Atos 28
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Titapulumuka choncho, tinamva kuti chilumbacho chimatchedwa Melita.
1 Ataiy ana dones ayey men yait ta aboyouw, naatu nuw imaibo ai’inan, aki i ana Malta nuw ayen.
2 Anthu a pa chilumbacho anatichitira zokoma zimene sizichitika kawirikawiri. Iwo anakoleza moto natilandira tonse chifukwa kumagwa mvula ndipo kumazizira.
2 Nuw sabuw merarayow gewasin maiyow hiti, ai merar hiyi wairaf hi’asir rari, anayabin toun i yarayar naatu tutuban ea’ani.
3 Paulo anatola mtolo wankhuni, pamene amayika pa moto, munatulukamo njoka chifukwa cha kutentha, ndipo inamuluma pa dzanja.
3 Paul ai heaf na wairaf wan yayara’aten, naatu kok wairaf wabuburin bai kayam tit, Paul uman yub fifin.
4 Anthu a pa chilumbacho ataona njokayo ili lende pa dzanja lake, iwo anawuzana kuti, “Munthu uyu akuyenera kukhala munthu wopha anthu; pakuti ngakhale wapulumuka pa nyanja, chilungamo sichinamulore kuti akhale ndi moyo.”
4 Nuw sabuw Paul umanamaim kok fifin inu’in hi’itin basit taiyuwih hio, iti orot i uman rara. Riy yan yawasin taiy na yen, baise koubaitotorayan ana god men ekokok boro yawasin nama.
5 Koma Paulo anayikutumulira pa moto njokayo, ndipo sanamve kupweteka.
5 Baise Paul uman ta’asiy kok wairaf wan yen earah naatu men abisa ta isan matar.
6 Anthu anayembekezera kuti thupi lake litupa kapena agwa ndi kufa mwadzidzidzi, koma anadikira nthawi yayitali. Ataona kuti palibe kanthu kachilendo kanamuchitikira anasintha maganizo awo nanena kuti iye ndi mulungu.
6 Sabuw hima hi’itin hinotanot i boro uman tadaw o an ta’uy tare tamorob. Baise manin maiyow hima hikakaif men abisa ta isan matar, imih hai not hibotabir hio, “Iti orot i god wari’en!”
7 Pafupi ndi malowa panali munda wa Popliyo, mkulu wa boma la pa chilumbacho. Iye anatilandira natisamala bwino masiku atatu.
7 Nati dones inan sisibin turin i orot wabin Publius ana bar merar. Publius i nati nuw hai orot gagamin. Ai merar yi, veya tounu ana nanawan na’atube bairi ama ituwi.
8 Abambo ake anali gone, chifukwa amadwala malungo ndi kamwazi. Paulo analowa mʼchipinda chake kukawaona, ndipo atapemphera, anasanjika manja ake pa iwo nawachiritsa.
8 Publius tamah sawow biyan ana fora’abin ra’at, naatu yan yub ana gem yan inu’in. Paul na ana bar run isan yoyoban, biyan butubun naatu yawas.
9 Zitachitika zimenezi, anthu onse odwala a pa chilumbacho anabwera ndipo anachiritsidwa.
9 Sawar iti mamatar ana tur hinowar, sabuw iyab nati nuwamaim hisawow hi’inu’in hinan etei hiyawas.
10 Anthuwo anatilemekeza ife mʼnjira zambiri ndipo pamene tinakonzeka kuti tiyambe ulendo, anatipatsa zonse zomwe tinazisowa.
10 Naatu hai kakaf gagamin na’in aki hiti, wa afe’en ayey ana veya ai remor isan abisa akokok etei hibaisi.
11 Patapita miyezi itatu, tinanyamuka pa sitima ina imene inakhala pa chilumbacho chifukwa cha kuzizira. Inali sitima ya ku Alekisandriya imene inali ndi chizindikiro cha milungu ya mapasa yotchedwa Kastro ndi Polikisi.
11 Sumar tounu ama’ama ufunamaim wa ta Alexandria’ane nan abai. Iti wa wabin, “God Kikifu” anayabin iti wa nanamaim i Kastor naatu Folux hairi hai yumat hikirum hi’inu’in. Rarab siba’u aki nati nuwamaim wa tafan ama in rarab siba’u sawar.
12 Tinakafika ku Surakusa ndipo kumeneko tinakhalako masiku atatu.
12 Wa abai atit an tafaram wabin Sarakus imaim arun veya tounu imaim ama.
13 Kuchokera kumeneko tinayenda ndi kukafika ku Regio. Mmawa mwake mphepo yochokera kummwera inawomba, ndipo tsiku linalo tinakafika ku Potiyolo.
13 Naatu nati’imaim atit anunuw ana Rhegium bar merar gagamin arun imaim a’in. Mar to waruw gurufune busuruf babin, naatu aki atit anunuw veya bairu’abin Puteoli arun.
14 Kumeneko tinapezako abale amene anatiyitana kuti tikhale nawo sabata limodzi. Ndipo kenaka tinapita ku Roma.
14 Nati’imaim baitumatumayah afa hima’am atitourih naatu hifefeyani bairi fur ta’imon ama. Imaibo aremor ana Rome atit.
15 Abale kumeneko atamva kuti tikubwera, anabwera kudzakumana nafe mpaka ku bwalo la Apiyo ndiponso ku nyumba za alendo zitatu. Atawaona anthu amenewa Paulo anayamika Mulungu ndipo analimbikitsidwa.
15 Baitumatumayah Rome hima’am aki anan bigai hinowar basit hina Apius ahar ana efan hitit, naatu afa hina Nanawan Bar Tounu hibatabat imaim hi’iti ai merar hiyi, Paul iti sabuw i’itih ana veya God ana merar yi naatu i koufair gagamin maiyow bai.
16 Titafika ku Roma, Paulo analoledwa kukhala pa yekha ndi msilikali womulondera.
16 Ana Rome atitit ana veya, Paul akisin ma isan ana baibasit hitin, naatu baiyowayah orot ta hiyai kaif hairi hima.
17 Patapita masiku atatu, Paulo anasonkhanitsa pamodzi atsogoleri a Ayuda. Atasonkhana, Paulo anawawuza kuti, “Abale anga, ngakhale kuti ine sindinachite kanthu kalikonse kulakwira mtundu wathu kapena miyambo ya makolo athu, koma anandigwira mu Yerusalemu ndi kundipereka mʼmanja mwa Aroma.
17 Veya tounu ufunamaim Jew orot ukwarih etei Paul eaf hiru’ay. Eaf hiruru’ay ana veya’amaim iuwih eo, “Taitu ayu i men kafa’imo ata sabuw isah asinaf kakaf, naatu uwatanah hai binanakwar abisa hibitit aigigimimih, baise Jerusalem imaim ayu hifatumu naatu hibuwu Rome gawan umanamaim hiya’u.
18 Iwo anandifufuza ndipo anafuna kundimasula chifukwa sanandipeze wopalamula mlandu woyenera kuphedwa.
18 Ayu ubar hitu bairi ao hinunutitiy au kakafin men ta hitita’ur boro ata morob, imih hikok boro hitabotaitu.
19 Koma Ayuda atakana, ine ndinakakamizidwa kupempha kuti ndikaonekere pamaso pa Kaisara, sikuti ndinali ndi kanthu konenezera mtundu wanga.
19 Baise Jew sabuw men hikok ayu hitabotaitu, imih ayu Caesar isan ai fefeyan. Iti asisinaf i men ata sabuw ubar baitih na’atube abiwa’an.
20 Pa chifukwa ichi ndapempha kuti ndionane nanu ndi kuyankhula nanu. Pakuti nʼchifukwa cha chiyembekezo cha Israeli ndamangidwa unyolo uwu.”
20 Ana’an iti isan ayu kwa aifefeyan kwatan kwata’itu bairit tatao isan. Ayu hifatumu dibur ama’am anayabin i Israel sabuw orot nati biyanamaim nuhih fot tema’am isan.”
21 Iwo anayankha kuti, “Ife sitinalandire kalata iliyonse yochokera ku Yudeya yonena za iwe, ndipo palibe mmodzi wa abale amene anachokera kumeneko anafotokoza kapena kunena kalikonse koyipa ka iwe.
21 Hiya’afut hio, “Aki Judea’ane men fef ta o isa abaimih, na’atube taituwat nati’ine men o asinaf isan naatu abisa isisinaf kakaf ana tur men ta na eo anowar.
22 Koma ife tikufuna kumva maganizo ako ndi otani, pakuti tikudziwa kuti ponseponse anthu akuyankhula zotsutsana ndi mpatuko umenewu.”
22 Baise aki akokok o anot i ku’o anowar, anayabin efan ta ta etei sabuw iti o a kou’ay boubun isan hio tegamigam anonowar.”
23 Iwo anakonza tsiku lina loti akumane ndi Paulo, ndipo anabwera anthu ambiri ku nyumba kumene amakhala. Kuyambira mmawa mpaka madzulo, Paulo anawafotokozera ndi kuwawuza za ufumu wa Mulungu ndipo anayesa kuwakopa kuti akhulupirire Yesu kuchokera mʼMalamulo a Mose ndiponso mʼmabuku a Aneneri.
23 Basit Paul bairi veya hiyai naatu nati veya’amaim sabuw rou’ay gagamin na’in hiru’ay. Paul ma’am ana efanamaim. Mar auman Paul busuruf God ana aiwob isan kubuna naatu eorerereb etei hinowar. Sinaftobon Moses ana ofafaramaim naatu dinab oro’orot hai turamaim sabuw botabirih Jesu dogoroh baitinin isan ma iuwih in veya re.
24 Ena anakopeka ndi zimene Paulo ananena, koma enanso sanakhulupirire.
24 Sabuw afa abisa eo i hitumatum, baise sabuw afa i men hitumatum.
25 Ndipo anayamba kuchoka popeza sanagwirizane pakati pawo Paulo atanena mawu awa omaliza akuti, “Mzimu Woyera anayankhula zoona za makolo anu pamene Iye ananena kudzera mwa Mneneri Yesaya kuti,
25 Taiyuwih wanawanahimaim Paul ana tur yomanin eo isan hibusuruf hibibas ufunamaim himisir hitit hin. Paul eo, “Anun Kakafiyin i turobe uwatanah isah dinab orot Isaiah iwan eo,
26 “Pita kwa anthu awa ndi kuwawuza kuti,
26 ‘Kwen sabuw iti isah kuo,
27 Pakuti mtima wa anthu ndi wokanika;
27 Anayabin nati sabuw fudirih i fokar.
28 “Chifukwa chake ine ndikufuna mudziwe kuti chipulumutso cha Mulungu chatumizidwa kwa anthu a mitundu ina, ndipo iwo adzamvera.”
28 Isan imih ayu akokok kwa kwanaso’ob, God ana yawas i Ufun Sabuw isah ebiyafar naatu i boro tur hinanowar!”
29 Paulo atanena mawu amenewa, Ayuda aja anachoka akutsutsana kwambiri.
29 Tur iti eo ufunamaim Jew hihamiy taiyuwih higam auman hin.
30 Paulo anakhala kumeneko zaka ziwiri zathunthu mʼnyumba yobwereka yomwe amalipira ndipo ankalandira aliyense amene amabwera kudzamuona.
30 Kwamur rou’ab tutufin Paul bar ta tutubun imaim ma naatu sabuw iyab itinamih hinan i mar etei hai merar yiy.
31 Molimba mtima ndi popanda womuletsa, Paulo analalikira za ufumu wa Mulungu ndi kuphunzitsa za Ambuye Yesu Khristu.
31 Nati’imaim ma’am men kafa’imo bir naatu men abisa ta ana ef ya’afutimih, baise God ana aiwob isan ma binan, naatu Jesu Keriso isan sabuw i’obaibiyih.
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Atos 28, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.