2 Timóteo 1
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Paulo mtumwi wa Khristu Yesu mwa chifuniro cha Mulungu. Anandituma kuti ndilalike za lonjezo la moyo umene uli mwa Khristu Yesu.
1 Ayu Paul Jesu Keriso ana tur abarayan, God ana kokomaim iyunu atit Keriso Jesu wanawananamaim yawas wanatowan eo’omatanit i ao’orereb.
2 Kwa Timoteyo, mwana wanga wokondedwa:
2 Iti fef o Timothy isa akikirum, ayu natu au yabow, isa ayoyoyoban manaw kabeber, baiwanbabanen, tufuw, God Tamat naatu Jesu Keriso ata Regahane isa nama.
3 Ndikuyamika Mulungu amene ndimamutumikira ndi chikumbumtima chosatsutsika, monga momwe ankachitira makolo anga. Usiku ndi usana ndimakukumbukira mosalekeza mʼmapemphero anga.
3 Ayu God isan abowabow au not wanawanan men ana kwarisin ta auman, baise turobe’emaim ana merar ayiy, uwai’inah hisisinaf na’atube. Au yoyobanamaim fai mar o anuhi God ana merar ayiy.
4 Ndikamakumbukira misozi yako, ndimalakalaka nditakuona kuti ndidzazidwe ndi chimwemwe.
4 O matur re’er i anotanot, fai mar etei au kok gagamin i mi’itube ata’iti maiye, saise atiyasisir.
5 Ndakumbukira za chikhulupiriro chako choona chimene chinayamba mwa agogo ako a Loisi ndi mwa amayi ako Yunike ndipo ndikutsimikiza mtima kuti chilinso mwa iwe.
5 O a baitumatum turobe isan i mar etei nuhu ekukusib, nati baitumatum i wantoro’ot o uwat Lois, naatu o hinat Eunice hairi hibitumatum, boun i ayu aso’ob anababatun o auman nati baitumatum ta’imon kubitumatum.
6 Nʼchifukwa chake ndikukukumbutsa kuti upemerere monga amachitira moto, mphatso imene Mulungu anakupatsa nditakusanjika manja.
6 Anayabin iti isan o nuhi akukusib, ayu umau tafa ayayara’ah ana veya God ana usar bit inababin maiye na’in nato’ab.
7 Pakuti Mzimu amene Mulungu anatipatsa, si Mzimu wotipatsa manyazi, koma Mzimu wotipatsa mphamvu, chikondi ndi kudzisunga.
7 Anayabin God Anunin bitit i men baibiruwit isan ititamih, baise Anun Kakafiyin bitit i fair, yabow naatu yawas rumutumutufurin bow isan itit.
8 Choncho usachite manyazi kuchitira umboni Ambuye athu, kapena kuchita manyazi chifukwa cha ine wamʼndende. Koma umve nane zowawa chifukwa cha Uthenga Wabwino, mothandizidwa ndi mphamvu za Mulungu.
8 Isan imih Regah ana tur orereb isan men biya na’ohow, na’atube ayu dibur ama’am isan men biya na’ohow, baise Tur Gewasin isan ayu biyau ebababan na’atube, obo aunowa biya nababan God fair ebit na’atube.
9 Iye anatipulumutsa ndipo anatiyitanira ku moyo oyera mtima, osati chifukwa cha chilichonse chimene tinachita, koma chifukwa cha chikonzero ndi chisomo chake. Chisomo chimenechi anatipatsa ife mwa Khristu Yesu nthawi isanayambe.
9 I iyawasit naatu afa’af kakafiyinamaim eafit tana yasairit ana sabuw nowanamih tamatar, ea’afit i men it ata bowabow gewasin tabowabow imaim itin eafitamih, baise i taiyuwin ana kokomaim naatu ana manaw ana kabeberamaim Jesu Keriso i’obaiyit ta’itin. Iti i marasika tafaram aneika yakitifuw.
10 Koma tsopano Mulungu watiwululira kudzera mʼkuoneka kwa Mpulumutsi wathu, Khristu Yesu, amene anathetsa mphamvu za imfa ndipo mwa Uthenga Wabwino anaonetsa poyera moyo umene sungafe.
10 Naatu boun ata baiyawasenayan Jesu Keriso nan ana veya sawar etei isat hirerereb, morob ana fair e’asabun naatu Tur Gewasinamaim yawas wanatowan i’obaiyit na irerereb.
11 Ine ndinasankhidwa kukhala wamthenga, ndi mtumwi ndi mphunzitsi wa Uthenga Wabwinowu.
11 Ayu i kob abarin naatu Tur Gewasin sabuw bai’obaiyih isan God rubinu,
12 Nʼchifukwa chake ndikuvutika monga ndililimu. Komabe zimenezi sizikundichititsa manyazi, popeza ndikumudziwa amene ndamukhulupirira ndipo ndikutsimikiza mtima kuti akhoza kusamalira chimene ndinamusungitsa mpaka tsiku lijalo.
12 anayabin iti isan ayu biyababan gagamin abaib. Baise biyababan abaib isan men biyou eo’ohowamih, anayabin ayu yait abitumitum i aso’ob, i boro ana fair natafafaru Tur Gewasin bitu anabotan nan yomanin ana Veya natit.
13 Zimene unamva kwa ine, uzisunge kuti zikhale chitsanzo cha chiphunzitso choona, mwa chikhulupiriro ndi chikondi mwa Khristu Yesu.
13 Tur anababatun abi’obaiyi inabukikin, mar etei nati bi’obaiyen ini’ufunun, naatu baitumatum, yabow Keriso Jesu bitit i wanawanamaim nama.
14 Samalira bwino zokoma zimene anakusungitsa. Uzisamalire mothandizidwa ndi Mzimu Woyera amene amakhala mwa ife.
14 God Anun Kakafiyin it wanawanatamaim ema’am i ana fairamaim sawar gewasih hitutumi hibit ina tafafar gewas.
15 Iwe udziwa kuti onse a mʼchigawo cha Asiya anandithawa, kuphatikizapo Fugelo ndi Herimogene omwe.
15 Inaso’ob sabuw Asia wanawanan hima’am etei ayu hihamiyu, na’atube Figelus naatu Hermogenes hairi auman ayu hihamiyu.
16 Mulungu achitire chifundo banja lonse la Onesiforo chifukwa ankandisangalatsa kawirikawiri ndipo sankachita nane manyazi ngakhale ndinali womangidwa ndi maunyolo.
16 Ayoyoyoban Regah mi’itube Onesiporus ana nibur bairi nakabibirih, anayabin mar etei ena ayu koufair ebitu, naatu dibur ama’am isan men kafai biyan eo’ohow.
17 Mʼmalo mwake, atangofika ku Roma, anandifunafuna ndipo anandipeza.
17 Baise na Rome titit ana veya ana kok i mi’itube ayu ta’itu, imih nuwuhu nan ayu titauru itu.
18 Ambuye amulole kuti adzalandire chifundo kwa Ambuye pa tsiku lijalo! Ukudziwa bwino momwe iye anandithandizira mʼnjira zosiyanasiyana ku Efeso.
18 Ayu ayoyoyoban mi’itube Regah baibatebat ana Veya iti orot takabibir, anayabin Ephesus imaim ayu isau bowabow gagamin maiyow bow bibaisu o iso’ob, o men kukakasiyomih.
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar 2 Timóteo 1, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.