Apocalipse 5

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI

Sair da comparação
AAI TUR GEWASIN O BAIBASIT BOUBUN
1 Kenaka ndinaona buku mʼdzanja la wokhala pa mpando waufumu uja. Bukulo linali lolembedwa mbali zonse ndipo linali lomatidwa ndi zomatira zisanu ndi ziwiri.
1 Imaibo orot urama’ama afe’en ma’am uman ana asukwafune Fef firorow roun roun hikirum, naatu mar etei seven hibikwah bobotanen aitin. Buk hifirorow naatu etei 7 hikwah|alt="Birny Boyd's scroll with seven seals" src="scroll-BB.tif" size="col" loc="Rev 5.1" ref="5.1"
2 Ndipo ndinaona mngelo wamphamvu akulengeza ndi mawu okweza kuti, “Ndani ali woyenera kumatula zomatira ndi kufutukula bukuli?”
2 Naatu tounamatar fairin aitin fanan aumetawat eorereb eo, “Orot yait gewasin boro iti fef firorow hikwah inu’in natafufur nabotawiy?”
3 Koma panalibe ndi mmodzi yemwe kumwamba kapena pa dziko lapansi kapena kunsi kwa dziko lapansi woti afutukule bukulo kapena kuona zamʼkati mwake.
3 Baise men yait ta maramaim, tafaramamaim, o me baban boro iti fef firorow nabotawiy naatu wanawanan nanuwariy.
4 Ndinalira kwambiri chifukwa panalibe amene anapezeka woyenera kufutukula bukuli kapena kuona zamʼkati mwake.
4 Ayu arerey men kikimin ta, anayabin men yait ta gewasin ma’am atita’ur boro iti fef firorow tabotawiy wanawanan tananuwariy.
5 Tsono mmodzi mwa akuluakulu aja anati kwa ine, “Usalire! Taona, Mkango wa fuko la Yuda, Muzu wa Davide, wapambana. Iye angathe kufutukula bukuli ndi kumatula zomatira zisanu ndi ziwirizo.”
5 Imaibo regaregah ai’in ta iuwu eo, “Ei! men inarerey! Lion Judah ana bigane David uwan orot iti sawar isnowahika. I karam boro iti fef firorow mar seven hikwahen ti’inu’in boro natafoforen nabotawiyen.”
6 Kenaka ndinaona Mwana Wankhosa akuoneka ngati wophedwa atayimirira pakatikati pa mpando waufumu uja ndi zamoyo zinayi zija ndi akuluakulu aja. Mwana Wankhosayo anali ndi nyanga zisanu ndi ziwiri ndi maso asanu ndi awiri omwe ndi Mizimu isanu ndi iwiri ya Mulungu yomwe anayitumiza ku dziko lonse lapansi.
6 Imaibo ayu Lamb hi’a’asabun i sawar yawasih ma’anih kwafe’en, naatu regaregah ai’in hi’ar bebera’uh nah yan foun urama’ama nanamaim batabat aitin. I ukwarinamaim ana rarag etei seven naatu matan etei seven, nati i wagabur seven God iyafarih hitit tafaram wanawananamaim.
7 Iye anabwera natenga buku lija limene linali mʼdzanja lamanja la wokhala pa mpando waufumuyo.
7 Lamb na urama’ama afe’en orot nati ma’am uman ana asukwafune fef firorow bosair.
8 Ndipo atalitenga, zamoyo zinayi zija ndi akuluakulu 24 aja anadzigwetsa pansi pamaso pa Mwana Wankhosa. Aliyense wa akuluakuluwo anali ndi zeze ndiponso mbale zagolide zodzaza ndi lubani. Lubaniyo ndi mapemphero a oyera mtima.
8 Naatu nati na’atube sisinaf anamaramaim sawar yawasih kwafe’en naatu regaregah ai’in 24 Lamb nanamaim hira’iy, ta’ita’imon umahimaim etei douduf hibow naatu fi’ufiu ana tew i gold. Imaim fi’ufiu hibiwanen auman hibow, nati i God ana sabuw hai yoyoban.
9 Ndipo ankayimba nyimbo yatsopano yakuti,
9 Naatu ew boubun hitabor,
10 Inu munawasandutsa kukhala mtundu waufumu ndi ansembe otumikira Mulungu,
10 O iti sabuw ibow firis ana aiwob iwowab matar ata God isan tanabow,
11 Kenaka nditayangʼananso ndinamva mawu a angelo ambiri, miyandamiyanda kuchulukitsa ndi miyandamiyanda. Anazungulira mpando waufumu pamodzi ndi zamoyo zija ndi akuluakulu aja.
11 Imaibo ayu anuw naatu tounamatar moumurih maiyow fanah anowar, tounamatar himour kwanekwan taniyab men karam thousand million na’atube. I urama’ama sawar yawasih kwafe’en naatu regaregah ai’in hi’arbebera’uhih.
12 Ndipo angelowo anayimba ndi mawu ofuwula akuti,
12 Fanah aumetawat na’in ew hitabor,
13 Kenaka ndinamva mawu a cholengedwa chilichonse kumwamba, pa dziko lapansi, kunsi kwa dziko lapansi, pa nyanja ndi zonse zili mʼmenemo zikuyimba kuti,
13 Imaibo ayu sawar yawasih bai’e’etawayah mar wanawanan, tafaram wanawanan, me wanawanan, riy wanawanan etei fanah sib hitatabor anowar.
14 Zamoyo zinayi zija zinati: “Ameni,” ndipo akuluakulu aja anadzigwetsa pansi napembedza.
14 Sawar yawasih ma’anih kwafe’en etei fanah hibora’ah hio, “Turobe!” regaregah ai’in yumatah aubabe hire hikwafir.

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Apocalipse 5, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.