Apocalipse 9
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Mngelo wachisanu anayimba lipenga lake, ndipo ndinaona nyenyezi ikugwa pa dziko lapansi kuchokera ku thambo. Nyenyeziyo inapatsidwa kiyi ya ku chidzenje chakuya.
1 Tounamatar bai five ana tour bababin ana veya, ayu anuwanuw maramaim daman hea’obow me yan rara’iy aitin. Naatu daman Sou Awan Wanu’umin botawiyin isan ana tufatan hitin.
2 Nyenyeziyo itatsekula pa chidzenje chakuyacho panatuluka utsi ngati wochokera mʼngʼanjo yayikulu. Dzuwa ndi thambo zinada chifukwa cha utsi ochokera mʼdzenjemo.
2 Naatu daman Sou Awan Wanu’umin ana tufatan uyi’uy ana maramaim sow agor kutikutin tit, ana’itin i ra’iy e’arah ana sow eyeyey na’atube. Sou Awan Wanu’umin ana sow yen veya matan naatu gagub etei gugum nuwayowanin en.
3 Ndipo mʼkati mwa utsimo munatuluka dzombe kukalowa mʼdziko lapansi ndipo linapatsidwa mphamvu zoluma ngati za zinkhanira pa dziko lapansi.
3 Sow yey wanawananamaim ir afu’afuw hirob hire hina me yan hitit, naatu kafukafus ana fair na’atube ir afu’afuw hitih.
4 Dzombelo linalamulidwa kuti lisawononge udzu wa pa dziko lapansi, kapena chomera chilichonse, kapena mtengo uliwonse, koma anthu okhawo amene analibe chizindikiro cha Mulungu pa mphumi zawo.
4 Naatu hi’uwih, “Men yen ana fotan o ana ai rourih men ta kwani’afiy, baise sabuw iyab God ana kwah nakwetahimaim men tema’am akisih kwani’afiyih.
5 Silinapatsidwe mphamvu yowapha koma yowazunza kwa miyezi isanu. Ndipo ululu umene anthuwo anawumva unali ngati wa chinkhanira chikaluma munthu.
5 Naatu hi’uwih men sabuw kwanayubih hinamorob, baise kwanayubih weweh nakwan sumar five nasawar, kafukafus eyubih weweh ekwanikwan na’atube.”
6 Masiku amenewo anthu adzafunafuna imfa koma sadzayipeza. Adzalakalaka kufa koma imfa izidzawathawa.
6 Nati sumar five wanawanan weweh nakwanikwan ana maramaim sabuw boro morob ana ef hinanuwet, baise morob boro men hinatita’ur hai kok i boro mi’itube hitamorob, baise morob boro nabihir nawa’ir.
7 Dzombe linkaoneka ngati akavalo okonzekera nkhondo. Pamitu pawo panali ngati zipewa zaufumu zagolide ndipo nkhope zawo ngati za anthu.
7 Ir afu’afuw biyah ana itinin i horse na’atube, yumatah ana itinin orot babin hai yumatabe, ukwarihimaim i sawar ta ana itinin kowas gold na’atube hiyara’aten auman baiyow isan hibobuna hitit.
8 Tsitsi lawo linali ngati la amayi, mano awo ngati a mikango.
8 Aribuh i baibin aribuhibe naatu wah i lion wahibe.
9 Dzombelo linavala za pachifuwa zachitsulo. Phokoso la mapiko awo linali ngati phokoso la magaleta ankhondo ambiri okokedwa ndi akavalo othamangira ku nkhondo.
9 Dogoroh hai ber isan i sawar ta iron na’atube hi’afuw dogoroh hiyafafar, naatu bebeh ana nidun i horse moumurih baiyow isan tikik’ayowen tinunuw ana nidun na’atube.
10 Linali ndi michira ngati zinkhanira ndi mbola. Mʼmichira yake munali mphamvu yozunza nayo anthu kwa miyezi isanu.
10 Urahine i yuh auman, naatu hinayubi wewe ekwanikwan ana naniyan i kafukafus eyub wewe ekwanikwan na’atube. Sumar five sabuw yubih biyababan baitih isan yuhine hai fair hibai.
11 Mfumu yawo inali mngelo wolamulira Chidzenje chakuya chija. Mʼchihebri dzina lake ndi Abadoni ndipo mʼChigriki ndi Apoliyoni (tanthauzo lake ndiye kuti, Wowononga).
11 Sou Awan Wanu’umin ana tounamatar i hai aiwob na’atube ma kaifih, tounamatar wabin Abaddon Hebrew fanahimaim, Greek fanahimaim i Apolion.
12 Tsoka loyamba lapita; matsoka ena awiri akubwerabe.
12 Biyababan aga’ag wantoro’ot i na sawar, naatu biyababan aga’ag rou’ab i boro tenan.
13 Mngelo wachisanu ndi chimodzi anayimba lipenga lake, ndipo ndinamva liwu lochokera ku ngodya zinayi za guwa lansembe lagolide lija lokhala pamaso pa Mulungu.
13 Tounamatar bai six ana tour bababin ana veya, God nanamaim gem gold ana tainih kwafe’en fanah ine titit anowar,
14 Liwulo linati kwa mngelo wachisanu ndi chimodzi amene anali ndi lipenga uja, “Masula angelo anayi amene anamangidwa pa mtsinje waukulu wa Yufurate.”
14 fanan ta i tounamatar bai six isan eo, “Euphrates harew gagaminamaim tounamatar kwafe’en hifatum tebatabat kurufamih!”
15 Ndipo anamasulidwadi angelo anayi aja amene anasungidwa kukonzekera ora ili, tsiku ili, mwezi uwu ndi chaka ichi kuti aphe limodzi la magawo atatu a anthu.
15 Naatu tounamatar kwafe’en hirurufimih ana veya, nati veya ta’imon, nati sumar naatu nati kwamuramaim tafaram auwaraunane sabuw etei rouw morob isan hibobunabuna.
16 Ndinamva chiwerengero cha ankhondo a pa akavalo aja, kuti chinali 200 miliyoni.
16 Orot baiyow isan himowaraboun tit hio anonowar etei i two hundred million na’atube.
17 Akavalo ndi okwerapo amene ndinaona mʼmasomphenya anga ankaoneka motere: Zovala za pachifukwa pawo zinali zofiira ngati moto, zobiriwira ngati utsi, ndi zachikasu ngati miyala ya sulufule. Mitu ya akavalowo inali ngati ya mikango ndipo mʼkamwa mwawo munkatuluka moto, utsi ndi sulufule.
17 Naatu au mimumaim horse moumurih tafahimaim orot boyeyah auman hima’am, hai itinin i iti na’atube, dogoroh hai ber ana woun i wairaf na’atube, ana furumin i saphire na’atube, naatu ana wairin i sulfur na’atube, naatu horse ukwarih hai itinin lion na’atube, naatu awahimaim wairaf, sow agor kutikutin naatu sulfur hititit.
18 Gawo limodzi la magawo atatu a anthu linaphedwa ndi miliri yamoto, utsi ndi sulufule zimene zinkachoka mʼkamwa mwawo.
18 Orot babin auwaraunane horse awahine sawow kakafih tounu, wairaf, sow naatu sulfur hititit imaim etei himorob.
19 Mphamvu za akavalowo inali mʼkamwa mwawo ndi mʼmichira mwawo; pakuti michira yawo inali ngati njoka; ndi mitu imene inkalumira.
19 Anayabin horse hai fair i awahimaim ma’am naatu yuhine auman ma’am, yuh hai itinin i kokobe ukwarih auman, nati’imaim sabuw tiyubih biyababan tibitih.
20 Anthu ena onse amene sanaphedwe ndi miliri imeneyi sanalapebe kuti asiye ntchito zawo zoyipa. Iwo sanasiye kupembedza ziwanda ndi mafano agolide, asiliva, amkuwa, amwala ndi amtengo, mafano amene sangathe kuona, kumva kapena kuyankhula.
20 Sabuw turih sawow kakafin men hibai himomorob i men dogor baikitabir hibai abisa umahimaim hisinaf himamatar hihamiyenamih. demon hikwakwafirih, gold murubih, silver, bronze, agim, ai aurih matah en, tainih en remor en, aibat hitar hima hikwakwafirih men hihamiyen.
21 Sanalapenso kuleka zakupha, zamatsenga awo, zachigololo zawo kapena umbava wawo.
21 Na’atube sabuw hi’asbunubunuw, hisew hikwerakwer, hibiwa’an kwanekwan, naatu hibabain men hihamiyen dogor baikitabiren hibaimih.
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Apocalipse 9, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.