2 Pedro 3
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Inu okondedwa, iyi ndi kalata yanga yachiwiri kwa inu. Ine ndalemba makalata onse awiri kuti ndikukumbutseni ndi kukutsitsimutsani ndi cholinga choti muzilingalira moyenera.
1 Are au ofonah baitumatumayah. Iti fef i mar bairu’abin kwa isa akirum abiyafar. Iti fef rou’ab wanawanahimaim mi’itube a not ata kura’ara’ah not gewasin kwatab sawar iti a notamaim hitama.
2 Ndikufuna kuti mukumbukire mawu amene anayankhulidwa kale ndi aneneri oyera mtima ndiponso lamulo limene Ambuye ndi Mpulumutsi wathu analipereka kudzera mwa atumwi.
2 Marasika God ana dinab kakafiyih kwa a tur hi’owen kwanonowar i a notamaim nama. Naatu ata Regah Jesu Keriso naatu ata Baiyawasenayan ana tarbaiyunen tur i kwa a turabarayah a tur hi’owen.
3 Poyamba mudziwe kuti mʼmasiku otsiriza kudzafika anthu onyoza, adzanyoza ndi kutsata zilakolako zawo zoyipa.
3 Abistan God ana dinab sabuw tur wantoro’ot hi’u’uwit i kwananot nukwarimaim kwanayai. Mar yomanin sabuw afa boro wanawanatamaim hinatit. Nati sabuw hai yawas i kakafinamaim ebobonawiyih. Kwa isa boro hini’i’iyab men kafaita.
4 Iwo adzati, “Kodi suja Ambuye analonjeza kuti adzabweranso? Nanga ali kuti? Lija nʼkale anamwalira makolo athu, koma zinthu zonse zili monga anazilengera poyamba paja.”
4 Naatu i boro hinao, “Regah eomatani namih rauw eo’o i men namih? Kwa’itin aki uwai’inah marasika himomorob boro’ika hai hubemaim ti’inu’in. God marasika tafaram sinaf matar inu’in ana’itinin ta’imon na’atuka ti’inu’in.”
5 Koma iwo akuyiwala dala kuti Mulungu atanena mawu, kumwamba kunakhalapo ndipo analenga dziko lapansi ndi madzi.
5 Baise aneika God ana obaiyunen turamaim eo, mar tafaram himatar. Harew ouyate yen tafaram matar naatu tafaram i harewamaim matar.
6 Ndi madzinso achigumula, dziko lapansi la masiku amenewo linawonongedwa.
6 Tafaram atamanin harew tit tafaram etei bufut naatu anababatun gurus sawar.
7 Dziko la kumwamba ndi lapansi la masiku ano akulisunga ndi mawu omwewo kuti adzalitentha ndi moto. Akuzisunga mpaka tsiku limene adzaweruza ndi kuwononga anthu onse osapembedza Mulungu.
7 God obaiyunen tur ta’imonaban eo, mar tafaram iti boun tama’am kaifen ya ti’inu’in boro wairafamaim na’afuyar. Sabuw iyab men God ana kokokomaim tema’am boro nibabatiyih. Nati ana veya’amaim tafaram iti boun tama’am God boro nagurus.
8 Koma abale okondedwa, musayiwale chinthu chimodzi ichi: Kuti pamaso pa Ambuye tsiku limodzi lili ngati zaka 1,000, ndipo zaka 1,000 zili ngati tsiku limodzi!
8 Baise au ofonah, iti sawar ta’imon i men nuhinaburumih. Regah God, veya ta’imon ebiyab ana’itinin i boun 1,000 na’atube naatu kwamur 1,000 ebiyab i boun veya ta’imon na’atube.
9 Ambuye sazengereza kuchita zimene analonjeza, monga ena amaganizira. Iwo akukulezerani mtima, sakufuna kuti aliyense awonongeke, koma akufuna kuti aliyense alape.
9 Imih Regah Jesu Keriso ana na isan eo’omatanit i men erurubirabir. Boun sabuw afa sinafumih tema tirurubirabir imaibo tenot tisisinaf na’atube’emih. Kwa isa ekakaif, anayabin i men ekokok ana orot ana babin ta kakafin wanawanan narun baimakiy nab. Baise i ekokok orot babin etei hai bowabow kakafih hinihamiyen, naatu men ekokok ta nakasiy.
10 Koma tsiku la Ambuye lidzafika ngati mbala. Pa tsikuli zinthu zakumwamba zidzachoka ndi phokoso lalikulu. Zinthu zonse zidzawonongedwa ndi moto, ndipo dziko lapansi ndi zonse zili mʼmenemo zidzapsa.
10 Baise Regah Jesu Keriso ana veya natitit it boro tana’ororsa’ir bainowan mowan etitit na’atube. Nati gagub narab nafufudir ana veya mar na’am saniwa’an naatu sawar maramaim boro etei na’am hinan. Naatu wairaf ana fora’abinamaim sawar maramaim tema’am etei boro hinadew, naatu tafaramamaim sawar sinaf himamatar boro owararin na’in.
11 Popeza kuti zinthu zonse zidzawonongedwa motere, kodi inu muyenera kukhala anthu otani? Muyenera kukhala moyo wachiyero ndi opembedza Mulungu
11 Imih ana efamaim kwanama. Anayabin God tafaram boro nagurus isan kwanakakaf a yawas etei mutuforomo kwanama.
12 pamene mukuyembekezera tsiku la Mulungu ndi kufulumiza kufika kwake. Pa tsiku limeneli zinthu zakumwamba zidzawonongedwa ndi moto, ndipo zidzasungunuka ndi kutentha.
12 Na’atube kwanama’am God ana veya boro saife’ewat natit. Sawar etei maramaim tema’am boro wairaf nikubar na’arah naatu sawar etei boro ana towa’amaim na’arah nadew.
13 Koma ife tikudikira kumwamba kwatsopano ndi dziko lapansi latsopano, zimene Mulungu analonjeza, mʼmene chilungamo chidzakhalamo.
13 Baise abistan God it eo’omatanit, isan tama tanuwanuw nati i mar tafaram boubun, ma gewas yawas roumutufuren ana efan ata baremih tanab tanama.
14 Chomwecho okondedwa, popeza inu mukudikira zimenezi, chitani changu kuti mukhale wopanda chilema kuti mukhale pa mtendere ndi Iye.
14 Isan imih, au ofonah, kwa aur kato en, ubar en naatu tufuwamaim kwanama kwanakakaif Regah ana Veya nab nanan gewasinamaim kwanama’am nabuwi.
15 Zindikirani kuti kuleza mtima kwa Ambuye kukutanthauza chipulumutso, monga momwe mʼbale wathu wokondedwa Paulo anakulemberaninso ndi nzeru zimene Mulungu anamupatsa.
15 A notamaim nama, Regah hamenam erurubirabir anayabin i ekokok sabuw etei yawas hinab. Ata of Paul auman God not rerekab itin kwa isa eo kirum.
16 Iye walemba chimodzimodzi makalata ake onse, kuyankhula za zinthu izi. Mʼmakalata ake mumakhala zinthu zina zovuta kuzimvetsa, zimene anthu osadziwa ndi osakhazikika amazipotoza, monga amachita ndi malemba ena onse, potero akudziwononga okha.
16 Ana fef etei kikirum i tur ta’imon eo kirum iti sawar isah. Paul ana tur afa kikirum i fokarih hai yabih men karam tanaso’ob. Bereberefiy hai baitumatum en, tur iti baifuwenamaim tebobotabir na’atube God ana Tur afa auman tebobotabir kakaf. Imih i taiyuwih hai kakafin bonawiyih egugurusih.
17 Nʼchifukwa chake, abale okondedwa, popeza mukuzidziwa kale zimenezi, chenjerani kuti musatengeke ndi zolakwa za anthu osaweruzika, mungagwe ndi kuchoka pamalo otetezedwa.
17 Baise au ofonah, kwa marasika kwaso’ob. Matatoniwa’an, nati baifufuwen bai’obaibiyenayah isah, saise kwa boro men hai bai’obaiyen kakafihimaim kwa nabonawiyi yawas ana ef kwanarusa’irimih.
18 Koma kulani mu chisomo ndi mʼchidziwitso cha Ambuye ndi Mpulumutsi wathu Yesu Khristu. Kwa Iye kukhale ulemerero tsopano mpaka muyaya. Ameni.
18 Baise ata Regah Jesu Keriso ata Baiyawasenayan ana kabeber naatu anaso’ob kwa wanawanamaim na’in natit. God tanifai tanabora’ar’ah boun naatu wanatowan! Amen.
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar 2 Pedro 3, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.