yenamih.
17 Ndipo Petro ndi Yohane anasanjika manja awo pa iwo, ndipo analandira Mzimu Woyera.
17 Imaibo Peter John hairi umah tafah hiyara’aten isah hiyoyoban naatu Anun Kakafiyinane hibai.
18 Simoni ataona kuti Mzimu anaperekedwa kwa iwo atumwi atawasanjika manja, iye anafuna kuwapatsa ndalama ndipo anati,
18 Sabuw tafah umah hiyara’aten Anun Kakafiyin re hibaib Simon i’itin ana veya, kabay baih tur abarayah itih naatu
19 “Inenso ndipatseni mphamvu imeneyi kuti aliyense amene ndimusanjika manja anga azilandira Mzimu Woyera.”
19 eo, “Ayu auman akokok nati fair ayu kwanitu, saise sabuw iyabowat tafah ayayara’aten i auman Anun Kakafiyin hinab.”
20 Petro anayankha kuti, “Ndalama zako utayike nazo pamodzi, chifukwa unaganiza kuti ungathe kugula mphatso ya Mulungu ndi ndalama!
20 Baise Peter iya’afut eo “O akabay airi mi’itube kwatamorob, anayabin o kunotanot God ana siwar i boro kabayamaim inatubun.
21 Ulibe gawo kapena mbali pa utumikiwu, chifukwa mtima wako suli wolungama pamaso pa Mulungu.
21 O a bowabow ta men aki biyai’imaim ema’am, anayabin o dogor God nanamaim i men mutufurinamih.
22 Lapa zoyipa zakozi ndipo upemphere kwa Ambuye. Mwina adzakukhululukira maganizo a mu mtima mwako.
22 Iti not kakafihine dogor kwikitabir naatu Regah isan kuyoyoban ta’itin a not kakafin nati dogoromaim ema’am boro nanotawiy.
23 Pakuti ine ndikuona kuti ndiwe wowawidwa mtima ndiponso kapolo wa tchimo.”
23 Anayabin ayu ai’iti o dogor wanawanan i bahiy iwansumi mata ebifefek naatu bowabow kakafin ana dibur irun kuma’am.”
24 Ndipo Simoni anayankha, “Mundipempherere kwa Ambuye kuti zisandigwere izi mwanenazi.”
24 Imaibo Simon iyafutih eo, “Regah isan kwayoyoban wainu, saise sawar iti na’atube men ta isou namataramih.”
25 Atatha kuchitira umboni ndi kulalikira mawu a Ambuye, Petro ndi Yohane anabwerera ku Yerusalemu, atalalikira Uthenga Wabwino mʼmidzi yambiri ya Asamariya.
25 Regah ana yawas hio’orereb naatu ana tur hibibinan ufunamaim, Peter John hairi himatabir maiye au Jerusalem hiyey ana veya, Samaria bar merar ta ta wanawanahimaim tur gewasin hibinan auman hin.
26 Mngelo wa Ambuye anati kwa Filipo, “Nyamuka pita chakummwera, ku msewu wa ku chipululu wopita ku Gaza kuchokera ku Yerusalemu.”
26 Imaibo God ana tounamatar Philip iu, “A ef asukwafune inab, arar yan ana ef Jerusalemane re in Gaza titit iwat inab inare inan.” Ethiopian orot Philip hairi hitar|alt="Ethiopian eunuch and Philip" src="cn01931B.tif" size="col" loc="Act 8.26" copy="©1978 David C. Cook Publishing Co." ref="8.26-30"
27 Ndipo ananyamuka napita, ndipo akuyenda anakumana ndi munthu wa ku Etiopia wa udindo waukulu woyangʼanira chuma cha Kandake, mfumu yayikazi ya ku Etiopia. Munthu ameneyu anapita ku Yerusalemu kukapembedza Mulungu,
27 Imih Philip misir ef nati butitiy inan founamaim Ethiopia orot gagamin hairi hitar. Iti orot i Ethiopia hai queen ana kabay etei ana nutitiyenayan gagamin, aiwob babin ana aiwob wabin i Kandis. Iti orot gagamin yena Jerusalem God kwafir sawar,
28 ndipo akubwerera kwawo atakwera pa galeta lake amawerenga buku la mneneri Yesaya.
28 me yan ana wa bai ana ubar matabir maiye re’er, ef yanamaim dinab orot Isaiah ana buk rusasar ma iyab auman inan.
29 Mzimu anamuwuza Filipo kuti, “Pita pa galeta ilo ndipo ukakhale pafupi nalo.”
29 Naatu Anun Kakafiyin Philip iu, “Kwen ni’i wa sisibinamaim kwiyubin.”
30 Pamenepo Filipo anathamangira ku galeta ndipo anamva munthuyo akuwerenga buku la mneneri Yesaya. Filipo anamufunsa kuti, “Kodi mukumvetsa zimene mukuwerengazi?”
30 Philip imaibo nunuw yen na iyubin, tainin i’abar dinab orot Isaiah ana tur biyab nowar, naatu Philip orot ibatiy, “Nati buk kubiyab anayabin iso’ob?”
31 Iye anayankha kuti, “Ndingamvetse bwanji popanda wina wondimasulira?” Ndipo iye anayitana Filipo kuti abwere ndikukhala naye mʼgaleta.
31 Orot iya’afut eo, “Mi’itube boro anaso’ob? Orot ta isou nakubuna boro anaso’ob?” Naatu Philip ifefeyan yen sisibin mare.
32 Mawu amene ndunayo imawerenga anali awa:
32 Orot gagamin i buk firorow wanawanan ana hanef iti rusasar ma biyab.
33 Iye ananyozedwa ndipo panalibe chilungamo pa mlandu wake.
33 Taiyuwin yare, ma gewas ana baitafen tutur isan men hinuwet gewas,
34 Ndunayo inamufunsa Filipo kuti, “Chonde, uzeni, kodi mneneri akuyankhula za ndani, za iye mwini kapena za munthu wina?”
34 Naatu Ethiopia orot Philip ibatiy, “Ku’o anowar, yait isan iti dinab orot eo? I taiyuwin isan, ai orot babin ta isan?”
35 Pamenepo Filipo anayambira pa malemba omwewo kumuwuza za Uthenga Wabwino wa Yesu.
35 Imaibo Philip Buk ana hanef menamaim busuruf biyab imaim tur gewasin Jesu isan ana tur eowen.
36 Akuyenda mu msewu anafika pamalo pamene panali madzi ndipo ndunayo inati, “Taonani madzi awa. Kodi pali chondiletsa kuti ndibatizidwe?”
36 Ef yan hire hinan auman hina harew soson ta’amaim hitit naatu orot gagamin eo, “Harew iti, tare bapataito kwitu.”
37 Filipo anati, “Ngati mukhulupirira ndi mtima wanu wonse mukhoza kubatizidwa.” Ndunayo inayankha kuti, “Ine ndikukhulupirira kuti Yesu Khristu ndi Mwana wa Mulungu.”
37 Philip iya’afut eo, “O karam boro bapataito inab, dogor tutufin etei inabitumatum na’at.” Iya’afut eo, “Ayu abitumatum Jesu Keriso i God Natun.
38 Ndipo analamulira galeta kuti liyime. Onse awiriwo, Filipo ndi Ndunayo anatsika ndi kulowa mʼmadzi ndipo Filipo anamubatiza.
38 Orot gagamin ana wa rowenatan naatu Philip hairi hire hin harew yan hire nati’imaim Philip orot bapataito itin.
39 Pamene iwo anatuluka mʼmadzimo, Mzimu wa Ambuye anamukwatula Filipo, ndipo Ndunayo sinamuonenso, koma inapitiriza ulendo wake ikusangalala.
39 Harewane hiyeye ana maramaim, Regah Anunin Philip bora’ah. Orot gagamin men itin maiye, baise ereyasisir auman ana ef rura’ah maiye remor in.
40 Koma Filipo anapezeka kuti ali ku Azoto ndipo anazungulira konse, kulalikira Uthenga Wabwino mʼmizinda yonse mpaka anakafika ku Kaisareya.
40 Nati ana veya’amaim Philip i Azotus imaim rouwatait, naatu in Caesarea tit, efamaim inan bar awan, awan run tit tur gewasin binan auman remor in.”

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Atos 8, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.