Apocalipse 10

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI

Sair da comparação
AAI TUR GEWASIN O BAIBASIT BOUBUN
1 Kenaka ndinaona mngelo wina wamphamvu akutsika kuchokera kumwamba. Anavala mtambo ndipo anali ndi utawaleza pamutu pake. Nkhope yake inali ngati dzuwa, ndipo miyendo yake inali ngati mizati yamoto.
1 Imaibo ayu tounamatar ta fairin marane tit sakuk wanawanan earmetan auman re nan aitin. Ukwarinamaim ana kaniy rouw naatu an ana itinin wairaf na’atube matan yafuyafun auman, ana yumat i veya na’atube rarasib.
2 Mʼdzanja lake munali kabuku kakangʼono kotsekulidwa. Phazi lake lamanja linaponda mʼnyanja ndipo phazi lake lamanzere linaponda pa mtunda.
2 Umanamaim fef firorow kikimin rusasar auman rena, an ana’asukwafune riy yan bat naatu an ana beyawane me yan bat,
3 Mngeloyo anafuwula kwambiri ngati kubangula kwa mkango. Atangofuwula, kunamveka kugunda kwa mabingu asanu ndi awiri.
3 fanan aumetawat na’in e’afa’af ananowarin i lion egagaran na’atube, eafa’af ufunamaim, gunum etei seven gugugug hiwa’an hiya’afut.
4 Mabingu asanu ndi awiriwo atangogunda, ine ndinkati ndizilemba; koma ndinamva mawu kuchokera kumwamba kuti, “Zisunge mu mtima zimene mabingu asanu ndi awiriwo anena ndipo usazilembe.”
4 Naatu hibiya’afut ana veya ayu ata kirumamih abubusuruf, baise marane fanan ta eo, “Abisa gunum seven hio inonowar ana wa’iwa’irin o akisimo inabotan men bukamaim inakirum!”
5 Kenaka mngelo amene ndinamuona ataponda mʼnyanja ndi ku mtunda uja, anakweza dzanja lake lamanja kumwamba.
5 Imaibo tounamatar riy yan naatu me yan bat ai’itin uman ana asukwafune au mar bora’ah.
6 Mngeloyo analumbira mʼdzina la Iye wokhala ndi moyo mpaka muyaya, amene analenga kumwamba ndi zonse zili kumeneko, dziko lapansi ndi zonse zili mʼmenemo, nyanja ndi zonse zili mʼmenemo, nati, “Pasakhalenso zochedwa tsopano!
6 Naatu orot nati wanatowan, wanatowan ema’am isan mar tafaram riy sawar etei sinafen wanawanan tema’am, Regah God wabinamaim eo baifaro eo, “Veya boro men ta au’uf tananawiyimih!
7 Koma patsala pangʼono kuti mngelo wachisanu ndi chiwiri uja awombe lipenga lake, chinsinsi cha Mulungu chidzachitika monga momwe analengezera kwa atumiki ake, aneneri.”
7 Baise tounamatar bai seven ana tour nabababin ana veya God ana kirikirifot abisa kurerereb ana dinab orot nonowar na’atube boro natit yomanin na’asa’ub.”
8 Pamenepo mawu amene ndinamva kuchokera kumwamba aja, anandiyankhulanso, anati, “Pita katenge buku lotsekulidwalo mʼdzanja la mngelo amene waponda pa nyanja ndi pa mtundayo.”
8 Imaibo fanan maramaim anonowar iban iuwu maiye eo, “Kwen buk nati tounamatar riy yan naatu me yan ebatabat umanamaim rusasar inu’in kubai.”
9 Choncho ndinapita kwa mngeloyo ndipo ndinamupempha kuti andipatse kabukuko. Iye anati, “Tenga, idya. Mʼmimba mwako kaziwawa koma mʼkamwa mwako kazizuna ngati uchi.”
9 Imih ayu ana tounamatar ai fefeyan buk kikimin baitu isan ao, iuwu eo, “Kubai naatu ku’aan, kamokam boro nitenkuyakuy baise awamaim ina’ani’an ana mumunin boro tafu’ube.”
10 Ndinatenga kabukuko mʼdzanja la mngeloyo ndipo ndinadyadi. Mʼkamwa mwanga kankazuna ngati uchi, koma nditakameza, mʼmimbamu munkawawa.
10 Tounamatar umanamaim buk firorow abai naatu aan, ani’aan ana mumunin i tafu’ube baise ani’aan ufunamaim kamoukamou itenkuyakuy.
11 Ndipo anandiwuza kuti, “Iwe uyenera kulalikiranso za mitundu yambiri ya anthu, za mayiko, ziyankhulo ndi za mafumu.”
11 Imaibo hi’uwu, “God ana tur sabuw moumurih, tafaram ta ta, tur ta ta, naatu aiwob ta ta isah ina’orereb maiye.”

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Apocalipse 10, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.