Apocalipse 14
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Kenaka ndinaona patsogolo panga panali Mwana Wankhosa, atayimirira pa Phiri la Ziyoni, ndipo Iye anali pamodzi ndi anthu 144,000 amene pa mphumi pawo panalembedwa dzina la Mwana Wankhosayo ndi la Atate ake.
1 Imaibo ayu anuwanuw nou’umaim oyaw Zion tafan Lamb batabat aitin, ana sabuw etei 144, 000 bairi. Naatu nati sabuw nakwetahimaim i Lamb wabin naatu Tamah wabin auman hikirumen.
2 Ndipo ndinamva liwu lochokera kumwamba ngati mkokomo wa madzi ambiri, ndiponso ngati kugunda kwamphamvu kwa bingu. Liwu limene ndinamvalo linali ngati a anthu akuyimba azeze awo.
2 Naatu maramaim nidun ta anonowar i harew tititit niduhibe, naatu gunum erab gugugug ebiwa’an na’atube. Niduw anonowar i taboroyah hai douduf terabirabibe.
3 Anthuwo ankayimba nyimbo yatsopano patsogolo pa mpando waufumu ndi zamoyo zinayi zija ndi akuluakulu aja. Palibe ndi mmodzi yemwe amene anatha kuphunzira nyimboyo kupatula anthu 144,000 aja amene anawomboledwa pa dziko lapansi.
3 Naatu urama’ama, sawar kwafe’en yawasih ma’anih naatu regaregah ai’in nahimaim hibat ew boubun hitabor, iti ew i boro men yait ta hini’obaiyih hinaso’ob, baise tafaram ana sabuw etei wanawanahimaim 144,000 hitutubunih akisihimo iti ew hiso’ob.
4 Awa ndiwo amene sanadzidetse koma anadzisunga ndipo sanadziyipitse ndi akazi. Anthu amenewa ndiwo ankatsatira Mwana Wankhosa kulikonse kumene ankapita. Ndiwo amene anagulidwa pakati pa anthu a dziko lapansi kuti akhale oyambirira kuperekedwa kwa Mulungu ndi kwa Mwana Wankhosa.
4 Iti oro’orot i biyah hikaif gewas uhew hima, men kafa’imo baibin bairi hi’in biyah gubagub mataramih. Mar etei Lamb menamaim inan i hibi’ufunun. Orot babin etei wanawanahimaim i akisihimo hitubunih, ai ro’oh wan tiyamur tafafayay na’atube, God ana Lamb hairi hai fayay na’atube hitih.
5 Iwo sananenepo bodza ndipo alibe cholakwa.
5 Men kafa’imo baifuwen ta awahimaim hitita’urihimih aurih ubar, en.
6 Kenaka ndinaona mngelo wina akuwuluka mu mlengalenga ndipo anali ndi Uthenga Wabwino wamuyaya woti akalalikire kwa anthu okhala pa dziko lapansi, kwa a mtundu uliwonse, a fuko lililonse, a chiyankhulo chilichonse ndi kwa anthu onse.
6 Naatu anuwanuw tounamatar ta auyom waruw wanawanan roberob aitin, wanatowan ana tur gewasin bai tafaramamaim sabuw, tafaram ta ta, big ta ta, tur ta ta naatu biyah ta ta, isah orerebamih.
7 Mngeloyo anayankhula mokweza mawu kuti, “Wopani Mulungu ndi kumutamanda, chifukwa nthawi yoweruza anthu yafika. Mumupembedze Iye amene analenga thambo, dziko lapansi, nyanja ndi akasupe amadzi.”
7 Fanan aumetawat na’in eo, “God kwanabiruw naatu kwanakakafiy! Ana gagamin kwanao kwanabora’ara’ah, anayabin baibabatiyen ana veya natit. God, mar, tafaram, riy, naatu harew ana sinafenayan kwanakwafir.”
8 Mngelo wachiwiri anatsatana naye ndipo anati, “Wagwa! Wagwa Babuloni womveka uja, amene anachititsa anthu a mitundu yonse kumwa vinyo wa zilakolako zake zachigololo.”
8 Tounamatar bairou’abin i’ufunun tit eo, “Babilon ra’iyeka! Babilon bar merar gagamin i ra’iyeka, anayabin tafaram wanawanan sabuw baiwa’an kwanekwan ana wine babin faramih etei hitom!”
9 Mngelo wachitatu anatsatana nawo ndi mawu ofuwula anati, “Ngati wina apembedza chirombo chija ndi fano lake ndi kulembedwa chizindikiro pa mphumi kapena pa dzanja,
9 Tounamatar baitounin i’ufunun tit fanan aumetawat na’in eo, “Orot yait sawaidab nakwafir naatu i ana itininabe auman nakwafir, ana ewow nibasit nab ukwarin o umanamaim na’uh nama’am,
10 nayenso adzamwa vinyo waukali wa Mulungu, umene wathiridwa popanda kuchepetsa mphamvu zake mʼchikho cha ukali wa Mulungu. Munthuyo adzazunzidwa ndi moto wamiyala yasulufure pamaso pa angelo oyera ndi pa Mwana Wankhosa.
10 i boro God ana yaso’ar wine natom. Nati wine i ana fairin tutufin etei yaso’ar kerowasamaim isuwei’ika ebatabat! O boro sulfur wanawanan inarun na’arah na’arfufuri biyababan gagamin maiyow tounamatar kakafiyih naatu Lamb bairi nahimaim inab.
11 Ndipo utsi wa moto wowazunzawo udzakwera kumwamba mpaka muyaya. Sikudzakhala kupumula usana ndi usiku kwa amene anapembedza chirombo chija ndi fano lake kapena kwa aliyense amene analembedwa chizindikiro cha dzina lake lija.”
11 Naatu fai mar biyababan bai’akir ana sow boro wanatowan, wanatowan na’in nayen, auyit o gugumin biyah tubaiwa’an isan ana veya men ta ema’am. Sawaidab ana kwafirenayah, naatu i ana yumatabe kwafirenayah na’atube sabuw iyab hibasit wabin ana ewow hibaib iti biyababan boro fai mar hinab.”
12 Pamenepa ndi pofunika kupirira kwa anthu oyera mtima amene amasunga malamulo a Mulungu ndi kukhalabe okhulupirika kwa Yesu.
12 God ana sabuw iti tur i kwanab, yatenanub nawainabi God ana obaiyunen tur kwanabukikin Jesu isan kwanabosunusunub.
13 Kenaka ndinamva mawu kuchokera kumwamba akuti, “Lemba kuti, Odala anthu amene akufa ali mwa Ambuye kuyambira tsopano mpaka mʼtsogolo.”
13 Imaibo maramaim fanan ta eo anowar, “Iti kukirum: sabuw iyab Regah wabinamaim himomorob boun ana veya ebubusuruf boro baigegewasin hinab.”
14 Ndinayangʼana patsogolo panga ndinaona mtambo woyera patakhalapo wina ngati Mwana wa Munthu, kumutu atavala chipewa chaufumu chagolide ndipo mʼdzanja mwake munali chikwakwa chakunthwa.
14 Imaibo anuw naatu nou’umaim wakasakas kwes aitin, tafanamaim Orot Natun ana itininabe, ukwarinamaim kowas gold naatu umanamaim i fafour ana kaifut auman.
15 Tsono mngelo wina anatuluka mʼNyumba ya Mulungu nafuwula mwamphamvu kwa uja wokhala pa mtamboyu. Mngeloyo anati, “Tenga chikwakwa chako ndipo kolola, pakuti nthawi yokolola ya dziko la pansi yakwana”
15 Naatu tounamatar ta Tafaror Barene tit orot nati wakasakas tafan ma’am isan fanan aumetawat na’in e’af, “A Kaifut kubai naatu masaw kufour, anayabin fourin ana veya i natit, tafaram i iyamur fourinamih.” Fafour ana kaiy|alt="sickle" src="cn02109B.tif" size="col" loc="Rev 14.15-19" copy="©1978 David C. Cook Publishing Co." ref="14.15-19"
16 Choncho wokhala pa mtambo uja anayamba kukolola dzinthu pa dziko lapansi ndi chikwakwa chakecho.
16 Naatu orot nati wakasakas tafan ma’am ana kaifut tafaram tafanamaim i’asakan naatu tafaram tutufin etei four.
17 Mngelo wina anatuluka mʼNyumba ya Mulungu kumwamba ndipo nayenso anali ndi chikwakwa chakunthwa.
17 Tounamatar tabo maramaim Tafaror Barene titit aitin, umanamaim i ana kaifut wan so’arin auman.
18 Kenaka mngelo winanso amene amalamulira moto, anatuluka kuchokera ku guwa lansembe nayitana mwamphamvu mngelo uja amene anali ndi chikwakwa chakunthwa chija, nati, “Tenga chikwakwa chako chakunthwacho yamba kudula mphesa za mʼmunda wamphesa wa pa dziko lapansi, pakuti mphesa zapsa kale.”
18 Iban maiye tounamatar ta wairaf ana kaifayan sibor ana gemane tit, naatu fanan aumetawat na’in e’af tounamatar uman ana kaifut wan so’arin bai batabat isan eo, “A kaifut wan so’arin kubai tafaram ana masaw yan grape umah ku’afuwen kwita’ay, anayabin grape i hiwu.”
19 Pamenepo mngeloyo anayambadi kugwiritsa ntchito chikwakwa chake nadula mphesa za dziko lapansi, naziponya mʼchopondera mphesa chachikulu cha ukali woopsa wa Mulungu.
19 Tounamatar ana kaifut kamar tafanamaim iasakan grape ro’oro’oh e’afuw hira’iy bow ta’asiyen God ana yaso’ar wine bunubunuw wanawanan hira’iy.
20 Mphesazo zinapondedwa mʼchopondera mphesa kunja kwa mzinda. Mʼchopondera mphesamo munatuluka magazi amene anayenderera ngati mtsinje, kuzama kwake mita ndi theka ndipo kutalika kwake makilomita 300.
20 Naatu wine ana bunubunuw bar merar gagamin ufunane hibun fesafesaren, rara wine ana bunubunuwane titit i harew titit na’atube re nunuw in 300 kilometres na’atube naatu ana taiy i sika kabokabom ana fofonin o kafa’imo 2 metres bai.
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Apocalipse 14, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.