Atos 23

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI

Sair da comparação
AAI TUR GEWASIN O BAIBASIT BOUBUN
1 Paulo anayangʼanitsitsa anthu a Bwalo Lalikulu nati, “Abale anga, ndakhala ndi chikumbumtima chabwino pamaso pa Mulungu mpaka lero lino.”
1 Paul nuw Kaniser itihkikin naatu eo, “Taituwau ayu au yawas tutufin etei God matanamaim men kafa’imo erekasiy auman ama na iti boun titamih.” Paul Jerusalem kanisel nahimaimbat tibibabatiy|alt="Paul speaking to council in Jerusalem" src="cn01975B.tif" size="col" loc="Act 23.1" copy="©1978 David C. Cook Publishing Co." ref="23.1-6"
2 Chifukwa cha mawu amenewa, mkulu wa ansembe Ananiya analamulira amene anali pafupi ndi Paulo kuti amumenye pakamwa.
2 Iti na’at eo basit Firis Gagamin wabin Ananias orot iyab Paul sisibinamaim hibatabat awan roufoforamih iuwih.
3 Pamenepo Paulo anamuwuza kuti, “Mulungu adzakukantha, iwe munthu wachiphamaso! Wakhala pamenepo kuti undiweruze ine monga mwalamulo, koma iweyo ukuphwanya lamulolo polamulira kuti andimenye!”
3 Baise Paul iu, “God o awa boro narufofoforen, yumat rah ana sis! O baibabatiyenayan orot wai, aisim o taiyuw ofafar ibai awau roufoforenamih sabuw kubiyunih!”
4 Anthu amene anayimirira pafupi ndi Paulo anati, “Bwanji ukunyoza mkulu wa ansembe wa Mulungu?”
4 Orot Paul sisibin hibatabat hio, “O God ana Firis Gagamin isan men tur kakafih inao’omih!”
5 Paulo anayankha nati, “Abale, ine sindinazindikire kuti ndi mkulu wa ansembe; pakuti kunalembedwa kuti, ‘Usayankhule zoyipa kwa mtsogoleri wa anthu ako.’ ”
5 Paul iyafutih eo, “Teutuwau ayu men aso’ob i Firis Gagamin. Buk Atamaninamaim eo, ‘O men tur kakafin a sabuw hai bonawiyenayan isan inao’omih.’”
6 Paulo atazindikira kuti ena mwa iwo anali Asaduki ndiponso ena anali Afarisi, anafuwula mʼbwalo muja kuti, “Abale anga, ine ndine Mfarisi, mwana wa Mfarisi. Ndikuweruzidwa chifukwa cha chiyembekezo cha kuuka kwa akufa.”
6 Imaibo nati ana maramain Kaniser sabuw Paul inanih, sabuw nati’imaim hiruru’ay afa i Sadducee afa i Pharisee, naatu Paul Kaniser sabuw isah fanan aumetawat eaf eo, “Teituwou! Ayu i Pharisee, naatu Pharisee orot natun. Ayu iti baibatiyen efanamaim abatabat anayabin abitumatum morobone misir maiye ana nuhufot abai ama’am isan!”
7 Iye atanena zimenezi, mkangano unabuka pakati pa Afarisi ndi Asaduki mpaka anthu kugawikana.
7 Iti na’atube eo ana maramaim, Pharisee naatu Sadducee bairi hitarayouw higam naatu kou’ay hikusib.
8 Asaduki amati kulibe kuuka kwa akufa, kulibenso ngakhale angelo kapena mizimu, koma Afarisi amakhulupirira zonsezi.
8 Anayabin Sadducee tibitumatum sabuw moroboyah boro men hinamisir maiye, naatu tounamatar men tema’am naatu afiy auman en. Baise Pharisee it sawar tounu etei isah tibitumatum.
9 Panali phokoso lalikulu, ndipo aphunzitsi ena amalamulo amene anali a gulu la Afarisi anayimirira natsutsa kwambiri. Iwo anati, “Ife sitikupeza cholakwa ndi munthu uyu, chifukwa mwina ndi mzimu kapena mngelo amene wayankhula naye.”
9 Naatu gamin gagamin na’in matar, Ofafar bai’obaiyenayah iyab Pharisee ana kou’ay himisir fanah sib higam hio, “Paul i men abisa ta kakafin sinafumih, men taso’ob afiy o tounamatar ta na hairi hio.”
10 Mkangano unakula kwambiri kotero kuti mkulu wa asilikali anachita mantha kuti mwina anthu angakhadzule Paulo. Iye analamulira asilikali ake apite kukamuchotsa pakati pawo mwamphamvu ndi kubwera naye ku malo a asilikaliwo.
10 Gamin ra’at sasa, naatu baiyowayah hai orot ukwarin bir eo, Paul boro hinarab hinatensisib, naatu baiyowayah iuwih hire hin kou’ay wanawanan hirun Paul umahine hiba’aruwih hibai hina hai bar hiyari’ay.
11 Usiku omwewo Ambuye anayimirira pambali pa Paulo nati, “Limba mtima! Monga wandichitira Ine umboni mu Yerusalemu, moteronso uyenera kundichitira umboni ku Roma.”
11 Nati gugumin Regah na Paul sisibinamaim bat eo “Koufair inab! Jerusalemamaim ayu isou i’orereb na’atube inan Rome imaim ef ta’imon inasinaf inaorerereb.”
12 Kutacha Ayuda ena anakonza chiwembu ndipo analumbira kuti sadya kapena kumwa mpaka atapha Paulo.
12 Marto, marauman Jew sabuw afa hina hita’imon hiyakitifuw naatu omatanen hiwa’an harew o bay men hinaa hinatom hinama’am Paul hinarab namorobabo.
13 Anthu amene anakonza chiwembuchi analipo makumi anayi.
13 Sabuw iyab Paul asabunin isan hiyayakitifuw nah etei i 40 na’atube tafanamaim auman.
14 Iwo anapita kwa akulu a ansembe ndi akuluakulu a Ayuda nakawawuza kuti, “Ife talumbira kolimba kuti sitidya kalikonse mpaka titapha Paulo.
14 Imaibo hin firis ukwarih naatu regaregah ai’in biyah hitit hio, “Aki etei omatanen fokarin a’obaifaro bay boro men anaa anama nan Paul ana’asabun imaibo boro bay anaa.
15 Tsopano inu pamodzi ndi akuluakulu a Bwalo Lalikulu mupemphe mkulu wa asilikali kuti akubweretsereni Paulo ngati kuti mukufuna kudziwa bwino za mlandu wake. Ife takonzeka kudzamupha asanafike kumeneko.”
15 Isan imih boun aki akokok kwa naatu Kaniser bairi tur kwaniyafar Rome Baiyowayan isan Paul nab kwa isa nare nan. Kwanifuw taiyuwin biyanamaim nuwet gewas kwanarouw kwanao nare nan. Baise aki boro efamaim anawa’ir anama’am nanan ana’asabun.”
16 Koma mwana wa mlongo wake wa Paulo atamva za chiwembuchi, anapita ku malo a asilikali aja namufotokozera Paulo.
16 Baise Paul rubin babin natun hiyayanuw nowar basit na barik bar tit run Paul ana tur eowen.
17 Paulo anayitana mmodzi wa wolamulira asilikali 100 aja, namuwuza kuti, “Pita naye mnyamatayu kwa mkulu wa asilikali. Iyeyu ali ndi mawu oti akamuwuze.”
17 Naatu Paul sorodiy orot ta isan eaf na iu, “Iti monokai kwabai kwan baiyowayan ukwarin biyan, i tur ta boro ana tur na’owen.”
18 Anamutengadi mnyamatayo napita naye kwa mkulu wa asilikali uja, nati, “Wamʼndende uja Paulo anandiyitana, nandipempha kuti ndibweretse mnyamatayu kwa inu chifukwa ali ndi kanthu koti akuwuzeni.”
18 Baiyowayah hai orot gagamin monokai bai in baiyowayan ukwarin biyan tit eo, “Dibur orot Paul eaf arun orot iti abai o isa anan anayabin i boro tur ta nao inanowar.”
19 Mkulu wa asilikali uja anagwira dzanja mnyamatayo napita naye paseli ndipo anamufunsa kuti, “Kodi ukufuna kuti undiwuze chiyani?”
19 Baiyow hai ukwarin orot uman bai nawiy nabin akisihimo hin naatu ibatiy, “O abisa kukokok boro inao ananowar?”
20 Mnyamatayo anati, “Ayuda agwirizana zoti akupempheni kuti mawa mubwere ndi Paulo ku Bwalo Lalikulu, ngati kuti akufuna kudziwa bwino za iye.
20 Orot iya’afut eo, “Jew orot gagagamih etei hibasit maras boro o hinifefeyani Paul inab inare Kaniser hai kou’ayomaim ana yare hinanuwetamih, baise nati i hai baifuwen.
21 Inu musawamvere, chifukwa pali anthu opitirira makumi anayi amene akumudikirira pa njira. Iwo alumbira kuti sadya kapena kumwa mpaka atapha Paulo. Panopa ndi okonzeka kale, akungodikira kuti muwavomere pempho lawo.”
21 Imih hai tur men inanowar, anayabin orot etei 40 tafanamaim auman boro efamaim hinawa’ir hinama hinakaif. Iti oro’orot i omatanen fokarin hio baifaro bay harew hairi boro men hinaa, hinama’am Paul hina’asabunibo bay hinaa harew hinatom. Etei i sinafumih hiyabuna sawar o anot abisa inao’o i hima tekakaif.”
22 Mkulu wa asilikaliyo anawuza mnyamatayo kuti apite koma anamuchenjeza kuti, “Usawuze munthu aliyense kuti wandifotokozera zimenezi.”
22 Baiyowayan ukwarin eo, “Men yait ta ana tur ina’owen abisa io anonowar.” Naatu orot iyafar tit in.
23 Kenaka mkulu wa asilikaliyo anayitana awiri a asilikali olamulira asilikali 100 nawalamula kuti, “Uzani asilikali 200, asilikali 70 okwera pa akavalo ndi 200 onyamula mikondo kuti akonzeke kupita ku Kaisareya usiku omwe uno nthawi ya 9 koloko.
23 Baiyowayah hai orot gagamih rou’ab eafih hina iuwih eo, “Baiyowayah 200 kwanabow, horse ana orot etei 70, naatu 200 ahay bowayah, kwanabobuna boun gugumin nine korok iti tafaram kwanihamiy kwanan Caesarea kwanatit.
24 Mumukonzerenso Paulo akavalo woti akwerepo kuti akafike bwino kwa bwanamkubwa Felike.”
24 Horse ta Paul kwanitin afe’en namare naatu kwanatafafar gewas kwanab kwanan Gawan Felix biyan kwanatit kwanitubar.”
25 Iye analemba kalata iyi:
25 Imaibo baiyowayah hai ukwarin mare fef kirum eo.
26 Ine Klaudiyo Lusiya,
26 “Ayu Claudius Lysias, O Felix gawan orot gewas
27 Munthuyo Ayuda anamugwira ndipo anali pafupi kumupha, koma ine ndinapita ndi asilikali nʼkukamulanditsa pakuti ndinamva kuti ndi nzika ya Chiroma.
27 Iti orot i Jew sabuw hibai kafa’imo
28 Ndinkafuna kudziwa mlandu umene anapalamula, choncho ndinapita naye ku Bwalo lawo Lalikulu.
28 Ayu akok i ataso’ob yabin
29 Ine ndinapeza kuti amamuyimba mlandu wa nkhani ya malamulo awo, koma panalibe mlandu woyenera kumuphera kapena kumuyika mʼndende.
29 Anunuwet men abisa kakafin iwa’an
30 Nditawuzidwa kuti amukonzera chiwembu munthuyu, ine ndamutumiza kwa inu msanga. Ine ndalamulanso amene akumuyimba mlanduwo kuti abwere kwa inu kudzafotokoza nkhaniyo.
30 Naatu
31 Pamenepo asilikali aja anatenga Paulo monga anawalamulira napita naye ku Antipatri usiku.
31 Baiyowayah hai bowabow hibitih na’atube hisinaf, Paul hibai gugumin wanawanan hinawiy hin kakafih hai wawa’ir ana sou Antipatris imaim hitubar.
32 Mmawa mwake iwo anabwerera ku malo a asilikali nasiya okwera pa akavalo kuti apitirire ndi Paulo.
32 Naatu marto baiyowayah ahiwat himatabir maiye hina yarir bar hitit, baise horse hai orot i Paul hinawiy bairi hin.
33 Asilikali okwera pa akavalowo atafika ku Kaisareya anapereka kalatayo kwa bwanamkubwa, namuperekanso Paulo.
33 Hinawiy hina Caesarea hitit fef gawan hitin naatu Paul auman hibai hirun umanamaim hiyai.
34 Bwanamkubwayo anawerenga kalatayo ndipo anamufunsa Paulo za dera limene amachokera. Atazindikira kuti amachokera ku Kilikiya,
34 Gawan fef iyab naatu Paul ibatiy ana tafaram menane na, naatu Paul ana tafaram Silisia’ane rouw eo nonowar ana maramaim
35 iye anati, “Ndidzamva mlandu wako okuyimba mlandu akabwera kuno.” Ndipo analamulira kuti asilikali adzimulondera Paulo ku nyumba ya mfumu Herode.
35 eo, “Ayu boro a kamabiy sabuw hinanabo inao anowar.” Imaibo iuwih hibai hin gawan ana bar gagaminamaim dibur bar hiyari’y.

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Atos 23, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.