Apocalipse 16

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs MNT

Sair da comparação
MNT Minaifia NT
1 Kenaka ndinamva mawu ofuwula kuchokera ku Nyumba ya Mulungu ija kuwuza angelo asanu ndi awiri kuti, “Pitani, katsanulireni pa dziko lapansi ukali wa Mulungu umene uli mʼmbale zisanu ndi ziwirizi!”
1 Imaibo ayu Tafaror Barene fanan gagamin ta tounamatar nah etei seven isah eo anowar. “Kwan God ana yaso’ar tew seven wanawanah tema’am tafaram tafanamaim kwaisuwa’en tera’iy”.
2 Mngelo woyamba anapita natsanula mbale yake pa dziko lapansi ndipo zilonda zoyipa ndi zowawa zinabuka pa anthu amene anali ndi chizindikiro cha chirombo chija, napembedza fano lake.
2 Tounamatar wan batabat tit ana tew isuwai me yan ra’iy. Feher yumatah kakafih naatu babanih kakafih anababatun, sabuw iyabowat sawaidab ana ewow hibai hima’am naatu sawaidab ana yumatabe hikwakwafir biyahimaim matar.
3 Mngelo wachiwiri anapita natsanula mbale yake pa nyanja ndipo madzi ake anasanduka magazi, magazi ake ngati a munthu wakufa. Chamoyo chilichonse cha mʼnyanjamo chinafa.
3 Imaibo tounamatar bairou’abin ana tew e’abar suwai riy yan ra’iy, matan botabir orot babin murubin ana rara’abe matar, naatu riy wanawanan siy yawayawasih etei himumurub.
4 Mngelo wachitatu anapita natsanula mbale yake pa mitsinje ndi akasupe amadzi ndipo zinasanduka magazi.
4 Ibanak maiye tounamatar baitounin ana tew harew gagamih yahimaim isuwai ra’iy naatu harew sosoh yahimaim auman isuwai ra’iy, harew etei matah botabir rara himatar.
5 Kenaka ndinamva mngelo wolamulira madzi uja akuti,
5 Naatu tounamatar harew ana ukwarin eo anowar,
6 pakuti iwo anakhetsa magazi a oyera anu ndi aneneri anu,
6 — ausente —
7 Kenaka ndinamva mawu ochokera ku guwa lansembe akuti,
7 Imaibo ayu fanan ta sibor ana gemane titit anowar,
8 Mngelo wachinayi anapita natsanula mbale yake pa dzuwa ndipo dzuwa linapatsidwa mphamvu yopsereza anthu ndi moto.
8 Naatu tounamatar baikwafe’enin ana tew bai veya matanamaim isuwai re, sabuw a’arahih isan ana fair bai ana fora’abin ra’at.
9 Anapserera nako kutentha kwakukuluko ndipo anatukwana Mulungu, amene anali ndi ulamuliro pa miliri imeneyi, koma anakana kulapa ndi kumulemekeza.
9 Veya wabuburin eafun tututurih biyah hikakoumih, naatu God iti feher kakafih ana fair bai ma sisinaf isan tur kakafih hio wabin hi’a’afiy. Naatu men hikokok boro dogor baikitabir hitab, God ana gagamin isan hitabora’ara’ah.
10 Mngelo wachisanu anapita natsanula mbale yake pa mpando waufumu wa chirombo chija ndipo mdima unagwa ponse pamene panali ufumu wake. Anthu analuma malilime awo chifukwa cha ululu.
10 Tounamatar bai five ana tew eabar suwai sawaidab ana urama’ama tafan ra’iy. Gugumin kakafin sawaidab ana aiwob etei tarsumih naatu sabuw menah hiboyobayob anayabin biyababan gagamin maiyow hibai.
11 Ndipo anatukwana Mulungu wakumwamba chifukwa cha maululu awo ndi zilonda zawo koma anakana kulapa pa zimene anachita.
11 Tur kakafih mar ana God isan hio, anayabin biyah hai babanih naatu feher hai babanih i hira’at kwanekwan. Baise sinaf kakafih i men hihamiyen.
12 Mngelo wachisanu ndi chimodzi anapita natsanula mbale yake pa mtsinje waukulu wa Yufurate, ndipo madzi ake anaphwa kuti pakhale njira yodzera mafumu ochokera kummawa.
12 Iban maiye tounamatar bai six ana tew eabar suwai Euphrates harew gagamin yan ra’iy, harew eosasa ef imatar aiwob veya yeninane isah.
13 Kenaka ndinaona mizimu yoyipa itatu imene inkaoneka ngati achule; inatuluka mʼkamwa mwa chinjoka chija, mʼkamwa mwa chirombo chija ndi mʼkamwa mwa mneneri wonyenga uja.
13 Imaibo afiy katokato’iy tounu takwey hai itininabe, farubarubar awanane, sawaidab awanane naatu dinab baifufuwenayan awahine hititit aitan.
14 Imeneyi ndiyo mizimu ya ziwanda imene imachita zizindikiro zodabwitsa ndipo imatuluka kupita kwa mafumu a dziko lonse, kukawasonkhanitsa ku nkhondo ya pa tsiku lalikulu la Mulungu Wamphamvuzonse.
14 Iti i demon ana afiy ina’inan sinafuyah, iti afiy tounu i titit ten tafaram tutufin wanawanan aiwob etei tiru’ayuwih God fairin maiyow ana veya gagaminamaim baiyow isan.
15 “Taonani, ndikubwera ngati mbala! Wodala munthu amene ali maso, nasunga zovala zake, kuti asayende maliseche kuti angaonetse maliseche ake.”
15 “Kwananowar ayu i bainowanabe anan. Orot yait matan to iwa’an ana waifuw ius ema’am i boro niyasisir, naatu boro men segar sabuw nahimaim erebiya’ohow nabat naremoramih.”
16 Kenaka mizimu ija inasonkhanitsa pamodzi mafumu ku malo amene mʼChihebri amatchedwa Armagedo.
16 Imaibo wagabur kakafih aiwob etei hiru’ayuwih hina efan wabin Armageddon, Hebrew turamaim hibiwab Armageddon imaim hitit.
17 Mngelo wachisanu ndi chiwiri anatsanulira mbale yake mu mlengalenga ndipo ku Nyumba ya Mulungu kunamveka mawu ofuwula kuchokera ku mpando waufumu kuti, “Kwatha!”
17 Imaibo tounamatar bai seven ana tew waruw wanawananamaim isuwai ra’iy, fanan gagamin Tafaror Bar wanawanan urama’ama’ane tit eo, “Iti i i’asa’ub sawar.”
18 Kenaka kunachitika mphenzi, phokoso, mabingu ndi chivomerezi choopsa. Chivomerezi ngati ichi sichinachitikepo chikhalire cha munthu pa dziko lapansi. Chinali chivomerezi choopsa kwambiri.
18 Nati’imaim namanamar bokiyakiyat, farafarar kakafin rab bitenkwarikwarir naatu iriyoy i men matar orot babin hi’itin na’atube mataramih, iriyoy iti i kakafin anababatun.
19 Mzinda waukuluwo unagawika magawo atatu ndipo mizinda ya mitundu ya anthu inagwa. Mulungu anakumbukira Babuloni Wamkulu namupatsa chikho chake chodzaza ndi vinyo wa ukali wa mkwiyo wake.
19 Bar merar gagamin i tarasib tounu himatar, naatu bar merar etei tafaram wanawananamaim hima’am etei gurusih. God Babilon gagamin isan not, naatu ana kerowasamaim wine Babilon itin tom, iti wine i God ana yaso’ar.
20 Chilumba chilichonse chinathawa ndipo mapiri sanaonekenso.
20 Nuw etei’imak hikasiy naatu oyaw etei na’am hin sawar.
21 Matalala akuluakulu olemera pafupifupi makilogalamu makumi asanu anagwa kuchokera kumwamba kugwera pa anthu. Ndipo anthu anatukwana Mulungu chifukwa cha mliri wa matalala popeza unali mliri woopsa kwambiri.
21 Taun kabay gagamih hai bit anafofonin 50 kilos na’atube, marane tounabe ihururuw orot babin tafahimaim hira’iy, naatu sabuw God hio bayubayuw, anayabin kabay gagamih tounabe yar re, iti gurugurusen i kakafin anababatun.

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Apocalipse 16, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.