Apocalipse 17
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Mmodzi wa angelo asanu ndi awiri aja amene anali ndi mbale zisanu ndi ziwiri anadza nati kwa ine, “Bwera ndikuonetse chilango cha mkazi wadama wotchuka uja amene akukhala pambali pa madzi ambiri.
1 Tounamatar sevenwanawanahimaim tounamatar ta tew bai seven bobotanen na eo, “Kuna ayu boro babin baiwa’an kwanekwaneyan wabin gagamin harew moumurih yan emamare’ere ana baimakiy ani’obaiy ina’itin.
2 Mafumu a dziko lapansi amachita naye chigololo ndipo okhala pa dziko lapansi analedzera ndi vinyo wa zigololo zake.”
2 Tafaram ana aiwob hina bairi hiwa’an kwanekwan naatu tafaram ana sabuw baiwa’an kwanekwan ana wine hitom hikoko’aw.”
3 Kenaka mngeloyo anandinyamula mwa Mzimu Woyera kupita nane ku chipululu. Kumeneko ndinaona mkazi atakhala pa chirombo chofiira chokutidwa ndi mayina a chipongwe ndipo chinali ndi mitu isanu ndi iwiri ndi nyanga khumi.
3 Anun Kakafiyin targabuw tounamatar bora’ahu nawiyu ana arar yan atit. Nati’imaim sawaidab biyan woun ukwarin seven naatu ana rarag ten afe’enamaim babin ma’am aitin, naatu sawaidab biyan tutufin etei baigigimen tur God isan hikirumen hi’inu’in aitan.
4 Mkaziyo anavala zovala za pepo ndi zofiira nadzikongoletsa ndi golide, miyala yapamwamba ndi ngale. Ananyamula chikho chagolide mʼdzanja lake, chodzaza ndi zinthu zonyansa ndi fungo loyipa la zigololo zake.
4 Babin ana faifuw i namar naatu woun anababatun ius, naatu biyanamaim i gold, ton wakek, sar, kwameton rira’ara’ah, naatu umanamaim i ana sinaf kakafih yumatah ta ta kerowas gold amaim hiwan awan karatan,
5 Pa mphumi pake panalembedwa dzina lodabwitsa:
5 nakwetanamaim i tur buriburin hikirum,
6 Ndinaona kuti mkaziyo anali ataledzera ndi magazi a oyera mtima, magazi a amene anachitira umboni Yesu.
6 Naatu babin God ana sabuw hai rara tom naatu sabuw Jesu ana tur hio’orereb hai rara tom bikoko’aw aitin, iti babin ai’itin ana veya’amaim ayu ai fofofor men kafaita.
7 Kenaka mngelo uja anati kwa ine, “Bwanji ukudabwa? Ndikufotokozera chinsinsi cha mkaziyu ndi chinsinsi cha chirombo chimene wakwerapochi chokhala ndi mitu isanu ndi iwiri ndi nyanga khumi.
7 Imaibo tounamatar eo, “Aisim kubifofofor? Ayu boro nati babin ana buriburin, naatu nati sawaidab ukwarin seven naatu ana rarag ten babin afe’en ma ereremor ana buriburih ana kubuna inanowar.
8 Chirombo chimene wachionachi chinalipo kale koma tsopano kulibe ndipo chidzatuluka ku chidzenje chakuya ndi kupita kukawonongedwa. Anthu okhala pa dziko lapansi amene mayina awo sanalembedwe mʼbuku lamoyo kuyambira pa kulengedwa kwa dziko lapansi adzadabwa pamene adzaona chirombocho, chifukwa chinalipo kale, tsopano kulibe, komabe chidzabwera.
8 Nati sawaidab i mat ma’am baise boun i men ema’am. Baise boro’omo murubih hai efan wanu’uminane nayen hinagurus. Sabuw tafaramamaim tema’am wabih tafaram matara’e ana veya, wanatowan ana bukamaim men hikikirum boro hinifofofor sawaidab hina’itin ana veya. Anayabin i marasika ma, boun i en baise boro nan.
9 “Zimenezi zikufunika kuganizira mwanzeru. Mitu isanu ndi iwiriyo ndi mapiri asanu ndi awiri pomwe mkazi uja amakhalirapo. Yomweyonso ndi mafumu asanu ndi awiri.
9 “Ukwar narerekab naatu tur iti naniyan kwanab gewas. Sawaidab ukwarin seven i oyaw seven babin afe’en ema’am ana itinin.
10 Mafumu asanu anagwa, imodzi ilipo ndipo ina sinabwere; koma pamene idzafika, idzayenera kukhala kwa kanthawi kochepa.
10 Naatu aiwob seven auman hai itinin. Five i himorob hire, ta’imon boun ebi’aiwob, naatu ta i boro enan, naatu i nanan ana veya i boro mar kafai ni’aiwob.
11 Chirombo chomwe chinalipo kale ndipo tsopano kulibe ndiyo mfumu yachisanu ndi chitatu. Iyo ndi ya mʼgulu la asanu ndi awiriwo ndipo ikupita kukawonongedwa.
11 Sawaidab marasika ma’am momorob i aiwob bai eight. Nati aiwob i iti aiwob seven ana kofan turin, naatu i auman enan gurugurusen wanawanan narunamih.
12 “Nyanga khumi unaziona zija ndi mafumu khumi amene sanapatsidwe ulamuliro, koma adzapatsidwa ulamuliro pamodzi ndi chirombo kwa ora limodzi.
12 Rarag etei ten i’itah i aiwob etei ten, tafaram bow bai aiwob isan ana fair i men ta hibai, baise mar kafai hour ta’imon ana fofonin boro aiwob rubabaruwin ana fair hinab sawaidab bairi hini’aiwob.
13 Mafumuwo ali ndi cholinga chimodzi ndipo adzapereka mphamvu ndi ulamuliro wawo kwa chirombocho.
13 Aiwob etei ten hai not i ta’imon naatu hai fair hai roubabaruwen etei boro sawaidab hinitin ni’aiwob.
14 Iwo adzachita nkhondo ndi Mwana Wankhosa, koma Mwana Wankhosayo adzawagonjetsa chifukwa Iye ndi Mbuye wa ambuye ndi Mfumu ya mafumu, ndipo amene adzakhala ndi Iye ndi oyitanidwa ake, osankhidwa ndi otsatira ake okhulupirika.”
14 Lamb bairi boro hinibabarfoten hiniyow, baise Lamb boro ana’afa’af sabuw, ana rourubinen sabuw naatu ana sabuw iyab hibosunusunub hibi’ufunun boro bairi hinabat hinarouw hinisbunih, anayabin i regaregah etei hai Regah, naatu aiwob etei hai Aiwob.”
15 Kenaka mngeloyo anati kwa ine, “Madzi amene unawaona pamene mkazi wadamayo anakhalapo ndiwo anthu ochuluka, mitundu ndi ziyankhulo.
15 Imaibo Tounamatar iti na’atube iuwu, “Harew nati babin baiwa’an kwanekwaneyan tafah ma i’i’itin, i sabuw biyah ta ta, kou’ay ta ta, tafaram ta ta, naatu tur ta ta.
16 Nyanga khumi ndi chirombo unazionazo zidzadya mkazi wadamayo. Zidzamufwifwitsa ndi kumusiya wamaliseche; zidzadya nyama yake ndi kumutentha ndi moto.
16 Sawaidab naatu rarag etei ten i’i’itih boro babin baiwa’an kwanekwaneyan hinifa’ifa’i, biyanamaim sawar etei boro hinabosaisiren segar hinihamiy nabat, biyan boro hina’aan naatu wairafamaim boro hina’afun biyan hinagurus.
17 Pakuti Mulungu wayika ichi mʼmitima mwawo kuti akwaniritse cholinga chake povomerezana kupereka mphamvu zawo zolamulira kwa chirombo, kufikira Mawu a Mulungu atakwaniritsidwa.
17 Anayabin God iti sawar i dogorohimaim yari’iy ana kok abisa eo hinasinaf hinisawar, etei boro hinibasit sawaidab hai fair hinitin nabonawiyih nanan God ana tur nan niturobe.
18 Mkazi unamuonayo ndi mzinda waukulu umene ulamulira mafumu a dziko lapansi.”
18 ‘Babin nati i’i’itin i bar merar gagamin, i tafaram wanawanan hai aiwob etei ebobonawiyih.”
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Apocalipse 17, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.