Atos 27
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Zitatsimikizika kuti tiyenera kupita ku Italiya pa sitima ya pa madzi, anamupereka Paulo pamodzi ndi a mʼndende ena kwa msilikali wolamulira asilikali 100, dzina lake Yuliyo, amene anali wa gulu la asilikali lotchedwa, Gulu la Mfumu.
1 Aki au Italy na’at na isan hinot hiyayabuna ufunamaim Paul naatu dibur sabuw afa bairi hibuwih Rome baiyowayah hai orot ukwarin babanamaim wabin Julius umanamaim hiya’i. Caesar baiyowayah orot hai kou’ay wabin Aiwob ana Baiyowayah. |alt="map" src="Paulrome.tif" size="col" ref="Acts 27.1"
2 Tinakwera sitima ya pamadzi yochokera ku Adramutiyo imene inali yokonzeka kale kupita ku madooko a ku Asiya, ndipo tinanyamuka. Aristariko, wa ku Makedoniya wa ku mzinda wa Tesalonika, anali nafe.
2 Aki wa tafaram Adaramitiamane na batabat abai, iti wa i Asia wanawanan awar etei run titamih nununuw abai. Masedonia orot wabin Aristakus ana tafaram Thessalonica i auman is ra’at bairi an.
3 Mmawa mwake tinafika ku Sidoni; ndipo Yuliyo, mokomera mtima Paulo, anamulola kupita kwa abwenzi ake kuti akamupatse zosowa zake.
3 Anan marto Sidon arun, Julius, Paul isan i igewasin, baibasit itin ana ofonah bainanawanihimih itih ana kokok abisa baibaisin isan iu.
4 Kuchokera kumeneko tinayambanso ulendo pa nyanja ndipo tinadutsa kumpoto kwa chilumba cha Kupro chifukwa mphepo imawomba kuchokera kumene ife timapita.
4 Nati’imaim atit maiye ana, baise yabat kufuti, imih aki wa abai ai kewakew Cyprus nuw sisibinamaim isinfafari anunuw an.
5 Titawoloka nyanja mbali ya gombe la Kilikiya ndi Pamfiliya, tinakafika ku Mura, mzinda wa ku Lukia.
5 Anunuw anan i atit are Silisia naatu Pamfilia hai riy yan foun autubun arabon ana Maira arun Laisia wanawanan.
6 Kumeneko wolamulira asilikali 100 uja anapeza sitima ya pamadzi ya ku Alekisandriya imene imapita ku Italiya, ndipo anatikweza mʼmenemo.
6 Nati’imaim Julius orot ukwarin Alexandria hai wa ta au Italy nununuw tita’ur, basit aki imaim yara’ahi.
7 Tinayenda pangʼonopangʼono kwa masiku ambiri ndipo tinakafika kufupi ndi Knido movutikira. Pamene mphepo sinatilole kupitirira ulendo wathu molunjika, tinadzera kummwera kwa chilumba cha Krete, moyangʼanana ndi Salimoni.
7 Veya moumurih maiyow efamaim aremor, yabat rabi auman awani ayey ana bar merar Sinidus anatabir. Baise yabat i ra’at men karam boro mutufor atanunuw, imih aki Kurit nuw isinfafari anunuw Samone sisibin rounane.
8 Timayenda movutikira mʼmbali mwa chilumbacho ndipo tinafika pa malo wotchedwa Madooko Okoma, pafupi ndi mzinda wa Laseya.
8 Kufuti auman awani tor rewarewan anunuw ana efan wabin Umabibin imaim atit, bar merar Lasea sisibinamaim Umabibin imaim arun.
9 Tinataya nthawi yayitali, ndipo kuyenda pa nyanja kunali koopsa chifukwa nʼkuti tsopano nthawi yosala kudya itapita kale. Choncho Paulo anawachenjeza kuti,
9 Nati’imaim veya manin maiyow ama naatu busurufin maiye na isan yabat i ra’at re sakirafut. Anayabin gagar ana veya i mar etei notawiyen ana hiyuw ufunamaim ebubusuruf. Imih Paul imatnuwih eo,
10 “Anthu inu, ine ndikuona kuti ulendo wathuwu ukhala woopsa ndipo katundu ndi sitima ziwonongeka, ngakhalenso miyoyo yathu.”
10 “Oro’orot ayu ai’itin it tanatit tananan i boro kakafin wan tanamara’at, wa boro nataseb, sawar etei boro tanisaroun naatu it auman boro tanamorob.”
11 Koma wolamulira asilikali 100 uja, mʼmalo momvera zimene Paulo amanena, anatsatira malangizo a woyendetsa sitimayo ndiponso mwini wa sitimayo.
11 Baise baiyowayan hai orot gagamih Julius, Paul ana tur men nowar, baise wa ana kaifenayan, naatu wa matuwan abisa hio hai tur i’ufunun.
12 Popeza kuti dookolo silinali labwino kukhalako nthawi yozizira anthu ambiri anaganiza kuti tichoke. Ife tinkayembekeza kukafika ku Foinikisi ndi kukhala kumeneko nthawi yachisanu. Ili linali dooko la ku Krete, limene limaloza kummwera cha kumadzulo ndiponso kumpoto cha kumadzulo.
12 Naatu nati awar wa rouwin rarab siba’u imaim ma isan men igewasin, imih orot etei hai kok i boro wa hitimtawiy takakaram na’at atarabon Phoenix imaim rarab siba’u atama. Phoenix awar i tafaram Kurit wanawanan naatu nati awar i gewasin anayabin umabibin oyaw na’atune veya ere’er boro ina’itin nare.
13 Mphepo yochokera kummwera itayamba kuwomba pangʼonopangʼono, anthuwo anaganiza kuti apeza chimene amafuna; kotero analowetsa nangula ndipo anayamba kuyenda mʼmbali mwa chilumba cha Krete.
13 Waruw kikimin gurufune tarsisin, orot hinotanot abisa hio i mamatar, imih aumor hitain hiyen naatu rarar hibora’aten Kurit dones sisibin akutitiy.
14 Pasanathe nthawi yayitali, mphepo yamkuntho yotchedwa Eurokulo, inayamba kuwomba kuchokera ku chilumbacho.
14 Baise men yok yabat gagamin wabin wowog oyawane babin re.
15 Mphepo yamkunthoyo inawomba sitima ija ndipo sinathe kulimbana nayo, kotero ife tinayigonjera ndi kuyamba kutengedwa nayo.
15 Wa rab, aki bai kewakew run maiye isan abiwa’an men karam basit yabat wan amara’at atit are.
16 Tikudutsa mʼmbali mwa kachilumba kakangʼono kotchedwa Kawuda, tinavutika kuti tisunge bwato lopulumukiramo.
16 Baise anunuw ana nuw kikimin wabin Kauda guruf na’atune bat aki sisibin umabibin isinfafari, naatu hifafair wa kikimin uranane atain yen,
17 Anthuwo atakweza bwatolo mʼsitima, anakulunga zingwe sitimayo kuti ayilimbitse. Poopa kuti angakagunde mchenga wa ku Surti, iwo anatsitsa nangula ndi kuyilola sitima kuti idzingoyenda ndi mphepo.
17 murab hibow hikiktatan gaigiwas, wa afe’en baginayah yabat buwih run Libia dones yen yara’ahih hirouw hibir, basit rar hitaiyen hire wa bat earuw.
18 Ife tinavutika kwambiri ndi namondwe kotero kuti mmawa mwake tinayamba kuponya katundu mʼmadzi.
18 Yabat i wan fus kubar rouw in marto, naatu wa afe’en sabuw sawar hibow hisrouruwen riy yan hire.
19 Pa tsiku lachitatu anaponya mʼnyanja zipangizo za mʼsitima ndi manja awo.
19 Naatu veya baitaunin i wa ana sawar afa: rar, murab, koutataren, naatu boy i hibow taiyan hitaiyen hire.
20 Sitinaone dzuwa kapena nyenyezi kwa masiku ambiri ndipo namondwe anapitirira kuwomba kwambiri, pomaliza ife tonse tinalibenso chiyembekezo choti nʼkupulumuka.
20 Tafaram etei gugum aki sumar, daman men a’itah veya manin maiyow yabat kutuw rouw inan aki etei akasiy yawas isan anotanot ai not etei sawar.
21 Anthu aja atakhala nthawi yayitali osadya, Paulo anayimirira pakati pawo ndipo anati, “Anthu inu, mukanamvera malangizo anga oti tisachoke ku Krete: zonsezi sizikanawonongeka ndi kutayika.
21 Orot nati wa afe’en veya bai’ab ama yabat rarabi bay men yait ta eaan, Paul misir nah yan foun bat eo, “Oro’orot kwa gewasin ayu fanau kwatanowar Kurit tatama’am iti sawar boro men hita’af naatu boro men ta yababan tab.
22 Koma tsopano ndikuti limbani mtima, chifukwa palibe aliyense wa inu amene adzataya moyo wake; koma sitima yokhayi idzawonongeka.
22 Baise boun i kwa abifefeyani koufair kwanab, anayabin kwa orot etei boro men ta inamorobomih. Wa akisinamo boro natafofor na’unun.
23 Usiku wathawu mngelo wa Mulungu, Mulungu amene ine ndili wake ndipo ndimamutumikira, anayima pafupi ndi ine,
23 Fai gugumin God ayu aru, naatu God ayu akwakwafir i ana tounamatar iyafar ayu sisibu’umaim bat,
24 ndipo iyeyu anati, ‘Usachite mantha, Paulo. Ukuyenera kukayima pamaso pa Kaisara; ndipo Mulungu mwa kukoma mtima kwake wakupatsa miyoyo ya anthu onse amene ukuyenda nawo.’
24 naatu iuwu, ‘Paul men inabir, o i boro Caesar nanamaim ubar hibit hinibabatiyi. God i ana kabeberamaim sabuw iti bairi wa afe’en kwanan hai yawas etei o umamaim ya, imih boro men yait ta namorob.’
25 Tsono limbani mtima, anthu inu, pakuti ine ndili ndi chikhulupiriro mwa Mulungu kuti zichitika monga momwe wandiwuzira.
25 Imih oro’orot koufair kwanab! Anayabin ayu God abitumitum abisa eo anonowar na’atube boro nasinaf.
26 Komabe tiyenera kukatsakamira pa chilumba china chake.”
26 Baise it i boro narabit tanan nuw ta ana donesamaim boro nayara’ahit.”
27 Pakati pa usiku wa tsiku la khumi ndi chinayi tikukankhidwabe ndi mphepo mʼnyanja ya Adriya, oyendetsa sitimayo anazindikira kuti timayandikira ku mtunda.
27 Yabat rabi Mediterenean tor yan areremor fur rou’ab sawar veya 14 baib ana veya nati ana gugumin imaim wa afe’en baginayah naniyah hibaib aki i ana tafaram abiyubin.
28 Iwo anatenga choyezera kuzama kwa nyanja ndi kupeza kuti kuzama kwake kunali mamita 36. Atayendanso pangʼono anatenganso choyezera chija napeza kuti kuzama kwake kunali 27.
28 Basit murab hibai aumor hi’utan hitaiy re taiy hifufufum ana fofonin i 40 metres naatu hima kafai naatu hifufun maiye hi’tin i 30 metres.
29 Poopa kuti tingagunde miyala, iwo anatsitsira anangula anayi mʼmadzi kumbuyo kwa sitimayo ndipo tinapemphera kuti kuche.
29 Naatu hai bir i ra’at yabin yabat boro wa nab anan ar afe’en nayara’ah, imih aumor etei kwafe’en wa uranane hitaiyen hire naatu mar saise to isan hima hiyoyoban.
30 Pofuna kuthawa mʼsitimayo, oyendetsa aja anatsitsira mʼnyanja bwato lopulumukiramo nʼkumachita ngati akufuna kutsitsira anangula mʼnyanjamo kutsogolo kwa sitimayo.
30 Imaibo wa afe’en bowayah wa baihamiyin bihiramih hima hiyakitifuw. Naatu wa kafai hirufam harew yan hitaiy re, hitifuwen wa nanane aumor baitaiyin hitarouw hitanan i aunah hitanamih.
31 Pamenepo Paulo anawuza wolamulira asilikali uja ndi asilikaliwo kuti, “Ngati anthu awa sakhala mʼsitima muno, inu simungapulumuke.”
31 Baise Paul baiyowayah hai orot ukwarin bobonawiyih naatu baiyowayah iuwih eo, “Iti wa afe’en bowayah wa afe’en men hinama’am na’at, kwa etei i men karam boro yawas kwanab.”
32 Pamenepo asilikaliwo anadula zingwe za bwatolo ndipo linagwera mʼmadzi.
32 Basit baiyowayah kaiy hibow wa kafai ana murab hi’afuw naatu hitumar e’aruw in.
33 Kutatsala pangʼono kucha, Paulo anawawumiriza anthu onse kuti adye. Iye anati, “Kwa masiku khumi ndi anayi mwakhala mukuda nkhawa ndipo simumadya kanthu kalikonse.
33 Mar sibisib auman, Paul orot etei iuwih eo, “Kwa i bay kwanaa, anayabin bay en kwama’am boun fur rou’ab sawar naatu ya wanawanan i men abisa ta ema’am.
34 Tsopano ine ndikukupemphani kuti mudye. Muyenera kudya kuti mupulumuke. Palibe ndi mmodzi yemwe wa inu adzataye ngakhale tsitsi limodzi la pamutu pake.”
34 Imih abifefeyani bay kwanaa fair kwanab, arib boro men ta nata’uy nare nakasiyomih.”
35 Paulo atanena zimenezi, anatenga buledi nayamika Mulungu pamaso pa onse. Ndipo ananyema bulediyo nayamba kudya.
35 Paul iti eo ufunamaim rafiy bai orot etei nahimaim God ana merar yi, imasib naatu busuruf eaan.
36 Onse analimba mtima nayamba kudyanso.
36 Etei hi’itin koufair hibai naatu etei’imak bay afa hibow yah hirutan.
37 Tonse pamodzi mʼsitimamo tinalipo anthu 276.
37 Naatu aki nati wa afe’en anan nai etei i 276.
38 Onse atadya, nakhuta anapeputsa sitimayo potaya tirigu mʼnyanja.
38 Orot etei bay hi’aa yah biw ufunamaim, wheat nati wa afe’en hi’iuin hibow harew yan hitaiyen hire wa kerer.
39 Kutacha, anthu sanazindikire dzikolo, koma anaona pomwe sitima zimayimapo pamodzi ndi mchenga wa pa gombe. Iwo anaganiza zokocheza sitimayo kumeneko ngati zikanatheka kutero.
39 Mar totoririb ana veya wa afe’en baginayah dones men hi’inan, baise umabibin ana dones hi’itin naatu wa hibai hisinaftobon nati dones yen baitet ra’ahin isan hinunuw.
40 Atadula anangula aja, nawasiya mʼnyanja, pa nthawi yomweyo anamasula zingwe zimene anamangira zowongolera sitimayo. Kenaka anayimika chinsalu chimene mphepo imakankha kuti sitima iyende, ndipo anayamba kupita ku gombe.
40 Wa ana aumor hi’afuw tai yan hi’in naatu gunig ana murab au ta’imon hirufam, imaibo rar hibora’ah wa bai aki au dones anunuw arun.
41 Koma sitimayo inagunda mchenga wobisika ndipo inayima. Mbali ya kutsogolo ya sitimayo inakanirira ndipo sinathe kuyendanso, ndipo mbali yakumbuyo inasweka ndi kuwomba kwa mafunde.
41 Baise wa nunuw rur yabat rab mamay yan yen naatu yara’ah nanane re tatab bai’etaw isan men karam, naatu uranane yabat rab tagurugurus.
42 Asilikali anaganiza za kupha amʼndende onse, kuti angasambire kupita pa mtunda ndi kuthawa.
42 Baiyowayah dibur etei rouw morob isan hiyakitifuw, men hikok boro hitataiy dones hitayen hitabihir.
43 Koma wolamulira asilikali uja anafuna kupulumutsa Paulo ndipo anawaletsa kuchita zimene anakonza. Iye analamulira asilikali kuti amene amatha kusambira kuti adziponye mʼmadzi ndi kuyamba kukafika pa mtunda.
43 Baise baiyowayah hai orot gagamin i Paul tiyawas imih baiyowayah abisa hinot hio i eotanih, naatu iuwih eo, “O yait itaiy isoso’ob wan kukununuw kure kutaiy kwen dones kuyen.
44 Otsalawo anayenera kugwira matabwa kapena tizidutswa ta sitimayo. Motero onse anapulumuka nakafika pa mtunda.
44 Naatu afa i boro uf hinare wa rab tatagurugurus rebarebah afe’eh hinayen hinataiy hinarun.” Aki iti na’atube asinaf etei yawasi ataiy an dones yan ayen men yait ta morob. Wa tafofor hire au dones tetataiy|alt="shipwrecked people making for shore" src="cn02045B.tif" size="col" loc="Act 27.44" copy="©1978 David C. Cook Publishing Co." ref="27.44"
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Atos 27, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.