Atos 22

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI

Sair da comparação
AAI TUR GEWASIN O BAIBASIT BOUBUN
1 Iye anati, “Inu abale anga ndi makolo anga, tamvani mawu akudziteteza kwanga.”
1 “Tamai’inah, naatu taitu tuwai’inah au wasfafaren ana tur anao kwananowar.”
2 Atamva iye akuyankhula Chihebri, anakhala chete.
2 Hebrew turamaim eo hinonowar ana veya etei surur binon tar.
3 “Ine ndine Myuda, wobadwira ku Tarisisi wa ku Kilikiya, koma ndinaleredwa mu mzinda muno, ndinaphunzitsidwa mwatsatanetsatane kusunga malamulo a makolo athu ndi Gamalieli ndipo ndinali wodzipereka pa za Mulungu monga mmene inu mulili lero.
3 “Ayu i Jew orot Tarsus imaim atufuw tafaram Silisia wanawanan, baise Jerusalemamaim ama ara’at. Gamaliel ana bai’obaiyen babanamaim ama, uwatanah hai ofafar etei ayu i’obaiyu, naatu ayu i baibobowenayan orot ta God ana ofafar tur isan, kwa boun iti kwama’am na’atube.
4 Ine ndinkazunza anthu otsatira Njirayi mpaka kuwapha. Ndinkagwira amuna ndi amayi ndi kuwayika mʼndende.
4 Sabuw iyab ef iti hibi’ufun abow ai’a’akirih arouw asbunubunuwen naatu afa abow ana dibur aya.
5 Mkulu wa ansembe ndiponso akuluakulu a Ayuda angathe kundichitira umboni. Iwowa anandipatsa makalata opita nawo kwa abale awo ku Damasiko. Ndipo ndinapita kumeneko kuti ndikawagwire anthu amenewa ndi kubwera nawo ku Yerusalemu kuti adzalangidwe.
5 Firis Gagamin naatu Kaniser tutufin etei abisa ao i hiso’ob turobe. Anayabin i fef hikirum hitu abai an Damaskas wanawanan, sabuw baitumatumayah nati’imaim hima’am fatumih bow na Jerusalem tit isan ayen an.”
6 “Nthawi ya masana, nditayandikira ku Damasiko, mwadzidzidzi kuwala kwakukulu kochokera kumwamba kunandizungulira.
6 “Ana Damaskas abiyubin auman i’ouyit, naniyan meyemeye marakaw namanamarabe bow marane ra’iy sisibu etei marakaw.
7 Ndinagwa pansi ndipo ndinamva mawu akuti, ‘Saulo! Saulo! Ukundizunziranji?’ ”
7 Ayu me yan ara’iy rabu naatu orot ta fanan anowar eo, ‘Saul! Saul! O aisim ayu kubi’a’akiru?’
8 Ine ndinafunsa kuti, “Ndinu ndani Ambuye?”
8 Ayu aibatiy ao ‘Regah o yait? Iyafutu eo,
9 Anzanga a paulendo anaona kuwalako, koma sanamve mawuwo, a Iye amene amayankhula nane.
9 Sabuw bairi anan marakaw hi’itin, baise orot ayu isou eo fanan men hinowar.
10 Ine ndinafunsa kuti, “Kodi ndichite chiyani Ambuye?”
10 Ayu aibatiy, ‘Regah ayu boro abisa anasinaf?’
11 Anzanga anandigwira dzanja kupita nane ku Damasiko, popeza kuwala kunja kunandichititsa khungu.
11 Naatu au sabuw bairi anan umou hibai hinawiyu an Damaskas atit, anayabin marakaw ana bonamanamarin re ayu matou yi ifim.
12 “Munthu wina dzina lake Hananiya anabwera kudzandiona. Iyeyu anali munthu woopa Mulungu ndi wosunga Malamulo. Ayuda onse okhala kumeneko amamupatsa ulemu waukulu.
12 Nati bar meraramaim i orot wabin Ananias God, ana orot ta ma’am, ofafar etei i bobosiyasiyar naatu Jew sabuw nati’imaim hima’am etei i hikakakafiy.
13 Iye anayimirira pafupi nane nati, ‘Mʼbale Saulo, penyanso!’ Ndipo nthawi yomweyo ndinapenya ndikumuona iyeyo.
13 Na biyou tit sisibu’umaim bat naatu eo, ‘Taiu Saul, mata ekubunai kunuw maiye!’ Mar ta’imon matau kubunai anuw Ananaias a’itin.
14 “Ndipo iye anati, ‘Mulungu wa makolo athu wakusankha iwe kuti udziwe chifuniro chake ndi kuona Wolungamayo ndi kumva mawu ochokera pakamwa pake.
14 Imaibo iuwu eo, ‘Uwatanah hai God o rubini i ana kok o so’ob isan, saise Orot ana Yawas Mutufurin boro ina’itin naatu abisa nao’o o taiyuw tainika fanan inanowar.
15 Iwe udzakhala mboni yake kwa anthu onse pa zimene waziona ndi kuzimva.
15 Anayabin o boro i isan inakubuna, abisa i’itin naatu inonowar sabuw etei hai tur ina’owen.
16 Ndipo tsopano ukudikira chiyani? Dzuka ndi kutama dzina la Ambuye mopemba, ubatizidwe ndi kuchotsa machimo ako.’
16 Imih boun abisa ao inonowar aisim boro inama inakaif? Kumisir bapataito kubai, naatu kuyoyoban a bowabow kakafih ekusouwen.’
17 “Nditabwerera ku Yerusalemu, ndikupemphera mʼNyumba ya Mulungu, ndinachita ngati ndakomoka.
17 “Ayu amatabir maiye ana Jerusalem atit naatu ayoyoyoban ana maramaim matou bora’ah ina’inanen ta aitin.
18 Ndinaona Ambuye akundiwuza kuti, ‘Fulumira! Tuluka mu Yerusalemu msangamsanga, chifukwa anthuwa sadzavomereza umboni wako wonena za Ine.’ ”
18 Nati matou bobora’ah ana maramaim Regah aitin naatu isou eo, ‘Mata nakabiy Jerusalem saisewat inihamiy, anayabin iti’imaim ayu isou inaorereb sabuw boro men hinitumatum.’
19 Ine ndinayankha Ambuye kuti, “Anthu awa akudziwa kuti ine ndinkapita ku sunagoge iliyonse ndipo ndinkawaponya mʼndende ndi kuwakwapula amene ankakhulupirira inu.
19 Ayu ai ya’afut ao, ‘Regah sabuw etei hiso’ob ayu Kou’ay Bar ta ta arun atit sabuw iyab o hibitutumi abow arow afatum dibur aya’ay.
20 Ndipo pamene ankapha Stefano, ine ndinali pomwepo kuvomereza ndi kusunga zovala za amene amamupha.”
20 Naatu Stephen orot wantoro’ot iti ef isan hirab ana rara re’er ana veya ayu i nati’imaim.’ Ayu auman aisaito hirab morob naatu sabuw iyab hi’a’asabun hai faifuw i ayu abotanen abat.
21 Pamenepo Ambuye anandiwuza kuti, “Nyamuka; Ine ndidzakutuma kutali kwa anthu a mitundu ina.”
21 Imaibo Regah ayu iuwu eo, ‘O abiyafari inan ef yok Ufun Sabuw isah.’”
22 Gulu la anthu linamvetsera mawu a Paulo mpaka pamene ananena izi, kenaka anakweza mawu awo nafuwula kuti, “Ameneyo aphedwe basi! Ngosayenera kukhala moyo!”
22 Sabuw hibat Paul eo hinowar in ana tur sawar. Baise iban maiye sabuw hibusuruf hitar koukuw hio? Sa’ab kwabai kwan! Kwa’asabun! Men karam boro nama!”
23 Akufuwula ndi kuponya zovala zawo ndi kuwaza fumbi kumwamba,
23 Hitar koukuw fah sib hai faifuw hibow hirudab, naatu fofob hibow asir hirouw kwanekwan.
24 mkulu wa asilikali analamulira kuti amutenge Paulo kupita naye ku malo a asilikali. Iye analamula kuti Paulo akwapulidwe kwambiri ndi kumufunsa kuti apeze chimene anthu ankafuwulira chotere.
24 Baiyowayan hai orot ukwarin iuwih Paul hibai baiyowayah hai bar wanawanan hirun naatu wabirin isan iuwih, saise biyan tababan tao hitanowar ana’an aisim Jew sabuw iti na’atube isan fanah sibisib.
25 Atamumanga kuti amukwapule, Paulo anati kwa msilikali wolamulira asilikali 100 amene anayima pamenepo, “Kodi malamulo amalola kukwapula nzika ya Chiroma imene sinapezedwe yolakwa?”
25 Baise wabirinamih hibai hifafatum ana veya Paul baiyowayan hai bonawiyenayan orot ukwarin ta i nati sisibinamaim batabat itin naatu ibatiy, “Orot Rome tafaram bai matuwan isan ana fef bai ema’am, baibatiyinae asir kwanarabirab boro ofafar kwana’astu’ub ai en?”
26 Wolamulira asilikali 100 uja atamva zimenezi, anapita kwa mkulu wa asilikali ndi kumufotokozera. Iye anafunsa kuti, “Kodi mukuchita chiyani ndi munthuyu amene ndi nzika ya Chiroma?”
26 Baiyowayah hai bonawiyenayan orot ukwarin iti tur nonowar ana veya in baiyowayah hai orot ukwarin ibatiy, “O abisa inasinafumih? Iti orot i Rome ana fef bai ema’am.”
27 Mkulu wa asilikali uja anapita kwa Paulo ndipo anamufunsa kuti, “Tandiwuze, kodi ndiwe nzika ya Chiroma?”
27 Naatu baiyowayah hai orot ukwarin na Paul ibatiy eo, “Kuo anowar, o i Rome ana fef ibai kuma’am?”
28 Kenaka mkulu wa asilikaliyo anati, “Ine ndinapereka ndalama zambiri kuti ndikhale nzika.”
28 Imaibo baiyowayah hai orot ukwarin eo, “Ayu iti tafaram bai matuwan isan kabay gagamin na’in au fef atubun.” Baise Paul iya’afut eo, “Ayu i Rome wanawanan atufuw.”
29 Iwo amene anati amufunse analeka nthawi yomweyo. Mkulu wa asilikali uja anachita mantha atazindikira kuti wamanga Paulo amene ndi nzika ya Chiroma.
29 Sabuw iyab baibatiyinamih hinan marta’imon au’uf hibat. Baiyowayah hai orot ukwarin ana bir ra’at, anayabin Paul Rome ana fef bai ma’am so’oba’e bai fatum.
30 Mmawa mwake, mkulu wa asilikali pofuna kupeza chifukwa chenicheni chimene Ayuda amamunenera Paulo, anamumasula ndipo analamula kuti akulu a ansembe ndi onse akuluakulu a Bwalo Lalikulu asonkhane. Ndipo iye anabweretsa Paulo namuyimiritsa patsogolo pawo.
30 Marto mar auman baiyowayah hai orot ukwarin kok taso’ob gewas, aisim Jew sabuw Paul hibubuw hi’u’u kwanikwaniy, Paul hifatum ma’am hirufamen, naatu firis ukwarih Kaniser tutufin etei iuwih hiru’ay. Imaibo Paul bai na nahimaim bat.

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Atos 22, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.