Atos 10
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Ku Kaisareya kunali munthu wina dzina lake Korneliyo, mkulu wa asilikali 100 wa gulu la Italiya.
1 Caesarea imaim orot wabin Cornelius Rome baiyowayah hai orot ukwarin baiyow ana kou’ay wabin Italian Regiment.
2 Iye ndi banja lake lonse amapembedza ndi kuopa Mulungu. Iye amathandiza osowa mowolowamanja ndipo amapemphera kwa Mulungu nthawi zonse.
2 Cornelius i God ana orot ta, i ana nibur tutufin etei God hikwakwafir, baibais gagamin maiyow yababan wairafih bitih, naatu mar etei God isan yoyoyoban. Cornelius eyoyoyoban|alt="Cornelius praying" src="cn01943B.tif" size="col" loc="Act 10.2" copy="©1978 David C. Cook Publishing Co." ref="10.2"
3 Tsiku lina, nthawi ili ngati 3 koloko masana, anaona masomphenya. Anaona bwino ndithu mngelo wa Mulungu, amene anabwera kwa iye ndi kuti, “Korneliyo.”
3 Veya ta rabirab three korok na’atube matan hibora’ah God ana tounamatar na run wabin su’ub eo, “Cornelius!”
4 Korneliyo anamuyangʼanitsitsa mngeloyo mwa mantha. Iye anafunsa kuti, “Nʼchiyani kodi Ambuye?”
4 Cornelius matan takiyat itinkikin erebirubir auman eo, “Regah abisa kukokok?”
5 Tsopano tuma anthu apite ku Yopa kuti akayitane munthu dzina lake Simoni Petro.
5 Imih boun orot afa iniyafarih hinan Joppa orot Simon, wabin ta Peter, i hinanawiy bairi hinan.
6 Iye akukhala ndi Simoni mmisiri wa zikopa, amene nyumba yake ili mʼmbali mwa nyanja.”
6 Simon bobaituw kanabihimaim sawar yumatah ta ta sakirayan i ana baremaim bairi tema’am, ana bar tor rewan ebatabat.”
7 Mngeloyo anayankhula naye anachoka, Korneliyo anayitana antchito ake awiri ndiponso msilikali mmodzi wa iwo amene ankamutumikira yemwe ankapembedza Mulungu.
7 Basit tounamatar hairi hio inan ufut, Cornelius ana bowayah orot rou’ab naatu baiyowayah orot ta’imon e’af ayuwih. Iti baiyowayan orot auman i God ana orot, Cornelius biyan ana tafafarayan orot.
8 Iye anawafotokozera zonse zimene zinachitika ndipo anawatuma kuti apite ku Yopa.
8 Sawar etei himamatar na’atube hai tur eowen, basit iyafarih hin Joppa hitit.
9 Mmawa mwake, nthawi ili ngati 12 koloko anthuwo atayandikira mzindawo, Petro anakwera pa denga kukapemphera.
9 Mar to orot efamaim hina Joppa hibiyubin auman, Peter auyit yen in bar tafan yoyoban isan.
10 Iye anamva njala ndipo anafuna chakudya, ndipo akukonza chakudyacho, iye anachita ngati wakomoka.
10 Basit bayumih morob ana kok i bay taa, bay hibogaigiwas bifotamih i matan taratan.
11 Iye anaona kuthambo kutatsekuka, ndi chinthu china chikutsitsidwa pansi chooneka ngati chinsalu chachikulu chomangidwa pa msonga zake zinayi.
11 Mar botawiy naatu sawar ta rar gagamin na’atube umasusun kwafe’en hikuhamihamiy re me yan titit itin.
12 Mʼmenemo munali nyama zonse zamiyendo inayi pamodzinso ndi zokwawa za dziko lapansi ndiponso mbalame zamlengalenga.
12 Nati wanawanan for yumatah ta ta, kok uma’ar, gabunam, naatu kutor mamu. Peter matan hibora’ah masanuw kakafih biyah gubagug auman itah|alt="Peter’s vision" src="cn01945B.tif" size="col" loc="Act 10.12" copy="©1978 David C. Cook Publishing Co." ref="10.12"
13 Petro anamva mawu akuti, “Petro, dzuka, ipha nudye.”
13 Orot fanan nowar eo, “Peter kumisir iti sawar kurouw ku’aa.”
14 Petro anayankha kuti, “Ayi, Ambuye! Ine sindinadyepo kanthu kosayeretsedwa kapena konyansa.”
14 Baise Peter iya’afut eo, “Men karam Regah, ayu men kafai sawar iti na’atube karitanih eregubagub auman aa’umih.”
15 Petro anamvanso kachiwiri mawu akuti, “Usachiyese chonyansa chimene Mulungu wachiyeretsa.”
15 Orot fanan iban bairou’abin e’af maiye, “Sawar abisa God eorereb gewasin rarouw men o a notamaim kakafin inarouw inao.”
16 Zimenezi zinachitika katatu ndipo nthawi yomweyo chinsalu chija chinatengedwanso kupita kumwamba.
16 Sawar iti na’atube mar tounu matar, imaibo naniyan meyemeye sawar matabir maiye yen mar run.
17 Petro akuganizira za tanthauzo la masomphenyawo, anthu amene Korneliyo anawatuma anapeza kumene kunali nyumba ya Simoni ndipo anayima pa chipata.
17 Peter matan hibora’ah sawar iti i’itin anayabin so’ob isan kasiy ma binotanot, orot Cornelius iyafarih hinan bar hitita’ur hina fur awan hibat.
18 Iwo anayitana nafunsa ngati Simoni amene amadziwika ndi dzina loti Petro amakhala kumeneko.
18 Hi’afariy hibatiyih hio, “Orot wabin Simon Peter iti a baremaim ema’am?”
19 Petro akuganizirabe za masomphenyawo, Mzimu Woyera anati kwa iye, “Simoni, anthu atatu akukufunafuna.
19 Peter matan hibobora’ah isan boro’ika ma binotanot, Anun Kakafiyin iu eo, “Simon, orot nah tounu o tenunuwihi.
20 Dzuka, tsika. Usakayike upite nawo pakuti ndawatuma ndine.”
20 Imih kumisir kura’iy bar baban, men a inakutan baise bairi kwanan, anayabin ayu aiyafarih hina.”
21 Petro anatsika ndipo anati kwa anthuwo, “Amene mukufunayo ndine. Mwabwera kuno chifukwa chiyani?”
21 Peter misir ra’iy naatu iuwih eo, “Ayu orotoban iti kwa ayu kwanunuwuhu, kwa a’an aisim kwana?”
22 Anthuwo anayankha kuti, “Ife tachokera kwa Korneliyo, mkulu woyangʼanira asilikali 100. Iye ndi munthu wolungama ndiponso woopa Mulungu, amene amalemekezedwa ndi Ayuda onse. Mngelo woyera anamuwuza kuti mupite ku nyumba yake kuti akamve mawu amene inu mukanene.”
22 Hiya’afut hio, “Aki i baiyowayan orot ukwarin wabin Cornelius iyafari ana. Iti orot ana yawas i gewasin, naatu God ebibiruw, Jew sabuw etei iti orot i tekakakafiy. Tounamatar kakafiyin iu, o tifefeyani itan ana bar, saise o abisa itao’o i tanowar isan.”
23 Pamenepo Petro anawalowetsa mʼnyumba ndipo anawasamala ngati alendo ake. Mmawa mwake Petro ananyamuka napita nawo ndipo abale ena a ku Yopa anapita naye pamodzi.
23 Basit Peter nah tounu buwih bar hirun bairi fai ta’imon hi’in.
24 Tsiku linalo Petro anafika ku Kaisareya. Korneliyo anawadikirira ndipo anali atawasonkhanitsa pamodzi abale ake ndi abwenzi ake a pamtima.
24 Veya baitonin hina Caesarea hitit. Cornelius i ma matan ef i’itin, taintuwan afa e’af ayuwih hina ana baremaim bairi hima Peter hikakaif.
25 Petro akulowa mʼnyumba, Korneliyo anakumana naye ndipo anadzigwetsa pa mapazi ake namulambira.
25 Peter na bar rur ana maramaim, Cornelius nanamaim sun yowen kwafir re.
26 Koma Petro anamuyimiritsa nati, “Imirira, inenso ndine munthu ngati iwe.”
26 Baise Peter imisiruw eo, “Kumisir ayu i orot o na’atube.”
27 Akuyankhula naye, Petro analowa mʼnyumba ndipo anapeza gulu lalikulu la anthu litasonkhana.
27 Peter tur busuruf auman Cornelius hairi hirun hin bar wanawanan hitit naatu sabuw kou’ay gagamin na’in hima’am kouh yen.
28 Iye anawawuza kuti, “Inu mukudziwa bwino kuti ndi kutsutsana ndi lamulo ngati Myuda ayanjana ndi Mkunja kapena kuyendera wina aliyense wa mtundu wina. Koma Mulungu wandionetsa ine kuti ndisatchule munthu aliyense kuti ndi wosayenera kapena wonyansa.
28 Iuwih eo, “Kwa etei kwaso’ob Jew hai ofafar men ebibasit boro Ufun Sabuw atinanawani bairi tatitayo’ay. Baise God i’obaiyu aitin ayu men orot ta biyan karitanin o gubagub anarouw anao.
29 Nʼchifukwa chake ndabwera mosawiringula pamene munandiyitana. Tsopano ndikufunseni,” Mwandiyitanira chiyani?
29 Imih ayu isou tur kwabiyafar, ayu men erekwahir auman anamih. Ayu kwa abibatiy, aisim ayu isou tur kwaiyafar ana?”
30 Komeliyo anayankha kuti, “Masiku anayi apitawo, nthawi yonga yomwe ino, 3 koloko masana ndimapemphera mʼnyumba mwanga. Mwadzidzidzi patsogolo panga panayimirira munthu wovala zovala zonyezimira.
30 Cornelius iya’afut eo, “Veya kwafe’en na’atube sawaraka, veya three korok na’atube rabirab au baremaim ayoyoyoban, naniyan meyemeye orot ana faifuw kwes nau’umaim bat eo,
31 Ndipo anati, ‘Korneliyo, Mulungu wamva mapemphero ako ndipo wakumbukira mphatso zako kwa osauka.
31 ‘Cornelius, ayoyoban God nowar naatu a siwar sabuw yababan wairafih ibitih imaim ana not kusib.
32 Tuma anthu ku Yopa akayitane Simoni wotchedwa Petro. Iye akukhala mʼnyumba ya Simoni mmisiri wazikopa amene amakhala mʼmbali mwa nyanja.’
32 ‘Orot ta kwiyafar en Joppa imaim orot wabin Simon wabin ta Peter i Simon bobaituw kanabihimaim sawar ta ta sakirayan ana bar tor rewanamaim ema’am biyan etit.’
33 Nʼchifukwa chake ndinatumiza anthu nthawi yomweyo ndipo mwachita bwino kuti mwabwera. Tsopano ife tonse tili pano pamaso pa Mulungu kuti timve zonse zimene Ambuye akukulamulani kuti mutiwuze ife.”
33 Imih o isa tur saisewat aiyafar, naatu gewasin maiyow o ina itit, naatu aki etei God nanamaim Regah sawar etei eo biyuni nowaramih ama akakaif.”
34 Ndipo Petro anayamba kuyankhula nati, “Zoonadi, tsopano ndazindikira kuti Mulungu sakondera.
34 Imaibo Peter busuruf binan eo, “Ayu bounabo aso’ob, God men orot babin ta’imon itin yan ebaibimih.
35 Koma amalandira anthu a mtundu uli wonse amene amaopa Iye ndiponso kuchita chilungamo.
35 Baise orot menan ta ta iyab i tibibiruw naatu abisa gewasin tisisinaf.
36 Uwu ndi uthenga umene Mulungu anatumiza kwa Aisraeli, kulalikira Uthenga Wabwino wamtendere mwa Yesu Khristu amene ndi Ambuye wa onse.
36 Tur God iyafar na Israel biyah titit i etei kwaso’ob, iti tur gewasin i tufuw Jesu Keriso wanawanamaim ema’am. It etei ata Regah.
37 Inu mukudziwa zimene zinachitika ku Yudeya konse, kuyambira ku Galileya pambuyo pa ubatizo umene Yohane analalikira,
37 Naatu kwaso’ob sawar abisa Judea wanawanan mamatar, John bapataito isan bibinan ufunamaim iti sawar i Galilee imaim busuruf.
38 kuti Mulungu, anamudzoza Yesu, wa ku Nazareti ndi Mzimu Woyera ndi mphamvu ndiponso mmene Iye anapita nachita zabwino ndi kuchiritsa onse amene anali pansi pa mphamvu ya mdierekezi, popeza kuti Mulungu anali naye.
38 Mi’itube Anun Kakafiyinamaim God Jesu Nazareth matuwan tafan eof nowah naatu fair tafan bisuwai i kwaso’ob. Naatu ana bowabow mi’itube run tit bow yawas gewasin sinaf, sabuw iyab afiy hai fairamaim hima’am etei biyawasih auman i kwaso’ob, anayabin God i hairi hima’am.
39 “Ife ndife mboni za zonse zimene anachita mʼdziko la Ayuda ndiponso ku Yerusalemu. Anamupha Iye pakumupachika pa mtengo,
39 Sawar abisa Jew hai me yan naatu Jerusalemamaim sisinaf etei i aki a’itah sif arurubon. Naatu onaf afe’enamaim hikubar momorob auman i aki aso’ob.
40 koma Mulungu anamuukitsa kwa akufa pa tsiku lachitatu, ndipo analola kuti aonekere poyera.
40 Baise veya tounu ufunamaim God morobone bora’ah maiye naatu iwa’an tit irerereb sabuw hi’itin.
41 Iye sanaonekere kwa anthu onse koma kwa mboni zimene Mulungu anazisankhiratu, kwa ife amene timadya ndi kumwa naye atauka kwa akufa.
41 Men sabuw etei hi’itin, baise sabuw iyab God rurubinihiwat, nati i aki iyab morobone mimisir maiye ufunamaim bairi a’aa atomatomawat.
42 Iye anatilamulira ife kuti tilalikire kwa anthu ndi kuchitira umboni kuti Iye ndiye amene Mulungu anamusankha kukhala woweruza wa amoyo ndi akufa.
42 Naatu eobaiyuni tur gewasin sabuw etei isah ana binan hai tur ana’owen Jesu i God Rubin sabuw yawayawasih naatu murumurubih baibabatiyih isan.
43 Aneneri onse achitira Iye umboni kuti aliyense amene akhulupirira Iye amakhululukidwa machimo chifukwa cha dzina lake.”
43 Dinab orot etei isan hibinan hio sabuw iyab i wabinamaim hinabitumatum boro hai bowabow kakafih nanotawiyen.”
44 Petro akuyankhulabe mawu amenewa, Mzimu Woyera unatsikira pa onse amene amamva uthengawo.
44 Peter iti na’atube bat eo inan wanawanan Anun Kakafiyin ra’iy sabuw iyab hima tur hinonowar tar gabuwih.
45 Abale a mdulidwe omwe anabwera ndi Petro anadabwa kuona kuti mphatso ya Mzimu Woyera yapatsidwanso kwa anthu a mitundu ina.
45 Jew baitumatumayah afa Peter bairi Joppa’ane hinan hifofofor men kafaita. God ana usar Anun Kakafiyin Ufun Sabuw auman tafahimaim isuwai re’ere isan.
46 Pakuti anamva iwo akuyankhula mʼmalilime ndi kuyamika Mulungu. Ndipo Petro anati,
46 Naatu sabuw menah botabir tur ta ta hio God hibora’ara’ah.
47 “Kodi alipo amene angawaletse anthu awa kubatizidwa mʼmadzi? Iwotu alandira Mzimu Woyera monga ifenso.”
47 “Iti sabuw boro yait harewamaim bapataito bain isan na’otanih? Anayabin Anun Kakafiyin it tabaib na’atube i auman hibaika.
48 Tsono iye analamula kuti abatizidwe mʼdzina la Yesu Khristu. Ndipo anthu aja anamupempha Petro kuti akhale nawo masiku angapo.
48 Basit iuwih Jesu Keriso wabinamaim bapataito hibai, naatu Peter veya bai’ab na’atube bairi ma isan hifefeyan nati’imaim bairi hima.
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Atos 10, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.