Apocalipse 15

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI

Sair da comparação
AAI TUR GEWASIN O BAIBASIT BOUBUN
1 Kumwamba ndinaona chizindikiro china chachikulu ndi chodabwitsa: angelo asanu ndi awiri ali ndi miliri isanu ndi iwiri yomaliza chifukwa Mulungu anakwiya kotheratu.
1 Naatu mar wanawanan kirikirifot ta gagamin naatu gewasin na’in ai’itin i oro’oror. Tounamatar etei seven umahimaim i sawow kakafih yumatah ta ta. Iti sawow kakafih i yomanin ana sawow, anayabin nati’imaim God ana yaso’ar etei boro nasinaf na’asa’ub.
2 Ndipo ndinaona chimene chinaoneka ngati nyanja yonyezimira yosakaniza ndi moto, ndipo pambali pa nyanjayo panayima amene anagonjetsa chirombo chija ndi fano lake, ndi nambala yotanthauza dzina lake. Anthuwo ananyamula azeze amene Mulungu anawapatsa.
2 Naatu ayu riy yan ana itinin kiyamabe wairaf auman hisartabir titit aitin. Naatu riy sisibinamaim sabuw iyab sawaidab, naatu sawaidab ana yumatabe, naatu sawaidab wabin ana ewow auman hibisnowah, i riy yan kiyamabe sisibinamaim umah God ana douduf bitih auman hibatabat aitih.
3 Iwo ankayimba nyimbo ya Mose, mtumiki wa Mulungu, ndi nyimbo ya Mwana Wankhosa. Nyimbo yake inkati,
3 Naatu God ana akir wairafin Moses ana ew hitabor naatu Lamb auman ana ew hitabor,
4 Inu Ambuye, ndani angapande kukuopani,
4 Regah, sabuw etei boro o hinabiruw hinakakafiyi?
5 Zitatha izi, ndinaona kumwamba Nyumba ya Mulungu imene ndi Tenti ya Umboni, atatsekula.
5 Iti Ufunamaim ayu anuwanuw maramaim Tafaror Bar ana etawan botawiy naatu Obaibasit Ana Sis batabat aitin.
6 Mʼnyumbamo munatuluka angelo asanu ndi awiri ndi miliri isanu ndi iwiri. Angelowo anavala nsalu zoyera bwino zonyezimira ndi malamba agolide pa zifuwa zawo.
6 Tounamatar seven umahimaim sawow kakafih hibotanen Tafaror Barene hititit aitih. Hai faifuw boubuh gewasih anababatun hi’osen, dogorohimaim gerogeror gold hiyon auman.
7 Ndipo kenaka chimodzi cha zamoyo zinayi zija chinapereka kwa angelo asanu ndi awiri mbale zisanu ndi ziwiri zodzaza ndi ukali wa Mulungu amene ali ndi moyo mpaka muyaya.
7 Imaibo sawar yawasih ma’anih kwafe’en wanawanahimaim ta tew, gold etei seven God ana yaso’ar awan hikartanen hibatabat bow tounamatar seven itih. Nati God i wanatowan, wanatowan ma’ama’anin.
8 Ndipo Nyumba ya Mulungu inadzaza ndi utsi wochokera ku ulemerero wa Mulungu ndi ku mphamvu zake, ndipo panalibe yemwe akanalowa mʼNyumbayo mpaka miliri isanu ndi iwiri ya angelo asanu ndi awiri aja itatha.
8 God ana fair naatu ana bonamanamarin sowamaim tit Tafaror Bar wanawanan awan karatan, naatu orot babin iti Tafaror Bar boro men hinarun. I boro hinama nanan sawow kakafih yumatah ta ta etei seven, tounamatar seven hai bowabow hinabow hinan yomanin hina’asa’ubibo.

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Apocalipse 15, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.