2 Tessalonicenses 2

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI

Sair da comparação
AAI TUR GEWASIN O BAIBASIT BOUBUN
1 Pa za kubweranso kwa Ambuye athu Yesu Khristu ndiponso za kusonkhana kwathu kuti tikumane naye, abale, tikukupemphani
1 Taitu, ayu au not gagamin ata Regah Jesu Keriso namatabir nan nabuwit tanan biyanamaim bairi tanabita’imon isan, i akokok anao kwananowar imaibo ana veya natit.
2 kuti musagwedezeke msanga mʼmaganizo kapena kuopsezedwa ndi uneneri, mbiri kapena kalata yokhala ngati yachokera kwa ife, yonena kuti tsiku lija la Ambuye linafika kale.
2 Nati ana veya’amaim sabuw afa boro hinatit hinao: Aki wagabur hiwani hio anowar Regah ana veya i natitaka, o dinabatur hinao, o fef tur abarayah biyahine bai na hinarouw hinao, men kwananowar a yan kwanabat kwana’oror sa’isa’ir kwanabirumih.
3 Musalole kuti wina aliyense akunamizeni mwa njira ina iliyonse. Pakuti tsikulo lisanafike, kudzakhala mpatuko waukulu kwambiri, ndipo kudzaoneka munthu woyipitsitsa uja, munthu woyenera kuwonongedwayo.
3 Men baifuwenamaim tur ta ta hinao kwa hinifufuwimih. Anayabin ma kakaf, fanasair, tenagogor i boro wan nabusuruf na’in nanan wanawananamaim, orot kakafin God ana rakit wairafin nan natit nirerereb. Iti orot sawar kakafih etei nabisawaren ufunamaim God ana baimakiy i boro nab.
4 Iyeyo adzatsutsa ndi kudziyika pamwamba pa chilichonse chimene anthu amachitcha mulungu kapena amachipembedza. Iyeyo adzadzikhazika mʼNyumba ya Mulungu ndi kudzitcha Mulungu.
4 Baise wan i boro sabuw hai god tafah hitumatum hima tekwakwafirih etei boro ni’ibih, nabow haw nayara’iyen naatu God ana Tafaror Bar wanawanan narun namare taiyuwin god narouw nao.
5 Kodi simukukumbukira kuti pamene ndinali nanu pamodzi ndinkakuwuzani zimenezi?
5 Bairit tama’am ana veya iti sawar isah ao kwanotanot?
6 Ndipo tsopano mukudziwa chimene chikumuletsa kuonekera, koma adzawululika pa nthawi yake yoyenera.
6 Naatu boun i kwa kwaso’ob abisa ana ef efutifut, saise ana veya anababatun nan natit imaibo Orot Kakafin nirerereb.
7 Pakuti mphamvu yobisika yoyipitsitsa ikugwira ntchito ngakhale tsopano; koma amene akutchinga mphamvuyo adzapitiriza kutero mpaka pamene wotchingayo adzachotsedwe.
7 Anayabin Orot Kakafin God ana rakit i wa’iwa’iramaim busurufika ebowabow. Baise orot yait ef efutifut i boro’ika nabat nanan, God nati orot nabobosa’ir
8 Ndipo kenaka woyipitsitsayo adzaonekera, amene Ambuye Yesu adzamugonjetsa ndi mpweya otuluka mʼkamwa mwake ndi kumuwononga ndi ulemerero wa kubwera kwake.
8 imaibo Orot Kakafin boro natit nirerereb, naatu ata Regah Jesu nanan ana marakaw bonamanamarinamaim boro na’afufur naatu awayourin ana fairamaim boro nababintatab.
9 Woyipitsitsayo adzabwera ndi mphamvu za Satana. Adzaonetsa mphamvu zake pochita zizindikiro ndi zodabwitsa zachinyengo.
9 Orot Kakafin boro Satan ana fairamaim nabo’awi’aw nan, sawar men ta’i’itah efa’efanin, ina’inan, naatu baifofofor yumatah ta ta boro nasinaf,
10 Iye adzagwiritsa ntchito mtundu uliwonse wachinyengo kupusitsa amene akuwonongeka. Iwo akuwonongeka chifukwa akukana kukonda choonadi ndi kuti apulumutsidwe.
10 sabuw iyab tur anababatun baiyabuwin nowar imaim yawas bain isan ana ef hikwahir sa’ab tenan, nati sabuw boro iti ina’inanamaim hinifufuwih hinan hinakasiy.
11 Chifukwa cha chimenechi, Mulungu akuwatumizira chinyengo chachikulu kuti akhulupirire bodza.
11 Anayabin iti isan God baifufuwen ana fair itih wanawanahimaim nabow saise baifuwen hinitumitum,
12 Choncho adzalangidwa onse amene sanakhulupirire choonadi, koma anakondwera mu zoyipa.
12 bowabow kakafin nitenmumunih hinasisinaf yomaninamaim boro God ana baimakiy wanawanan hinarun. Anayabin turobe men hinitumatum.
13 Koma tiyenera kuyamika Mulungu chifukwa cha inu abale okondedwa mwa Ambuye, pakuti Mulungu anakusankhani pachiyambi pomwe kuti mupulumuke chifukwa cha ntchito yoyeretsa ya Mzimu ndi chikhulupiriro chanu mʼchoonadi.
13 Igewasin aki merarayow mar etei God anitin kwa isa, kwa i Regah ebiyabuwi taitu. Anayabin sabuw etei wawanahimaim kwa i God rubini Anun Kakafiyin ana fairane yasairi turobe kwaitumatum yawas kwabai.
14 Iye anakuyitanirani zimenezi kudzera mwa uthenga wathu wabwino, kuti mulandire nawo ulemerero wa Ambuye athu Yesu Khristu.
14 Iti tur gewasin aki ana abinan kwanonowar imaim God kwa eafi, saise nati wanawananamaim nabonawiy ata Regah Jesu Keriso ana aiwob bairi kwanafaram.
15 Kotero tsono, abale, imani mwamphamvu ndi kugwiritsa ziphunzitso zimene tinakupatsani kudzera mʼmawu apakamwa kapena kudzera mʼkalata.
15 Isanimih taituwau, kwanabatkikin naatu turobe abinan kwanonowar o fefemaim akirum abi’obaiyi i kwanabukikin.
16 Ambuye athu Yesu Khristu mwini ndi Mulungu Atate wathu, amene anatikonda ife ndipo mwachisomo chake anatipatsa kulimba mtima kwamuyaya ndi chiyembekezo chabwino,
16 Ata Regah Jesu Keriso taiyuwin naatu Tamat God it ebiyabuwit. I ana manaw ana kabeber wanawanamaim, wanatowan ana koufair nitit nuhit nafot tanama.
17 akulimbikitseni ndi kukupatsani mphamvu yogwirira ntchito ndi kuyankhula zabwino zilizonse.
17 Naatu dogor ana koufair nitin naora’ah saise mar etei aturamaim naatu asinafumaim gewasih kwanasinaf.

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar 2 Tessalonicenses 2, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.