Apocalipse 22

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs MNT

Sair da comparação
MNT Minaifia NT
1 Ndipo mngeloyo anandionetsa mtsinje wamadzi amoyo, oyera ngati mwala wa krustalo ukutuluka ku mpando waufumu wa Mulungu ndi wa Mwana Wankhosa,
1 Imaibo retab yan yawas ana harew matan kiriyamiyamin crystal na’atube God ana urama’ama naatu Lamb ana urama’ama’ane nunuw re’er i’obaiyu aitin.
2 Ukuyenda pakati pa msewu waukulu wa mu mzindawo. Mbali iliyonse ya mtsinjewo kunali mtengo wamoyo, utabala zipatso khumi ndi ziwiri. Kubereka zipatso mwezi uliwonse. Ndipo masamba a mtengowo ndi mankhwala wochiritsa anthu a mitundu ina.
2 Iti harew i bar merar gagamin ana ef na’in yan foun in nununuw. Naatu harew rewan roun roun i yawas ana ai hibatabat aitah, iti ai i kwamur ta’imon wanawanan mar etei twelve ebiw, sumar matan eyiy, naatu ai rourin i tafaram ana yawas.
3 Sipadzakhalanso temberero lililonse. Mpando waufumu wa Mulungu ndi wa Mwana Wankhosa udzakhala mu mzindawo, ndipo atumiki ake adzamutumikira.
3 Nati bar merar gagamin wanawanan God ana orarafen ta boro men inatita’ur. God ana urama’ama naatu Lamb ana urama’ama boro nati bar merar gagaminamaim hinama ana akir wairafih i hinakwafirih.
4 Iwo adzaona nkhope yake ndipo dzina lake lidzalembedwa pa mphumi zawo.
4 Yumatan boro hina’itin naatu wabin boro nakwetahimaim nakirum hinama.
5 Sipadzakhalanso usiku. Sadzafuna kuwala kwa nyale kapena kwa dzuwa pakuti Ambuye Mulungu adzakhala kuwala kwawo. Ndipo adzalamulira kwamuyaya.
5 Nati’imaim gugumin boro en. Ramef ana marakaw naatu veya ana marakaw boro en, anayabin Regah God boro marakaw nitih, naatu i boro bairi hini’aiwob wanatowan, wanatowan.
6 Mngeloyo anandiwuza kuti, “Mawu awa ndi okhulupirika ndi owona. Ambuye Mulungu wa mizimu ya aneneri anatumiza mngelo wake kudzaonetsa atumiki ake zinthu zimene ziyenera kuchitika posachedwapa.”
6 Imaibo tounamatar iuwu, “Iti tur i anababatun turobe initumatum. Regah God sawar abisa boro hinamamatar isan i Anunin ana dinab orot hai tur eowen, naatu ana tounamatar iyafarih abisa boro’omo hinamamatar isan ana akir wairafih i’obaiyih.”
7 “Taonani, ndikubwera posachedwa! Wodala ndi amene asunga mawu oneneratu za kutsogolo a mʼbuku ili.”
7 Kwananowar, ayu i boro’omo anan, dinabatur iti buk wanawanan hikikirum o yait inabifanabow boro baigegewasin inab.
8 Ine Yohane, ndine amene ndinamva ndi kuona zinthu izi. Ndipo pamene ndinamva ndi kuona izi ndinagwa pansi kuti ndipembedze mngelo amene amandionetsa zimenezi.
8 Ayu John taiyuwu iti sawar fanah anowar naatu aitah naatu iti sawar fanah anowar ai’itah ana maramaim anamaim ara’iy tounamatar iti sawar bi’obaiyu akwafir.
9 Koma mngeloyo anandiwuza kuti, “Usatero ayi! Ine ndine wotumikira monga iwe pamodzi ndi abale ako aneneri ndi onse amene amasunga mawu a mʼbuku pembedzani Mulungu.”
9 Baise iuwu, “Men iti na’atube inasinaf, o ayu airit i God ana akir wairafit, taituwa baitumatumayah dinab oro’orot iyab iti buk wanawanan tibifanabow bairit. God akisin inakwafir.”
10 Kenaka anandiwuza kuti, “Usabise mawu onena zamʼtsogolo a mʼbuku ili chifukwa nthawi yayandikira.
10 Imaibo iuwu, “Dinabatur buk wanawanan hikirum inu’in men inarufut inikwah anayabin veya i nakabom.
11 Wochita zoyipa apitirire kuchita zoyipazo; wochita zonyansa apitirire kuchita zonyansazo; wochita zabwino apitirire kuchita zabwinozo; ndipo woyera mtima apitirire kukhala woyera mtima.”
11 Yait ma kakafih esisinaf kwaihamiy ema kakafih esinaf. Yait ma yawas ebigugumas kwaihamiy ema igugumas. Yait ma mutufor esisinaf kwaihamiy ema mutufor esinaf. Yait taiyuwin ya’asair kakafiyinamaim ema’am kwaihamiy kakafiyinamaim ema.”
12 “Taonani, ndikubwera posachedwa! Ndikubwera ndi mphotho zanga kuti ndidzapereke kwa aliyense malinga ndi zimene anachita.
12 “Kwananowar! ayu i boro’omo anan, umau’umaim i au baiyan abai auman naatu kwa ta’ita’imon abisa kwasisinafumaim boro anit.
13 Ine ndine Alefa ndi Omega, Woyamba ndi Wotsiriza, Chiyambi ndi Chimaliziro ndine.
13 Ayu i Alpha naatu Omega, ayu i An naatu Yomanin, Busurufin naatu Baisawarin.
14 “Odala amene achapa mikanjo yawo, kuti akhale ndi ufulu wopita ku mtengo wamoyo ndi kuti akalowe mʼzipata za mu mzindawo.
14 “Iyab hai faifuw hisouwen hibigewasin i hai baibasit ema’am boro yawas ana ai ro’on hina’aan baigegewasin hinab, naatu hai ef mutufor inu’in bar merar gagamin ana etawan hinarun.
15 Kunja kuli agalu, amatsenga, achiwerewere, akupha anthu, opembedza mafano ndi aliyense amene amakonda bodza ndi kulichita.
15 Bar merar gagamin ufunane i sabuw kakafih haru’ube tema’am. Nati sabuw i farumayah, baiwa’an kwanekwaneyah, asbunubunuwayah, God ana baimataren sawar kwafirenayah, naatu sabuw iyab hai tur hai bowabowamaim tibifufuwen i tema’am.
16 “Ine Yesu, ndatuma mngelo wanga kuti achitire umboni uwu ku mipingo. Ine ndine Muzu ndi Chipatso cha Davide ndipo ndine Nthanda Yonyezimira.”
16 “Ayu Jesu iti sawar kwa ekaleisia isa orereb isan au tounamatar ai yafar na. Ayu i David uwan naatu ana rara, naatu mar auman ana Maragias ana marakaw.”
17 Mzimu Woyera ndi mkwatibwi akuti, “Bwerani!” Ndipo amene akumva anena kuti Bwerani! Iye amene ali ndi ludzu abwere, ndipo aliyense amene afuna alandire mphatso yaulere ya madzi amoyo.
17 Anun Kakafiyin naatu tabin ana babitai hio, “Kuna!” Naatu iyab tur tenonowar i auman hinao, “Kuna! Naatu yait sikan emamamah kwaihamiyih tena, naatu yait nakokok yawas ana harew tomamih kwaihamiy ena ana siwaramih ebai etom.”
18 Ndikuchenjeza aliyense amene akumva mawu onena zamʼtsogolo a mʼbukuli kuti, “Ngati wina awonjezerapo kalikonse, Mulungu adzamuwonjezera miliri imene yalembedwa mʼbuku ili.
18 Ayu John kwa sabuw etei dinabatur iti buk wanawanan kwanonowar i abimatnuwi. Orot yait iti tur tafan nayaya’abar na’at, sawow kakafih yumatah ta ta iti buk wanawanan hio, God boro ibo tafan naya’abar baimakiy nitin.
19 Ndipo wina akachotsapo mawu onena zamʼtsogolo a mʼbuku ili, Mulungu adzachotsa gawo lake pa mtengo wamoyo ndi la mu mzinda woyera zimene zanenedwa mʼbuku ili.”
19 Naatu orot yait dinabatur iti buk wanawanan hikikirum ta nabobosa’ir na’at, i aunowan yawas ana ai ro’on naatu bar merar gagamin isan hio, God boro nabosair.
20 Iye amene akuchitira umboni pa zinthu izi akuti, “Inde, Ine ndikubwera posachedwa.”
20 Orot iti sawar eo’orereb, eo, “Isa’amih, ayu boro’omo anan.” Turobe. Regah Keriso, kuna.
21 Chisomo cha Ambuye Yesu chikhale ndi anthu onse. Ameni.
21 Manaw kabeber ata Regah Jesu’une kwa God ana sabuw etei isa nama. Amen.

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Apocalipse 22, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.