Apocalipse 3

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI

Sair da comparação
AAI TUR GEWASIN O BAIBASIT BOUBUN
1 “Lembera mngelo wampingo wa ku Sarde kuti:
1 “Iti tur i Sardis ekaleisia ana tounamatar isan inakirum.
2 Dzuka! Limbitsa zimene zatsalira zomwe zatsala pangʼono kufa, pakuti ndaona kuti ntchito zako nʼzosakwanira pamaso pa Mulungu.
2 Kwamisir! Abisa kikimin biyamaim ema’am koufair kwanitinibo namorob nasawar, anayabin kwa abisa kwasisinaf au God matanamaim atitita’ur i men gewasin anababatun.
3 Choncho, kumbukira zimene unalandira ndi kumva; uzisunge ndipo ulape. Koma ngati sudzuka, ndidzabwera ngati mbala ndipo sudzadziwa nthawi imene ndidzabwere kwanu.
3 Abisa kwanowar kwabaib i kwananot, kwanabosiyasiyar naatu dogor hinikitabir. Baise men kwanamimisir na’at, ayu boro bainowan mowan na’atube anan, naatu veya boro men kwa kwanotanotamaim ananamih.
4 Komabe uli ndi anthu angapo mu Sarde amene sanadetse zovala zawo. Amenewa adzayenda ndi Ine atavala zoyera popeza ndi oyenera kutero.
4 Baise kwa Sardis wanawanan ekaleisia matan ta a faifuw i kwasouwen kwama’am, a faifuw kwes kwa’osen ayu bairi taremor tanan, anayabin kwa asinaf i gewasin.
5 Amene adzapambane adzavala zoyera ngati ena aja. Sindidzafafaniza dzina lake mʼbuku lamoyo, koma ndidzamuchitira umboni pamaso pa Atate anga ndi angelo ake.
5 Orot yait baiyow fokarin bisnowah i boro ana faifuw kwes na’us, naatu ayu wabin wanatowan ana bukamaim boro men anasafam, baise wabin boro anaorereb Tamai nanamaim na’atube tounamatar nahimaim.
6 Amene ali ndi makutu, amve zimene Mzimu akuwuza mipingo.”
6 Yait tainin nama’am na’at Anun Kakafiyin ekaleisia isan abisa eo inanowar.”
7 “Lembera mngelo wampingo wa ku Filadefiya kuti:
7 “Iti tur i ekaleisia Piladelfia wanawanan tema’am ana tounamatar isan inakirum,
8 Iye akuti, ‘Ine ndimadziwa ntchito zako. Taona, ndakutsekulira pa khomo ndipo palibe wina amene angatseke. Ndikudziwa kuti uli ndi mphamvu zochepa komabe wasunga mawu anga ndipo sunandikane.
8 Ayu aso’ob kwa asinaf, naatu kwana’itin, ayu kwa isa etawan i abotawiy naatu boro men yait ta nahir, ayu aso’ob kwa afair i kikimin, baise ayu au bai’obaiyen kwabosiyasiyar kwabi’ufunun naatu wabu men kwayayoub.
9 Amene ndi mpingo wa Satana, amene amadzitcha kuti ndi Ayuda pamene sali choncho, koma ndi onama, ndidzawabweretsa kwa inu ndi kuwagwetsa pansi pa mapazi anu kuti adzazindikire kuti ndimakukondani.
9 Kwananowar! Sabuw iyab Satan ana Kou’ay Baremaim tema’am, taiyuwih hifufuwih tibijew moyamoy boro anao kikinih hinan kwa amaim hinakwafir hinare, naatu hinaso’ob kwa i ayu abiyabuwi.
10 Popeza mwasunga mawu anga woti mupirire ndipo mwawugwira mtima, Inenso ndidzakupulumutsani nthawi ya mayesero imene idzabwera pa dziko lonse lapansi kuyesa onse okhala pa dziko lapansi.
10 Anayabin kwa au obaiyunen tur kwabai yatenubamaim ewawainabi, routobon nati tafaramamaim boro enan sabuw iyab nati me yan tema’am routubunih isan, ayu boro kwa anatafafari.
11 Ine ndikubwera msanga. Gwiritsitsa chimene uli nacho kuti wina angakulande chipewa chako chaufumu.
11 “Ayu boro’omo anan. Abisa kwabobotan i kwanabukikin, saise boro men yait ta kwa a kowas nabosair.
12 Iye amene adzapambane ndidzamusandutsa mzati wa mʼNyumba ya Mulungu wanga. Sadzatulukamonso. Pa iye ndidzalemba dzina la Mulungu wanga ndi dzina la mzinda wa Mulungu wanga, Yerusalemu watsopano, umene ukubwera pansi kuchokera kumwamba kwa Mulungu wanga; ndipo pa iye ndidzalembanso dzina langa latsopano.
12 Orot yait baiyow fokarin ebisnowah, i boro Tamai God Ana Bar ana wabat namatar. Naatu nati Tafaror Bar boro men nihamiyimih. Ayu boro Au God wabin biyanamaim anakirum naatu au God ana bar merar wabin anakirum. Jerusalem boubun au God biyan marane ere’ere, naatu ayu auman boro wabu boubun imaim anakirum.
13 Amene ali ndi makutu, amve zimene Mzimu akuwuza mipingo.’ ”
13 O yait tain nama’am na’at, tur iti Anun Kakafiyin ekaleisia isan eo inanowar.”
14 “Lembera mngelo wampingo wa ku Laodikaya kuti:
14 “Tur iti inakirum Laodicea ekaleisia ana tounamatar isan.
15 Ine ndimadziwa ntchito zako, kuti sindiwe wozizira kapena wotentha. Ndikanakonda ukanakhala wozizira kapena wotentha!
15 Ayu kwa a bowabow i aso’ob, kwa men siba’u’i o men fora’abi, akokok i mi’itube iti ta’ane kwatama.
16 Tsono popeza ndiwe wofunda chabe, sindiwe wotentha kapena wozizira, ndatsala pangʼono kuti ndikulavule mʼkamwa mwanga.
16 Baise ana itinin i a fora’abin kikimin, men siba’u’un naatu men towa anababatun, imih ayu boro awou’umaim ana kwai’atait kwanatit.
17 Iwe umati: ‘Ndine wolemera, ndine wachuma ndipo sindisowa kanthu.’ Koma sudziwa kuti ndiwe wovutika, womvetsa chisoni, waumphawi, wosaona ndi wamaliseche.
17 Kwa taiyuw i totobuyoy wairaf kwarouw kwao, naatu sawar etei aur karamin kwarouw kwao, naatu men kwakokok boro sawar ta kwanab, baise kwa taiyuw men kwa’inani kwaso’obamih, kwa i kakaf, tenakuyakuy, bai’akirayah, mata fim, segar.
18 Ndikukulangiza kuti ugule kwa Ine golide woyengedwa ndi moto kuti ukhale wolemera. Ugule zovala zoyera kuti uvale ndi kuphimba umaliseche wako wochititsa manyaziwo. Ndiponso ugule kwa Ine mankhwala a mʼmaso kuti uwone.
18 Ayu biyau’umaim gold kwatutubun isan a tur aowen not ait, gold wairafamaim hi’afun hirurububunai inu’in kwatatutubun kwa boro totobuyoy wairaf kwatamatar. Naatu faifuw kwes kwata’us, saise a biya’ohow ana segar kwatasum. Naatu fiyow kwatatubun mata kwatasouw, saise mata takubunai kwatanuw gewas.
19 Amene ndimawakonda ndimawadzudzula ndi kuwalanga. Choncho chita changu ndipo lapa.
19 “Sabuw iyab ayu abiyabuwih i akwararih ayayamutufurih, imih akokok gewasinamaim dogor baikitabir kwanab.
20 Taonani ndayima pa khomo ndikugogoda. Ngati wina amva mawu anga natsekula chitseko, Ine ndidzalowamo ndi kudya naye, Ine ndi iyeyo.
20 Ayu i iti, a etawan awan abat arurukikitar, orot babin yait fanau nanowar ana etawan nabobotawiy na’at, ayu boro anarun airi anafarambonen anaa anatom. Jesus a etawan erurukikir|alt="Jesus knocking on door" src="cn02107B.tif" size="col" loc="Rev 3.20" copy="©1978 David C. Cook Publishing Co." ref="3.20"
21 Amene adzapambana, ndidzamupatsa ufulu wokhala nane pamodzi pa mpando wanga waufumu monga mmene Ine ndinapambana ndi kukhala pansi ndi Atate anga pa mpando wawo waufumu.
21 “Orot yait baiyow nabisnowah, ayu boro baibasit anitin au urama’ama’amaim namare, ayu baiyow aisnowah Tamai ana urama’ama’amaim amare airi ama’am na’atube.
22 Amene ali ndi makutu, amve zimene Mzimu akuwuza mipingo.”
22 O yait tain nama’am na’at, iti tur Anun Kakafiyin ekaleisia isah eo inanowar!”

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Apocalipse 3, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.