Apocalipse 6
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Ndinaona pamene Mwana Wankhosa anatsekula chomatira choyamba cha zomatira zisanu ndi ziwiri zija. Ndipo ndinamva chimodzi mwa zamoyo zinayi zija chikunena liwu lomveka ngati bingu kuti, “Bwera!”
1 Imaibo buk etei seven hikwahen hi’inu’in Lamb ta bai bobotawiy aitin, naatu sawar yawasih ma’anih kwafe’en, ta fanan gunum na’atube e’af, “Kuna!”
2 Nditayangʼana patsogolo pake ndinaona kavalo woyera! Wokwerapo wake anali ndi uta ndipo anapatsidwa chipewa chaufumu, ndipo anatuluka kupita kukagonjetsa anthu ena.
2 Ayu anuwanuw horse biyan kwes, tafanamaim orot uman few auman ma’am aitin. Naatu nati orot ukwarinamaim i kowas gold hiyara’ah sabuw rouw baigegsairihimih tit.
3 Mwana Wankhosa atatsekula chomatira chachiwiri, ndinamva chamoyo chachiwiri chija chikuti, “Bwera!”
3 Buk bairou’abin hikwah inu’in Lamb bai kwibikwib ana veya, ayu sawar yawasih ma’anih bairou’abin e’afa’af fanan anowar eo, “Kuna!”
4 Pamenepo kavalo wina wofiira anatulukira. Wokwerapo wake anapatsidwa mphamvu yochotsa mtendere pa dziko lapansi ndi kuchititsa anthu kuti aziphana wina ndi mnzake. Iyeyu anapatsidwa lupanga lalikulu.
4 Naatu horse tabo biyan woun anababatun tafanamaim orot baibiyow kaiy hitin auman titit aitin. Nati orot i tafaram wanawanan tufuw bosairin wouyinin isan ana baibasit hitin, saise sabuw hitiyaso’aso’ar taiyuwih hitayuwih hitatarih hitimumurub isan.
5 Mwana Wankhosa atatsekula chomatira chachitatu, ndinamva chamoyo chachitatu chikuti, “Bwera!” Nditayangʼana patsogolo panga ndinaona kavalo wakuda! Wokwerapo wake anali ndi masikelo awiri mʼmanja mwake.
5 Buk baitounin hikwah inu’in Lamb bai kwibikwib ana veya, ayu sawar yawasih ma’anih baitounin fanan anowar eo, “Kuna!” Ayu anuwanuw horse biyan fufum tafanamaim orot uman siker rou’ab hitin bobotanen aitin.
6 Ndinamva ngati liwu kuchokera pakati pa zamoyo zinayi zija likuti, “Kilogalamu imodzi ya tirigu mtengo ndi malipiro a tsiku limodzi ndipo makilogalamu atatu a barele mtengo wake ndi malipiro a tsiku limodzi koma usawononge mafuta ndi vinyo!”
6 Naatu ayu nidun ta anonowar ana nowarin i sawar yawasih wanawanahimaim ta fananabe anowar eo, “Rafiy sum kikimin ana baiyan i veya ta’imon baiyan ana fofonin, naatu rafiy sum gidigidih tounu hai baiyan i veya ta’imon baiyan ana fofonin. Baise raiy naatu wine men kwani’afiyen!”
7 Mwana Wankhosa atatsekula chomatira chachinayi, ndinamva chamoyo chachinayi chija chikunena kuti, “Bwera!”
7 Buk baikwafi’inin hikwah inu’in Lamb bai kwibikwib ana veya, ayu sawar yawasih ma’anih baikwafi’inin fanan anowar eo, “Kuna!”
8 Nditayangʼana patsogolo panga ndinaona kavalo wotuwa! Wokwerapo wake dzina lake linali Imfa ndipo Hade inali kumutsatira pambuyo pake. Anapatsidwa ulamuliro pa gawo limodzi la magawo anayi a dziko lapansi kuti aphe ndi lupanga, njala, mliri, ndi zirombo zakuthengo za mʼdziko lapansi.
8 Ayu anuwanuw horse biyan wair tafanamaim orot wabin Morob ma’am aitin, naatu orot ta wabin Morobana’efan ufunika i’ufunun hairi hinanan aitin. Iti orot rou’ab i tafaram wanawanan auwaraunane turin ana fofonin sabuw kaiyomaim tar morob isan, baimar botaitin isan, sawow yumatah ta ta, sigarafor yubih morob isan ana fair hitih.
9 Mwana Wankhosa atatsekula chomatira chachisanu, ndinaona kunsi kwa guwa lansembe kunali mizimu ya anthu amene anaphedwa chifukwa cha Mawu a Mulungu ndi chifukwa chochitira umboni.
9 Buk bai five hikwah inu’in Lamb kwibikwib ana veya, sabuw iyab God ana tur hibibinan isan, naatu hikukurereb isan hirouw himomorob, ayubih sibor ana gem babanamaim hima’am aitih.
10 Iwo anafuwula kuti, “Mudzawaleka mpaka liti, Inu Ambuye wamkulu, woyera ndi woona, osawaweruza anthu okhala mʼdziko lapansi ndi kulipsira magazi athu?”
10 Naatu iti sabuw fanah aumetawat hirerey hio, “Regah fair maiyow kakafiyi naatu turobe anababatun! Regah mar boro biy tafaram ana sabuw iyab aki hi’asbuni amomorob isan inibatiyih, aisa inabow baimakiy initih?”
11 Pamenepo aliyense wa anthuwo anapatsidwa mwinjiro woyera ndipo anawuzidwa kuti adikire pangʼono kufikira chiwerengero cha anzawo ndi abale awo amene anayeneranso kuphedwa ngati iwo, chitakwanira.
11 Etei’imak faifuw kwes ta’ita’imon hifaramih hi’osen naatu hi’uwih, mar kafai kwanakaif, kwa hi’asbuni kwamomorob na’atube akir wairafih, taituwa, hinarouw hinamorob nan ana fofonin nab.
12 Ndinayangʼanitsitsa pamene ankatsekula chomatira chachisanu ndi chimodzi. Ndipo panachitika chivomerezi champhamvu. Dzuwa linada ngati chiguduli chopanga ndi bweya wambuzi wakuda. Mwezi wonse unafiira ngati magazi,
12 Buk bai six hikwah inu’in Lamb bai kwibikwib ana veya, iriyoy gagamin na’in tit, veya matan fufum matar, watur tibifufum na’atube, sumar matan tutufin etei iwuwun rara matar,
13 ndipo nyenyezi zakuthambo zinagwa pa dziko lapansi ngati muja zimagwera nkhuyu zotsalira mu mtengo mphepo yamphamvu ikawomba.
13 maramaim daman hihururuwih me yan hire, fafou ro’oh ahiy wowog ebabin tibihururuwih na’atube.
14 Thambo linachoka ngati amayalulira mphasa ndipo phiri lililonse ndi chilumba chilichonse zinachotsedwa pa malo pake.
14 Fef tafifirorow na’atube mar taiyuwin firorow menika in, oyaw etei naatu nuw etei hai efanamaim sa’asa’abin hin.
15 Kenaka, mafumu a pa dziko lapansi, ana a mafumu, atsogoleri a ankhondo, olemera, amphamvu, kapolo aliyense, ndi mfulu aliyense anakabisala kumapanga ndi pakati pa matanthwe a ku mapiri.
15 Imaibo tafaram ana aiwob, orot wabih gagamih, baiyow hai ukwarih, sabuw sawar wairafih, sabuw fairih, akirwairafih, sabuw iyab men akir wairafih, etei hinunuw oyaw an watu wanawanah hirun, naatu kabay wa’aroh hirun hiwa’ir.
16 Iwo anafuwulira mapiri ndi matanthwe kuti, “Tigwereni ndi kutivundikira kuti asatione wokhala pa mpando waufumuyo ndi kupulumuka ku mkwiyo wa Mwana Wankhosa!
16 Imaibo hi’af ra’at oyaw naatu kabay toto hi’uwih re tounihimih hio, “Men akokok orot urama’ama afe’en ema’am matanamaim anama naatu Lamb ana yaso’ar wanawanan anarun.
17 Pakuti tsiku lalikulu la mkwiyo wawo lafika ndipo ndi ndani angathe kulimbapo?”
17 Anayabin hai yaso’ar gagamin ana veya i natitaka, naatu yait boro iti yaso’ar nanafut?”
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Apocalipse 6, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.