Apocalipse 2
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 “Lembera mngelo wa mpingo wa ku Efeso kuti:
1 “Tur iti i Ephesus ekaleisia ana tounamatar isan inakirum:
2 Ine ndimadziwa zochita zako, ntchito yako yowawa ndi kupirira kwako. Ine ndimadziwa kuti sungalekerere anthu oyipa amene amadzitcha atumwi pamene sichoncho, unawayesa, ndipo unawapeza kuti ndi abodza.
2 Ayu aso’ob o abistan isinaf, ayu aso’ob o yatenub wainabi bowabow fokarin men sanet ibow, ayu aso’ob o men karam boro sabuw kakafih bairi kwanikofan, naatu iyabowat tur abarayah hirouw hio, baise o ifufunih i en, naatu isusu’ubih i baifufuwenayah.
3 Iwe wapirira ndipo wakumana ndi zovuta chifukwa cha dzina langa, ndipo sunatope.
3 Ayu wabu’umaim kwa biyababan fokarih wanawanan kwarur men kwahahar kwai hamiyu’umih.
4 Komabe ndili ndi chotsutsana nawe: Wataya chikondi chako chapoyamba.
4 Baise iti i ayu au yaso’ar tur kwa isa, marasika kwabiyabuwu na’atube boun men kwabiyabuwu.
5 Kumbukirani kuti munagwa kuchokera patali. Lapa ndikuchita zinthu zimene unkachita poyamba. Ngati sulapa ndidzabwera ndikukuchotsera choyikapo nyale chako pamalo pake.
5 Kwa anamanin men sanet kware’ere i kwaso’ob, imih bowabow kakafihine kwanamatabir naatu marasika abistan kwasisinaf i kwanasinaf maiye. Baise kakafihine men kwanamamatabir, ayu boro isa anan a ramef hai batabat hai efanamaim anabosair.
6 Komabe chokomera chako ndi chakuti umadana ndi zochita za Anikolai, zimene Inenso ndimadana nazo.
6 Baise sawar ta’imonamo i kusisinaf gewas. Nikolas sabuw hai sinaf kakafih i o men kukokok, ayu auman men akokok.
7 Amene ali ndi makutu, amve zimene Mzimu akuwuza mipingo. Amene adzapambana, ndidzamupatsa ufulu wakudya zipatso za mtengo wopatsa moyo umene uli ku paradizo wa Mulungu.
7 Tain hinama’am na’at Anun Kakafiyin ekaleisia isan eo kwanowar! Sabuw iyabowat bai’akir hibisnowah ayu karam boro yawas ana ai ro’on anitih hina’aan, ai nati i God ana masaw Paradise wanawanan ebatabat.”
8 “Lembera mngelo wa mpingo wa ku Simurna kuti:
8 “Iti tur inakirum Simena ekaleisia ana tounamatar isan.
9 Ine ndimadziwa masautso ako ndi umphawi wako, chonsecho ndiwe wolemera! Ndikudziwa zimene amakusinjirira anthu amene amati ndi Ayuda pamene sizili choncho, koma ndi a mpingo wa Satana.
9 Ayu kwa abai’akir, naatu a sawar en kwabi’akir i ayu aso’ob, baise anababatun kwa i sawar wairaf. Naatu sabuw hibijew moyamoy kwa isa tur kakafih hio i ayu aso’ob, nati sabuw i men Jew anababatun, nati sabuw i Satan ana kou’ay!
10 Musachite mantha ndi zimene muti musauke nazo posachedwapa. Ndithu, Satana adzayika ena a inu mʼndende pofuna kukuyesani, ndipo mudzazunzika kwa masiku khumi. Khalani okhulupirika ngakhale zitafika pa imfa, ndipo Ine ndidzakupatsani chipewa cha ulemerero wamoyo.
10 Bai’akir wanawanan kwanarur men kwanabir, kwananowar Demon mowan boro nabonawiy dibur nayariyi routobon nit, veya etei ten ana fofonin biyababan kwanab. Kwanabatkikin, morob na’at kwanamorob, naatu ayu boro ma’ama wanatowan ana kowas anit.
11 Amene ali ndi makutu, amve zimene Mzimu akuwuza mipingo. Amene adzapambana sadzapwetekedwa ndi pangʼono pomwe ndi imfa yachiwiri.
11 O yait tain ema’am, abistan Anun Kakafiyin ekaleisia sabuw isah eo inanowar. Orot yait bai’akir bisnowah boro men morob bairou’abin ana biyababan nab.”
12 “Lembera mngelo wa mpingo wa ku Pergamo kuti:
12 “Iti tur inakirum Pergamum ekaleisia ana tounamatar isan.
13 Iye akuti, ‘Ine ndimadziwa kumene mumakhala, kumene kuli mpando waufumu wa Satana. Komabe inu ndinu okhulupirika kwa Ine. Simunataye chikhulupiriro chanu pa Ine, ngakhale mʼmasiku a Antipa, mboni yanga yokhulupirika, amene anaphedwa mu mzinda wanu, kumene amakhala Satana.
13 Ayu aso’ob nati bar merar o kuma’am i Demon Ana Aiwob ana urama’ama efan, baise o i turobe ayu wabu’umaim kuma’am, naatu men sawar afa’amaim a baitumatum fatumimih, nati ana veya Demon nati’imaim ma’am, imih ayu au baitumatumayan Antipas hirab morob.
14 Komabe, ndili ndi zinthu zingapo zotsutsana nanu. Kumeneko muli ndi anthu ena amene amatsata ziphunzitso za Balaamu, uja amene anaphunzitsa Baraki kukopa Aisraeli kuti azidya nsembe zoperekedwa ku mafano ndi kumachita chigololo.
14 Baise sawar afa kusisinaf isan ayu men abiyasisir. Nati biyamaim i sabuw afa Balam ana bai’obaiyen hibai hima’am, Balak hi’obaiy Israel sabuw bonawiyih bay aibat isah hisisibor hi’aa bowabow kakafih sinafuyah himatar hima tibiwa’an kwanekwan.
15 Chimodzimodzinso inuyo muli ndi ena amene amatsatira ziphunzitso za Anikolai.
15 Ef nati ta’imon sabuw afa nati wanawanahimaim i Nikolas ana sabuw bai’obaiyen ta’imon tibi’ufunun.
16 Tsono tembenukani mtima. Mukapanda kutero, ndidzabwera kwanuko posachedwa ndipo ndidzachita nanu nkhondo ndi lupanga lotuluka mʼkamwa mwanga lija.
16 Isan imih bowabow kakafihine dogor kwanikitabir kwanatit, o en ayu boro’omo anan kaiy iti awau’umaim bairi aniyow.
17 Amene ali ndi makutu, amve zimene Mzimu akuwuza mipingo. Kwa amene adzapambane ndidzamupatsa chakudya chobisika cha mana. Ndidzamupatsanso mwala woyera wolembedwapo dzina latsopano, lodziwa iye yekha amene walandirayo.’ ”
17 O yait tain nama’am na’at Anun Kakafiyin ekaleisia isah eo nanowar! Orot yait bai’akir ebisnowah i boro wa’iwa’irin ana bay anitin, naatu kabay biyan kwes tafanamaim wabin boubun hikirum inu’in auman boro anitin, nati boro men yait ta naso’ob baise orot ebaib akisinamo.”
18 “Lembera mngelo wampingo wa ku Tiyatira kuti:
18 “Iti tur inakirum Taiyatira ekaleisia ana tounamatar isan.
19 Iye akuti: Ndimadziwa ntchito zanu, chikondi chanu ndi chikhulupiriro chanu, kutumikira kwanu ndi kupirira kwanu. Ndikudziwa tsopano kuti ntchito zanu ndi zabwino kuposa zoyamba zija.
19 O abisa kusisinaf i ayu aso’ob, o a yabow, a baisnubanub, a bowabow, naatu anutanub, naatu boun abisa kusisinaf i tafan hiya’abar wan isisinaf i inatabir.
20 Komabe ndili ndi chinthu chokudzudzula nacho. Umamulekerera mkazi uja Yezebeli amene amadzitcha yekha kuti ndi mneneri. Iye amaphunzitsa atumiki anga kuti azichita zadama ndi kumadya zansembe zoperekedwa ku mafano.
20 Baise sawar ta o wanawananamaim ema’am isan ayu men abiyasisir, anayabin o babin wabin Jezebel taiyuwin God ana dinab babin rouw eo, o airi kwaikofan, ana bai’obaiyenamaim ayu au akirwairafih nawiyih ef hisa’ir hin baiwa’an kwanekwan wanawanan hirun naatu bay aibat isah hisisibor hibow te’aau.
21 Ndamupatsa nthawi kuti aleke zachigololo zake koma sakufuna.
21 Ayu i veya aitin ana bowabow kakafihine dogor baikitabir tab isan, baise i men ekokok baiwa’an kwanekwanane dogoron nikitabir.
22 Tsono ndidzamugwetsa mʼmasautso ndipo amene amachita naye zadama zakezo ndidzawasautsa kwambiri akapanda kulapa ndi kuleka njira za mkaziyo.
22 Imih ayu boro biyababan ana gem tafan ana yara’ah naatu iyabowat bairi hibiwa’an boro bai’akir kakafin maiyow hinab biyah nababan. Baise iyab babin ana kakafihine hinabihir hinatitit i boro anihamiyih.
23 Ana ake ndidzawakantha ndi kuwapheratu. Kotero mipingo yonse idzadziwa kuti Ine ndine uja amene ndimafufuza mʼmitima mwa anthu ndi mʼmaganizo mwawo. Aliyense wa inu ndidzachita naye monga mwa ntchito zake.
23 I natunatun auman boro ana rouw hinamorob. Imaibo ekaleisia etei boro hinaso’ob ayu i orot babin dogoroh naatu hai not etei anuteteyan aso’ob, imih abisa kwasisinafumaim boro wan anay anit.
24 Tsopano ndikunena kwa enanu a ku Tiyatira, kwa inu amene simunatsate chiphunzitso cha mkaziyo ndipo simunaphunzire zimene iwo amati ndi ‘zinsinsi zonama’ za Satana. Kwa inu mawu anga ndi akuti sindikuwunjikirani malamulo ena.
24 Baise kwa turin nati Taiyatira wanawanan kwama’am iti bai’obaiyen kakafin men kwabi’ufunun, kwa ‘Satan ana bai’obaiyen buriburih men kwaso’ob,’ imih ayu boro men bit ta anitimih.
25 Inu mungogwiritsa zimene munaphunzira basi, mpaka Ine ndidzabwere.
25 Baise abisa biyamaim ema’am i kwanabukikin kwanama’am ayu anan.
26 Amene adzapambana ndi kuchita chifuniro changa mpaka kumapeto, ndidzamupatsa ulamuliro pa mitundu yonse ya anthu.
26 Orot yait bai’akir nisnowah naatu au kokomaim nama nasinaf nan yomanin natitit ayu boro fair anitin tafaram etei isah.
27 Adzayilamulira ndi ndodo yachitsulo ndipo nadzayiphwanyaphwanya ngati mbiya. Ulamuliro umenewu ndi omwe ndinalandira kwa Atate anga.
27 Naatu i boro ana fair tutufin etei nab sabuw nabonawiyih,
28 Ine ndidzamupatsanso nthanda, nyenyezi yowala mʼmamawa ija.
28 Ayu boro marauman Maragias anitin.
29 Amene ali ndi makutu, amve zimene Mzimu akuwuza mipingo.
29 O yait tain nama’am na’at Anun Kakafiyin Ekaleisia isah tur eo inanowar!”
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Apocalipse 2, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.