Apocalipse 13
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Ndipo ndinaona chirombo chikutuluka mʼnyanja. Chinali ndi nyanga khumi ndi mitu isanu ndi iwiri. Pa nyanga iliyonse chinavala chipewa chaufumu, ndipo pa mutu uliwonse panali dzina lonyoza Mulungu.
1 Naatu sawaidab riyanane yey aitin, ukwarin etei seven naatu ana rarag etei ten, rarag tafahimaim kowas etei ten yara’aten, naatu ukwarin ta’ita’imon kowas tafahimaim wab kakafih maiyow, baigigimen tur God isan hio hikirumen.
2 Chirombo chimene ndinachionacho chinali ngati kambuku, mapazi ake ngati chimbalangondo, kukamwa kwake ngati kwa mkango. Chinjoka chija chinapatsa chirombocho mphamvu zake, mpando wake waufumu ndiponso ulamuliro waukulu.
2 Sawaidab ana itinin i tiger ana yumatabe, baise an i bear an, naatu awan i lion awan. Farubarubar ana fair, ana urama’ama naatu ana roubabaruwen fair etei sawaidab itin.
3 Umodzi wa mitu wa chirombocho unkaoneka ngati uli ndi bala losati nʼkupola, koma nʼkuti balalo litapola. Dziko lonse linadabwa ndipo linatsatira chirombocho.
3 Naatu iti sawaidab ukwarin ta hirab taseb gawud matar, baise na kafuw maiye, tafaram wanawanan sabuw etei iti ina’inan matar hinonowar hifofofor men kafaita naatu sawaidab hi’ufunun.
4 Anthu anapembedza chinjoka chija chifukwa chinapereka ulamuliro wake kwa chirombocho. Nachonso chirombo chija anachipembedza nʼkumafunsa kuti, “Ndani angafanane ndi chirombochi? Ndani angachite nacho nkhondo?”
4 Orot etei farubarubar hikwafir anayabin roubabaruwen ana fair etei sawaidab itin, naatu sawaidab auman hikwafir hio, “Yait i sawaidababe? Yait boro nibabarafut hairi hiniyow?”
5 Chirombo chija chinaloledwa kuyankhula mawu onyada ndi achipongwe kwa Mulungu. Chinapatsidwa mphamvu zolamulira pa miyezi 42.
5 God ma itinimo sawaidab misir ora’ara’at tur naatu baigigimen gagamin maiyow God igigim naatu roubabaruwen ana fair itin sumar 42 wanawanan sabuw bonawiyih.
6 Ndipo chinayamba kuyankhula mawu achipongwe onyoza Mulungu, dzina lake, malo okhalamo ndi onse amene amakhala kumwamba.
6 Nati ana veya’amaim awan kerer baigigim gagamin maiyow God iu igigim. Wabin auman igigim na’atube ana ma’ama efan naatu sabuw iyab maramaim hima’am auman iuwih igigimih.
7 Chinaloledwa kuchita nkhondo ndi oyera mtima ndi kuwagonjetsa. Ndipo chinapatsidwanso mphamvu zolamulira anthu a fuko lililonse, mtundu uliwonse ndi chiyankhulo chilichonse.
7 Naatu God iban fair sawaidab itin God ana sabuw rouw wastatanen isan. Naatu roubabaruwen ana fair itin big ta ta, biyah ta ta, tur ta ta, tafaram ta ta wanawananamaim bonawiyih isan.
8 Anthu onse okhala pa dziko lapansi adzapembedza chirombocho, aliyense amene chilengedwere cha dziko lapansi dzina lake silinalembedwe mʼbuku la amoyo la Mwana Wankhosa anaphedwa uja.
8 Sabuw tafaram wanawanan etei boro sawaidab hinakwafir, baise sabuw iyab tafaram matara’e ana veya wabih wanatowan ana bukamaim hikikirum boro men hinakwahir, nati buk i Lamb marasika hi’a’asabun nowan.
9 Iye amene ali ndi makutu, amve.
9 “Imih o yait tain nama’am na’at inanowar gewas.
10 “Woyenera kupita ku ukapolo,
10 Yait dibur yara’iyinamih ema’am boro hinayara’iy, yait kaiyomaim yinamih ema’am boro hinay namorob. Imih God ana sabuw kakafiyih iti afa’af hibaib i yateh nanub bosunusunubamaim nawainabih.”
11 Kenaka ndinaona chirombo china chikutuluka mʼnthaka. Chinali ndi nyanga ziwiri ngati mwana wankhosa koma kuyankhula kwake ngati chinjoka.
11 Imaibo sawaidab tabo me wanawanan taseb yey aitin, ana rarag rou’ab Lamb ana rarag na’atube, baise ana tur eo i farubarubar eo’obe.
12 Chinalamulira ndi mphamvu zonse za chirombo choyamba chija, ndipo chinachititsa kuti dziko lapansi ndi anthu okhalamo alambire chirombo choyamba chija, chimene bala lake losati nʼkupola linali litapola.
12 Naatu sawaidab wantoro’ot ana obababaruwen fair hibitin etei i iti sawaidab me’ene yey i ia’ait, naatu tafaram tutufin etei na’atube sabuw tutufin etei eo kikinih sawaidab wan hirab ana fit kakafuw i hikwafir.
13 Ndipo chinachita zizindikiro zazikulu zodabwitsa, mpaka kumagwetsa moto pa dziko lapansi kuchokera kumwamba anthu akuona.
13 Sawaidab bairou’abin ina’inan gagamih sinaf naatu ina’inan afa fokarih men tasisinaf i sinafen, naatu eo wairaf marane ra’iy sabuw etei matah yan hi’itin.
14 Chifukwa cha zizindikiro zimene chinaloledwa kuchita mʼmalo mwa chirombo choyamba chija, chimene bala lake linapola, chinanyenga anthu okhala pa dziko lapansi. Chinalamula anthu kuti apange fano mopereka ulemu kwa chirombo chimene chinavulazidwa ndi lupanga, koma nʼkukhalabe ndi moyo.
14 Ina’inan sisinafumaim, fair hitin tafaram ana sabuw moumurih na’in ifufuwih bow sawaidab wan nan isan, naatu sabuw iuwih sawaidab wan na hirab morob yawas maiye ana feher kakafuw ana yumatabe hitar.
15 Chirombo cha chiwirichi chinapatsidwa mphamvu zakupereka mpweya kwa fano la chirombo choyamba chija kuti liyankhule ndi kuphetsa aliyense wokana kupembedza fanolo.
15 Fair hitin sawaidab wan nan ana yumatabe ai’imaim hitar ara’ar tainen ana waruw itin, saise tamisir tur tao, naatu sabuw iyab i ana yumatabe ai’imaim hitaritar men hikwakwafir tarouw hitamorob.
16 Chinakakamiza aliyense, wamngʼono, wamkulu, wolemera, wosauka, mfulu ndi kapolo kuti alembedwe chizindikiro pa dzanja lamanja kapena pa mphumi.
16 Naatu sabuw etei eokikinih. Sabuw gagamih, gidigidih, guguw wairafih, men guguw wairafih, roufamen sabuw, akir sabuw, etei umah asukwafune o ukwarihimaim ana ewow baitih isan eo,
17 Chinkachita zimenezi kuti wina aliyense asaloledwe kugula kapena kugulitsa kanthu ngati alibe chizindikiro chimenechi, chimene ndi dzina la chirombocho kapena nambala yotanthauza dzina lake.
17 saise orot babin yait sawar etotobon o sawar yataiten tetotobon i sawaidab ana ewow nabaibo, nati ewow i wabin o ana number.
18 Pano pafunika nzeru. Munthu amene ali ndi nzeru atanthauze nambala ya chirombocho, pakuti nambalayo ikutanthauza munthu. Nambala yake ndi 666.
18 O yait ukwar rerekab isa nama’am boro sawaidab ana number iniyab yabin inaso’ob. Anayabin iti i orot wabin, naatu ana number i 666.
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Apocalipse 13, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.