Apocalipse 20

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI

Sair da comparação
AAI TUR GEWASIN O BAIBASIT BOUBUN
1 Ndipo ndinaona mngelo akutsika kuchokera kumwamba ali ndi kiyi ya ku chidzenje chakuya chija atanyamula mʼdzanja lake unyolo waukulu.
1 Naatu ayu marane tounamatar umanamaim efan wanu’umin ana tufatan naatu ana chain bitan auman botan renan aitin.
2 Iye anachigwira chinjokacho, chinjoka chakalekale chija, amene ndi Mdierekezi kapena kuti Satana, ndipo anamumanga zaka 1,000.
2 Farubarubar bai rab, kik owe’owen ana kok, wabin Demon o Satan naatu fatum kwamur one thousand na’atube nama.
3 Anamuponya ku chidzenje chakuya chija namutsekera ndi kiyi ndi kumatirira pa khomopo kuti asatulukenso kukanyenga mitundu ya anthu mpaka patapita zaka 1,000. Zikadzatha zakazo, adzamumasula kwa kanthawi pangʼono chabe.
3 Ta’asiy sou wanu’umin wanawanan ra’iy etawan tufabon naatu ikwah, saise i boro men tafaram ni’afiy maiye kwamur one thousand nasawarabo. Nati ufunamaim i boro hinabotait mar kabumin nama.”
4 Ndinaona mipando yaufumu pamene anakhalapo anthu amene anapatsidwa mphamvu zoweruza. Ndipo ndinaona mizimu ya amene anadulidwa makosi chifukwa cha umboni wa Yesu ndi chifukwa cha Mawu a Mulungu. Iwo sanapembedze nawo chirombo kapena fano lake ndipo sanalembedwe chizindikiro chake pa mphumi zawo kapena pa manja awo. Iwo anakhalanso ndi moyo nalamulira pamodzi ndi Khristu zaka 1,000.
4 “Ayu urama’ama tafanamaim sabuw iyabowat baibatiyen isan ana fair hibitih himarir hima’am aitih. Naatu sabuw Jesu isan hio’orereb isan sikah hi’a’afuw naatu God ana tur isan sikah hi’a’afuw etei ayubih hima’am aitih. Iti sabuw i men kafa’imo sawaidab naatu i ana yumatabe hikwafirihimih, naatu ana ewow auman umahimaim o nakwetahimaim men hikirumimih. Etei hiyawas naatu Keriso bairi kwamur one thousand na’atube hi’aiwob.
5 (Akufa ena onse sanaukenso mpaka zitatha zaka 1,000). Uku ndiko kuuka kwa akufa koyamba.
5 Murumurubih afa men hiyawas na’atuka hima kwamur one thousand in sawar. Iti i murumurubih hai misir wantoro’ot.
6 Odala ndi oyera mtima amene adzaukitsidwa nawo pa kuukitsidwa koyamba. Imfa yachiwiri ilibe mphamvu pa iwo koma adzakhala ansembe a Mulungu ndi a Khristu ndipo adzalamulira naye pamodzi zaka 1,000.
6 Yasisir naatu baigegewasin i sabuw iyabowat wantoro’ot morobone himimisir maiye isah. Morob bairou’abin i isah i aurin fair en, baise i boro God ana firis naatu Keriso ana firis hinamatar Keriso bairi hini’aiwob kwamur one thousand nab.”
7 Zaka 1,000 zikadzatha, Satana adzamasulidwa ku ndende yake
7 Kwamur etei one thousand nasasawar ufunamaim, Satan boro i ana dibur barene hinabotait.
8 ndipo adzapita kukanyenga mitundu ya anthu kumbali zonse zinayi za dziko lapansi, Gogi ndi Magogi, kuwasonkhanitsa kuti akachite nkhondo. Kuchuluka kwawo kudzakhala ngati mchenga wa mʼmbali mwa nyanja.
8 naatu natit nan tafaram Gog naatu Magog ana huhun kwafe’en sabuw etei nifufuwih narunawiyih baiyow isan, naatu nati sabuw baiyow isan hinaruru’ay ana itinin riy sisibin dones na’atube.
9 Iwo anayenda ponseponse pa dziko lapansi nazinga msasa wa anthu a Mulungu, mzinda umene Iye amawukonda. Koma moto unatsika kuchokera kumwamba ndi kuwanyeketsa.
9 Naatu me yabarin yan tasasar hitit hiremor hin God ana sabuw hai ma’ama sis naatu God ana yabow bar merar etei hi’ar bebera’uhih, baise marane wairaf ra’iy na bo’ara’ara’ahih.
10 Ndipo Mdierekezi amene anawanyenga, anaponyedwa mʼnyanja ya sulufule wotentha, kumene kunaponyedwa chirombo chija ndi mneneri wonama uja. Iwo adzazunzika usiku ndi usana kwamuyaya.
10 Naatu Demon mowan bifufuwih hibai hita’asiy wairaf in bitakir wanawanan ra’iy eafufur, sawaidab naatu dinab baifuwenayan hairi hita’asiyih hire’ere’emaim. Nati’imaim boro fai mar hini’akir wanatowan, wanatowan.
11 Kenaka ndinaona Mpando Waufumu waukulu woyera ndi Iye amene anakhalapo. Dziko lapansi ndi kumwamba zinathawa pamaso pake ndipo panalibenso malo awo.
11 Imaibo ayu ura ma’ama kwes gagamin tafanamaim God ma’am aitin. Mar tafaram i nanamaim earouwasa’ir, naatu nati’imaim i aurih efan en.
12 Ndipo ndinaona akufa, aakulu ndi aangʼono omwe atayimirira patsogolo pa Mpando Waufumu ndipo mabuku anatsekulidwa. Buku lina linatsekulidwa limene linali Buku Lamoyo. Akufa anaweruzidwa monga mwa zimene anachita monga mmene zinalembedwera mʼmabuku.
12 Naatu ayu sabuw murumurubih aitih, gagamin re in kikimin ura ma’ama nanamaim hibatabat, naatu buk etei hibotawiyen. Buk ta hibobotawiy i yawas ana buk. Murumurubih abisa hisinaf bukamaim hikirum hi’inu’in imaim hibabatiyih.
13 Nyanja inapereka amene anaferamo ndipo imfa ndi Hade zinapereka akufa ake ndipo munthu aliyense anaweruzidwa monga mwa ntchito zake.
13 Riy wanawanan murubih kwahiren, naatu morob naatu morob ana efan, murumurubih hikwahirih. Naatu orot ta’ita’imon hai sinafumaim hibabatiyih.
14 Kenaka imfa ndi Hade zinaponyedwa mʼnyanja ya moto. Nyanja yamoto ndiyo imfa yachiwiri.
14 Imaibo murumurubih naatu murubih hai efan i hita’asiyih wairaf ana kukuf wanawanan hira’iy, iti wairaf i morob bairou’abin.
15 Ngati dzina la wina aliyense silinapezeke mʼBuku Lamoyo, anaponyedwa mʼnyanja yamoto.
15 Yait ta wabin men yawas ana bukamaim hititita’ur i hita’asiy wairaf ana kukuf wanawananan rara’iy.

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Apocalipse 20, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.