Apocalipse 8
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Atatsekula chomatira chachisanu ndi chiwiri, kumwamba kunakhala chete mphindi makumi atatu.
1 Fef firorow bai seven hikwah inu’in Lamb bai kwibikwib ana veya maramaim etei hinutanub mar kafai, hour turinawat, agugum hima.
2 Ndipo ndinaona angelo asanu ndi awiri aja amene amayimirira pamaso pa Mulungu, akupatsidwa malipenga asanu ndi awiri.
2 Naatu tounamatar etei seven tour seven hitih hibotanen God nanamaim hibatabat aitih.
3 Mngelo wina amene anali ndi chofukizira chagolide anabwera nayimirira pa guwa lansembe. Anapatsidwa lubani wambiri kuti amupereke pamodzi ndi mapemphero a anthu onse oyera mtima pa guwa lansembe lagolide patsogolo pa mpando waufumu.
3 Tounamatar ta umanamaim fi’ufiu ana kerowas gold bai auman na sibor ya’aya ana gemamaim batabat aitin. Naatu fi’ufiu gagamin na’in hitar hiwan God ana sabuw kakafiyih hai yoyoban auman bai gem gold nanamaim bat eot ra’ah.
4 Fungo la lubani pamodzi ndi mapemphero a oyera mtima zinakwera kumwamba kwa Mulungu kuchokera mʼdzanja la mngeloyo.
4 Fi’ufiu ana sow naatu sabuw kakafiyih hai yoyoban tounamatar umanane yen God nanamaim tit.
5 Kenaka mngeloyo anatenga chofukizira nachidzaza ndi moto wochokera pa guwa lansembe ndi kuponya pa dziko lapansi ndipo nthawi yomweyo panachitika mabingu, phokoso, mphenzi ndi chivomerezi.
5 Imaibo tounamatar fi’ufiu ana kerowas bai sibor ana gem tafanamaim wairaf bai kerowas wanawanan iwan rouw me yan re’ere ana veya namanamar bokiyat gunum rouware gugugug iwa’an naatu iriyoy tit.
6 Angelo asanu ndi awiri anakonzekera kuyimba malipenga asanu ndi awiri.
6 Tounamatar etei seven umahimaim tour hibobotanen babinen isan awahimaim hiya.
7 Mngelo woyamba anayimba lipenga lake ndipo kunabwera matalala ndi moto wosakanizana ndi magazi ndipo unaponyedwa pa dziko lapansi. Gawo limodzi la magawo atatu a dziko lapansi linapsa, gawo limodzi la magawo atatu a mitengo linapsa ndi gawo limodzi la magawo atatu a udzu wauwisi linapsanso.
7 Naatu tounamatar wantoro’ot batabat ana tour bababin ana veya, toun kabay totomar wairaf rara auman sartabir yar re me yan tit, tafaram auwaraun tutufin etei earah, ai nati tafaram auwaraunane hibatabat etei hi’arat, naatu fotan nati tafaram auwaraunane hituw hi’inu’in etei hi’arat.
8 Mngelo wachiwiri anayimba lipenga lake, ndipo chinthu china chooneka ngati phiri lalikulu loyaka moto, chinaponyedwa mʼnyanja. Gawo limodzi la magawo atatu a nyanja linasanduka magazi.
8 Tounamatar bairou’abin ana tour bababin ana veya sawar ta gagamin na’in oyaw tomar fudir tafan wairaf to’ab auman nunuw in riy yan re, riy auwaraunane tutufin etei rara matar.
9 Gawo limodzi mwa magawo atatu a zolengedwa zonse zamoyo za mʼnyanja, linafa, ndipo gawo limodzi la sitima za pamadzi linawonongedwa.
9 Riy auwaraunane wanawanan sawar yawasih ma’anih etei himorob, naatu wa nati riy auwaraunane hibatabat etei hitaseseb.
10 Mngelo wachitatu anayimba lipenga lake, ndipo nyenyezi yayikulu, yoyaka ngati muni inachoka kumwamba nigwera pa gawo limodzi la magawo atatu a mitsinje ndi pa akasupe amadzi.
10 Tounamatar baitounin ana tour bababin ana veya daman gagamin na’in matan hinowabe in toto’ab maramaim hea’obow tafaram auwaraun ana harew naatu ana harew sosoh yan ra’iy.
11 Dzina la nyenyeziyo ndi Chowawa. Gawo limodzi la magawo atatu a madzi anasanduka owawa ndipo anthu ambiri anafa chifukwa cha madzi owawawo.
11 Nati daman wabin i Tubatub, naatu Tubatub tafaram auwaraunane ana harew yah re’er harew etei tenakuyakuy himatar naatu sabuw iyab nati harew tenakuyakuy hitomatom etei himorob.
12 Mngelo wachinayi anayimba lipenga lake, ndipo chimodzi cha zigawo zitatu za dzuwa, za mwezi ndi za nyenyezi zinamenyedwa kotero chimodzi mwa zitatu za zonsezi zinada. Panalibenso kuwala pa chimodzi mwa zigawo zitatu za usana, ndi chimodzimodzinso usiku.
12 Tounamatar baikwafi’inin ana tour bababin ana veya, veya matan auwaraunane, sumar matan auwaraunane, daman matah auwaraunane etei himabiy. Imih sawar iti etei rebah auwaraunane higugum hin. Naatu auyit auwaraunane men marakaw, na’atube gugumin auwaraunane auman.
13 Ndinayangʼananso ndipo ndinaona ndi kumva chiwombankhanga chimene chinkawuluka mlengalenga kwambiri chikuyankhula mofuwula kuti, “Tsoka, Tsoka! Tsoka lalikulu kwa anthu okhala mʼdziko lapansi, angelo otsala aja akangoyimba malipenga awo!”
13 Imaibo ayu anuwanuw mamu ikou mar ana yan foun rererey fanan anowar, “Ago, ago, ago! Kwa sabuw iyab tafaramamaim kwama’am tounamatar tounu hai tour hinabababin ana veya biyababan boro kakafin maiyow kwanab!”
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Apocalipse 8, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.