Atos 11
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Atumwi ndi abale a ku Yudeya konse anamva kuti anthu a mitundu ina analandiranso Mawu a Mulungu.
1 Tur Abarayah naatu baitumatumayah Judea wanawanan Ufun Sabuw God ana tur hibaib isan tur hinowar.
2 Tsono Petro atafika ku Yerusalemu, abale amene anali a mdulidwe anamutsutsa iye,
2 Imih Peter yena Jerusalem titit ana veya baitumatumayah hai ar afu’afuw himisir higam hio,
3 ndipo anati, “Iwe unalowa mʼnyumba ya anthu osachita mdulidwe ndi kudya nawo.”
3 “O in Ufun Sabuw hai ar mo’oh tutufih bairi kwama kwa’aa kwatomatom iti ina.”
4 Koma Petro anayamba kuwafotokozera zonse mwatsatanetsatane momwe zinachitikira kuti,
4 Naatu Peter busuruf aneika abisa mamatar i kubuna hai tur eowen eo.
5 “Ine ndimapemphera mu mzinda wa Yopa ndipo ndili ngati wokomoka ndinaona masomphenya. Ndinaona chinthu chokhala ngati chinsalu chachikulu chikutsika kuchokera kumwamba chogwiridwa msonga zake zinayi, ndipo chinatsikira pa ine.
5 “Veya ta Joppa ama ayoyoyoban ana maramaim matau hibora’ah sawar ta rar gagamin na’atube tainin kwafe’en marane hikuhamihamiy rena sisibu’umaim nutanub.
6 Ine ndinayangʼana mʼkati mwake ndipo ndinaona nyama za miyendo inayi za mʼdziko lapansi, zirombo, zokwawa, ndi mbalame zamlengalenga.
6 Ayu anunuwariy for yumatah ta ta a’itan, uma’ar, kok, uway naatu mamu aitah,
7 Kenaka ine ndinamva mawu akuti, ‘Petro, Imirira. Ipha, nudye.’
7 basit orot ta fanan anowar iuwu eo, ‘Peter kumisir sawar iti kurouw ku’aa.’
8 “Ine ndinayankha kuti, ‘Ayi, Ambuye! Pakuti chinthu chodetsedwa ndi chonyansa sindinadyepo pakamwa pangapa.’
8 Baise ayu ao, ‘Regah men karam, anayabin bay kakafih naatu gubagub auman men kafa’imo awau’umaim narunamih.’
9 “Mawu ochokera kumwamba ananenanso kachiwiri kuti, ‘Chimene Mulungu wachiyeretsa usanene kuti ndi chodetsedwa.’
9 Baise orot fanan iban maiye marane eafare eo, ‘Sawar abisa God kurereb gewasin eo, o men kakafin inarouw inao’omih.’
10 Zimenezi zinachitika katatu ndipo kenaka zonse zinatengedwa kupita kumwamba.
10 Sawar iti i mar tounu matar, basit yomaninamaim sawar tutufin etei matabir maiye in mar wanawanan run.
11 “Nthawi yomweyo anthu atatu amene anatumidwa kuchokera ku Kaisareya anayima pa nyumba yomwe ndimakhalayo.
11 Nati ana veya’amaim orot tounu Caesarea’ane ayu isou hiyafarih hina bar ama’ama imaim hitit.
12 Mzimu anandiwuza kuti ndisakayike, koma ndipite nawo. Abale asanu ndi mmodzi awa anapitanso nane ndipo tinalowa mʼnyumba ya munthuyo.
12 Anun Kakafiyin iuwu bairi kwanan men inakwahir, naatu Joppa’ane taitu nah six hituru bairi an Caesarea atit naatu orot wabin Cornelius ana bar arun.
13 Iye anatiwuza mmene anaonera mngelo atayimirira mʼnyumba mwake ndi kumuwuza kuti, ‘Tumiza anthu ku Yopa kuti akayitane Simoni wotchedwa Petro.
13 Cornelius ana bar wanawanan Tounamatar mi’itube irerereb i’itin i ai tur eowen naatu tounamatar iu, ‘Orot afa iniyunih hinan Joppa orot wabin Simon Peter biyan hinatit.
14 Iye adzakuwuza uthenga umene udzapulumutsa iwe ndi a pa banja ako.’
14 Naatu i boro ayawas ana tur nab nan nao kwananowar, naatu nati turamaim o a nibur bairi naatu taituwa afa bairi kwama’am boro yawas kwanab.’
15 “Nditangoyamba kuyankhula, Mzimu Woyera anafika pa iwo monga momwe anafikira pa ife poyamba paja.
15 “Naatu ayu abusuruf ao anan ana maramaim Anun Kakafiyin re targabuwih, anamaim it tatar gabuwit na’atube.
16 Kenaka ndinakumbukira zimene Ambuye ananena kuti, ‘Yohane anabatiza ndi madzi, koma inu mudzabatizidwa ndi Mzimu Woyera.’
16 Imaibo ayu Regah abisa eo i anot, ‘John i harewamaim bapataito it, baise kwa boro Anun Kakafiyinamaim bapataito kwanitih.’
17 Tsono ngati Mulungu anawapatsa iwo mphatso yomweyo imene anatipatsa ife, amene tinakhulupirira Ambuye Yesu Khristu, ndine yani kuti nditsutsane ndi Mulungu?”
17 Imih iti i bebeyan, God siwar ta’imon Ufun Sabuw itih, it Regah Jesu Keriso tabitumitum ana maramaim bitit na’atube. Imih ayu yait God abisa sisinaf boro ata’otan?”
18 Iwo atamva zimenezi analibenso chonena ndipo anayamika Mulungu nati, “Potero Mulungu wapatsa anthu a mitundu ina mwayi wotembenuka mtima ndi kulandira moyo.”
18 Iti tur hinonowar ana veya hai gamin sawar, God hibora’ara’ah hio, “Turobe. God Ufun Sabuw auman kakafih baihamiyen yawas bain isan hai ef botawiy itih.”
19 Tsopano amene anabalalika chifukwa cha mazunzo amene anayamba ataphedwa Stefano, anapita mpaka ku Foinike, ku Kupro ndi ku Antiokeya, ndipo ankalalikira kwa Ayuda okha.
19 Biyababan bai’akir kakafin Stephen hirab momorob ana maramaim matar, baitumatumayah tarbounih hitit nanabin hin. Afa hin Fonisia, Cyprus, naatu Antioch imaim hitit Jew akisihimo isah tur gewasin hifaram.
20 Komabe, ena pakati pawo ochokera ku Kupro ndi ku Kurene anapita ku Antiokeya ndipo iwo anayamba kuyankhulanso kwa Agriki, nawawuza za Uthenga Wabwino wa Ambuye Yesu.
20 Baise baitumatumayah afa Cyprus naatu Sairini hima’am hin Antioch hitit Ufun Sabuw auman isah hibinan tur gewasin Jesu Keriso isan hai tur hi’owen.
21 Mphamvu ya Ambuye inali nawo ndipo anthu ambiri anakhulupirira natembenukira kwa Ambuye.
21 Regah ana fair tafah mara’at hibinan sabuw moumurih na’in hitumatum Regah isan hitatabir.
22 Mbiri imeneyi inamveka ku mpingo wa ku Yerusalemu ndipo iwo anatumiza Barnaba ku Antiokeya.
22 Abisa hisisinaf ana tur in Jerusalem ekaleisia hinowar, basit Barnabas hiyafar na Antioch tit.
23 Atafika ndi kuona chisomo cha Mulungu pa iwo, anakondwa ndi kuwalimbikitsa anthu onsewo kuti apitirire kukhala woona mu mtima mwa Ambuye.
23 Natitit ana maramaim God sabuw mi’itube bigegewasinih itih, basit yan sisir naatu koufair itih eo, dogor tutufin etei kwaniturobe Regah sisibinika kwanama.
24 Barnabayo anali munthu wabwino, wodzazidwa ndi Mzimu Woyera ndi chikhulupiriro ndipo gulu lalikulu la anthu linabwera kwa Ambuye.
24 Barnabas i orot gewasin, Anun Kakafiyin biyan karatan naatu ana baitumatum fairin, imih sabuw moumurih na’in bow hina Regah biyan hitit.
25 Kenaka Barnaba anapita ku Tarisisi kukafuna Saulo,
25 Imaibo Barnabas Saul nuwihinamih in Tarsus tit.
26 ndipo pamene anamupeza anabwera naye ku Antiokeya. Barnaba ndi Saulo anasonkhana ndi mpingo kwa chaka chimodzi naphunzitsa anthu ambirimbiri. Okhulupirirawo anayamba kutchedwa Akhristu ku Antiokeya.
26 Nuwih inanan baib ana maramaim nawiy hairi hina Antioch hitit, imaim kwamur ta’imon tutufin ekaleisia nati’imaim bairi hima. Naatu sabuw bai’ufununayah boubuh kou’ay gagamin na’in hi’obaibiyih. Imih bai’ufununayah tafaram Antioch imaim wab iti Kirisiyan teo imaim matar.
27 Masiku amenewo ku Antiokeya kunafika aneneri ena ochokera ku Yerusalemu.
27 Nati ana veya’amaim dinab orot afa Jerusalemane hina Antioch hitit.
28 Mmodzi wa iwo dzina lake Agabu, anayimirira ndipo Mzimu anamutsogolera kunenera zamʼtsogolo kuti padzakhala njala yayikulu pa dziko lonse lapansi. (Izi zinachitikadi nthawi ya ulamuliro wa Klaudiyo).
28 Naatu dinab orot ta wabin Agabus Anun Kakafiyin ana fairamaim misir eo, “Baimar kakafin boro’omo tafaram wanawanan namatar.” Iti baimar i Claudius i’aiwob ma’ama ana veya’amaim matar.
29 Ophunzirawo, aliyense monga mwakupata kwake, anatsimikiza kuthandiza abale okhala ku Yudeya.
29 Bai’ufununayah hai not hibogaigiwas i hai mour ana fofonin na’atube tuwahinah Judea hima’am baibaisih isan hio,
30 Izi anazichitadi ndipo anatuma Barnaba ndi Saulo kukapereka mphatsozo kwa akulu a mpingo.
30 naatu hisinaf. Imaibo Barnabas, Saul hairi umahimaim hiyafar hibai hin ai’in Jerusalem hima’am hitih.
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Atos 11, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.