Atos 12

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI

Sair da comparação
AAI TUR GEWASIN O BAIBASIT BOUBUN
1 Inali nthawi yomweyi imene mfumu Herode anamanga ena a mu mpingo ndi cholinga chakuti awazunze.
1 Nati ana veya’amaim Herod busuruf sabuw afa hina ekalesia ana kou’ayamaim hima’am bow fatum bai’akir kakafin maiyow itih.
2 Iye analamula kuti Yakobo mʼbale wa Yohane, aphedwe ndi lupanga.
2 Naatu John tuwah James uwih hibai kaiyomaim hiyi morob.
3 Ataona kuti zimenezi zinakondweretsa Ayuda, anawonjeza ndi kugwiranso Petro. Izi zinachitika pa nthawi ya Chikondwerero cha Buledi wopanda Yisiti.
3 Iti na’atube sinaf Jew sabuw hibiyasisir itih, basit, Faraw Wanawanan Yeast En ana hiyuw hi’aa ana mar eo Peter hibai hifatum.
4 Atamugwira Petro, namutsekera mʼndende, anamupereka kwa magulu anayi a asilikali kuti amuyangʼanire, gulu lililonse linali ndi asilikali anayi. Herode anafuna kumuzenga mlandu pamaso pa anthu onse chikondwerero cha Paska chitapita.
4 Peter hibai hifafatum ufunamaim hibai hin dibur hiyari’iy, baiyowayah etei 16 hima’uh hima.
5 Kotero Petro anasungidwa mʼndende, koma mpingo unamupempherera kolimba kwa Mulungu.
5 Imih Peter diburamaim hibotan hima, baise ekaleisia dogoroh tutufin etei God isan hiyoyoban.
6 Usiku woti mmawa mwake Herode amuzenga mlandu, Petro amagona pakati pa asilikali awiri, atamangidwa maunyolo awiri, ndiponso alonda atayima pa khomo.
6 Nati gugumin ta’imon Pilate yayakitifuw mar tatot tibatiyimih, Peter baise ma’utenayah orot rou’ab hai founamaim uman rororon chain hi’utan. Naatu au waraunane i ma’utenayah umah hi’utan naatu i matan fot in. Dibur etawan auman ma’utenayah hibat hikakaif.
7 Mwadzidzidzi mngelo wa Ambuye anaonekera ndipo kuwala kunawunika mʼchipindamo. Mngeloyo anamugwedeza Petro mʼnthiti ndi kumudzutsa. Iye anati, “Fulumira, imirira!” Ndipo maunyolo anagwa kuchoka mʼmanja a Petro.
7 Naniyan meyemeye Regah ana tounamatar run bat naatu marakaw bar wanawanan kusisiar re, tounamatar Peter tuwabun bai ibunibun eo, “Mata enuw kumisir saife.” Mar ta’imonamo Peter uman chain hiha’obow hire. Tounamatar na Peter ebibunibun|alt="Angel awaking Peter" src="cn01953B.tif" size="col" loc="Act 12.7" copy="©1978 David C. Cook Publishing Co." ref="12.7"
8 Kenaka mngelo anati kwa iye, “Vala zovala ndi nsapato.” Ndipo Petro atachita izi mngeloyo anamuwuzanso kuti, “Funda chovala chako ndipo unditsate.”
8 Imaibo tounamatar Peter iu, “A faifuw kwiyoun naatu a baibiyon kwiyoun.” Peter na’atube sinaf naatu tounamatar eo, “A faifuw tafan baibiyon naiw kufifin naatu kwi’ufnunu.”
9 Petro anatsatira natuluka mʼndende, koma sanazindikire kuti zimene mngeloyo amachita zimachitikadi; iye amaganiza kuti amaona masomphenya.
9 Peter i’ufunun hairi hitit dibur bar ufunane hire, baise Peter men kafa’imo so’ob tounamatar abisa sisinaf, i notanot i mimim rouw.
10 Iwo anadutsa gulu loyamba ndi lachiwiri la asilikali ndipo anafika pa chitseko chachitsulo cholowera mu mzinda. Chitsekocho chinatsekuka chokha ndipo anadutsa. Pamene anayenda kutalika kwa msewu umodzi, mwadzidzidzi mngelo uja anachoka.
10 Hitit ma’utenayah etawan wan hibatabat naatu etawan bairou’abin hibatabat hinatabirih. Naatu hina etawan gagamin in bar merar titit awanamaim hitit, etawan akisin botawiy hitit ef yan hire. Ef nati hibutitiy hin yomaninamaim hitit, basit tounamatar sa’iwa’an.
11 Pamenepo Petro anazindikira nati, “Tsopano ndikudziwa mosakayika kuti Ambuye anatuma mngelo wake kudzandipulumutsa mʼmanja mwa Herode, ndi ku zoyipa zonse zimene Ayuda amafuna kundichitira.”
11 Peter imaibo matan to iwa’an eo, “Turobe, iti sawar i anababatun ayu isou matar. Regah ana tounamatar iyafar Herod ana fairane naatu Jew sabuw sawar abisa hinotanot mataramih i umahine ayu iyawasu.
12 Atazindikira zimenezi anapita ku nyumba ya Mariya amayi ake a Yohane, wotchedwanso Marko, kumene kunasonkhana anthu ambiri ndipo amapemphera.
12 Peter ana not kukubunai ufunamaim na John Mark hinah Mary ana bar tit. Nati’imaim sabuw moumurih na’in hiru’ay hima hiyoyoyoban.
13 Petro anagogoda pa chitseko cha panja, ndipo mtsikana wantchito dzina lake Roda anabwera kuti adzatsekule chitseko.
13 Peter na etawan ufunane bat rukikitar, naatu bowabow babitai wabin Rhoda etawan botawiyinamih na.
14 Atazindikira mawu a Petro anakondwa kwambiri ndipo anabwerera osatsekula ndipo anafuwula kuti, “Petro ali pa khomopa!”
14 Baise Peter fanan i’inan ana maramaim yan wanawanan yasisir awan karatan etawan botawiyina’e i matabir nunuw run e’af eo, “Peter na ufun ebatabat.”
15 Anthuwo anati kwa iye, “Wopenga iwe!” Atalimbikira kunena kuti zinali zoona, iwo anati, “Ameneyo ndi mngelo wake.”
15 Sabuw hi’u, “O anot i kwaris.” Baise i ana yanibebemaim, imih hio, “Nati i Peter ayubin.”
16 Koma Petro anapitiriza kugogoda ndipo atatsekula chitseko ndi kumuona, anthuwo anadabwa kwambiri.
16 Baise Peter bat rurukikitar etawan hibotawiy, naatu hi’i’itin ana veya hifofofor men kafaita.
17 Petro anakweza dzanja ndi kuwawuza kuti akhale chete ndipo anawafotokozera mmene Ambuye anamutulutsira mʼndende. Iye anati, “Uzani Yakobo ndi abale ena za zimenezi.” Kenaka anachoka napita kumalo ena.
17 Peter umanamaim iman awah bofot naatu Regah mi’itube diburane bobotait hai tur eowen, “Iti i James ana tur kwana’owen naatu taitu auman hai tur kwana’owen.” Imaibo ihamiyih tit efan ta’amaim in.
18 Pamene kunacha kunali phokoso lalikulu pakati pa asilikali, iwo anafunsa kuti, “Kodi chamuchitikira Petro ndi chiyani?”
18 Mar auman baiyowayah wanawanahimaim kasiy gagamin na’in matar, taiyuwih hibabatiyih hio, “Peter isan mi’itube’emih iti na’atube matar?”
19 Herode atamufunafuna ndipo wosamupeza, anawafunsa asilikali ndipo analamulira kuti asilikaliwo aphedwe.
19 Herod kwararih hin hinuwih, baise men hitita’ur. Basit ma’utenayah orot nah 16 buwih ibabatiyih sawar eo hibow hin hirouw himorob.
20 Herode anakwiyira anthu a ku Turo ndi Sidoni; anthuwo anagwirizana zoti akambirane naye. Atapeza thandizo kuchokera kwa Blasito, wantchito wokhulupirika wa mfumu, anapempha kuti pakhale mtendere, chifukwa dziko lawo limadalira dziko la mfumuyo pa chakudya chawo.
20 Herod ana yaso’ar gagamin na’in Taiya naatu Sidon sabuw isah biyaso’aso’ar. Imih sabuw kou’ay hibai Herod itinamih hina. Wantoro’ot aiwob ana orot gagamin wabin Blastus yan hiyi rabon isahine bat imaibo hina Herod biyan hitit tufuw isan hifefeyan. Anayabin hai tafaram ana bay i Herod ana tafaramane nan.
21 Pa tsiku limene anasankha Herode, atavala zovala zake zaufumu, anakhala pa mpando wake ndipo anayankhula kwa anthuwo.
21 Veya hirurubin na’atube aiwob hai gub ana faifuw bai iyoun ana urama’ama’amaim mare ma sabuw isah binan.
22 Anthuwo anafuwula nati, “Amenewa ndi mawu a mulungu osati a munthu ayi.”
22 Sabuw tur hinonowar hio, “Iti men orot ebibinanumih, baise god.”
23 Nthawi yomweyo mngelo wa Mulungu anamukantha chifukwa sanapereke ulemu kwa Mulungu ndipo anadyedwa ndi mphutsi nafa.
23 Mar ta’imon Regah ana tounamatar Herod rab re morob biyan motamot hi’an morob, anayabin sabuw bora’aten hibitin men bai God itinimih.
24 Koma Mawu a Mulungu anapitirirabe kufalikirafalikira.
24 Naatu God ana tur ra’at tasasar tit sabuw etei hinowar.
25 Barnaba ndi Saulo atamaliza ntchito yawo anachoka ku Yerusalemu, atatenga Yohane wotchedwanso Marko.
25 Barnabas, Saul hairi hai bowabow hibisawar ufunamaim Jerusalemane himatabir maiye John Mark hibai bairi hin.

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Atos 12, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.