Atos 20

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI

Sair da comparação
AAI TUR GEWASIN O BAIBASIT BOUBUN
1 Litatha phokoso, Paulo anayitanitsa ophunzira ndipo atawalimbikitsa anawatsanzika ndipo ananyamuka kupita ku Makedoniya.
1 Sabuw hibuyuw in sawar nuwarob ea’afuw ufunamaim, Paul bai’ufununayah etei e’af ayuwih koufair tur itih naatu eo tuturih. Imaibo ihamiyih au Masedonia na’at in.
2 Iye anayendera madera a kumeneko, nalimbitsa mtima anthu, ndipo pomaliza pake anapita ku Grisi.
2 Naatu Masedonia ana uman men sanet imaim bar merar ta ta run tit baitumatumayah isah binan koufair itih remor na Greek tit.
3 Kumeneko anakhala miyezi itatu. Popeza kuti Ayuda anakonza zomuchita chiwembu pamene amati azinyamuka kupita ku Siriya pa sitima ya pamadzi, iye anaganiza zobwereranso kudzera ku Makedoniya.
3 Nati’imaim sumar tounu ma, naatu au Syria na’at na isan bobobuna Jew sabuw rabinamih hiyayakitufuw tur nowar. Imih i ana not bogaigiwas matabir maiye Masedonia awat na.
4 Iye anapita pamodzi ndi Sopatro mwana wa Puro wa ku Bereya, Aristariko ndi Sekundo a ku Tesalonika, Gayo wa ku Derbe ndi Timoteyo, ndipo a ku Asiya anali Tukiko ndi Trofimo.
4 Orot iti na’atube i hitur bairi hin, Berea bar merarane i orot Fairahus natun Sopater, Thessalonica’ane i Aristakus, Secundus hairi, Derbe’ine i Gaius, naatu Asia’ane i Tychicus, Trofimus hairi, naatu Timothy.
5 Anthu amenewa anatsogola ndipo anakatidikira ku Trowa.
5 Iti oro’orot i wa ta hibai wan hirabon Troas imaim hima aki hikaifi.
6 Koma ife tinayenda pa sitima ya pamadzi kuchokera ku Filipi chitatha Chikondwerero cha Buledi wopanda Yisiti. Patapita masiku asanu tinakumana nawo enawo ku Trowa, ndipo tinakhala kumeneko masiku asanu ndi awiri.
6 Faraw Wanawanan Yeast En ana hiyuw sasawar ufunamaim Philipi imaim wa abai, veya umat roun ufunamaim Troas imaim ai ta’imon, nati’imaim fur ta’imon ama.
7 Pa tsiku loyamba la Sabata, tinasonkhana kuti tidye mgonero. Paulo analalikira kwa anthu chifukwa anaganiza zoti achoke tsiku linalo, ndipo analalika mpaka pakati pa usiku.
7 Fur antoro’ot ebubusurufimaim, bai’ufununayah etei rafiy kakafiyin baimasibin isan abita’ay ana veya, Paul binan sabuw iuwih naatu mar natot boro nan, imih kutuw binan in fainaiwan tit.
8 Munali nyale zambiri mʼchipinda chammwamba mʼmene tinasonkhanamo.
8 Naatu bar tafan aki ama’amamaim i ramef moumurih na’in hitoto’ab.
9 Pa chipinda chachitatu chammwamba cha nyumbayo, pa zenera, panakhala mnyamata wina dzina lake Utiko, amene ankasinza pomwe Paulo amayankhulabe. Atagona tulo, iye anagwa pansi kuchokera pa chipinda chammwamba ndipo anamutola atafa.
9 Bar ana sou awanamaim i orot boubun wabin Eutikas ma Paul ana binan nonowar. Baise Paul kutuw binan ma nowar inan busuruf matan fot taf koukuw. Naatu naniyan meyemeye matan anababatun fot ikitabir bar noyate tafan ana tet tounu imaim hima’am raiy rab easabun, hire murubin hibai hibora’ah.
10 Paulo anatsika, nadziponya pa mnyamatayo, namukumbatira. Paulo anati, “Musadandaule, ali moyo!”
10 Baise Paul raiy orot isnowah kwafure rouh eo, “Men kwaniyababan, yawasin inu’in.”
11 Kenaka Paulo anakweranso, mʼchipinda muja nanyema buledi nadya. Atayankhula mpaka kucha, anachoka.
11 Imaibo matabir maiye yen bar tafan rafiy bai imasib eaan. Naatu fai manin ma binan in mar tot basit ihamiyih.
12 Anthu anatenga mnyamatayo kupita kwawo ali moyo ndipo anatonthozedwa mtima kwambiri.
12 Orot yawasin hibai hin au bar dogoroh ereyasisir auman.
13 Ife tinatsogola kukakwera sitima ya pa madzi kupita ku Aso, kumene tinayembekeza kukatenga Paulo. Iye anakonza motero chifukwa amayenda wapansi.
13 Wa abai arabon an Asos atit naatu Paul iu’uwi na’atube baiwaninamih arun, anayabin i ababawat boro ufui rarabon.
14 Pamene anakumana nafe ku Aso tinamutenga ndipo tinapita ku Mitilene.
14 Tafaram Asos imaim bairi abitar ana veya na wa afe’en yen bairi ana Mitilin atit.
15 Mmawa mwake tinachoka kumeneko pa sitima ya pamadzi ndipo tinafika pafupi ndi Kiyo. Tsiku linalo tinawolokera ku Samo, ndipo tsiku linanso tinafika ku Mileto.
15 Mar to wa ainatit ana Kios nuw aihamiy, veya bairou’abin ufunamaim Samos nuw a’afuwabon, naatu veya baitounin ana Miletus atit.
16 Paulo anali atatsimikiza kuti alambalale Efeso kuopa kutaya nthawi ku Asiya, pakuti ankafulumira kuti akafike ku Yerusalemu kuti ngati nʼkotheka kuti tsiku la Pentekosite akakhale ali ku Yerusalemu.
16 Paul Ephesus baihamiyin mutufor yan rabon isan ana not bogaigiwas, men kok boro veya gagamin Asia wanawananamaim tama, anayabin bimatkabiy ana kok i Jerusalem natitabo Pentecost ana veya nab.
17 Paulo ali ku Mileto, anatumiza mawu ku Efeso kuyitana akulu ampingo.
17 Miletus imaim Paul Ephesus ekaleisia orot ukwarih na bairi o isan isah tur iyafar.
18 Iwo atafika, Paulo anati, “Inu mukudziwa mmene ndinakhalira nanu nthawi yonse imene ndinali nanu kuyambira tsiku loyamba limene ndinafika ku Asiya.
18 Naatu hina hititit ana veya iuwih eo “Ayu boubuntoro’ot ana Asia wanawanan atit bairi mi’itube tama’am i kwa kwaso’ob.
19 Ndinatumikira Ambuye modzichepetsa kwambiri ndiponso ndi misozi, ngakhale ndinayesedwa kwambiri ndi ziwembu za Ayuda.
19 Taiyuwu ayara’iyu Regah ana akir wairafin na’atube yawas fokarin wanawanan wainabu abow eremamaturu auman, Jew sabuw asabunu isan hiyakitifuw men anot.
20 Inu mukudziwa kuti, sindinakubisireni kanthu kalikonse kopindulitsa koma ndinakuphunzitsani poyera komanso nyumba ndi nyumba.
20 Kwa kwaso’ob ayu kwa isa abibinan ana veya men kafa’imo abir, a baibais ana tur ta abotanimih, en baise etei bebeyanamaim bar arun atit a binan kwanowar.
21 Ine ndinawuza Ayuda komanso Agriki kuti ayenera kutembenukira kwa Mulungu polapa ndikuti akhulupirire Ambuye athu Yesu.
21 Jew sabuw naatu Ufun Sabuw isah i bebeyan hai kakafih baihamiyen God isan tatabir naatu Regah Jesu baitutumin isan auwih.
22 “Ndipo tsopano, mokakamizidwa ndi Mzimu, ndikupita ku Yerusalemu, sindikudziwa zimene zikandichitikire kumeneko.”
22 Naatu boun Anun kakafiyin fatumu, i ana kokomaim au Jerusalem anan, men aso’ob nati’imaim boro abisa isou namatar.
23 Chimene ndikudziwa ndi chakuti Mzimu Woyera wandichenjeza mu mzinda uliwonse kuti ndende ndi mavuto zikundidikira.
23 Ta’imonamo Anun Kakafiyin bimatnuwu i aso’ob, bar merar ta ta anarun anatitit dibur naatu biyababan i nati’imaim hima tekakaifu.
24 Koma sindilabadira konse za moyo wanga ngati kuti ndi wa mtengo wapatali kwa ine, malingana ndikatsirize ntchito yanga ndi utumiki umene Ambuye Yesu anandipatsa, ntchito yochitira umboni Uthenga Wabwino wachisomo cha Mulungu.
24 Baise ayu taiyuw au yawas ai’itin i men sawar gagamin ta. Ayu au kok i bowabow Regah Jesu bitu i ana bow yomanin ana’asa’ub, naatu nati bowabow i tur gewasin God ana manaw ana kabeber isan anao rerereb.
25 “Tsopano ndikudziwa kuti inu nonse amene ndinakuyenderani ndi kumakulalikirani ufumu wa Mulungu simudzaonanso nkhope yanga.
25 Naatu boun kwa iyab wanawanamaim ama aremor God ana aiwob isan a binan kwanonowar aso’ob boro men kwana’itu maiye.
26 Chifukwa chake, ine ndikukuwuzani lero kuti ndilibe mlandu ndi munthu aliyense.
26 Isan imih boun kwa etei matamaim akukurereb, o yait ef inasa’ir inan inamomorob ana bit men ayu anab.
27 Pakuti sindinakubisireni pokulalikirani chifuniro chonse cha Mulungu.
27 Anayabin God abisa not yayakitifuw etei akurereb kwanowar sawar men ta abotan au’uf abatamih.
28 Mudziyangʼanire nokha ndiponso muyangʼanire gulu lankhosa limene Mzimu Woyera anakuyikani kuti mukhale oyangʼanira ake. Khalani abusa a mpingo wa Mulungu umene Iye anawugula ndi magazi ake.
28 Taiyuw mata toniwa’an kwanakaifi, naatu bobaituw Anun Kakafiyin kwa babamaim ya’aya kwanakaifih. God ana ekaleisia kwaninabatan gewas, anayabin i taiyuwin Natun momorobomaim sinaf nati sabuw hina nowan himatar.
29 Ndikudziwa kuti ndikachoka ine, padzafika mimbulu yolusa pakati panu imene sidzalekerera gulu lankhosalo.
29 Ayu aso’ob kwa ana bihamiy ufunamaim haru kakafih boro hinan wanawan hinarun bobaituw hinatar giyigiyih.
30 Ngakhale pakati pa inu nokha padzapezeka anthu oyankhula zonama ndi cholinga chofuna kukhala ndi ophunzira kuti awatsate.
30 Kwa taiyuw a kou’ay wanawananamaim auman orot afa boro hinamisir turobe hinabotabir hinifufuwen, saise bai’ufununayah boro i hini’ufnunih.
31 Tsono inu, samalani! Kumbukirani kuti kwa zaka zitatu, usana ndi usiku ndiponso ndi misozi sindinaleke kuchenjeza aliyense wa inu.
31 Imih mata toniwa’an! Kwamur tounu bairi tama fai mar erematuru abimatnuwih i kwananot.
32 “Tsopano ine ndikukuperekani kwa Mulungu ndiponso kwa mawu a chisomo chake, amene ali ndi mphamvu zokulitsa inu ndi kukupatsani chuma pakati pa onse amene anayeretsedwa.
32 Naatu boun kwa i God ana tafafarenamaim ayayariyi naatu i ana manaw ana kabeber turamaim nawowabi kwanayen abisa ana sabuw baitihimih eo kwa auman nowamih nit.
33 Ine sindinasirire siliva kapena golide kapena zovala za munthu aliyense.
33 Ayu men kafai orot babin ta ana gold o ana silver isan abahiy o ana ar ana faifuw isan abahiyamih.
34 Inu nomwe mukudziwa kuti manja angawa ananditumikira kuti tipeze zimene ine ndi anzanga tinkazifuna.
34 Kwa etei kwaso’ob, ayu taiyuwu umau’umaim sawar abisa isah abiyababan asinaf himatar abow, naatu bow turou’unah hibiyababan afaram hibow karam.
35 Pa zonse zimene ndinachita, ndinakuonetsani kuti pogwira ntchito molimbika motere tiyenera kuthandiza ofowoka, pokumbukira mawu a Ambuye Yesu akuti, ‘Kupereka kumadalitsa kuposa kulandira.’ ”
35 Ayu ef etei ai’obaiyi, kwanabow raro nababan, saise nati’imaim boro sabuw aurih fair en kwanibaisih. Ata Regah Jesu taiyuwin awanamaim iti tur eo i kwananot ’Baitinin ana baigegewasin i ra’at men tabaib na’atube.”
36 Atanena zimenezi, anagwada pansi pamodzi ndi ena onse, napemphera.
36 Paul eo sasawar ufunamaim sun yowen bairi hiyoyoban.
37 Onse analira pamene amamukumbatira ndi kupsompsona.
37 Sabuw etei erererey auman hirouh himamay naatu hio tutur.
38 Chimene chinamvetsa chisoni kwambiri ndi mawu ake akuti sadzaonanso nkhope yake. Kenaka iwo anamuperekeza ku sitima yapamadzi.
38 Etei hai yababan ra’at anayabin tur iti na’atube eo isan, ayu boro men ana’iti maiye naatu hinawiy bairi hin wa biyan hitit.

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Atos 20, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.