Atos 26
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Ndipo Agripa anawuza Paulo kuti, “Takulola kuti unene mawu ako.” Paulo anatambasula dzanja lake nayamba kudziteteza kuti,
1 Agripa iu, “O i baibasit abit taiyuw isa inao.” Paul uman bora’ah naatu taiyuwin wasfafar eo,
2 “Mfumu Agripa ine ndikudziyesa wa mwayi kuyima pamaso panu lero lino ndi kudziteteza, kutsutsa zonse zimene Ayuda andinenera,
2 “Aiwob Agripa, ayu i abiyasisir anayabin boun o namaim Jew sabuw abisa isan ayu ubar hibitu i boro ana wasfafaru anao inanowar. Paul aiwob Agripa isah ibibinan|alt="Paul speaking to crowd" src="cn01993b.tif" size="col" loc="Act 26.2" copy="©1978 David C. Cook Publishing Co." ref="26.1-2"
3 ndipo makamaka chifukwa inu mukudziwa bwino miyambo yonse ya Chiyuda ndiponso zonse zimene amatsutsana. Nʼchifukwa chake ndikukupemphani kuti mundimvetsere moleza mtima.
3 Iti ao i turobe, anayabin o i Jew sabuw hai binanakwar naatu hai ofafar iso’ob kwanekwan, imih o abifefeyani yatenanub inama ana’o inanowar.
4 “Ayuda onse akudziwa za moyo wanga mmene ndakhalira kuyambira ndili mwana, kuchokera pachiyambi cha moyo wanga mʼdziko lathu ndiponso mu Yerusalemu.
4 Jew sabuw etei ayu kek ana veya mi’itube ama’am i hiso’ob, ayu au yawas no aneika au tafaramamaim mi’itube ama’am ana Jerusalem atit ama’ama etei i hiso’ob.
5 Iwo akundidziwa kuyambira kalekale ndipo angathe kuchitira umboni kuti ndakhala ndili Mfarisi moyo wanga wonse, mmodzi wa gulu limene limasamala chipembedzo chathu koposa.
5 Ayu i manin maiyow bairi ama, imih ayu i hisu’ubu kwanekwan. Hinakokok na’at hina’orereb. Anaika ayu i Pharisee orot, kwafiren ana ofafar fokarin wanawanan i ayu ama, naatu men kafa’imo ofafar ta astu’ub.
6 Ndipo tsopano ndikuyimbidwa mlandu lero chifukwa cha chiyembekezo changa pa zimene Mulungu analonjeza makolo athu.
6 Naatu boun ayu iti ubar tibitu anayabin God ana’omatanen ai a’agir bitih imaim ayu nuhufot ama’am isan, ubar hitu bairi tao.
7 Ili ndi lonjezo limene mafuko athu khumi ndi awiri akuyembekezera kuti likwaniritsidwe pamene akupembedza Mulungu molimbika usana ndi usiku. Wolemekezeka Mfumu, nʼchifukwa cha chiyembekezo chimenechi Ayuda kuti akundiyimba mlandu.
7 Iti omatanen i aki ai big etei 12 hibitumitum mi’itube hita’itin titurobe, imih fai mar dogoroh tutufin etei God hikwakwafir, naatu anayabin iti baitumatum isan. Aiwobomon, Jew sabuw ayu ubar hitu iti tao.
8 Nʼchifukwa chiyani ena a inu mukuganiza kuti nʼkosatheka kuti Mulungu aukitse akufa?
8 Kwa Jew sabuw iyab iti kwabatabat aisim God sabuw murumurubih ibiyawasih baitutumin isan kwa isa efofokar?
9 “Inenso ndimaganiza kuti ndimayenera kuchita zinthu zambiri pofuna kuthana ndi dzina la Yesu wa ku Nazareti.
9 Ayu auman mat i na’atube anot, sawar moumurih na’in ata sinaf Jesu Nazareth mowan wabin ati’ib isan.
10 Ndipo izi ndi zimene ndinazichita ku Yerusalemu. Ndi ulamuliro wa akulu a ansembe, ine ndinayika mʼndende oyera mtima ambiri, ndipo pamene amaphedwa, ine ndimavomereza.
10 Naatu nati na’atube Jerusalemamaim asinaf. Firis ukwarih biyahine fair abai God ana sabuw moumurih maiyow abow dibur aya. Naatu rouw morobomih teo ana veya ayu auman aibasit terouw temomorob.
11 Nthawi zambiri ndinkapita mʼsunagoge iliyonse kuti alangidwe, ndipo ndinayesera kuwakakamiza kuti achitire chipongwe Mulungu. Mu mkwiyo wangawo, ndimapita ngakhale ku mizinda yachilendo kuti ndikawazunze.
11 Mar moumurih maiyow Kou’ay Bar efan tata’amaim abow biyababan aitih, naatu hai baitumatum baihamiyin isan a’okikimih. Na’atube hai baitumatum baigigimin isan a’okimih, naatu atit an menah tatabirih hai bar hai meraramaim bai akir kakafin maiyow aitih.
12 “Pa ulendo wina wotere, ndikupita ku Damasiko ndi mphamvu ndi ulamuliro ochokera kwa akulu a ansembe,
12 Ana’an iti isan ayu firis ukwarih biyahine fair hitu hiyunu an Damaskas atit.
13 Wolemekezeka Mfumu, nthawi ya masana pamene ndimayenda pa msewu, ndinaona kuwala kuchokera kumwamba koposa kuwala kwa dzuwa kutandizungulira ine pamodzi ndi anzangawo.
13 Baise efamaim anan bi’auyit auman, Aiwobomon, marakaw no marane, mamarakaw men veya na’atube, marakaw kwanekwan re ayu au sabuw bairi anan tarbebera’uhi.
14 Tonse tinagwa pansi ndipo ndinamva mawu mʼChihebri akuti, ‘Saulo, Saulo chifukwa chiyani ukundizunza Ine? Nʼkovuta kulimbikira mtunda wopanda madzi.’ ”
14 Aki etei’imak me yan are, naatu ayu orot fanan anowar Hebrew turamaim iuwu eo, ‘Saul! Saul! aisim ayu irabu kubia’akiru? Ayu kubi’a’akiru i o taiyuw biya irab kubi’a’afiy.’
15 Ndipo ine ndinafunsa kuti, “Ndinu ndani Ambuye?”
15 Ayu aibatiy ao, ‘O yait Regah?’ Naatu Regah eo, ‘Ayu i Jesu, o irabu kubia’akiru.
16 Tsopano dzuka ndipo imirira. Ine ndaonekera kwa iwe kuti ndikusankhe kuti ukhale mtumiki ndiponso mboni ya zimene waziona za Ine ndiponso zimene ndidzakuonetsa.
16 Baise kumisir kubat, ayu o isa abirerereb ana rubini isou inabow naatu boun abisa isa mamatar sabuw afa hai tur ina’owen. Naatu abisa isa namamatar boro ani’obaiyi.
17 Ine ndidzakulanditsa mʼmanja mwa anthu a mtundu wako ndiponso mwa anthu a mitundu ina. Ine ndikukutuma kwa iwo,
17 Ayu o a sabuw Jew umahine naatu Ufun Sabuw umahine boro anatafafari. Ayu abiyafari nati sabuw wanawanahimaim inan,
18 kuti ukatsekule maso awo kuti atembenuke mtima kuchoka ku mdima ndi kulowa mʼkuwala, kuchoka ku mphamvu za Satana ndi kupita kwa Mulungu, kuti alandire chikhululukiro cha machimo awo ndi kukhala mʼgulu la amene akuyeretsedwa chifukwa chokhulupirira Ine.
18 matah inabotawiy naatu guguminane inanawiyih hinatit marakawamaim hinarun. Naatu Satan umane inabow God initin, saise bowabow kakafihine notawiyen hinab, naatu God ana rourubin sabuw wanawanahimaim hai efan hinab hinamare.’
19 “Nʼchifukwa chake Mfumu Agripa, sindinakane kumvera masomphenya wochokera kumwamba.
19 Nati isan Aiwobomon Agripa, ayu abisa marane re ai’itin men ai fanasair.
20 Kuyambira kwa anthu a ku Damasiko, a ku Yerusalemu, a ku Yudeya konse ndi kwa anthu a mitundu inanso, ndinalalikira kuti akuyenera kulapa ndi kutembenukira kwa Mulungu ndikuti aonetse kulapa kwawo mwa ntchito zawo.
20 Bowabow wantoro’ot i Damaskas imaim abusuruf naatu ana sabuw iyab Jerusalem hima’am isah atit, Judea wanawanan etei abinan naatu Eteni Sabuw wanawanahimaim auman a binan. Abibinan anayabin sabuw bowabow kakafihine God isan hitatatabir naatu hai bowabowamaim titurobe i dogor baikitabir hibai.
21 Ichi nʼchifukwa chake Ayuda anandigwira mʼbwalo la Nyumba ya Mulungu nafuna kundipha.
21 Ana’an nati isan Jew sabuw ayu Tafaror Bar wanawanan ana sebosebomaim hibuwu hifatumu rabu morobomih hiwa’an.
22 Koma Mulungu wakhala akundithandiza mpaka lero lino. Ine ndayima pano kuti ndichitire umboni kwa anthu onse otchuka ndi anthu wamba. Ine sindikunena zina zowonjezera koma zimene Aneneri ndi Mose ananena kuti zidzachitika.
22 Baise God tafafaru yawasu ama ana it boun atit, imih o namaim abat orot babin kikimin yen in orot babin gagamin etei matahimaim abisa isou mamatar i ao’orerereb. Ayu au tur ao i dinab oro’orot naatu Moses sawar abisa mataramih hi’o inu’in mamatar imaim ao.
23 Iwo ananena kuti Khristu adzamva zowawa ndipo popeza Iye adzakhala woyamba kuuka kwa akufa, adzalalikira za kuwunika kwa anthu a mtundu wake ndiponso kwa anthu a mitundu ina.”
23 Roubininenayan boro biyan nababan ni’akir naatu morobone, moroboyah wanawanahimaim i boro wan namisir marakaw ana yawas Jew sabuw naatu Ufun Sabuw isah nakurereb.”
24 Paulo akudziteteza, Festo anakweza mawu nati, “Wazungulira mutu Paulo! Kuphunzira kwako kwakuchititsa misala.”
24 Paul iti na’atube taiyuwin wasfafar eo inan auman Festus Paul isan iwow eo, “O i kubikoko’aw so’obamaim nawiyi in kubikoko’aw!”
25 Paulo anayankha nati, “Wolemekezeka Festo, sindine wozungulira mutu. Zimene ndikunena ndi zoona ndiponso za nzeru.
25 Paul iya’afut eo, “Ayu i men abikoko’aw, au Aiwobomon! Tur abisa ao i turobe hai yabih auman.
26 Mfumu ikuzidziwa bwino zinthu izi, ndipo ndikuyankhula momasuka kwa iyo. Ine ndikukhulupirira kuti palibe kanthu nʼkamodzi komwe kamene sukukadziwa, chifukwa izi sizinachike mseri.
26 Aiwob Agripa, ayu o namaim men erebir auman ao’omih, anayabin iti sawar etei o iso’ob, naatu sawar iti himamatar boro men karam nuhinaburumih. Anayabin iti sawar men ta umasusunamaim mataramih.
27 Mfumu Agripa, kodi mumakhulupirira mawu a aneneri? Ine ndikudziwa kuti mumakhulupirira.”
27 Aiwob Agripa o dinab orot kubitutumih? Ayu aso’ob o kubitumatum!”
28 Kenaka Agripa anati kwa Paulo, “Kodi ukuganiza kuti mʼkanthawi kochepa kotere ungandikope kuti ndikhale Mkhristu?”
28 Aiwob Agripa Paul iya’afut eo, “O kunotanot iti veya ta’imon o boro ayu dogorou inikitabir anan Kirisiyan anamatar?”
29 Paulo anayankha kuti, “Ngakhale kanthawi kochepa kapena nthawi yayitali, ine ndikupempha kwa Mulungu kuti osati inu nokha koma aliyense amene akundimva lero lino akhale monga ine, kupatulapo maunyolo okhawa.”
29 Paul iya’afut eo, “Veya kabumin o veya manin ayu au yoyoban God isan i men o akis baise kwa iyab iti boun ao kwanonowar i mi’itube kwatan ayu ama’am na’atube kwatamatar. Baise men akokok hinafatum dibur hinayariyi kwanama.”
30 Mfumu inayimirira pamodzi ndi bwanamkubwa ndi Bernisi ndiponso anthu onse amene anakhala nawo pamodzi.
30 Naatu Aiwob orot, gawan orot Bernis, naatu sabuw afa hima’am etei himisir.
31 Inatuluka mʼchipindamo, ndipo pamene imayankhula inati, “Munthu uyu sanachite kanthu koyenera kuphedwa kapena kumangidwa.”
31 Efan hima tur hinonowar hihamiy hitit, naatu taiyuwih turahinah bairi hibidudur hio, “Iti orot i men abisa ta kakafin sinaf boro namorob o dibur narun.”
32 Agripa anati kwa Festo, “Munthu uyu akanamasulidwa akanakhala kuti sanapemphe zokaonekera kwa Kaisara.”
32 Naatu Aiwob Agripa Festus isan eo, “Iti orot Caesar isan baifefeyanina’e tama’am, iti boun boro ata botait.”
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Atos 26, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.